Tanyiwa inu ndiakatundu bwanji kusowa mtima wanga ndimava bwino ndikava mau anu ndi abon kalindo ndi dj mnyanane inu matiinilila ife ndi dpp utm afod ndi udf tikulowa muboma chikangawa achoke basi
Mtanyiwa ndiwetu Katundu,, Ndipo musatope kutipatsa ma update a zonse zomwe Chikangawa wakonza, apa wapita kukabisa umboni wa Zotsatira za Kugwa kwa Ndege.
Some of your productions Mr Ntanyiwa are not good chief try to improve your station production especially when you doing your program we know u still growing as a radio koma try to be more creative with your productions.
😂😂😂Akulila awo ndi chikangawa anzawowo kkkk izatelo 2025 kutayaka moto ku mangochi nde manyazitu ufumu Wa mcp uzathela pompo kuti ng'ambi😅😅😅😅 love you muthu wankulu big man muthu wankulu Peter Ana a school anyamata ati profeti yawo ndi egrish km azigona njala. Takana ife ❤❤❤
Takunyadiradirani adadi tikufuna mubwerere basi zinthu zavuta mu malawi tatopa ife amalawi 💃💃💃💃♥️♥️♥️
Chipani cha uzimu , umuthu, chilungamo, dpp my vote forever ❤❤
All the time ndimaona Ngati amapanga zokomera mzika.
Apapa ndadziwa Kuti ukupanga za chipani.
Bola Winiko amwene
Eheeee a mcp mwanyaaaa manyiiii khalamba wa zeru , oopa mulungu, osapha , osaba , wachitukuko , osati chikanga satanayo , bulutu chakwela , nfiti , abwerere ku chipiku
Tanyiwa inu ndiakatundu bwanji kusowa mtima wanga ndimava bwino ndikava mau anu ndi abon kalindo ndi dj mnyanane inu matiinilila ife ndi dpp utm afod ndi udf tikulowa muboma chikangawa achoke basi
Koma wa bakili muluzi TV alipo?????
@@FatimaUmali-pc8syuyu watulutsa video inaaa uyu pompano wa Bakili Muluzi TV ndimakinanso naye eeeee😂😂😂
Mtanyiwa ndiwetu Katundu,, Ndipo musatope kutipatsa ma update a zonse zomwe Chikangawa wakonza, apa wapita kukabisa umboni wa Zotsatira za Kugwa kwa Ndege.
mtanyiwa machine
Dpp 🔥🔥🔥🔥
D.P.P nde boma lathu panopa tagwilizana tonse amene tikukhala Kuno ku Joni tikubwera kudzavotera Adad
Mtanyiwa ❤
Chitukuko,chilungamo ndi nsima imeneo nde D.P.P . A.P.M 2025 boma tithokoze gwilizano umenewu gwape chakwera umanama
Tatumizani zithunzizo kuti tizione zigawenga za police
Thanyuwa mumakwana big
❤❤❤❤ Mthanyiwa
Boma ilo my vote not chikangawa mubusa wa satana
Mtanyiwa tililimozi komkuno eti
Munthu wanzeru zake ndi owopa mulungu kumakhala bizy ndi mcp mene alilili Malawi pano ufiti chani aaaaa dpp woye 2025 boma kufuna osafuna kulowa basi moto kuti buuuuu
Amene akumatulukawo akuchita because ndi akazitape koma awona kut ku dpp kulibe chinyengo
chikangawa akuva nyunyunyu antanyiwa, kom achikangawa alimoyo ndizimene zichitika kukomesa
Zabwino zonse adad
Moto buuuuuu!!!!
Wa Bakili Muluzi TV ndamuonaso konkuno😢
He was there
Amen
Chikangawa akumva kuwawa
Apa zilibwino osaopa till pambuyo pa adadi
Tighting security without a machine gun what is that?
MCP yadzimbidwa ndi convention ya DPP
Opposition ndiyomweyi sitikusintha 🔥
APM my VOTI
My Chipani ine ntimau myaaaaaaa
❤thanyuwa
If you are a freedom fighter u don't support any party .Galu iwe
Iweyo ndiye galu weni weni mwana woyipitsitsa kwambiri mwana wa satana m'dyelekezi iwe
Asiyeni agogo akaleke zidzukuru
Mtanyiwa mmakwa kuno kunapeya kumachinga
Boma ilo!!!!!!!!!!!
kkkkk zinamizanani agalu inu ife phee a utm atatu aaaa ife phee ndi pp , fp n PDP mcp boma 2025
Mumatibvesa kukoma
Akanika kuchedzera chifukwa cha ukalamba
For security reasons, he is most wanted after chilima. He is threat to MCP
Akachezere Ku convention ngati kape
Zabwino zonse apm
Some of your productions Mr Ntanyiwa are not good chief try to improve your station production especially when you doing your program we know u still growing as a radio koma try to be more creative with your productions.
Ndikufuna nsalu ya DPP
Mmmmmm inenso ndasimikiza kuti Dpp ndi 1 bc enawa akutizuzawa nrhawi yao yatha basi
Bodzalo DPP inatha kale nkhalamba
Zikomo zikutheka zikukuwawa kod wanya ase
Wanu nyamata uja Mr chikangawa akutan
Yantha ndi MCP chikangawa part 😅😅😅
I think ameneyu satana akumuzemberera
😂😂😂Akulila awo ndi chikangawa anzawowo kkkk izatelo 2025 kutayaka moto ku mangochi nde manyazitu ufumu Wa mcp uzathela pompo kuti ng'ambi😅😅😅😅 love you muthu wankulu big man muthu wankulu Peter Ana a school anyamata ati profeti yawo ndi egrish km azigona njala. Takana ife ❤❤❤