Munapereka chitsanzo cha Sauli ndi David. Nde munazatinso 2019 Peter atawina inu munkauzabe anthu kuti Chakwera ndi amene anawina mpakana 2020 zinaonekadi poti Mulungu mau ake sapita pachabe. Now tikaona za David sanakakamize ayi, sankamemeza anthu kuchita chipolowe mpakana nkutenga ufumu, ndi Sauli amene ankalimbana ndi David koma David sankabwenzera pomwe zinazi ndibwino musafananize chifukwa zinali zokakamiza. Komanso Mulungu kunena zoona mene zinthu zikuchitikira ku Malawi kuno olo munthu oti sawerenga mau a Mulungu sangavomereze kuti Mulungu anatisankhira mtsogoleri. Kodi zikuchitika ku Malawi kuno ndi mdalitso kapena thembelero? Izizi kupanda kusamala mayiko ena atengera chitsanzo pa Malawi kuti Mulungu siomuseweretsa.
We need to know that mulungu akamayankhula ndiye kuti akutikonda. Olo mu bible atsogoleri amalangizidwa ndi ma prophet.izi sizachilendo..komanso ma prophet omwe ayitanidwa kulakira the pure gospel of God alipo..uyu calling yake is to give counsell to the goverment. Zinthuzi zimafunika kuzimvetsa..Liabunya sakunama.
Ubwino wake opemphelanu takuonani zochita zanu nde sitingamvela zakozo..iwe si Mulungu.. Auze anthu za ufumu wa Mulungu ..lalikilani kut anthu tilape pliz..mukupangazi ndi gospel ya ntundu wina..kukuyang'ana mmaso mwakomo I 've lead your mind..
Ukayang'anatu ndi diso la uzimu zimu koma uli mwana wa njoka,,,,,,,,,alosi onyenga inu mmodzi wa Satanism iwe mmmmmmmmmmmmm ngati mwadya ndalama za uyo mukumuti ndi ofatsayo nonse ana anjoka,,,,,,,,,,,,,,,ofatsa wake tsiluyo!
Please the man of God teach people about Jesus not politics please please.
Do not despise prophecies, but test everything; hold fast what is good.( 1 Thessalonians 5 v 20 -21 ).
iweyo mboliyako iweyo siwe opephela
Munapereka chitsanzo cha Sauli ndi David. Nde munazatinso 2019 Peter atawina inu munkauzabe anthu kuti Chakwera ndi amene anawina mpakana 2020 zinaonekadi poti Mulungu mau ake sapita pachabe. Now tikaona za David sanakakamize ayi, sankamemeza anthu kuchita chipolowe mpakana nkutenga ufumu, ndi Sauli amene ankalimbana ndi David koma David sankabwenzera pomwe zinazi ndibwino musafananize chifukwa zinali zokakamiza. Komanso Mulungu kunena zoona mene zinthu zikuchitikira ku Malawi kuno olo munthu oti sawerenga mau a Mulungu sangavomereze kuti Mulungu anatisankhira mtsogoleri. Kodi zikuchitika ku Malawi kuno ndi mdalitso kapena thembelero? Izizi kupanda kusamala mayiko ena atengera chitsanzo pa Malawi kuti Mulungu siomuseweretsa.
We need to know that mulungu akamayankhula ndiye kuti akutikonda.
Olo mu bible atsogoleri amalangizidwa ndi ma prophet.izi sizachilendo..komanso ma prophet omwe ayitanidwa kulakira the pure gospel of God alipo..uyu calling yake is to give counsell to the goverment. Zinthuzi zimafunika kuzimvetsa..Liabunya sakunama.
Chitsiru Ichi sadziwa pano Kuti mulungu akulilira Moyo wakoyo fiti iwe .do you knew Kuti nthawi yatha pompano okudzayo akudza.mulungu akusithe chifukwa yemwe ndimudziwa akuva chisoni ndi dziko
Timusiye Mulungu mwini Mphamvu asnkhe yekha msogoleri Kwa ife ndikuponda Bondo.
akafuteso seda yakoyo
Ubwino wake opemphelanu takuonani zochita zanu nde sitingamvela zakozo..iwe si Mulungu.. Auze anthu za ufumu wa Mulungu ..lalikilani kut anthu tilape pliz..mukupangazi ndi gospel ya ntundu wina..kukuyang'ana mmaso mwakomo I 've lead your mind..
Wabodza iwe,, busy wit politics rather than kulalikila uthenga wabwino,, busy kuchita predict zoipa za moyo Wa wina
Ukayang'anatu ndi diso la uzimu zimu koma uli mwana wa njoka,,,,,,,,,alosi onyenga inu mmodzi wa Satanism iwe mmmmmmmmmmmmm ngati mwadya ndalama za uyo mukumuti ndi ofatsayo nonse ana anjoka,,,,,,,,,,,,,,,ofatsa wake tsiluyo!
Kkkkk misatisrketse aku broker ndani aprophet😊
Munali so kwa chakwera pompano aprophet
Opemphera amasiku ano Mmmmm mwataya njira ya Yesu khristu mukulimbana Ndi ndale xa
😂😂😂 mwayiwala anthu awa kunthamangira ndalama basi wayiwala kalekale za Yesu . uyu
Lalikani za uthenga wabwino wa Yesu inu osati za ndale
He might be telli
ng the truth
Ok malawi amakhulupila utaona
Auzeni anthu za Yesu. Is this the new gospel?
Apm yomweyo
🤣🤣🙌
Mtima wanjiru, munthu wa Mulungu mabodza,mwana wa satana iwe, a professor timakonda ndife, pita ukalalikire anthu akumidima
Ndizowona munthu si pitalayekhayu anzake achitepo
Iwe prophet iwe ndiwe wa chamba kwambiri wamva?osangojoina ndale bwanji?Anzako a Mbewe adayambaso choncho koma pano si awo anayambitsa chipani.
Akunenazo ndi zoona Koma osati zachokela Kwa Mulungu ayi God has nothing to do with this satanic parties
What he saying is not from God,he trie to be a politician
Kkkkkkkk forsake kagwere uko iwe wasuta chamba
What are you trying to say mr prophet?
Fake
Akunama uyu
Just start politics Mr prophet than Malo mumatiuza mawu a mulungu.
Man of God stimuli kumalawi eti anthu akuvutika kuno
Zachikunja izi auzeni anthu za yesu.