Asilikali 62 a Rwanda alowa mdziko la Malawi motsogozedwa ndi General wamkulu kwambiri.

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 17 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 231

  • @lyiemax
    @lyiemax Рік тому +4

    Mmm MCP itipweteketsa ndithu, go deeper our own informant, love you, proud of you always 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @onester4946
    @onester4946 Рік тому +13

    This journalist is genius. Umafufuza aise. Big up. I like how you use deep knowledge to research news. Chakwera is killing refugees.

    • @bernadakim6544
      @bernadakim6544 Рік тому +1

      Kod ndinu muli ndi ka UA-cam Channel kanu kopepela mumakatcha bakili muluzi 🤣🤣🤣, zot kutali pass out week yatha ya ma cadet simumaziwa? Zot kunafika ma general from different countries like Zambia, Rwanda, eswantin, Mozambique,Kenya, Tanzania pamwambowo chifukwa ena mwa omwewa amapanga pass out are from those countries simukuziwa iyayi?
      Page iyiyi yazaza NDI ma bulutu.. very foolish, stupid and ignorant.. ka school kaja pena pake kamathandiza

    • @devlinebhema2729
      @devlinebhema2729 Рік тому

      @@bernadakim6544 bulutu nd iwe aise palibe akukukukamamiza kut uzinvela

  • @TONYJUSTIN-cx7yt
    @TONYJUSTIN-cx7yt Рік тому +7

    Iweyo ase the best of the best history in malawi 🇲🇼 👌

  • @ancientnkhata1137
    @ancientnkhata1137 Рік тому +5

    This journalist is very great.

  • @LUCKYM4787
    @LUCKYM4787 Рік тому +3

    Ohoho thanks very much bg mn respect ndawi zonse

  • @obimonegev5579
    @obimonegev5579 Рік тому +22

    Anthu ngat iweyo ndiyamene akufunika kumakhala dziko muno, receive your flowers 🎉

    • @francistonysanena5349
      @francistonysanena5349 Рік тому +2

      I don't think that the government has to review everything to the public

  • @thomassimbaya197
    @thomassimbaya197 Рік тому +1

    Watching from Zambia muchinga province God bless you,you are the best,

  • @successngoma
    @successngoma Рік тому +9

    Malawi 🇲🇼 God help us

  • @EmmanuelThom2-xf6ij
    @EmmanuelThom2-xf6ij Рік тому +3

    More thanx bro 4 keeping us updated

  • @matamandonkhoma8163
    @matamandonkhoma8163 Рік тому +3

    You stand for Us Boss

  • @yasinkamwendo-jf7sc
    @yasinkamwendo-jf7sc Рік тому +2

    Big up brother King 🤴 of history ❤❤❤

  • @honourablemcgregorysc97tv
    @honourablemcgregorysc97tv Рік тому +11

    One of the best Channel🔥🔥🔥🙏🙏😍

  • @argentchilanga3246
    @argentchilanga3246 Рік тому

    Zikachitika timvera Kwa inu big man give us more zomwe zikuchitika mziko lathu from South Africa

  • @misianguisheraufi4803
    @misianguisheraufi4803 Рік тому

    This is nice narration, evidence based journalist

  • @WilliamChopika-d1z
    @WilliamChopika-d1z Рік тому

    Inuyo munadalitsika boss much respect, izizi nde zikufunikila mu dziko lathu lino

  • @andersonmaster8055
    @andersonmaster8055 Рік тому +1

    Best chanel than ever

  • @drbanda6105
    @drbanda6105 Рік тому +1

    Bbe up♥️♥️♥️

  • @rashidstamburi2705
    @rashidstamburi2705 Рік тому +5

    Big up 💪🏻

  • @davenchimadzi6529
    @davenchimadzi6529 Рік тому +7

    Asazakunamizeni chakwela sanali m'busa wa mulungu. Awawa ndmaplan omwe akupanga kukhomzekela zisankho gyz tisamale kufa anthu kuno😭😭😭😭

    • @ManuelMalunga-fl3vq
      @ManuelMalunga-fl3vq Рік тому +1

      Yaaaaah oooooh!! Point iyi zedi thanks brother Wanga 😢😢

  • @mateyudyton4739
    @mateyudyton4739 Рік тому

    Good work brother keep on informing us

  • @mathiasmajamanda5797
    @mathiasmajamanda5797 Рік тому

    This is great and well explained

  • @farookousmane715
    @farookousmane715 Рік тому +1

    King of history!

