Це відео не доступне.
Перепрошуємо.

KWAGWANJI - KUSANTHULA ZOMWE ZACHITIKA KU UTM 12 July 2024

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 11 лип 2024

КОМЕНТАРІ • 252

  • @cassimyusuf6683
    @cassimyusuf6683 Місяць тому +40

    UTM have made a brilliant decision, simungakhale limodzi ndi anthu ankhaza, okhesa mwazi

  • @FrankKambwani
    @FrankKambwani Місяць тому +2

    Mtsikana wamzeru amati akafunsilidwa ndi mamuna panjira asanalore amapita kukawafotokozera abale ndi makolo ake cholinga onse adziyendera limodzi ndi mtsikanayo mumaganizo...Apapa vuto ndidaliwona ine pa Usi atasankhidwa kuti akhale vp sadapite kwamakolo(utm)kukakhala nao pansi adangoti ndatola banja dzotsatila dzake makolo akudzamuzimudziwa mamuna uja kuti ndi chimbalangondo it's too late ana akwatilana kale.Usi adzikhweza ndithu.😅😅

  • @augustMag
    @augustMag Місяць тому +11

    Kuganiza mwanzeru UTM palibe chokhalira mu gwirizano pamene mwini wake amene anasayinira kulibe ❤❤❤

    • @user-ty1vq9lq6w
      @user-ty1vq9lq6w Місяць тому

      Achita bwino kutulukamo ngati ankaonetsa nkhanza chilima alipompo

    • @DinesiKafukiza
      @DinesiKafukiza 29 днів тому +1

      Mbambande zakhalabwinokwambili

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza Місяць тому +14

    Zandikomela izi till pambuyo panu a utm osafooka

  • @user-im7sc2my4w
    @user-im7sc2my4w Місяць тому +14

    Tingopempha kuti amene atenge mpando wa chilima akhale munthu wokhwima nzeru ,kuti ma members asabalalike. Mr Usi ,ndi munthu wanzeru ,mumuwone zomwe apange ,musiyeni amalize term yoyambaonga mwa Mr malemu Chilima Mr Usi akhalabe wa UTM ,mudzandikhulupilila

  • @mkhulukinyata5198
    @mkhulukinyata5198 Місяць тому +1

    Well done UTM..You have made the good decision for being separate it yourself from the Killer's .. I'm from Zimbabwe but my fore-fathers are Malawian's.. So they've been telling us about how Harsh MCP was on that past years ago ..Mapanga bino kuchokha ku muwanthu wakuyipa yawa ..

  • @user-tf7yi9fp2u
    @user-tf7yi9fp2u Місяць тому +11

    UTM is intact and is more united after the death and infact many people have joined UTM but don't just see the NEC only. We are set with votes in 2025. Whatever will come out as UTM we will cling to the principles no matter what come may. Viva UTM. If agreement was respected there would have been cordial working relationship. Why out of the full support, campaigning for you and you choose to ill treat him the whole of four years mmmmm not true of being a true Malawian and a Christian. So what is your conscious telling you today? Remember there is always tmrw. Be good to people as you will soon need them. Viva UTM

    • @JohnTchirati
      @JohnTchirati Місяць тому +1

      MCP imapha kuyamba kare historically, komabe Chakwela is not involved but people around him.

    • @JohnTchirati
      @JohnTchirati Місяць тому

      Just the remarks oti ndizaimanso? Pa alliance??????

  • @jacobstvn7995
    @jacobstvn7995 Місяць тому +6

    Malawi lost a visionary leader because MCP greedy behavior....UTM has moved out, let them enjoy the seats!! As Malawi we have not benefited from this alliance....we have been hurt even more!! So disappointing!!

  • @StiveKantiki
    @StiveKantiki Місяць тому +3

    Banja linali la amayi amagonesedwa nyumba yo dontha lelo amai amwalila mukagulile anawo nyumba adabwa anawo ndi ulemu ukubwelawo amai awo samaziona achitabwino kutuluka l ❤ utm more 🔥

  • @user-fd6oh2vc1c
    @user-fd6oh2vc1c Місяць тому

    You guys so massive.Wonder u r so wise dear brother….we are proud of you three Big boys.

