ZAULULIKA// Dan Lu waulura zinsinsi zina zomwe zikuchitika mu music industry ya ku Malawi.
Вставка
- Опубліковано 15 вер 2024
- Factory265 caught up with legendary artist Dan Lu to shed more light on what has prompted him to start thinking of quitting music.
😢😢😢Ehhhhh Sorry ajangu nambo basi ngayiw^enga mmwejo amdala basii, ngadandaula
Ndale ndizomwe zimakupha oyimbanu ma supporter a mcp sangakukondeni big siyani ndale ukhale oimba basi
A MCP ndye ndindaninso??
Kaya zako izo! Kaya zako izo, uziupezaaa uziupeza
MCP ndi ufiti weniweni komanso osaphunzira ndipo anapha Chilima
I love Dan's old songs koma zomwe akutimba pano zotukwanazi mmmm
p
Zangowavuta awa avomereze.... Time comes time goes
Dan Lu old song was very fantastic but now mmmmmh whow bad😢
Big artist, don't be discouraged
A Danlu vuto loyamba ndi kuyimba zotikwana mmmm kungova imene ija mmmm ayi.
Chachiwiri kuyimba za ndale zimapangitsa kuluza fans.
Nanuso ndale zake zit🤔
Mmm dan ifetu timakukondani mwalekelanj kuimba music 😔
Ndamuvesa sakufuna zausatana
Napman anadandauulapo nkhani imeneyi kuponderezana
Real fact
do like what aba'le do.makape asakudyere work with local DJs, youtube bloggers tidzivera ifeyo
Sanasiye but he is contemplating to : because the industry is now a non regulated mixed bag
Kumatchula mwachindunji Dan,,kagulu ka athu asataniki ndiwe odala bro,kuzindikira zakumidima ndikutheka anamupasa poison aja ndi asatanic .
WACHIYAWO WANGALUSA BRASA.MATIVESA KUKOMA
Ndakuvetsetsa mwana wakwathi
nyimbo zako azikavera. ndi APM ife ai
umachulutsa kutukwana nyimbo zanu brother inde pumani 😅😅😅😅 ine ndiye nyimbo zako phone Mwanga mulibe
Ati group of people not groups of people ,tazingoyankhulani chichewa abale
Zimavuta kumavomelezah koma wakuluwa zawabvuta ndithu avomeleze
Things are changing each and every day...Dan akanangokhala mu industry yake osati kuona za ena chifukwa sangasinthe zinthu zomwe oyimba apano akupanga
Sinyimbo zonse zomwe amatukwana
Mmesa wachiyawo wangalutsa Sono. Zikuti bwanji
Inu mumatha bro kuyimba osafooka ai
Awa alibe nzeru
Uwetu ayao uwetu wamanyi ❤❤❤
Muli ndi anger tu phiri. Inuyo osaimba mangelengelewo bwanj anthu akonde???? Umadzimva iwe
It is true broh akulemekeza chibwana
Ndi zoona big... Pano music mmm mwalowa zina
Anthu anakutuluka dan since unaimba nyimbo yotukwana ija ukuphunzitsa chani kwaachinyata manager wakoyo anatolia bwanji kuimba zopusazo
Dan Lu umatha anthu gerous basi
Musamapange comment ngati mukulankhulana ndi Dan Lu😂😂😂page yitu siya Dan Lu awa angopangapo post nkhaniyi
Amawerenga nawo so brh zimenez
Mumatha ndpo tlip ambr okhala kumbar yanu zandaleazitengele ku music aaaa sbwn😢😢
Pano zimene mkuyimba ana ama 2 pin ife ndi mbola kuli anatu kuno akiphulisa music
Ingobonani phiri mudziimbila mulungu basi
Dan lu , iwe shupi usafalitse kacholombo kako , nyimbo yokoma usasiye kuyimba
Anatha awa thawi yake inatha
Wati samafuna zopusa
Inuyo mumantha kuimba
vuto ndiwekha azikuvera APM
Oimba kungoyamba ndale anthu amaku tulula bas apapa amukonde dan lu ndi a DPP bas azipani enawa sangamukonde Dan Lu tsogolo loimba waliononga ekha ndiwe oimba wabwino nyimbo za ndizokoma km mawanga a DPP wobasi ndamene awononga zinthu sorry bro
Nkhani yavuta ndindalama😂 koma to be honest Dan Lu kalekale muja umaimba nyimbo za dzeru hvy
zavuta ku mpanje
Hmmm ndamumvetsa Dan, that's what happens in music industry, and nzapakanthawi. In other words, muli satana mu music,
Zomereza unatha basi vuto munalowa ndale ndizomwe zinakitsitsa aise
Aaa he's first one kupanga zandale??
