Nde mukuvutikilanji ndi chizungu chosecho alipamenepo ndi anthu ot amava chichewa cholinga winayo akhale ndi mantha muwine likubwela tsiku muzuzayankha zimenezi
muthu oti akudya bwinobwino sangarowe muchele ndikumadula mitengo? kod simukwaona amene akudula ndalama za malawi za misongo simumamanga? koma odula mitengo nde eeee☠️☠️💀💀💀💀😭
Zangovuta abale chakwera wandikwana,.Maka moyo ophanawu ai
Mukanati muzitero milandu iliyonse bwezi zilibwino koma mumapangira asauka okhaokha komanso mukulimbana ndizithu zomwe sizingathandize amalawi olopangono koma koma mulungu oziwa kulanga akulangeni ma judge nonse Malawi muno🙏
Kkkkkkk koma kumalawi kulizinthu 😂😂😂chizungu ngat vizungu shame my pipokkkkkk
Mukumanga osawuka mukusiya akuba Gold ndi misonkho ya amalawi why amalawi? Ziwani chomwe chinapangisa kuti akalowe kunkhalango ndinu amu boma no jobs. And magesi amangoyaka 2 hours mukuganiza kuti amphawi iwe tiphirachani mumakomboni? Yambani kumanga akuba mubomawo ndi ena then pezani njira zabwino zathandizia amphawi.
Uyu mumusiye. Chakwela ndi chilima ndinuyo munaba ndalama zambiri. Mulungu athane nanu
Sibwino munthu amayiwala.abweze.foni
Mzaziii basi mukusiya kulimbana ndimbamva zomwe zikuba ndalama za boma mmmmhh koma mulungu akulangeni ndithu
Mukuitha magay big up
Kkkkkk tiyeni tziyankhula chichewa apa zizungu si chathu ichi
Nkhalango mwamaliza maliza kugulitsa mitengo kwa olemela lero muli bzy nd mphawi
Zopusa zeni zeni kusiya mbava zeni zeni zomwe zikuononga dzikoli kumakalimbana ndi munthu osauka ngati ameneyo azimbambo akulu akulu ngati inu mulibe manyazitu
Chizungu mukuwuza ndani simuzatheka dziko losauka koma vizungu kkkkk
Nonse akhoti pantumbopanu mukulimbana ndiwodula mtengo koma wokuba ndalama zambilimbili mboma mukumusiya mbuzi muzatipeza
Onena chilungamo ndiye mukumanga chilungamocho asananene
Basi inu peya peya kupit kukaona pomwe padulidwa mitengo mulungu akukhululukileni akuba ali mbweee misokho yathu mukulimbana ndizopelelazo
Boni yambomayo ndiye mbavayo kufuna kupaka phawiyo
Nde mukuvutikilanji ndi chizungu chosecho alipamenepo ndi anthu ot amava chichewa cholinga winayo akhale ndi mantha muwine likubwela tsiku muzuzayankha zimenezi
Ena akuba ma billion mulibe nawo ntchto kma kulimbana ndi mphw chifkwa cha mtengo umoz,inuyo ndi amuyaya? Enawa mukuwaponya Pat?
Á malawi mukufuna umukhale ngati nafni skúti tidzizungu izitu ndi zopusa með mukutizunzatu tikamasauka kukhala opanda chuma
muthu oti akudya bwinobwino sangarowe muchele ndikumadula mitengo? kod simukwaona amene akudula ndalama za malawi za misongo simumamanga? koma odula mitengo nde eeee☠️☠️💀💀💀💀😭
Kupusa basi munaonapo mzungu akuyangura chichewa?
choyamba mukuyenera kudziwa kuti dziko lanthu ndilosawuka
Malawi dziko lotembereredwa kupondereza anthu osauka pamene aboma Akuba mabilioni aboma pamene munthu odura mtengo woti adyetse banja alake
Kumamanga osauka kusia olemera popeza ndrama zao zuchitira umbon
Ndiye mwati milanduyu njowona kapena ndimacheza chabe?
Ndisewero
@@limbanimponda2721 ok koma samamaliza kaya eishhhh
Zoputsa mkuvutitsa anthu osauka musiyaokuba.
Ndipo
Za ziiii.
Y not arrest leston Lazaro chilima Joyce peter bingu in gravy yard
Chichewarising🤣🤣🤣
Eya kaya chichewa is our language
Ndinu opusa nose
Agalu inu munthu akusowa ntchito mumati ndiana azidya chani agalu inu koma inu ndiye kumaba ndalama muzalangidwa mizimutu ikakwiya
Kupusa
Kodi ndi drama chani??
Nane ndidziwe nawo
Zachibwana 😠😠😠😠
Yr fools
Amalawi English is not urs