Atanyiwa ndinali pa Malo ena ake dela lomwe ndimakhala koma koma seriously anthu akumvela Limpopo ndimangomva nyimbo ya Limpopo ija program ikamayamba, wooozaaaa chikangawa ndinu number 1🎉🎉
Eish!, mtima wanga unagunda nditayamba kuwelenga title ya lero ya nkhanga zawona ndipo nditafika poti " NTANYIWA WAPHEDULA ", ndimawona ngati akuti NTANYIWA WAPHEDWA, eish!, nditawelenganso ndapeza kuti pali mawu oti NTANYIWA WAPHEDULA😂😂, may ALLAH guide and protect all the freedom fighters in Malawi Ameen 🤲🤲🤲
Umakwana ine zayatsa wanga Candle wakuda ndi yellow kumaliza kupempherako aziwe Kuti chawera ndi ntembo peter Thomas port Erazabeth we sick & tired because of him chakwera
Kain kain iwe amalawi awuzeni komwe munamubisa chilima Limpopo FM ndi imeneyi ndimaziwa ine with comrade ntanyiwa kp it up Mr God bless wherever you are. Koma iwe I Kain mwazi wa chilima ukukanthe uziona Chaka chake nchino
Akadulitsa kandulo tiyatsa nyani using paraffin akakwezanso tizikadzula udzu kutchire kumayasa till the truth come out and face consequences kaini gwenembe🙄
Kodi chakwera unasiya kuyenda kunja pomakatha 4years kuchoka Lero pa July 15 ndidzakhala ndi takupedza man iwe udzisaka enao ine (I'm looking for u 😢😢😢
What profit if, some one kill some body, the results is chilango Chifukwa chilango Chima yambira pansi pomwe pano, Chakwera amaganiza zoti wabisala Osaziwa Kuti pa maso pa Yehova palibe chinsinsi, Yudas ada zipha yekha Chakwera azipha Chifukwa choipa chisata mwini,wa Chipani chaMcp ayembe keze kuona mazanga zime
Atanyiwa ndinali pa Malo ena ake dela lomwe ndimakhala koma koma seriously anthu akumvela Limpopo ndimangomva nyimbo ya Limpopo ija program ikamayamba, wooozaaaa chikangawa ndinu number 1🎉🎉
Mkuluyu amatha (Mtanyiwa) ❤❤❤❤.
Zoona,zoona mr chikangawa ndi satana mumakwana ampingo ife tikufuna yesu ❤ it
Salute comrade Ntanyiwa mwambo wa ma candle sitisiya mo fire mpaka chakwera atanyeledwa
Number one Radio station
Mumakwana comrade❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Conglatulations🎉🎉🎉🎉🎉
Powerful message from comrades Ntanyiwa❤❤❤
Power Limpopo 🙌🙌🙌
😢😢😢 achakwera muona dzosaona ndi mwazi munathila
Akonzekere next year kumangdwa chakwera . Galu okupha
Km akuluakulu ndikupempha nyimboyi amene alinayo chonde tigaileni
Wonderful
Mukundifika mumtima
Bwanji❤I ❤u❤😂😂
😂😂😂😂Inenso bro 😂😂
Eish!, mtima wanga unagunda nditayamba kuwelenga title ya lero ya nkhanga zawona ndipo nditafika poti " NTANYIWA WAPHEDULA ", ndimawona ngati akuti NTANYIWA WAPHEDWA, eish!, nditawelenganso ndapeza kuti pali mawu oti NTANYIWA WAPHEDULA😂😂, may ALLAH guide and protect all the freedom fighters in Malawi Ameen 🤲🤲🤲
Ineso nnawerenga choncho iiiii
Welcome back Limpopo fm. We listen your channel everyday from Mozambique.
