Mwanva zomwe ayamba anthu Aku Dowa😳😳😳😳

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 144

  • @patrickmacheso5062
    @patrickmacheso5062 9 днів тому +11

    Well said,,, Chilungamo kuchiswa zeni zeni Ochewa.

  • @Maxielyies
    @Maxielyies 7 днів тому +1

    Boma lochitsa manyazi kulephela kusamala anthu ake

  • @CharlesBanda-v8k
    @CharlesBanda-v8k 9 днів тому +9

    Boma lagubuduzika basi😂 APM MY VOTE

  • @abgi.doctor.august
    @abgi.doctor.august 8 днів тому +1

    Tikafika APa ndiye kuti mzimu wa Chilima Ndi Anthu 8 yakwiya sikubweza Maganizo m mbuyo ayi boma la MCP ulendo basi APM my vote 💃💃💃💃💃💃

  • @MaryChavula-jz3di
    @MaryChavula-jz3di 9 днів тому +6

    Munanyanya kuthamanga ndi dzilombo kulanda boma aziwona kkk Apm my vote💙💙💙 kazikambilanani kkkkkk

  • @AlexanderChikusa
    @AlexanderChikusa 7 днів тому +1

    Ritchard Chimwendo alibe mzeru komaso umunthu

  • @SaidyKamala-jj7lo
    @SaidyKamala-jj7lo 9 днів тому +7

    😅😅😅😅😅😂😂😂😂 malawi anakoza kkkk america nayoso atimana ma ARV 😂😂😂

  • @BridgetGunde-w9c
    @BridgetGunde-w9c 7 днів тому +1

    apeka mayina a subsidyRichard ndi Samuel... anthu amewa agwetsa boma😂😂🙌

  • @FidelisNthenda-qq5sg
    @FidelisNthenda-qq5sg 9 днів тому +4

    😅😅😅 kwaoli, kwavunda😜😜😜

  • @ThokoMsonkho-hy4uc
    @ThokoMsonkho-hy4uc 9 днів тому +3

    Munthu wanzeru sangavotere Chakwera chifukwa ndimunthu opepera amangovomereza maganizo a nzungu. Nzungu Akati mugwetse kwacha iye kuvomera kuiwala kuti dziko muno simapanga katundu ogulitsa kunja ndizi katundu kukwera daily. Tikuvutika ndi njala chifukwa feteleza sakupezeka mopweka. Chakwera sangatukule dziko

  • @RaheemMoosaraheem
    @RaheemMoosaraheem 9 днів тому +3

    Nyau zafatsa2😂😂😂😂😂

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 9 днів тому +5

    APM waku State House, confirmed by Malawian cameras💙💙💙💙💪🏿💪🏿💪🏿💪🏿💪🏿💪🏿💪🏿

  • @justinmalala-e4o
    @justinmalala-e4o 4 дні тому

    Koma ndizoyenera kupanga brame nduna ziwili zokha. Aaaa ku mcp kulibe wina wamzeru kuposa mzake. Ndi boma la anthu osaganiza basi. Minister of finance komanso president, onse zawavuta

  • @SUNGANANIGONANI-l5d
    @SUNGANANIGONANI-l5d 9 днів тому +4

    Akuti aziunike government ngati boma😂😂😂😂

  • @peterthawi
    @peterthawi 9 днів тому +2

    ine ndine m 'chewa...ndipo zomwe boma ili likupanga ndi 0 pa 10

  • @EsnartGirivin
    @EsnartGirivin 9 днів тому +5

    Yakwiya ndi mizimu😮😮

  • @YasinterKapinga
    @YasinterKapinga 9 днів тому +2

    Malawian cameras ❤❤ munali pomwepo kodi kkkkk anthuwa anadekhatu 😂😂😂

  • @OfesiMakuwalo
    @OfesiMakuwalo 8 днів тому

    I love u Malawi Cameras 😂

  • @JamesRoben-dy7bx
    @JamesRoben-dy7bx 9 днів тому +3

    Kkkkk koma ndaseka chakwela sazava mafuta kulibe akupita kokapanga za mages zosephan mcp mulipo

  • @cmsanyama200
    @cmsanyama200 9 днів тому +4

    Ukakhala niwana amapasa umagona chagada kuti Wana oyamweko.

