God bless this thinking, ineso wad like why keeping poor malawians in a bandage yangongole mmalo mokaika mankhwala mzipatara, kutsitsa katundu, kuwaonjezera aziphuzitsi ma salaries kuti aliyese azifikira zinthu mosavuta. Izi zikungoperekaso mwayi kwa mbava za m,bomazo kuti ziziba ndalama in the name of kupereka ngongole kwa amalawi mxiiiii
Anthu siyani kaduka.. mulungu simunthu.. Mulungu anaziwa kale kuti Usi azakhalapo vice president wa dziko la Malawi. Tivomereze chifunilo cha yehova pa dziko lathu la Malawi.
@@GregoryMatambo khalani ndi umunthu inu nde ubwino wakuba ndalama ndi uti? Mesa kumangophelatu dziko chithyola anamupeza nazo zana president nkumati musiyeni azipita what doesn't mean you're rubbish
Ndi ntchito yabwino kuti akuzipanga available to the public anthu apempha ngongole kuti upange boost capital chomwe ndi chabwino koma zimafunika kuti ayambile kukonza moyo wa ma customer amene ali anthu ogwila ntchito m'boma ndinso ma labour onse azipasidwa ma salaries omwe atazipanga match kukwera kwa mitengo ya zinthu omwe ndi ma buyer ama businesses amene akuvuta kupita pa tsogolo
Fundo ikuvuta pafunika azipita pa point first osati kudzifotokoza Za mmbuyo mwawo ....komanso kukamba Za chipani chawo or ofunika mulangizi adziwauza zokamba ku mtundu waanthu
Mfiti zopemphera Chakwera ndi mbale wake Usi ndipo anthu inuyo Mulungu akuyendelereni mwapadera ( SKC FOREVER IN OUR HEARTS 💔)
ayambe ayendera amayako
Amen
Powerful prayer,anazolowera sewero kwambiri
Inu agaru yehova wake uti,kupusa ziwanda yehova wamoyo sakhala ndimbava akuba akumpha, mulungu azakulangani osapota zopusa ukule garu iwe chairman
Don't judge anyone only god can judge
Awus mulibe nselu misimu yah andu 8 yinkukusatilani nkomaso awusseni amalawi ndege yinangwa bwanji osat samanyi munkunenaso mulungu ankuphasani matenda onyassa phamodsi ndi ashankwela mulungu anankuwonani 👌👌👌👌🙏
@@esaMoha-dm4kj inu mulungu????
@@esaMoha-dm4kj pelepa kuwecheta iseseni. Ambuje Mlungu akunde yakuti uchimbichimbi uyiche kwa mmwejo. Ajaliwe wakulungwa.
Mcp chipan chonunkha kwambiri 😢😢
@@BlessingsKatopola chonunkhila ndichiti???
Kupha
Kodi ngongole imasitha dziko poti mukufuna mwaonjezere anthu mamvuto musise katundu osati ngongole
Ndipo live atsitse katundu
Ngongole pa campaign aoneke abwino
God bless this thinking, ineso wad like why keeping poor malawians in a bandage yangongole mmalo mokaika mankhwala mzipatara, kutsitsa katundu, kuwaonjezera aziphuzitsi ma salaries kuti aliyese azifikira zinthu mosavuta. Izi zikungoperekaso mwayi kwa mbava za m,bomazo kuti ziziba ndalama in the name of kupereka ngongole kwa amalawi mxiiiii
@@JamesChiphwanya-m4v maona Ngati ndi thandidzo angobitsa Chichewa kodi NDI ngongore yangati ya fincca adzaole tidziwiya ,adzatenge timinda NDI tinyumba akalephera kubwedza
Zimayamba wez wez, sungapangile zinthu pakamodzi
Anthu siyani kaduka.. mulungu simunthu..
Mulungu anaziwa kale kuti Usi azakhalapo vice president wa dziko la Malawi. Tivomereze chifunilo cha yehova pa dziko lathu la Malawi.
Chifuniro cha mulungu kuti chilima aphedwe?