  • @SandforeKadzamira
    @SandforeKadzamira Місяць тому +12

    Brian Banda,sitidzampezanso presenter ngati iwe

  • @juliusnjerengo2610
    @juliusnjerengo2610 Місяць тому +1

    The combination of Brian, Jona and Wonder it is same as Aki, Paw Paw and Sam Loko. Very Entertaining.

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i Місяць тому +4

    Akanatuluka kalekale chilima sanakamwalila 😢

  • @ThaboMoffia-j7p
    @ThaboMoffia-j7p Місяць тому +1

    Big up UTM ndipo zamanganyazo ndizosagwiladi mtima zatha zatha osabwelela mbuyo

  • @user-pv9uk6sc3w
    @user-pv9uk6sc3w Місяць тому +4

    Jona pankuku ukunena zoon, Usi si wa UTM, bwanji amakaimila u mp as independent pamene ali mu UTM. Manganya ndi wa MCP basi.

  • @JohnChiwaya-ym5me
    @JohnChiwaya-ym5me Місяць тому +3

    Ma guys , you have scrutinised the politics well. Ndakunyadilani zeedi

  • @stanleymatolabanda5460
    @stanleymatolabanda5460 Місяць тому +4

    Ndangwirizana nazo zomwe chipani changa cha UTM chachita ndipo MCP iyiwale zotenga boma ndipo Chewa Muziwona kwanu kwatha akupha inu

    • @MayorMagombo
      @MayorMagombo Місяць тому

      You are a liar , mcp is there to stay , you are just waste your time. DPP HAS MANIPULATED YOU SICK PEOPLE.

    • @lillynhlema9656
      @lillynhlema9656 Місяць тому

      Ndipo achita bwino kwabasi

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg Місяць тому +3

    Achita bwino a UTM kusiyana nadzo dzigawenga dza MCP dzamagazi mmanja 😢😢

  • @WilsonMagongwa
    @WilsonMagongwa Місяць тому

    Ngati pali kugawikana ku utm koma ochokawo apanga chiganizo chabwino ndale za a Michael Usi zitipwetekesa akufuna iwo okha ziziwayendela bwino kusiya 20 million people omwe akuvutika.

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 28 днів тому +1

    Chilima was the only perfect leader to utm party enanu ndiye worse wat makes you better than the other political leaders, the problem is that you guys simukufuna usi kudzakhala acting president because of your stiggy minds trust God on this he might guide you better than akhungu okhaokha kutsongorerana njila , that's means your don't love Malawi but being proud to your self intrest

  • @Aqiec09
    @Aqiec09 28 днів тому +1

    Can you pliz build your own better Malawi than criticizing others , I mean all those with meaningless coments , because I see no one Will ever be perfect on this

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t Місяць тому +3

    Ndevu zamwayi munthu wanzeru kwambiri

  • @user-wi8xw9qh7n
    @user-wi8xw9qh7n Місяць тому +4

    Sitikuwaopa sitifooka mcp must goooo

  • @ahmedwyson4865
    @ahmedwyson4865 Місяць тому +3

    Apapa nde ma team akumana
    Ndikamamvera nganizi chaaa ndimachita kumva kukhoma

  • @batsong.chitseko5903
    @batsong.chitseko5903 Місяць тому +3

    Usi ngwa MCP. kuchoka mu mgwilizano a UTM achita bwino.

  • @VincentKatimba
    @VincentKatimba Місяць тому +1

    That's a good distion wamkulu akakhala kuyipa sachita kumuuza amaonera mphepo tiripambuyo panu utm oyeee am I ❤🎉tikulira chilima ife timamukonda kwambiri 😂😂😂😂

  • @AndersonChiponola
    @AndersonChiponola Місяць тому +1

    Koma to be honest utm Ikuyenera kukhala pasi kusankha munthu wa nzeru otherwise chipani chawo chitha kudzakhala chopanda tsogoro because to be honest wisdom ya Chilima simugafanizira Anthu amene angoyankhulawa chifukwa foundation ya utm akudziwa bwino ndi Chilima koma vuto anafa Anthu asanawauze zithu. UDF ngati inatha tsogoreri alipo kuli bwanji UTM leader anamwalira kwa ine is no future ku UTM

  • @ChimwemweBottomani-hc5ju
    @ChimwemweBottomani-hc5ju Місяць тому +1

    This is brilliant Utm u made a right decision my advice is...dont let USI to join you hes evil like chakwera...congrats team

  • @ChifundoNinje
    @ChifundoNinje Місяць тому +4

    Mwaganiza mwa mzelu a utm km mubwerere kumeneko munachokela

  • @Christophermalema-o8t
    @Christophermalema-o8t Місяць тому

    Thanks for your constructive decision UTM.You have made a right channel which will attract some people even to join you & vote for you in 2025 elections.May the almighty God paveway for you.