  • @wilsonsawasawa3794
    @wilsonsawasawa3794 Рік тому

    You are the best! Big up

  • @chitimbethegreat-pc1bp
    @chitimbethegreat-pc1bp Рік тому +5

    Chakwera ndi mzake chilima have change Malawi to den of robbers

  • @ahmedmsume1489
    @ahmedmsume1489 Рік тому +7

    Koma ase iweyu u can rule Malawi coz u know history alot

  • @emmanuelkhosa-ze6fl
    @emmanuelkhosa-ze6fl Рік тому +3

    Please tell us about the story of the people leaving in moon

  • @josuahkachali1489
    @josuahkachali1489 Рік тому

    Keep it up Mr

  • @khamaneizarif4491
    @khamaneizarif4491 Рік тому +1

    Good job

  • @chekiamaabdul5083
    @chekiamaabdul5083 Рік тому +1

    Asilikali a Malawi ndiye kuti ntchito Samatha??? Mpaka kuwabweletsela asilikali adziko lina aaaaaa shame

  • @martinkhozombah
    @martinkhozombah Рік тому

    Keep up the good work boss

  • @levisondaka6392
    @levisondaka6392 Рік тому

    This is true story I remember well my friend from Rwanda who were taken to that country they were killed by this guy's truly you can feel bad what I Saw that time please work up Malawi

  • @ziwani3682
    @ziwani3682 Рік тому +2

    BIG 👍

  • @nickmagola278
    @nickmagola278 Рік тому

    You are a machine in history

  • @NgaboJeanvier-iw4yu
    @NgaboJeanvier-iw4yu Рік тому

    Great documentary from intelligent man... true story of best killer in our continent..big up man

  • @YunusuOfesi
    @YunusuOfesi Рік тому +1

    Mumakwana big ❤

  • @JeanMarieNsengiyumva-qu9vm
    @JeanMarieNsengiyumva-qu9vm Рік тому

    😭😭😭😭😭yoooooohhh Mulungu Tetezelani ana akoo

  • @johnchavula3282
    @johnchavula3282 Рік тому +1

    Thanks but please do Hosni Mubarak

  • @irenechirwa9710
    @irenechirwa9710 Рік тому +1

    Brother bwanji mungopanga zoti muzapikjsane nawo pa chisankho cha upule tizakuvotelani ife pls.

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 Рік тому +1

    Chakwera khala serious osaononge dziko la Malawi ndi nkhondo, ona ku DRC nkhondo yemwe amalimbikitsa ndi Kagame yemweyonso,kulira kulowetsa zigawenga m'dziko zoona, watitopetsa ndiwe munthu osaganiza.

  • @kamwendoderek6567
    @kamwendoderek6567 Рік тому

    TRUE GOD IS GOING TO FIGHT FOR THIS ARMY,

  • @ChembeSolomon
    @ChembeSolomon Рік тому +2

    Never give up

  • @HestingsBellow
    @HestingsBellow Рік тому

    Crying for my mother Malawi

  • @titomethiwa4213
    @titomethiwa4213 Рік тому +4

    Ndimakunyadilani big man koma ndimafuna ndifunse zikuwoneka kuti kangame ndimuthu oipa kwambiri koma sangakusakeni inuyo chifukwa ndimuthu oipa

