Prophetic Advice to Professor MUTHARIKA of DPP in Malawi

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 30 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 36

  • @OdgessMedson
    @OdgessMedson 3 дні тому

    Please the man of God teach people about Jesus not politics please please.

  • @charlesnankumba9991
    @charlesnankumba9991 Місяць тому

    Do not despise prophecies, but test everything; hold fast what is good.( 1 Thessalonians 5 v 20 -21 ).

  • @Felixbanda-q6p
    @Felixbanda-q6p 4 дні тому

    iweyo mboliyako iweyo siwe opephela

  • @sylessmaduka466
    @sylessmaduka466 2 місяці тому

    Munapereka chitsanzo cha Sauli ndi David. Nde munazatinso 2019 Peter atawina inu munkauzabe anthu kuti Chakwera ndi amene anawina mpakana 2020 zinaonekadi poti Mulungu mau ake sapita pachabe. Now tikaona za David sanakakamize ayi, sankamemeza anthu kuchita chipolowe mpakana nkutenga ufumu, ndi Sauli amene ankalimbana ndi David koma David sankabwenzera pomwe zinazi ndibwino musafananize chifukwa zinali zokakamiza. Komanso Mulungu kunena zoona mene zinthu zikuchitikira ku Malawi kuno olo munthu oti sawerenga mau a Mulungu sangavomereze kuti Mulungu anatisankhira mtsogoleri. Kodi zikuchitika ku Malawi kuno ndi mdalitso kapena thembelero? Izizi kupanda kusamala mayiko ena atengera chitsanzo pa Malawi kuti Mulungu siomuseweretsa.

  • @ericchilinjala481
    @ericchilinjala481 3 місяці тому

    We need to know that mulungu akamayankhula ndiye kuti akutikonda.
    Olo mu bible atsogoleri amalangizidwa ndi ma prophet.izi sizachilendo..komanso ma prophet omwe ayitanidwa kulakira the pure gospel of God alipo..uyu calling yake is to give counsell to the goverment. Zinthuzi zimafunika kuzimvetsa..Liabunya sakunama.

  • @GodfreyjcBinguh
    @GodfreyjcBinguh 2 місяці тому

    Chitsiru Ichi sadziwa pano Kuti mulungu akulilira Moyo wakoyo fiti iwe .do you knew Kuti nthawi yatha pompano okudzayo akudza.mulungu akusithe chifukwa yemwe ndimudziwa akuva chisoni ndi dziko

  • @witneymunthali8371
    @witneymunthali8371 2 місяці тому

    Timusiye Mulungu mwini Mphamvu asnkhe yekha msogoleri Kwa ife ndikuponda Bondo.

  • @Felixbanda-q6p
    @Felixbanda-q6p 4 дні тому

    akafuteso seda yakoyo

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 8 місяців тому

    Ubwino wake opemphelanu takuonani zochita zanu nde sitingamvela zakozo..iwe si Mulungu.. Auze anthu za ufumu wa Mulungu ..lalikilani kut anthu tilape pliz..mukupangazi ndi gospel ya ntundu wina..kukuyang'ana mmaso mwakomo I 've lead your mind..

  • @GiftGift-d6u
    @GiftGift-d6u 8 місяців тому

    Wabodza iwe,, busy wit politics rather than kulalikila uthenga wabwino,, busy kuchita predict zoipa za moyo Wa wina

  • @BFWCPHIRI1978
    @BFWCPHIRI1978 8 місяців тому

    Ukayang'anatu ndi diso la uzimu zimu koma uli mwana wa njoka,,,,,,,,,alosi onyenga inu mmodzi wa Satanism iwe mmmmmmmmmmmmm ngati mwadya ndalama za uyo mukumuti ndi ofatsayo nonse ana anjoka,,,,,,,,,,,,,,,ofatsa wake tsiluyo!

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 місяці тому

    Kkkkk misatisrketse aku broker ndani aprophet😊

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 місяці тому

    Munali so kwa chakwera pompano aprophet

  • @alexgweje8610
    @alexgweje8610 8 місяців тому +1

    Opemphera amasiku ano Mmmmm mwataya njira ya Yesu khristu mukulimbana Ndi ndale xa

    • @frezarphiri3480
      @frezarphiri3480 8 місяців тому

      😂😂😂 mwayiwala anthu awa kunthamangira ndalama basi wayiwala kalekale za Yesu . uyu

  • @BridgetZingani-gb8yf
    @BridgetZingani-gb8yf 8 місяців тому +1

    Lalikani za uthenga wabwino wa Yesu inu osati za ndale

  • @mabletungande349
    @mabletungande349 7 місяців тому

    He might be telli
    ng the truth

  • @GamaChifundo
    @GamaChifundo 2 місяці тому

    Ok malawi amakhulupila utaona

  • @Owen-n1v
    @Owen-n1v 8 місяців тому +1

    Auzeni anthu za Yesu. Is this the new gospel?

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 2 місяці тому

    Apm yomweyo

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 3 місяці тому

    🤣🤣🙌

  • @AbdulChemkwanda
    @AbdulChemkwanda 8 місяців тому

    Mtima wanjiru, munthu wa Mulungu mabodza,mwana wa satana iwe, a professor timakonda ndife, pita ukalalikire anthu akumidima

  • @MavutoChekeni
    @MavutoChekeni 8 місяців тому

    Ndizowona munthu si pitalayekhayu anzake achitepo

  • @NevesonChirwa-tt5eg
    @NevesonChirwa-tt5eg 8 місяців тому

    Iwe prophet iwe ndiwe wa chamba kwambiri wamva?osangojoina ndale bwanji?Anzako a Mbewe adayambaso choncho koma pano si awo anayambitsa chipani.

  • @MisheckChapomba-lr8kz
    @MisheckChapomba-lr8kz 8 місяців тому

    Akunenazo ndi zoona Koma osati zachokela Kwa Mulungu ayi God has nothing to do with this satanic parties

  • @samsonhavenoyayshonga2609
    @samsonhavenoyayshonga2609 8 місяців тому

    What he saying is not from God,he trie to be a politician

  • @MuhammadSamson-yz1kl
    @MuhammadSamson-yz1kl 8 місяців тому

    Kkkkkkkk forsake kagwere uko iwe wasuta chamba

  • @johnkumbanga3369
    @johnkumbanga3369 8 місяців тому

    What are you trying to say mr prophet?

  • @YoungMwacho
    @YoungMwacho 8 місяців тому

    Fake

  • @YoungScott-p7e
    @YoungScott-p7e 8 місяців тому

    Akunama uyu

  • @eliasMwamba-q5f
    @eliasMwamba-q5f 8 місяців тому +1

    Just start politics Mr prophet than Malo mumatiuza mawu a mulungu.

  • @ClarencePophiwa
    @ClarencePophiwa 8 місяців тому

    Zachikunja izi auzeni anthu za yesu.