Osaopa mulungu wa abraham, Davite,yakobo,yosef,shadrec, misheki ndi abitinego awatetezera azitsogoleri amenewa.mwachitsanzo kuti mudziwe kuti mulungu alinafe chiwembu chilichose chimene akupanga mulungu akuchiika poyera tiyeni tipephere mokweza mulungu alinafe
Limpopo number 1 sirens
Ntanyiwa umanivetsa kukoma ndipo nimakonda for ever❤
🤣🤣Zafika pokuti antha kumukhwimira sikono sopano 😂😂😂
Yomweyoo azibambo mwaimba bwino kwambiri! Salute Comlade
Eeeeee mpaka kwa nsing'anga😂😂😂
Makandulo ayake bas akumva kutentha thupi mwake satana 😂😂😂
Kkkkkk kumalawi kulibe kupuma,satana chokere yemweyoooo
🎉🎉kod Abale tizangolusa ndikuwathamangitsa obwelawa
Umakwana ine zayatsa wanga Candle wakuda ndi yellow kumaliza kupempherako aziwe
Kuti chawera ndi ntembo peter Thomas port Erazabeth we sick & tired because of him chakwera
More fire Ntanyiwa. Kodi ayamba kale kikhwima hetii
Kain kain iwe amalawi awuzeni komwe munamubisa chilima
Limpopo FM ndi imeneyi ndimaziwa ine with comrade ntanyiwa kp it up Mr God bless wherever you are.
Koma iwe I
Kain mwazi wa chilima ukukanthe uziona Chaka chake nchino
More fire Ntanyiwa❤❤❤❤❤
Inu ndi mtunda akatundu oyankhula Chilungamo chokha chokha Limpopo FM ndi Ntanyiwa 🔥🔥♥️
Mukamva ndafa mmudzimu, Chakwera wandipha. Uyu ndiye andipha
Kkkkkkkk simufa mu mdzina la Yesu khristu.
Ndipo ndikuweruka ❤❤
Zoona ma candle aziyatsidwa masana tizitha kumaona chikubwela mfundo yabwino.
Osamasowa Mtanyuwa ❤ u masiku akupitatu awa hot hot tsopano
Koma mukazawombela Atupele ziwani kuti tsiku lomwelo muzasamuka ku state house kukhala ku Chile ndinena ndi inu
Zikavuta toyasa khuni 😂😂😂😂aonaso
Koma ntanyiwa umanivetsa kukoma ❤😂😂😂😂😂
Mavuto kuwaputadala Anthony osalakwa vuto nimagazi adawalowelela alandila zolowazawo mulungu adaona zone amen
Nkhani ndi kaini chilima alikuti iwe😭😭😭🔥🔥🔥
Welcome bwana, following.
AYEREKEZE KUOMBERA ALIYENSE MWA ASOGOLERI AMENEWA TIKAGUMULAPO STATE HOUSE TRY IT SITIKUOPA AYI🎉🎉🎉🎉
🤩🤝🤩
Manganya wauyasa ulendo ndi Richard chilundi Banda wakwasing'anga kkkkk
Waimba ndani tipange download...ndaikonda
Following from Armageddon
Mukapha ena, muphenso tonse, mutsalepo nokha pano. 😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭😭👀👀👀👀👀👀😎😎😎😎😎😎
Yes
Mthanyiwa more fire
Nthnyiwa iweyo mulungu akupatse moyo wautali aboma ndi zisilu
kma Limpopo ndayikonda
Moore fireeee😊
Akadulitsa kandulo tiyatsa nyani using paraffin akakwezanso tizikadzula udzu kutchire kumayasa till the truth come out and face consequences kaini gwenembe🙄
Mwaswela bwaji anthanyiwa
Kumupasa moni mnthu wankulu kp it up kkkk😊😊
Ndipo ndiyatsadi masana ma candle
Chakwela unya manyi 2025 nyau party out forever
Nyimboi Antanyiwa tikuifuna zedi tipatsen link
Kodi chakwera unasiya kuyenda kunja pomakatha 4years kuchoka Lero pa July 15 ndidzakhala ndi takupedza man iwe udzisaka enao ine (I'm looking for u 😢😢😢
Kodi mwati amakatani kwenikweni ku lingadziko apulezidentiwo komatu akumana nazo ulaliki opposite nyimbo opposite madzimadzitu
Kkkkkkkk comrade umakwana
Koma nyimboyi sidayimbidwe ku Lingadzi ndiyachigwirizano chabambo
Mtanyiwa akumva nae kuwawa
😂😂😂 chakwera ndi opusa size
Nyimboyo osazayiwara pa kampeni ikubwera Mutu wake Kain Kain kapena iwe chifunga
Ntanyuwa mulungu adzikusunga ndi kukuteteza chifukwa zambili popanda iweyo zikanachitika..koma chilungamo cha nkhaniyi ya kuchikangawa chidzadziwika boma likasintha
😂😂😂😂😂😂😂😂 mwazi wa munthu simasewela ayi sanati
Ndipo mcp yalozedwa ndinthu
Ife tikupeohereea Malawi wathu..