  • @KennyPhiri-zg1kr
    @KennyPhiri-zg1kr Місяць тому

    UTM sopano ilibe msogoleri amen anthu angamu votere kuliana okha DPP yinaramura kale no vote UTM MCP alephera yesani Aford kapena UDF sopano coz mukayikaso DPP muzaliraso Murakami 5 years again.

  • @user-je8jm5uy1q
    @user-je8jm5uy1q Місяць тому

    UTM yachita bwino kuchoka mu ngwilizano so Manganya osadandaula naye analowa kale kale mu MCP ndipo ndi modzi mwa Yudasi isakaliyoti

  • @user-oj2fy7vx1z
    @user-oj2fy7vx1z Місяць тому

    Best analysis

  • @JohnConar-kq4hi
    @JohnConar-kq4hi Місяць тому +1

    That's what I was waiting utm be strong 💪

  • @RobertGoliat-gt2qh
    @RobertGoliat-gt2qh Місяць тому +1

    Usi ndi wamzeru zakuya and tsiku lina azalankhulanso zamzeru kma UTM yachita bwino kutuluka mumgwirizano

  • @user-tl9xg4fg9x
    @user-tl9xg4fg9x Місяць тому

    Zachitabwino mubwelele kumene munachoka kuti tichose chigawengachi

  • @Lunnah-b1t
    @Lunnah-b1t Місяць тому

    Mwayakhula bwino zedi ,wakumva wamva,mumatiyimilira guys love from cp,more fire

  • @BittonRashid
    @BittonRashid Місяць тому

    Koma azibambo tikuyamikileni siyamika mukulowa mmanda mumatilankhulila odana nanu ndiodana ndichilungamo.ndakamba izi chifukwa mbalizonse mumagundako osanva asanve zikomo azibambo ❤

  • @YOMALO.
    @YOMALO. Місяць тому +1

    😂guys, you're making the show enjoyable

  • @brainsmkumbwa6267
    @brainsmkumbwa6267 Місяць тому

    Iam over the moon for the decision made by U.T.M,zaunetsa kuti Chilima wasiya anthu oganiza moyenelera

  • @gabrielchimangeni4376
    @gabrielchimangeni4376 Місяць тому

    Brain munthu wa bwino komaso opemphera mukayime nawo Ku coveshon bwana ngati presdent wa Utm bwana

  • @user-co3wr3rn4h
    @user-co3wr3rn4h Місяць тому

    Ife tilinganga pambuyo pa utm phee

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Місяць тому

    Palibe chokanila ,,iwe wonder,,,chipanichi chikulondoledwa ndi anthu ,,anachita bwino kukana mafuso

  • @AboudujanahMawulidi
    @AboudujanahMawulidi Місяць тому

    UTM yaganidza bwino kwambiri potuluka mugwilizano

  • @mphatsosadiki4983
    @mphatsosadiki4983 Місяць тому

    Its not too late for UTM kubwelera Kwa make komwe anachokera.......🎉🎉🎉.I would love ma alliance akamachitika azinena zomwe agwilizana .

  • @TonnyDyton
    @TonnyDyton Місяць тому +1

    Likamatha banja or palafini wamunyali amapopedwamo

  • @GodfreyWhayo-hh1dm
    @GodfreyWhayo-hh1dm Місяць тому

    A MCP adakwera pachulu ndikulengeza kuti wina afune Kaya asafune iwowo adzapambana chisankho ndi 70% . Kodi kapena anaconda kale mwala ?

