Kod ndinu muli ndi ka UA-cam Channel kanu kopepela mumakatcha bakili muluzi 🤣🤣🤣, zot kutali pass out week yatha ya ma cadet simumaziwa? Zot kunafika ma general from different countries like Zambia, Rwanda, eswantin, Mozambique,Kenya, Tanzania pamwambowo chifukwa ena mwa omwewa amapanga pass out are from those countries simukuziwa iyayi? Page iyiyi yazaza NDI ma bulutu.. very foolish, stupid and ignorant.. ka school kaja pena pake kamathandiza
This is true story I remember well my friend from Rwanda who were taken to that country they were killed by this guy's truly you can feel bad what I Saw that time please work up Malawi
As malawian citizens I will never allowed this nonsense to happen m"boma liyenela kuwasiya anthuwa tizikhalanawo mwantendele ngatimene timakhaliramu osamati kumazuka ndikumasawusa mitima yaanthu osalakwa
Whaooww 😲😲 I can't believe that in Malawi you have such brilliant journalist 🤔🤔 Tell them, teach them 😂😂😂 Many people don't know exactly what we be the consequences of the presence of this rwandeses on the Malawi land
Km iziz sizabwino these ppo came here bcoz they wanted peace and they hav sweat alot fo them to get wat ever they hav now penapake ndbwino kumaganiza kut ndtakhala ine ndkupangidwa zimenezo ndnganve bwanj, God must be the only helper
Malawi lero Ali pa mpeni vuto ili Matsatatsata Amalawi lero ndi izi Ntchito Qne million zija ma Mega farm aja Kudya katatu kuja ndikumeneku amalawi kususuka lero ndi nkhondo iyo
Mmm MCP itipweteketsa ndithu, go deeper our own informant, love you, proud of you always 🔥🔥🔥🔥🔥
This journalist is genius. Umafufuza aise. Big up. I like how you use deep knowledge to research news. Chakwera is killing refugees.
Kod ndinu muli ndi ka UA-cam Channel kanu kopepela mumakatcha bakili muluzi 🤣🤣🤣, zot kutali pass out week yatha ya ma cadet simumaziwa? Zot kunafika ma general from different countries like Zambia, Rwanda, eswantin, Mozambique,Kenya, Tanzania pamwambowo chifukwa ena mwa omwewa amapanga pass out are from those countries simukuziwa iyayi?
Page iyiyi yazaza NDI ma bulutu.. very foolish, stupid and ignorant.. ka school kaja pena pake kamathandiza
@@bernadakim6544 bulutu nd iwe aise palibe akukukukamamiza kut uzinvela
Iweyo ase the best of the best history in malawi 🇲🇼 👌
This journalist is very great.
Ohoho thanks very much bg mn respect ndawi zonse
Anthu ngat iweyo ndiyamene akufunika kumakhala dziko muno, receive your flowers 🎉
I don't think that the government has to review everything to the public
Watching from Zambia muchinga province God bless you,you are the best,
Malawi 🇲🇼 God help us
More thanx bro 4 keeping us updated
You stand for Us Boss
Big up brother King 🤴 of history ❤❤❤
One of the best Channel🔥🔥🔥🙏🙏😍
Zikachitika timvera Kwa inu big man give us more zomwe zikuchitika mziko lathu from South Africa
This is nice narration, evidence based journalist
Inuyo munadalitsika boss much respect, izizi nde zikufunikila mu dziko lathu lino
Best chanel than ever
Bbe up♥️♥️♥️
Big up 💪🏻
Asazakunamizeni chakwela sanali m'busa wa mulungu. Awawa ndmaplan omwe akupanga kukhomzekela zisankho gyz tisamale kufa anthu kuno😭😭😭😭
Yaaaaah oooooh!! Point iyi zedi thanks brother Wanga 😢😢
Good work brother keep on informing us
This is great and well explained
King of history!