    • @ManuelMalunga-fl3vq
      @ManuelMalunga-fl3vq Рік тому

      Amakhala Kuti iyeyonso Ali well safeguarded by his people boss

  • @daviemafunga
    @daviemafunga Рік тому

    Munabadwa masiku okwanira brother mumakwana heavy

  • @justicenyirenda2049
    @justicenyirenda2049 Рік тому +2

    Timva zinthu🙌

  • @gesinasutherland9241
    @gesinasutherland9241 Рік тому +1

    ndakugomelani..ndipo umantha...abusa sadapange bwino ndipo asilikali amenewa anyamuke

  • @isaactembo6164
    @isaactembo6164 Рік тому +3

    Tikhale ndi airport ya asilikali payokha iyo ndi public airport, sikofikila asilikali.

  • @promisemakawa1556
    @promisemakawa1556 Рік тому +3

    Atsogoleri aku Malawi ndi zitsiru

  • @nelsonmacken7662
    @nelsonmacken7662 Рік тому

    Koma bwanji Mr president Alola zimenezi

  • @anafieintuka8090
    @anafieintuka8090 Рік тому

    Inu ndiye mozi kwa history

  • @NeversonGonthi-fg3zm
    @NeversonGonthi-fg3zm Рік тому +1

    Chitetezo cha Malawi chalowa mbola,aganiza bwanji abusa?

  • @alfredbanda886
    @alfredbanda886 Рік тому +4

    Chakwela alionetsa Zinthu Dziko Lamalawi

  • @oscarkachale9234
    @oscarkachale9234 Рік тому

    Live them

  • @professorsafuta3936
    @professorsafuta3936 Рік тому +1

    Mmmm koma ndiye zosakhala bwino ndithu, eeish

  • @wensleyshumba8205
    @wensleyshumba8205 Рік тому +3

    Chakwela ndichitsiru kwambili angalole bwanji asilikale alowe mu mziko ngat muli khondo , Nundwe naye angokhala ngat alibe mutu zautsilu kwabwas nkondo yili ku ukraine not ku malawi

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 Рік тому

    Chakwera ndichitsilu mbolo yamake wakupha!! Guys we vote for wrong person , chosadzi nafenso!! Big up my brother for your good research!!

  • @AlexKaunda-ir6rz
    @AlexKaunda-ir6rz Рік тому

    Zikhare ng'oma mbuzi yamunthu mulizelu m'menemo Mutu unangokula 😂😂😂❤

  • @jaykar-issa706
    @jaykar-issa706 Рік тому

    Gen Nyakarundi Vincent is Army chief for intelligence, Imachedwa Department Military Intelligence ( DMI)... ndi anthu oopsa zedi! 😢😢😢

  • @mathewsmwale20
    @mathewsmwale20 Рік тому

    Lazarus chakwera is not fair why can he allow such people to enter his country maybe he knows something and they offered him some money

  • @AlexKaunda-ir6rz
    @AlexKaunda-ir6rz Рік тому +1

    Chakwera mbolo yako sure Ngati dziko lakurephela zisiye panyapako😂😂😂❤

  • @DicksonMulinde
    @DicksonMulinde Рік тому

    Abusa sakuchitadi bwino Dr chakweka

  • @josephychisoni8628
    @josephychisoni8628 Рік тому

    Ndiye mvuto ndichani mesa akutenga akwawo Ngati akutenga a Malawi 🤷🤷

  • @Razarusmbavachakwera
    @Razarusmbavachakwera Рік тому +1

    As malawian citizens I will never allowed this nonsense to happen m"boma liyenela kuwasiya anthuwa tizikhalanawo mwantendele ngatimene timakhaliramu osamati kumazuka ndikumasawusa mitima yaanthu osalakwa