@@tingamasi106 eya
Mulungu okupha ameneyo siwakumwambayu ai
Sewelo leni leni tikufelanji apapa pangosowa mulelemba
😂😂
Eya pakusowatso make sikono ndi winiko
Dramatising politics .this guy is useless
Nde mwati ndinu a UTM? Muzivere chisoni bwana😢😢
Nde anthu mukuwona akakupasani ngongolezo mulemela mumene Zinthu zikudulilamu tsiku ndi tsiku ndalama ya ngongole siyingakupindulileni asise zinthu pandalama yanu yochepayo ikupindulilani 😢
Palibeletu Fundo apa koma A vp awa he's only proud kuti ndi vice president
Kape uyu
@@madakabichi2251kape umamudziwa koma 😂😂😂😂 mesa kape amakhala osauka ngat iweyo
Amalawi tichenjere😢 kwambiri. Timva zinthu.lets think and work together.Tiwunikilane. and love each other ❤
Mwamchitq bwino munthu wakupha ameneyo angampeleke chilima zoona
Midzimu yakwiya😂😂😂😂😂😂
Is that soccer player from chirimba?
We need a system that everyone fine support without being influenced by any political figure. Dr Usi reflect on this.
Ambuye akupaseni moyo wautali me utsi muzina loti musinthe malawi wathu
Ufumu unasata Daved kuubus chifukwa choti mulungu sakuva zaanthu
Akuwa patipo anthuwo yogulisira kut tionere imeneyo? Zopoila
Abale mundiuzireko a vp nzeru alibe chifukwa iwo amayenera asanayambe kulankhura kunkhalakaye cohete ose pasonkhanowo popereka ulemu kwa skc ndikunena zimu wawo uutse mtentere kenako kuwapepesa a malawi zaifa ya chilima kwinako mkumakamba mbwerera zakezo
Kod m'mene zinthu zilili pansikapa osamba zosisa mitengo ya zinthu bwa? Paja mwakwera muntengo apansife mulibe nafe ntchito
Bwana micle usi athu amakukondani kwambili!! Koma pa game yomwe mukusewela ndichakwelayi athu akutulukani chifukwa azindikila kuti inu muli under M.C.P mukanakhala kuti mukutengapo gawo muma program ama candle 🕯 komanso kuchita zomwe anthu ena a UTM akuchita mukanayenda moyela kwambili komanso zikuwoneka kuti mukufuna kuzutsa chipani chanu cho odya zake alibe mulandu!!! Ife tikanakuvotelani chifukwa cha chilima koma mwaluza basi!!! Pepani bwana usi!!!
Mbuzi iyi ya MCP. Usi usanamize anthu ndiwe wa MCP. Wavala za MCP osati UTM. Ukunamiza ndani nyani iwe. Pamtumbo pako Usiku.
Galu kwambiri ndipo akundinyansa kwambiri
Osaiwalatu ndimazimbabwe awaa@@ManganiStanley
Anthu owopa mulungu ngati abusa a chakwera
Mizimu ya anthu 13 yayamba kuonesa unya nawo ayise kufupika ngt mchimba
😂😂😂😂😂😂
Nde munayenda basi nkumawauza anthu zoti ndinkavala ma kabudula awiri ..zitithandiza chani ngt a Malawi
Uyudi ndi manganya srs ,masewero paliponse
Ngongole muyambe mwaona tikuyandikila mavoti 4 years munalikuti kuti muwapase ngongole mwabwera nthawi yochedwa inu mwapha chilima nde mukuona kumene ali chilima akusangalala muvutikapo apa panya panu ana anjoka inu
Ngongole ilibe nthawi , utha kutenga olo tsiku lovota
You can say this again, anthu tavutika all these years iwowa qnali pheee ,kumangokweza zinthu ndalama akusungira campaign? Rubbish
@@prettytambala5687 eti nde panopa akimalubwa zausilu aba ndalama za amalawi ena agwidwa nazo zana
@@GregoryMatambo khalani ndi umunthu inu nde ubwino wakuba ndalama ndi uti? Mesa kumangophelatu dziko chithyola anamupeza nazo zana president nkumati musiyeni azipita what doesn't mean you're rubbish
Osamatenga amphawi kuwaika pa udindo amangofuna kuba kt athane ndi umphawi wawo
Ine ndikufuna Dr usi ife tikufuna thandizo lawo ngongole atipase
Ndiye kukuwa mwalemba pa munthu wa nkhanipo akuwa pati reporter wa bodza iwe
😂😂😂😂 😂😂😂 always cadet amatero mix mizimu yama albino
The guy has a good heart
Which good heart ndi oipa uyu trust me
Mau onveka bwino avp anthu my God bless u, ndili pambuyo panopa maka pankhani yangongoleyo, odya zake alibe mulandu
Kodi Bwanausi ndi Bwanaisa mpachibale?