  • @InnocentEdasi
    @InnocentEdasi Місяць тому +4

    UTM osafooka🔥🔥🔥. , mzimu wa Chilima wuse mumtendele

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn Місяць тому +1

    Amwene awa ali pakatiwa sindimawavesesa zokamba zawo serious

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr Місяць тому

      Ndipo ngati ndinu nokha kkk amamuikilanji kaya. Apapa ikanabeba akanakhalapo a Chunga not Jonayo aaa. Amangodziwa kusokosa ndipo muli fundolesi 😂 mudzitimverako plz a times we love you but uyoyo wavala blueyo apume mu programyi. Ndinakupemphaninso to bring Mr Kapito John, Asowa and muli mutu mmenemuja 😂

  • @SamuelAntone-mz6nq
    @SamuelAntone-mz6nq Місяць тому

    Zakhala bwino tidakalila ife malilo wanthu panopa

  • @samalanimacdonald9373
    @samalanimacdonald9373 Місяць тому

    Ndenvu zamwayi koma abanda akulakwila chiyan

  • @Cathy-oc7vd
    @Cathy-oc7vd Місяць тому

    Gwirizano sunathe pano ayi.. unatha 2 years ago, this is just formal panopo

  • @user-ml2vw1dc9c
    @user-ml2vw1dc9c Місяць тому +1

    Lef nthawi coach adachoka 😢😢😢

  • @BlessigsChabzola
    @BlessigsChabzola Місяць тому +2

    Achita bwino kutuluka chakwera angakhale oyamba kupereka kalata ya upulezidenti kuchipani chawo, osakumbukira zosawakhuza zomwe anasayinira ndi malemu.

  • @BittonRashid
    @BittonRashid Місяць тому

    Ganizolabwino malinga the way Malawi pathing through

  • @omarmkwanda2184
    @omarmkwanda2184 Місяць тому

    Micheal usi ndi njoka mu udzu, alibe mtsogolo

  • @BlessingMkonda
    @BlessingMkonda Місяць тому

    Wakupha Sadyrra naye Segwaa imodzi

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Usi is good guy, he is not far behavior like Chilima. UTM members don't destroy party because of losing Chilima. Once you will start pointing figure someone in a party you will realize tomorrow when party is going to an end

  • @user-zh9kb2sj2i
    @user-zh9kb2sj2i Місяць тому +1

    Inu musapusisike mcp ndiyomweinanenakuti zagwilizano sakuzidziwa

  • @LawrentNyasulu
    @LawrentNyasulu Місяць тому

    Koma apamkuku banja latsopabo anthu amagona 4pm akuti usiku umafupika

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u Місяць тому

    A mcp ndi akupha
    Chakwela ndiwe munthu oipa machende ako

  • @HappyKanyangala-oq1kk
    @HappyKanyangala-oq1kk Місяць тому +1

    Amabodxa inu

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u Місяць тому

    I'm coming to malawi I want to meet you guys well done

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Місяць тому

    Ungakonde mwana wanga kudana ndi ine bambo wake? Usi wachoka kuti

  • @leonardgondwe1470
    @leonardgondwe1470 Місяць тому

    Zoonadi kuti Mr usi wabalalika chifukwa chakuti masapota a utm sakufuna mgwirizano pomwe a usi ndi a vice a boma😊😊😊

  • @user-oc8nj3or6y
    @user-oc8nj3or6y Місяць тому

    We're not afraid anymore ndipo we're going to register with the aim of goin to vote ❤on a serious note,,,we cannot fail to survive that's because of Michel Utsi,,,nono let him do what he can

  • @user-px5tz4kb5s
    @user-px5tz4kb5s Місяць тому

    Chawezi Banda ndidzanena Kuti chapita

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u Місяць тому

    Malawi we lose chilima adalakwitsa kusakha ausi simunthu wabwino

  • @RemaniBanda-u2n
    @RemaniBanda-u2n Місяць тому +1

    achita bwino awonezina

  • @BlessingMkonda
    @BlessingMkonda Місяць тому

    Sats true words

  • @lillynhlema9656
    @lillynhlema9656 Місяць тому +1

    Koma decision ndaikondq
    That's part of kumulemekezq chilima after all the torture he went through with mcp

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r Місяць тому

    Mcp chipani chakupaa chama gaziii chakwela fitiii

  • @grantnantchito2919
    @grantnantchito2919 Місяць тому

    To us🎉we had no questions on the Statement made 😢 Don't put us words in our mouths. Decision well made on our behalf

  • @MadaKanene
    @MadaKanene Місяць тому

    Komatu band yagawana zida vinyo atantha kale 😮,,, I think is too late 🕐,,,, when justice delays become injustice