You are the best! Big up
Chakwera ndi mzake chilima have change Malawi to den of robbers
Koma ase iweyu u can rule Malawi coz u know history alot
Ndipo zedi brother ndidolo uyu zed
Please tell us about the story of the people leaving in moon
Keep it up Mr
Good job
Asilikali a Malawi ndiye kuti ntchito Samatha??? Mpaka kuwabweletsela asilikali adziko lina aaaaaa shame
Keep up the good work boss
This is true story I remember well my friend from Rwanda who were taken to that country they were killed by this guy's truly you can feel bad what I Saw that time please work up Malawi
BIG 👍
You are a machine in history
Great documentary from intelligent man... true story of best killer in our continent..big up man
Mumakwana big ❤
😭😭😭😭😭yoooooohhh Mulungu Tetezelani ana akoo
Thanks but please do Hosni Mubarak
Brother bwanji mungopanga zoti muzapikjsane nawo pa chisankho cha upule tizakuvotelani ife pls.
Chakwera khala serious osaononge dziko la Malawi ndi nkhondo, ona ku DRC nkhondo yemwe amalimbikitsa ndi Kagame yemweyonso,kulira kulowetsa zigawenga m'dziko zoona, watitopetsa ndiwe munthu osaganiza.
TRUE GOD IS GOING TO FIGHT FOR THIS ARMY,
Never give up
Crying for my mother Malawi
Ndimakunyadilani big man koma ndimafuna ndifunse zikuwoneka kuti kangame ndimuthu oipa kwambiri koma sangakusakeni inuyo chifukwa ndimuthu oipa
Amakhala Kuti iyeyonso Ali well safeguarded by his people boss
Munabadwa masiku okwanira brother mumakwana heavy
Timva zinthu🙌
ndakugomelani..ndipo umantha...abusa sadapange bwino ndipo asilikali amenewa anyamuke
Tikhale ndi airport ya asilikali payokha iyo ndi public airport, sikofikila asilikali.
Ndipo kwambiri zoona ada koma MCP ayi zikomo
Atsogoleri aku Malawi ndi zitsiru
Koma bwanji Mr president Alola zimenezi
Inu ndiye mozi kwa history
Chitetezo cha Malawi chalowa mbola,aganiza bwanji abusa?
Chakwela alionetsa Zinthu Dziko Lamalawi
Live them
Mmmm koma ndiye zosakhala bwino ndithu, eeish
Chakwela ndichitsiru kwambili angalole bwanji asilikale alowe mu mziko ngat muli khondo , Nundwe naye angokhala ngat alibe mutu zautsilu kwabwas nkondo yili ku ukraine not ku malawi
Chakwera ndichitsilu mbolo yamake wakupha!! Guys we vote for wrong person , chosadzi nafenso!! Big up my brother for your good research!!
Very bad my Malawi😢😢😢😢😢
Zikhare ng'oma mbuzi yamunthu mulizelu m'menemo Mutu unangokula 😂😂😂❤
Gen Nyakarundi Vincent is Army chief for intelligence, Imachedwa Department Military Intelligence ( DMI)... ndi anthu oopsa zedi! 😢😢😢
Lazarus chakwera is not fair why can he allow such people to enter his country maybe he knows something and they offered him some money
Chakwera mbolo yako sure Ngati dziko lakurephela zisiye panyapako😂😂😂❤
Koma adaha😄😁😁😆😅🤣😂😂
Abusa sakuchitadi bwino Dr chakweka
Ndiye mvuto ndichani mesa akutenga akwawo Ngati akutenga a Malawi 🤷🤷
As malawian citizens I will never allowed this nonsense to happen m"boma liyenela kuwasiya anthuwa tizikhalanawo mwantendele ngatimene timakhaliramu osamati kumazuka ndikumasawusa mitima yaanthu osalakwa
Mmmmm kagame ndiwachabe
Mwatisuka mmaso apa boss 🎉😊
❤❤❤
Pena ndkaikhala ndi kumawona ngati kamuzu anasiya buku lina rake kuchipani cha m.c.p lophuzitsa dza ulamurilo wawo 😢😢
Exactly the way i think.