Blantyre inachulukadi mbuzi,am from by city koma delali ndi la nkhumba basi
Munachuluka amoya 😂😂😂😂
Powerful prayer 🙏
Usi Khala serious ukulongosola zithu zisamveka kutundu wa malawi
Ndiye amuwowoza patipo tikusikatu mboli yako
Fundo palibe bwana ingodyelanitu basssssss😂😂😂😂😂😂
*wayankhulapotu .. Koma ndege inagwa chifukwa chani bwana*??
Inuso ndinu a boza pena nanga akuwa pati apa chimutima cha nyawu icho
Mwayankhula bwana koma ndege inagwa bwanji boss 😂inuyo bwana ndinu opanda mnzelu mulungu akukantheni chisanathe chaka muyankha mulandu
Umayankhula bho heavy
@@JumaGadaff kafuseni mulungu kuti ndege inagwa bwanji chifukwa ndamene amadziwa chilichose
Ndipo akudziwapo kanthu uyu
Musamatichotse feel nanu......penapake muzingodula pofunikila pokhapo.
Ma Bandle akuvuta kale awa😢😢😢😢
Olo opepherayo akuona ngati akupanga sewero ndi manganya
Zaka 4 zimenezi zinalikuti ?
Zopepela zakozo osamantchula mulungu ukuwona ngati mulungu ndiwosewela naye
Amalawi chonde osayelekeza kuvotela izi
Ndani angavotere Manga? 😂😂😂
Musova
😅😅😅
Chirimba one love!!!!!🎉🎉🎉🎉❤❤❤❤🎉 mwana wapaden Manganya
Koma this man, alindinzeru kwabasi. Amandisutha kwabasi
Ndiye mwati chani😂😂😂😂 ine sindinatolepo mfundo atah olo pang'ono
❤❤
Ndi ntchito yabwino kuti akuzipanga available to the public anthu apempha ngongole kuti upange boost capital chomwe ndi chabwino koma zimafunika kuti ayambile kukonza moyo wa ma customer amene ali anthu ogwila ntchito m'boma ndinso ma labour onse azipasidwa ma salaries omwe atazipanga match kukwera kwa mitengo ya zinthu omwe ndi ma buyer ama businesses amene akuvuta kupita pa tsogolo
Seweloli kodi ndilapamajiga?
Musanayambe kukamba zasewerozo mutatiyankhako kaye funso likumatisowesa mtendereri, Kodi ndege inayenda bwanji ku chikangawa? Zangongole zanuzo ifeyo ayi, munali kuti ndi chakwera wanuyo? Nkhani ndikusisa katundu, zinazo mukakambirane ku state house
Chisilu iwe
@@AbdulhameedWyson tangopita ukalandire nawo ngongoleyo munthu iwe
Fundo pa line katundu anali azanu anja inu ndi achimulilenji sakusiyan
MP wachinyamata and chi player mbambande🤜🤜🤜, msikawo akonzedi eee
Ndiumenewotu u .vice president.munkaufunauja mpaka kupherapu nzanu chilima tiyeni nawoni mulibe ngakhale thenthi lomwe
Ndinaonela atapanga comedy as a president of the republic of Malawi lelo izo
Kodi Dr. Micheal Usi ndiu wa DPP kapena wa UTM///////////////// Nanga slogun ya woyeee ndi ya UTM
100 percent walankhula zondigwira ntima bale
Kkk
Zaziii
Zimayamba wez wez am sure manganya akonza zinthu, very soon katundu atsikaso
Iweyo Usi ukamalankhula kumatchula dzina la chakwela , panyapako kwambir
😂😂😂😂😂😂😂akutopetsadi bwanji ameneyu
Akuti kukhalatu ma Team ampira uku 😂 😂
A chairman wo akalamba😂😂😂
Palibe chanzelu ndamvapo apo ...manganya akupanga za chakwera mbuzi ya munthu
Am still feeling sorry for my country.
We seem to be a cursed nation.
Tikungoyang'anira 2025 mwina tizawona madakiso
Zamakabudula akowo anthu apindula nazo chani pomwe anthu akugona ndinjala. Dzuno pamenepo panali ena lelo ndiwe ndipo mawa ndi ena samala osatenga Malawi kusowa zochita.
