CHIHANA NDI NANKHUMWA AVUTA UKU |

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 21 чер 2024

КОМЕНТАРІ • 126

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 17 днів тому +7

    Nduona ngati akuopaa kkk ufulu weni weni tilibe kweni kweni

  • @MzikaPhiri
    @MzikaPhiri 16 днів тому +4

    Big up Mr Chihana though sinamveere zomwe mwayankhula ndangowona anthu akuyamikira

  • @JIMMYWATHONJE
    @JIMMYWATHONJE 17 днів тому +3

    Straight to the point Mr Chihana

  • @Edson-sj8vn
    @Edson-sj8vn 17 днів тому +11

    Mawa lisathe kalindo amasulidwe chakwera &usi tionana 2025

  • @user-un6qv6sj3h
    @user-un6qv6sj3h 17 днів тому +4

    Dzaka 60 really 😢😢😢 Malawi udzakula liti 60 years still kuvala pampaz shame on you kunkuyu

  • @JohnsonRannel18
    @JohnsonRannel18 17 днів тому +10

    Ufulu wake ndiye wutiwo mungomanga adzanu ndi kuphaso azanu

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf 17 днів тому +2

    Memories will remain fresh even after 100 years. Let's remember them in a special way and continuously pray for their Souls to rest in eternal peace.

  • @user-jd9yz5hp7y
    @user-jd9yz5hp7y 17 днів тому +3

    Anthu amenewo ofufuzawo pls Mr Chihana muwonetsetse kuti asachokele ku Butchery kumene amatinamiza kuja kuti akagura Feteleza anthu akuba awa ndi kupha oyipa a MCP

  • @user-nf3ik3ff6y
    @user-nf3ik3ff6y 17 днів тому +3

    Good Mr Chihana

  • @BillyKalambo-jx3vf
    @BillyKalambo-jx3vf 15 днів тому

    Nkukuyu ungotaya nthawi kulankhula zopusazo asakuziwa kuti Chakwera ndi nsogoleri ndani sangalalani ndi gulu lanulo LA uchigawenga mcp 😭😭😭😭😭🐊🐊🐊🐊

  • @ChristinaLigomeka
    @ChristinaLigomeka 17 днів тому +5

    Amene adzapite ku mapephero amenewo mutu wake suyenda bwino mwalo mopangitsa mapephero olapa mudzikapephera chani Mulungu akamva zimenezo magazi akuyenda Malawi mo simukuwawona, mwazi wa anthu osalakwa ukufuulawo simukuoona mapephero achani mudziwerenga bible before kuchita zithu za ziiii mudzikapha Ana azanu ngati khuku mtendere simudzaupeza mpaka mutabwera poyera kulula

  • @PaulMwachande
    @PaulMwachande 17 днів тому +3

    Nankhumwa wayamba kulankhula chifukwa sanamusankhe kukhala vp

  • @user-zi8pj5ey4t
    @user-zi8pj5ey4t 17 днів тому +3

    A kunkuyu mzimu wa witika muli nao pamutupo

  • @ulemujumbe8501
    @ulemujumbe8501 16 днів тому

    Bring back Bon Kalindo

  • @EdwardMukholi
    @EdwardMukholi 16 днів тому

    Nanga anthu amene mukuwamangao mukutathauza kuti mukulira bodza bwanji Mr president