Sirius
Fact brother
Akuyanjana ndi anthu oipa kufuna kusokoneza bziko la Malawi
Politicians ndi anthu onyasa zochitika zawo
Kagame He going mad naw
Chakwera ndi Mbuzi yamunthu ameneyi angobwerera Ku church basi
chakwela sure bt niphala la munthu angalowese asilikali a ku ruward sure
Ok
We don't want war here in Malawi
Chiopsezo chiliso kwaife pamenepo dziko lilibe security ili😣😣
😢😢
Awa atipwetekesa sure
Whaooww 😲😲
I can't believe that in Malawi you have such brilliant journalist 🤔🤔
Tell them, teach them 😂😂😂
Many people don't know exactly what we be the consequences of the presence of this rwandeses on the Malawi land
Munthu wogwila kuchipiku angalamulire dziko anazolowela kunyamula mathumba akamba bas mbuz yeniyeni
MAY TRUE GOD SAVES THE LIFE OF INNOCENT PEOPLE LIFES,,, MAY THOSE REFUGES DEPEND REFUGE IN GOD ALMIGHTY GOD AND JESUS CHRIST, THE OWNER OF LIFE
😢Yo
Zomvetsa chisoni, ku mchinji anachita kubwera asilijali nkumamatchola ma shop nkumauza anthu kut azitulutsa katundu, God over everything
Shaaaaa kom zomvesatu chisoni mpakana kwatengela zinthu mushop pali uzimu apa
Mmmmmmmm zachitika litiro zimenezi?😢😢😢😢😢 Koma Chakwera guys ai zikomo 😭😭😭😭
@@eunicemoyo6024Ndagwetsa nsonzi inee😭
Chakwala ndikamukonsa koma mmmm ndaona kuti ndi manyi amuthu
be an advicer to our govt officials eish......
Apapa zayambika, Chakwela akusewela ndi team((Rwandan Solders) imene sakiyidziwa. Anthuwa amalora kupeleka ndalama iliyonse cholinga aketse mwazi(Blood) basi. Mukaitsatila bwino nkhani mupeza kuti boma la Malawi lalandira ndalama za nkhani nkhani cholinga Ma Refugees asowe mtendele basi. Si izi Zayayambika ku Chileka ndi madela ena ndi ena.
Very shameful
Km iziz sizabwino these ppo came here bcoz they wanted peace and they hav sweat alot fo them to get wat ever they hav now penapake ndbwino kumaganiza kut ndtakhala ine ndkupangidwa zimenezo ndnganve bwanj, God must be the only helper
Koma chakwerayu ndi buzi yamunthu akulolawesa zigawenga ziko zoo a
Malawi lero Ali pa mpeni vuto ili
Matsatatsata Amalawi lero ndi izi
Ntchito Qne million zija ma Mega farm aja
Kudya katatu kuja ndikumeneku amalawi kususuka lero ndi nkhondo iyo
Koma mulungu akuwaona sangasanglale muthu akuvutika chocho
Tikati tiwonesese panopa azisogoleri athu kumalawi akuwonjezera kutiyika mmavuto. Mayiko ambiri adananafesopano. Ife amene tirimoyenda like Mayiko akunja tizikhala tikuzudzidwa kaamba kanyasi zimene akupanga azisogoleri akumalawi povomereza kuzunza anthu obwera komaali osalakwa. Pamapeto azonse zikolathu la malawi tizakhala mmavuto azawoneni 😢😢😢😢😢
Azisogoleri mukuloleranji izii. 😢😢😢 umphawiwathu malawi ukutipangisa kuziyang'anira pansii😢😢
Kkkkkkk pot ndi akuda akanakhala ogalukila achizungu mukana khala chete
But the question is
How many richest people are leaving in out of the country?
Chakwela please treat well the pples
Im afraid to comment......Zikhale Ng'oma ndimunthu wabwino.
Umakwana bakili muluzi tv
Zikhale asabwerere mmbuyo kufikila awavachoke basi akakhale ku chitipa pakati padziko ayi ati takana amalawi amasomphenya
Marefugees sakhala pakati padziko ayi uyu amalandila ndalama kuti azitchuka ndi zinthu zopweteka amalawi azake mtayeni
Wait Malawi idzazindikira bwino patsogolo
Kagame anayambitsa nkondo mu drc,njira zimene anazera mukulowa drc ndizimene ukuzera kuyambitsa nkondo ku Malawi!
Funso nkumati kodi ma Hutuh kwao ndikuti ngati akukhala mothawathawa dziko laku Rwanda?
Bulutu chakwela mbuziiiii meeeeeeee chitsiru chamunthu