Pamene ukulankhurapo nzimu wa achilima ukukantha ñdkuuuza, km Malawi ndinu anthu omvesa chison kwambiri kd mcp ndi chipan chochitsatira anthu akupha
Ndipo inu ngo'nazenizeni mcp
Iiiii ausi kuendatu kuposa malemu iiiii agwilizana zichani ndi chakwela aah Anthu-wa ndi amozi sure akuziwana
Nanga bwanji asilikari sadaseke maso popemphera bwanji
Bambo asikono ife sitikufuna ngongole ai, coz ngongole yo ndiye mavuto oooopsa Kwa ana anthu. Koma pangani zoti zinthu zisike pansinka kuti aliyese athe kufikira mtengo wakatundu osiyana siyana emwe mtengo wake wachita kuopsa ngati muja uchitila mkango
Akuluwa alindifundo dxopusa kobasi adximuudxa Chakwela dxoti mulungu simuthu amasithadi kom osati kwaife ndiwe galu kobasi
Tengani ndalamazo or musazabweze Ayi ndi misonkho anu atuzuza thawi yayitali tengani zaulere
Zaziiiiiii zopanda mntchele masewelo
It's so sad to see Malawian are still fooled by MCP.what a hell
Munthu ukamangitse okusakira mtchele
Zomwe akulimbana nazo athu awa zaziiii, noe mukuyenera kutsitsa zithu mtego komaso mudziwe kt kugwa kwandarama yathu yakwacha mukuyenera kuganiza kwambili mukapanda kutelo zithu zizativuta mpakana kale
Kujaila kungongola ndiye mulephere kubweza ndalamazo.
Dziko la malawi latha ili. Ma president ake ndi akuba onse.
Awaso nde ayi, athu akuvutika osamuuza za umphawi wanu muli ndalama osamatipusitsa
Ndikuon ngat Anthu anu okuthandiziran sadakuthandizen
Kungokhal ngat sewer sinthan okuthandiziranio
Powerful boss
Ngongole mumupatse munthu ogulitsa zitumbuwa mwati
Za ziii zeni zeni zopanda ndi Schererville womwe
Amalawi azanga Pena mukamalakhula muziganiza osamangokamba zithu zopanda umboni musiyeni usi ndi thawi Yake iyi yakwana
Ndiyeno gulu lose ilo nkumayimba / nkuyankha anthu 5 , manyanzi bwanji usi pamenepo.
Komanso ndi ana akuyakha usi
Aka manganya ngati adalephela mayeso awumphunzitsa nde lelo angatukule Malawi
Zasewerooo bas usiì
Ndrama yangongoleyo ipititseni Kuchimanga ndi feteleza kuti zitsike mtengo chooooooondeeeeee a VP
Malawi 🇲🇼 dziko lovetsa chisoni kwabasi 😢😢😢😢
Cheptsani mapemphero otamanda munthu mmalo motanda Mulungu mwini zonse wa kumwamba chonde imvani chimenechi
Tamangodyani ndalamazo bas,uku tikudikira report la kuchikangawa,koyenda ndege ma hours 3800, ngati imayenda wapansi
Ndipo inu
Mmalo moti asise zinthu ziko lonse aaa koma mr vc presdent mwaganiza bwanji poti ngongolezo ziziaonjezera mavuto mmalo mopita chisogole azibwedzanso zinthu mmene zakwereramo aaa
Pepani amalawi dziko ndiutsogoleliwathu ndi wa sewelo musiiletu kulakhula zopusa asogoleni mukuendela galimoto komanso mafuta ,zogulandi ndalama misokho a osauka manyazi mulibe mbuzi
Usi mu ma speech akewa mmmm chikondi chikupelewera bwenzi ali mu chisoni 🙏
Zamasiye ndizovuta muonekera ng'amba
Landirani ndalama zathu zimenezo. No need to pay back.
Ndangotaya nthawi yanga kumvesera zopusazo manganya munthu wankhaza uyu
Fundo ikuvuta pafunika azipita pa point first osati kudzifotokoza Za mmbuyo mwawo ....komanso kukamba Za chipani chawo or ofunika mulangizi adziwauza zokamba ku mtundu waanthu
Vmufiti lyi yinapeleka mzake
Nkhani ndiyoti osamacheza ndi Mulungu.
Anthu a ku Blantyre mulibe so nzeru mpaka mkumati woyela
Mudakakhala ena mukadamati tikutsika katundu amalawi akadamvako bwino koma zangongolezo ndikuwawonjezera umphawi
Ngongole sisitha zithu bwana ..mungowawonjezela mavuto
Kasiseni zithu kuma shop full stop
Aaaaaa zaziiii atikwanatu uyuu
Slogan imeneyi siya utm,ok asanditayitse nthawi.
Kodi muli pa campaign 😢😢 kodi
Ndipo ngongolezo 4 yrs ago zinali kut mungonena kut mukugawa ndalama zakapeni.
Mutsitse mitengo yakatundu osat ngongolezo .....kod ngongolezo atapindule ndangat ? .....pangan zot athu ovutika apindulenao osat zangongolezo