  • @georgekalichero7829
    @georgekalichero7829 Рік тому

    Mmmmm kagame ndiwachabe

  • @evancenasoro922
    @evancenasoro922 Рік тому

    Mwatisuka mmaso apa boss 🎉😊

  • @rosseshaibu1576
    @rosseshaibu1576 Рік тому +2

    ❤❤❤

  • @HakeemSilaji
    @HakeemSilaji Рік тому +2

    Pena ndkaikhala ndi kumawona ngati kamuzu anasiya buku lina rake kuchipani cha m.c.p lophuzitsa dza ulamurilo wawo 😢😢

  • @marthankhoma1063
    @marthankhoma1063 Рік тому

    Akuyanjana ndi anthu oipa kufuna kusokoneza bziko la Malawi

  • @idrissaeliassa
    @idrissaeliassa Рік тому +4

    Politicians ndi anthu onyasa zochitika zawo

  • @molicieeosama8877
    @molicieeosama8877 Рік тому

    Kagame He going mad naw

  • @maxgulani1391
    @maxgulani1391 Рік тому

    Chakwera ndi Mbuzi yamunthu ameneyi angobwerera Ku church basi

  • @AlickNyirongo-cp1dn
    @AlickNyirongo-cp1dn Рік тому

    chakwela sure bt niphala la munthu angalowese asilikali a ku ruward sure

  • @GanetStambuli
    @GanetStambuli 2 місяці тому

    Ok

  • @jimmyzgambo9928
    @jimmyzgambo9928 Рік тому

    We don't want war here in Malawi

  • @eunicemoyo6024
    @eunicemoyo6024 Рік тому +2

    Chiopsezo chiliso kwaife pamenepo dziko lilibe security ili😣😣

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 Рік тому +1

    Awa atipwetekesa sure

  • @yampanyamulenda9377
    @yampanyamulenda9377 Рік тому

    Whaooww 😲😲
    I can't believe that in Malawi you have such brilliant journalist 🤔🤔
    Tell them, teach them 😂😂😂
    Many people don't know exactly what we be the consequences of the presence of this rwandeses on the Malawi land

  • @wensleyshumba8205
    @wensleyshumba8205 Рік тому +2

    Munthu wogwila kuchipiku angalamulire dziko anazolowela kunyamula mathumba akamba bas mbuz yeniyeni

  • @kamwendoderek6567
    @kamwendoderek6567 Рік тому

    MAY TRUE GOD SAVES THE LIFE OF INNOCENT PEOPLE LIFES,,, MAY THOSE REFUGES DEPEND REFUGE IN GOD ALMIGHTY GOD AND JESUS CHRIST, THE OWNER OF LIFE

  • @NeoMaphango
    @NeoMaphango Рік тому +1

    😢Yo

  • @jermahkell8538
    @jermahkell8538 Рік тому +3

    Zomvetsa chisoni, ku mchinji anachita kubwera asilijali nkumamatchola ma shop nkumauza anthu kut azitulutsa katundu, God over everything

    • @eunicemoyo6024
      @eunicemoyo6024 Рік тому

      Shaaaaa kom zomvesatu chisoni mpakana kwatengela zinthu mushop pali uzimu apa

    • @ManuelMalunga-fl3vq
      @ManuelMalunga-fl3vq Рік тому

      Mmmmmmmm zachitika litiro zimenezi?😢😢😢😢😢 Koma Chakwera guys ai zikomo 😭😭😭😭

    • @ManuelMalunga-fl3vq
      @ManuelMalunga-fl3vq Рік тому

      ​@@eunicemoyo6024Ndagwetsa nsonzi inee😭

  • @Rafiki-pk7hw
    @Rafiki-pk7hw Рік тому +1

    Chakwala ndikamukonsa koma mmmm ndaona kuti ndi manyi amuthu

  • @greychizaka4088
    @greychizaka4088 Рік тому

    be an advicer to our govt officials eish......