  • @OmarManjawira-up3ns
    @OmarManjawira-up3ns 17 днів тому +1

    Chihana well spoken,

  • @GRACIOUSKENAN
    @GRACIOUSKENAN 17 днів тому +6

    Boon kalindo ndikumufuna osat inuo,chokan apaaaa

  • @user-kr4wb2th9i
    @user-kr4wb2th9i 16 днів тому +1

    Anawo akhala osabereka

  • @hanifahmponda8711
    @hanifahmponda8711 16 днів тому

    Aaa atenga anthu osadziwika cholinga choti adzattwudze mabodza ANTHU AKADZAMANENA KUTI CHILUNGAMO ACHIBUTSA ADZIMANGIDWA NDE MCP IMENEYO NDEGE YOTI DZIPANGIDZO DZINA ANACHOTSA MO MA PHONE KUTENGA KUMAFUFUDZA POKAPELEKA MA FON AFUTAMU CHILICHOTSE AAAAA amalawi mufunilanji omboni wina apa zawoka dzokha kuti chiwembu chokodza MR CHIHANA THANKS U SO MUCH KOMA A MCP AKATULUTSA BODZA LAWOLO ngati inu mudzayankhule potsusana a MCP mudzayembekedzele kumangidwa CHIFUKWA PANO DZIKO LA MALAWI LAFIKA ULAMULILO WACHIPANI CHIMODZI CHAKAKA NYALENDA NDADZANU ENA MUNATILAKWILA AMALAWI MUDZIWE DZIMENEDZO

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 16 днів тому +1

    Iwowa mituyao sigwira kunkuyu ndi chakwera wakoyo ndinu mbuzi mukati ufulu odziramulira what do you mean? Momwe mukuyendetsera boma lero mukuona ngati dziko liri pa ufulu popeza muli busy kupha anthu komaso kumanga anthu omwe akukudzudzulani ndiye nkumati dziko liri pa ufulu inu agalu kwabasi zigawenga

  • @user-hp4rl8cv3h
    @user-hp4rl8cv3h 16 днів тому +1

    Chihana very good

  • @EdwardMathuwa
    @EdwardMathuwa 16 днів тому

    Dzaka 60 za democracy minus 4 ya chakwela tikusangala dzaka 56 coz dzaka 4 za chakwela kulibe ufulu

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 17 днів тому +4

    Akuna adzakondwerere kuti zomwe.amafuna zatheka pokupha chilima

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 17 днів тому +1

    Agalu mumuziwaso Mulungu

  • @robertnambazo9936
    @robertnambazo9936 16 днів тому +1

    Akuziwa kuti anthu sazapitako awatuluka anthu awa

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 17 днів тому +1

    Ukuona ngati anthu akukukhululukini mwanya akupha

  • @viennasamuel2976
    @viennasamuel2976 16 днів тому +1

    Mwamasukatu mpaka zikhulupiliro zosakhala bwino? Globe vaccine akukupatsani thandizowo ndi ayesu? OK.

  • @user-lr5bz7qk2d
    @user-lr5bz7qk2d 17 днів тому +1

    Agalu kumkuyu mapwala ako

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 17 днів тому +1

    Muchoseko zaka 4 zomwe mwalamulilaz kulibe ufulu ndiye kt tili ndi zaka 56 xaufulu

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 15 днів тому

    Musatinyasepo apa ufulu womwe mukunena ndiye wuti Malawi wake wuti womwe Muli wufulu za ziiiii

  • @GiftManuel-er7yh
    @GiftManuel-er7yh 17 днів тому +1

    Amaio akunama mwana sangabadwe kutha miyedzi 6 asanamupitenao ku chipatala ku scale

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 17 днів тому +1

    Mbudzi iwe

  • @storytambala6088
    @storytambala6088 16 днів тому

    Hmm iwe Kunkuyu, ndi Chakwera musatiputsitse apa.

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo 16 днів тому +1

    Kodi ufulu ulikuti, ku malawi kulibe ufulu chifukwa achina kamulepo ndi kalindo mudawamanga chifukwa chomenyera ufuluo, komatu Boma ili litipweteka ndithu

  • @victorauwana7258
    @victorauwana7258 16 днів тому

    Ziko la Malawi lakwanisa zaka 60 pokweza pasogolo umphawi wathu

  • @HeedsonJere
    @HeedsonJere 16 днів тому +1

    Chihana anamumana udindo ku tonse allias

  • @JacksonChayibu
    @JacksonChayibu 17 днів тому +2

    Ife tikufuna bon kalindo mawa atulusidwe

  • @eliaskhofielias8152
    @eliaskhofielias8152 17 днів тому +1

    Ngakhale atapanga zokoma bwanji a mcp kuphiphilitsa za imfa ya chilima even atati apereka nseu wot chilima road sadzawinabe awa.ndinu okupha okupha basi munapha nzanu mbili sizafufutika.