  • @user-kj7hr2jf1l
    @user-kj7hr2jf1l Місяць тому

    Utm yaganibo heve usi apite ku ufiti zizake ku mcp

  • @AnthoniohMazengera
    @AnthoniohMazengera Місяць тому

    Brian iweo mbambande and your coligis their

  • @fumumdolo7341
    @fumumdolo7341 Місяць тому

    UTM has made the right political decision. Deputy President was supposed to lead to put the house in order. The guy lacks stamina to judge Malawians mind. USI can't afford to unite UTM it's lost opportunity, he could have demonstrated in presence of his boss. Very tricky situation to USI and MCP.

  • @LinlyNakombe
    @LinlyNakombe Місяць тому

    Good decision

  • @SlindileAyanda-sz4zw
    @SlindileAyanda-sz4zw Місяць тому

    That's great idea utm

  • @HenryMkoko-sx2yv
    @HenryMkoko-sx2yv Місяць тому

    😂😂😂😂 Ndemwati tikakwatirana 4 o'clock timakhala tayambapo kudya bwemba usiku umakhala waufupi?

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Місяць тому

    Muziyagana kuno guys mukuopa?

  • @user-du9qs4tb6u
    @user-du9qs4tb6u Місяць тому

    Ausi si wa utm ndi anthu usana

  • @allahslave7177
    @allahslave7177 Місяць тому

    Usi ali ngati munthu wa banja amene ali ndi chibwenzi panja ndipo nachipanga value chibwenzi pamaso pa banja ndiye ankhoswe abanjawo they come to know , thats alibe intereste mwa Usi a Utm

  • @user-ev4or2kg4z
    @user-ev4or2kg4z Місяць тому

    Ndikavote pano tilibe boma

  • @dondamissonchdziwe3958
    @dondamissonchdziwe3958 Місяць тому

    Achoka mochedwa atawaphera Kale Chilima,kuimba chiminingo Njobvu zaononga zapita Kale

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h Місяць тому +6

    Achita bwino ndithu ❤❤❤

    • @ManninLongwe
      @ManninLongwe Місяць тому

      Ngati mwatelemu mwathesa mugwilizano amene azayimila usogoleri kumbali yanu ya utm yomwe azakhala pa baluti ndindani?

  • @ProgloKazembe2-eu7hn
    @ProgloKazembe2-eu7hn Місяць тому

    Zamphamvu Guys

  • @francisvisage2705
    @francisvisage2705 Місяць тому

    Body language ya Ndevu Zamwayi can tell Kuti anadyako Chibanzi from MCP

  • @lukepeter8290
    @lukepeter8290 Місяць тому

    A banda mwati anatani 😅

  • @kotking-xg7pp
    @kotking-xg7pp Місяць тому

    sanabwele bwino ndithu kkkkkkkk

  • @user-dg5pc6rz1b
    @user-dg5pc6rz1b Місяць тому +1

    Mcp yatha koma vuto ndilakuti libela mavoti mfunso nkumati inu azipani mukukonzekela chani kuti nchitidwe obela mavoti usadzachitike?

    • @ProsperBanda-ju2mq
      @ProsperBanda-ju2mq Місяць тому

      Mcp singathe Koma chipani chathuchi ndichimene chingathe

  • @jameskamanga628
    @jameskamanga628 Місяць тому

    Zovuta kwambiri

  • @FrancisDominic-w1s
    @FrancisDominic-w1s Місяць тому +1

    Ausi ngati sasamara azafera kusata

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 Місяць тому

    It's too early for questions

  • @lawrencekauwa8005
    @lawrencekauwa8005 Місяць тому

    Bliriant decision finally made

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r Місяць тому

    Zilibwino kwambilili mmm sha,,,wakwiya ndi fit😂😂

  • @VanaKhama
    @VanaKhama Місяць тому

    Amene anathawqpo a yufi ngati ine sangadabwe

  • @user-uv5rf4zt5q
    @user-uv5rf4zt5q Місяць тому

    It's a right decision if they moved out early chilima could be alive today.

  • @user-le9su3mt7r
    @user-le9su3mt7r Місяць тому

    Brian yomwe ni busa kkkkk

  • @LeviChakwira
    @LeviChakwira Місяць тому

    This is a great move❤❤❤❤