  • @jacquesnsabiyaremye3166
    @jacquesnsabiyaremye3166 Рік тому

    Apapa zayambika, Chakwela akusewela ndi team((Rwandan Solders) imene sakiyidziwa. Anthuwa amalora kupeleka ndalama iliyonse cholinga aketse mwazi(Blood) basi. Mukaitsatila bwino nkhani mupeza kuti boma la Malawi lalandira ndalama za nkhani nkhani cholinga Ma Refugees asowe mtendele basi. Si izi Zayayambika ku Chileka ndi madela ena ndi ena.

  • @alannyirenda588
    @alannyirenda588 Рік тому +1

    Very shameful

  • @frankmajawa528
    @frankmajawa528 Рік тому +1

    Km iziz sizabwino these ppo came here bcoz they wanted peace and they hav sweat alot fo them to get wat ever they hav now penapake ndbwino kumaganiza kut ndtakhala ine ndkupangidwa zimenezo ndnganve bwanj, God must be the only helper

  • @bayview4554
    @bayview4554 Рік тому +1

    Koma chakwerayu ndi buzi yamunthu akulolawesa zigawenga ziko zoo a

  • @lewisbonongwe8518
    @lewisbonongwe8518 Рік тому

    Malawi lero Ali pa mpeni vuto ili
    Matsatatsata Amalawi lero ndi izi
    Ntchito Qne million zija ma Mega farm aja
    Kudya katatu kuja ndikumeneku amalawi kususuka lero ndi nkhondo iyo

  • @pastonmoda-pk4uj
    @pastonmoda-pk4uj Рік тому +1

    Koma mulungu akuwaona sangasanglale muthu akuvutika chocho

  • @sayidimisessa
    @sayidimisessa Рік тому

    Tikati tiwonesese panopa azisogoleri athu kumalawi akuwonjezera kutiyika mmavuto. Mayiko ambiri adananafesopano. Ife amene tirimoyenda like Mayiko akunja tizikhala tikuzudzidwa kaamba kanyasi zimene akupanga azisogoleri akumalawi povomereza kuzunza anthu obwera komaali osalakwa. Pamapeto azonse zikolathu la malawi tizakhala mmavuto azawoneni 😢😢😢😢😢
    Azisogoleri mukuloleranji izii. 😢😢😢 umphawiwathu malawi ukutipangisa kuziyang'anira pansii😢😢

  • @henrymunthali1280
    @henrymunthali1280 Рік тому

    Kkkkkkk pot ndi akuda akanakhala ogalukila achizungu mukana khala chete

  • @Mohamedkotwal
    @Mohamedkotwal Рік тому

    But the question is
    How many richest people are leaving in out of the country?
    Chakwela please treat well the pples

  • @rickiez
    @rickiez Рік тому

    Im afraid to comment......Zikhale Ng'oma ndimunthu wabwino.

  • @LimbaniYassin
    @LimbaniYassin 2 місяці тому

    Umakwana bakili muluzi tv

  • @mansonchinkhuzi
    @mansonchinkhuzi Рік тому

    Zikhale asabwerere mmbuyo kufikila awavachoke basi akakhale ku chitipa pakati padziko ayi ati takana amalawi amasomphenya

  • @mansonchinkhuzi
    @mansonchinkhuzi Рік тому

    Marefugees sakhala pakati padziko ayi uyu amalandila ndalama kuti azitchuka ndi zinthu zopweteka amalawi azake mtayeni

  • @nashoniclifford172
    @nashoniclifford172 Рік тому +1

    Wait Malawi idzazindikira bwino patsogolo

  • @kuziririzaisabatosiitegeko7088

    Kagame anayambitsa nkondo mu drc,njira zimene anazera mukulowa drc ndizimene ukuzera kuyambitsa nkondo ku Malawi!

  • @georgechikafutwa1334
    @georgechikafutwa1334 Рік тому

    Funso nkumati kodi ma Hutuh kwao ndikuti ngati akukhala mothawathawa dziko laku Rwanda?

  • @alfredbanda886
    @alfredbanda886 Рік тому +2

    Bulutu chakwela mbuziiiii meeeeeeee chitsiru chamunthu