  • @chimwemwekamwana787
    @chimwemwekamwana787 17 днів тому +1

    Mukuopa kut anthu akutukwanani.. nanga mmene mukuoneramu amalawi tili pa ufulu ifeeee.. ai muli ndi manyazi ndithu

  • @user-mj2te7vl6p
    @user-mj2te7vl6p 16 днів тому +1

    Bodza limenero manyazi achakwera

  • @ShaliyaMusa
    @ShaliyaMusa 16 днів тому

    Ndiwomwewo mfiti. Chikwelayo paribe kikna

  • @ElizabethKhosa-gx3wt
    @ElizabethKhosa-gx3wt 16 днів тому

    Chingawenga choopya cha chakwela panopa chikufuna kuphe bon kalindo

  • @yusufbakali
    @yusufbakali 17 днів тому +1

    Kukhuyu zikhare chimwendo chakwela osewa adyeretu chaka chamawa chawoo palibe anthu tinavota kare kufa kwa chilima

  • @user-rd2ft5uk3q
    @user-rd2ft5uk3q 17 днів тому +2

    Ufulu wake utiwo

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 17 днів тому +1

    Ofufuza akhare a independent osati oziwana ndi mcp ai sipamveka black box ili kutiko choyamba?

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 14 днів тому

    Kunkuyu uzipemphela kwambili kuti boma lisasinthe ...boma kungosintha iwe uzafela kumdende ....unapha allan witika chifukwa cha mkazi .....munthu wopusa iwe kwambili mbuzi

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 17 днів тому +2

    Iwe mukuyu matako yako wapulika chakwel nayo pathako pake

  • @QueneteCatundulo
    @QueneteCatundulo 17 днів тому +1

    Good

  • @richardManemba
    @richardManemba 16 днів тому

    Ayii akupangila kt ufulu wa amalawi uchoke km osalola kungolola bas zabwelela zakale

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 17 днів тому +1

    Ndipo ofufudza sakuyenera kuitanidwa kuchoka ku boma cos ndiwomwe analephela kupulumutsa anthu, in other way, boma ndilimwe lapha anthu

  • @feehasaidid.r.d
    @feehasaidid.r.d 17 днів тому +1

    Wanena zoona chihana

  • @DennisDonework
    @DennisDonework 17 днів тому +1

    Afiti inu palibe ufulu nanga born kalindo akutani ku selo

  • @VanPaul-sv9yx
    @VanPaul-sv9yx 16 днів тому

    Nanu tazingodurani nkhani zofunikirazo ndikumaponya apa osati ndi nkhani zopoira zomwe

  • @user-tn2qg1vs9j
    @user-tn2qg1vs9j 17 днів тому +1

    Inu nosenu ndinu agalu kwabasi ifetu tikungo funa kuti bon Kalindo wathuyo tipaseni achainiyakefe

  • @JamesOsman-cz9cw
    @JamesOsman-cz9cw 17 днів тому +2

    Mcp people machende anu nonse

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 16 днів тому

    Muvesen akunena ufulu obela a malawi galuyu okukuda kukeqma

  • @user-mk3fy9nl2u
    @user-mk3fy9nl2u 16 днів тому

    Inunso mukuziziwa zimenezo

  • @Musa1828-l5d
    @Musa1828-l5d 16 днів тому

    Akuopa kuti akakuwidwa ku 6 July 😂😂😂😂 mwabalalika makape

  • @user-nr4mi7pt8g
    @user-nr4mi7pt8g 16 днів тому

    Ma billion chikondwererowo nde tigawanepotu sizausiru apa

  • @user-nn7sv5yb8h
    @user-nn7sv5yb8h 17 днів тому +1

    Kunkuyu udzinena kuti presdent wakoyo wanena kuti osati walamula ai

  • @josephchirwa-jt7jx
    @josephchirwa-jt7jx 17 днів тому +2

    Kodi ku malawi kuliso ufulu?