Yomweyo mtanyiwa
Visambwazeni viwanthu vakupha ivi
Abwana masiku 4 osafika mmmm koma takunyadilan
❤❤❤❤
🤣🤣🤣🤣🤣 tiziyatsadi masana ma kandulowo
Nice song 👍💪💪🇲🇼
😂😂😂😂😂😂😂😂 abhiyeni munawaphelanji
Akhawura chakwera 2025 kupha athu asarakwa ineso pomwepa pazambia ndikuyatsa makendo😢😢😢😂😂😂😂❤❤❤ ndimakuva tanyiwa
Mmm koma mtanyiwa
Koma sanathe apitanso kwa yaya sanathe
😂😂😂😂 zafika pomapita Kwa asimg'angaso? 😂😂😂 A vice president 😂😂
Malawians must work up Malawi is not is not a company of Chakwela
wina apenga misala kkkkk
Real nkhanga zaona
zowooona kumayatsadi masana ambuye ali kumbali yanthu llv limpompo
Aaaa nzeru palibe man,koma ku DRC akayiwerenga kkkkk
Powerful 💪💪💪
Next year yatalika alamula bwanji ma percentage atatsika achoke pompano
Ntanyiwa woyeeeee🎉
Tidikila inu antanyiwa azayasidwe basi
Pafupi ndi mount view lomwe ndimaphunzira kkkkk Kwa agogo Ake athoko😂😂😂😂 Kwa gulumba
Komaaaaa
Mpaka kwa ng'anga
Makwana matimilira
Osatiyiwala ku Durban kuno tilipo ambiri. Tisayaze makandulo 😊
Ntanyiwa sangamupeze ndipo tilimbali yake Ntanyiwa bwerani muzasake muzionela nokha kmwe kuno kut aphedwe ndani tikudikila inuyo kuno
What profit if, some one kill some body, the results is chilango Chifukwa chilango Chima yambira pansi pomwe pano, Chakwera amaganiza zoti wabisala Osaziwa Kuti pa maso pa Yehova palibe chinsinsi, Yudas ada zipha yekha Chakwera azipha Chifukwa choipa chisata mwini,wa Chipani chaMcp ayembe keze kuona mazanga zime
Ndiye mukuti bambo asikono anali kokhwima yoooooo!!!!????
Amutanyiwa makenduro tiyasedi kuno koma nafeso kuno tikufuna ti voter nawoooooooooo🎉🎉🎉
MDF ,ngati ndizoona kut mdzko muno muli zigawenga methane nazo
Udindo wamasiye omwewo mpaka kunkhwimila koma akuyendadi ndi nzimu wa ma drama basi
Eyadi makandulowa muziyatsadi masana kuti oipawa adzioneka .kuli koyera..zoonadi Antanyiwa
Nae mosesi kunkuyu kungosiya kuonesa video show kwamanase anvekere mcp yomweo,!!! Wanya
Nyimbo imeneyi title yake ndi chani
Wachikulire timakunyadirani
Koma yah ntanyiwa umatha
More fire ntanyiwa mumatiyimilira ngakhale ena amaona ngt mukunama
Asilikani changa ukani chonde, candle boladi masana