Kuimba ngati kuli Mbali yake sangasiye Koma ngati isali Mbali yake Asiya komaso politics ndiyoipa amapha luso la oyimba chifukwa kuyimba umafunika uzosangalatsa anthu onse ndiye ukapita Ku politics zimavuta Kuti zitero chifukwa Mbali yomwe iwe Uli pankhani ya politics ndikomwe anthu amakusapota kwinako ayi so oyimba Aku Malawi musamalowe kwambili kumeneku luso limantha chinsazo ndi mkasa komaso tikapita kuzambia organise family nthawi ya edigar Lungu anatheratu chifukwa anali Mbali inayi panopa sindikunkhulupilia ngati anthu ambiliachipani cholamula angavere nyimbo Za Dan Lu
Akufuna angopuma awa
Mr lufani musatisiye musakwiye musa foke tihansizeni tima phuzila zambili kwainu
Sanachite bwino kugwa mphwayi ndi artist wankulu anakakhala azingokankha
Malawi
hhhhhhhh koma kumalawi anthu mukuvutika bwanji ife pheee achina DKY olo kudyera mnkhwani
Dan ife timakunyadila kuyambila kale
Kuzolower kupondelezana bc malawi🤪🤪🤪🤪
mmmmm
Siyani mwalimbana nako kulimbana wabwino 😅😅
Vuto kutukwana kwako mnyimbo so athu anakutuluka
Anyama ambili amene zikuwayendera bwino pano Kuti muone samalowa Dale bwinaso amene abwera pa mbuyo pake komaso pankhani ya nyimbo omvera ndiamene amanena Kuti ndiyabwino osati oyiyimba ndiye anthu akusankha kumvera zimene mukuziwona ngati akumangokuwazo komaso chinthu China Malawi samafuna munthu oyankhula kwambili
Siya kuyimba zandale iwe pamtumbo pako
Game yathinatu....😅
Zabwino zonse brother musiyedi kuyimba mwapanga chisankho chabwino
Komaso Ku Malawi tili ndi vuto poyamba munthu zinthu zikamamuyendera timkati ndiwonkhwima pano tasintha tikuti satanic ok!!! Zikatero one ndimangokumbukila nyimbo ya fuko ya Malawi Kuti amene anayimba nyimbo imeneyi anaziwona ndipo anapangadi kafukufuku kumuziwa bwino mmalawi mmalawi samafuna kumuwona mzake zikumuyendera ayi, chikwa chakuti nthawi zambili sitimaziwa anthu Anja Kuti adutsa motani mwachinsazo sent nthawi Ina anali ndi interview amafotokoza mmene anayambila ena sangankhulupire Koma ine ndinankhulupila chifukwa ndimkamuwona zikuchita so let's put satanic pambali enawa adutsa mwambili ndipo akumana ndizambili Kuti afike pamenepo
olo wa satanic pano ali mmaluzii😅😅
Ndiye ukhale kutali ndi Mulungu uzikhalaso mmaluzi aaaaa hell is waiting as well
Dan luuuu akunena zoona anyamata ambiri ayamba satanic anthu ambiri sakuchuka pa okha
Awopa mcp kumupha
Amupha bwanji iyeyo popeza ndiwasatanic