  • @user-lr2wx5xd9d
    @user-lr2wx5xd9d 17 днів тому +1

    Following

  • @MatiasChimsakasa
    @MatiasChimsakasa 16 днів тому

    Komano bwanji anthu anasangalala polumbilitsa olemekezeka a vp koma 6jly ayi Kodi undiuthenga wanji mukupeleka kwa ife achinyamata

  • @GeraldMkwewu-gd5eb
    @GeraldMkwewu-gd5eb 17 днів тому +1

    Chakwera ndi lwe nkukuyu agalu nose mapemphera achani fiti lnu nose ndi manganya tikulira chilima wanthu lnu mumumasure bon kalindo ndi kamulepu boma lakhaza lri mwayiwara kt mupeze ma udindo ndi chilima nose 😢

  • @AndrewMukhwapa-qj4vo
    @AndrewMukhwapa-qj4vo 17 днів тому +2

    Very good a Chihana

  • @TwayibuChimbama
    @TwayibuChimbama 17 днів тому +1

    Kusilamulila kwake kopa anthu

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 17 днів тому +1

    Iweyo Kumkuyu ndi Chakwera wakoyo God must punish you, Mukukamba za kukhudza Maliro a Dr Chilima chonsecho mukungotiphimba kumaso.

  • @mussakathumba128
    @mussakathumba128 14 днів тому

    Komanotu kunena chilunga amalawife tikufatsa kwambiri plus ulemu too much.chakwera wationjeza akungopha anthu ngati khuku tinayenera kumuchotsa before mavoti

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 14 днів тому

    Mulila bwanji poti mwachita kumupha chilima koma ndizokhumudwisa kwambili

  • @SarahMusama-eu7wt
    @SarahMusama-eu7wt 17 днів тому +1

    Koma kachere anachulukitsa kulibe dzina lina

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 17 днів тому +1

    Mukut mulira maliro nanga chowangira anthu mukulira maliro ndi chan?

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 17 днів тому +1

    Well done Enoch chihana utsogoleri ndiumeneo. Tikufuna tiwaziwe anthu amene achoka ku Germany ofufuza za ngozi ya vice president ndi azathu 9. Awapeza bwanji anthu aku Germany owo aboma anene.

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 16 днів тому

    Masiran born kalindo kaye mukubisa chan pomumanga iyeyo

  • @Eric-gb9ms
    @Eric-gb9ms 16 днів тому

    Akuti muli wufulu m'malawi zoona

  • @ZungeniBanet
    @ZungeniBanet 17 днів тому +1

    Inu ti onana 2025 mukutuluka inu

  • @LamieTiger-ff7cj
    @LamieTiger-ff7cj 17 днів тому +1

    Chakwera mukanangot kukhala Za satanic metsa inu ndi satana

  • @princedetbozsmallboy1749
    @princedetbozsmallboy1749 17 днів тому +1

    Zaziiii

  • @user-jl6sq3ph1b
    @user-jl6sq3ph1b 16 днів тому

    Mufika kumeneko nonsenu kumeneko za chamba 6 July muzakhalamulibe moyo inu agalu eti mboloyako

  • @ThomasMunyolowa
    @ThomasMunyolowa 17 днів тому +1

    Osati kuopa ku kuwizidwa

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 17 днів тому +1

    Chokani ana amahule inu kungokhalira umoyo wauchigawenga

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll 17 днів тому +1

    Opemphera ake ndani zigawenga inu?

  • @user-xf6dn7pv9b
    @user-xf6dn7pv9b 16 днів тому

    Chakwera ndiwe mbuzi wamva , galu , nyani chittsru cha munthu

  • @user-fh7sd6gp3f
    @user-fh7sd6gp3f 16 днів тому

    Mapemphero ake ati komanso abusa achokera mpingo uti
    Please leave God alone please

  • @JosephKuyeli-rc9on
    @JosephKuyeli-rc9on 15 днів тому

    Or mpunga wa nyama tisadyenso?? 😢😢😢

  • @AlexKaunda-ny2eg
    @AlexKaunda-ny2eg 17 днів тому +1

    Dzaka 60 yoh bwanji dziko lili paumphawi 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 shame

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 16 днів тому

    Iwe kumkuyu ndiiwe mbuz et ufulu wake ulikut popeza mungomanga aliyese brushit zako

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma 16 днів тому

    Akunkuyu machende

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q 17 днів тому +4

    KOMA BOMA LA MCP 😢😢😢
    AWA SI ANTHU KOMA AFITI ASATANIKI

  • @louisgolden
    @louisgolden 15 днів тому

    Kodi July yili Liti Koti muyambe kunena Za 6 July

  • @clintonhodda9830
    @clintonhodda9830 16 днів тому

    Anthu tili ndi mafunso kumene

  • @charlesvenacio9773
    @charlesvenacio9773 16 днів тому

    Malawi muno mulibe umfulu

  • @user-kk4uj8ko8k
    @user-kk4uj8ko8k 17 днів тому +1

    😂😂😂😂😂

  • @ClementMinyanga
    @ClementMinyanga 15 днів тому

    Ufulu wake ulikut???

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 14 днів тому

    Kunkuyu panyapako galu iwe

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 17 днів тому +1

    Inet imfa yachilima ndalota utsiku tapephera mosweka mtima akundilakhula kuti pangoz damulumuka koma anthu adandipha pondikhapa mendo zanga ndiy achakwera musamalet enafe ndi daniel tikapephera mulungu amayakha kumaloto athu mudapha inu pomukha chilima ndi zikwanje munyaaaaa nane daniel omasulira maloto kuuulurani

    • @ChristinaLigomeka
      @ChristinaLigomeka 17 днів тому +1

      😭😭😭 Km kulakwatu uku ayaluka awa akusewera ndi Mulungu km😭😭😭😭

    • @ManifoldPhiri
      @ManifoldPhiri 17 днів тому

      Usatchure dzina la mulungu wako pachabe mingochimwa nazo izi

    • @ChristinaLigomeka
      @ChristinaLigomeka 17 днів тому +2

      @@ManifoldPhiri atchula pacha be pempherani nanu mosweka mtima Mulungu sapepusa PEMPHELO losweka mtima Koditu amakani nu choona muchidziwa posachedwapa mwazi ukufula ohoooo wanthu 9 mmmmmm anthu mimba zamangidwa kufuna kudziwa choona chochoka kumwamba anthu kukugonedwa mapili kufuna kudziwa nchoonadi chochoka kumwamba inu ngati mafoloko alimanja daily musaganize ngati dziko lonse anthu avula dzuwa liliphweeee mukucheza ndi Mulungu

    • @SheenahMwalabu-iz3pr
      @SheenahMwalabu-iz3pr 17 днів тому +1

      ​@@ChristinaLigomekakunena zoona imfa iyiyi sikundigonetsa tulo ndizowawa ndipo ngati bodza Chilima kulibe zoona. Mulungu munaloleranji? 😢 ndikufuna tidziwe zoona

  • @user-vh9uk1jy7w
    @user-vh9uk1jy7w 17 днів тому +1

    Mbolo zanu

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 15 днів тому

    Ufulu wake utiwo?????

  • @Sugerman-tw4do
    @Sugerman-tw4do 16 днів тому

    Zopusainu

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 17 днів тому +1

    Chakwera is a mbolicious guy.

  • @LazaroSinerioSineiro
    @LazaroSinerioSineiro 17 днів тому +1

    Zoona akufunikadi kunthandizidwa