  • @MemoryNdhlovu-e4w
    @MemoryNdhlovu-e4w 8 днів тому

    Angavotere mcp ndi utm mitu sigwira chifukwa mavuto osewa tikukumana nawo adabwera chifukwa cha Chilima adafunisisa kukhala msogoleli wa ziko pano bwezi Ali president ku dpp koma kunyoza ndi kusava pano alikuti adamudya

  • @TressLuka
    @TressLuka 9 днів тому +1

    Chikangawa pa ulendo basi. Akwiye akwiyeee 😅😅😅😅😅

  • @LevieLinya
    @LevieLinya 9 днів тому +2

    Welcome. Malawian camera 📸

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 9 днів тому

    This should now be Malawian Eyes ....Cameras yachepa😂😂

  • @FytonRichard-t3w
    @FytonRichard-t3w 9 днів тому +2

    Ine chewa km nunena zoona ineyo boma suluyenda bwino yayi tere😢

  • @EdwinMakwangwala
    @EdwinMakwangwala 8 днів тому

    God bless Malawi.

  • @AdamAhamad-g7u
    @AdamAhamad-g7u 9 днів тому

    Kumtumbo kwanu agalu a MCP mwatiwonongela dziko

  • @petertengani
    @petertengani 9 днів тому +1

    Lero si mawa, tidzikhala anthu okondana. Denis Mahata, chonde azungulireni anthu ku Dowa.
    😆😆❤️🙏🏾.

  • @dickyhuwa1723
    @dickyhuwa1723 9 днів тому +5

    Achewa sitikondwa oro pag ono

  • @LinlyMathewe
    @LinlyMathewe 9 днів тому +1

    Zaziii umbuli eti UTM my vote ❤❤❤❤

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 9 днів тому +2

    Simmene kuliri 😂😂😂😂😂😂❤

  • @SamLongwe-y9b
    @SamLongwe-y9b 9 днів тому +2

    Macadet azako ameneo ndipo dpp singabweleleso muboma

    • @WatisoniKadewele
      @WatisoniKadewele 9 днів тому

      Uyanya wena😮

    • @ThokoMsonkho-hy4uc
      @ThokoMsonkho-hy4uc 9 днів тому

      Umuuze Chikangawa wakoyo mbolo yake mkadzi wake misempha mikono ngati nyani.Afumu akwanu mbolo yawo ngati ndi akadzi nyini yawo komanso abambo ako machende awo ndipo ngati anamwalira ndikutukwana mafupa awo mandamo

    • @Mavisbunny346
      @Mavisbunny346 9 днів тому +1

      Pepani Kaya ndinu wamamuno Kaya wamkazi chonde Mulungu analenga munthu aliyense​ ndichifanizo cha Mulungu, mudziyankhula mfundo osati kutukwana mwa phunzo mulandira temberero. Ine si wa MCP koma kutukwana kwanu mpaka munthu wakufa. Chonde sinthani mayankhulidwe oterewo.

  • @ELLENZAPS
    @ELLENZAPS 9 днів тому +1

    Akut anthu akusangalala mulungu sangakondwe Kut anthu ena azivutoka tsogoleli azikonda anthu ose poti ose ndi amalaw mosatengera ntundu not kukondwera ndeno inu amene mukusangalala ndi boma lachakwera mudziwe Kut anzanu akuvutika musamalitse pamenepo mukamayamikira chakwera poti mukukhuta

  • @rashidadan2533
    @rashidadan2533 9 днів тому +3

    HlS exllent professor Peter muthalika
    The president of the republic of MALAWl 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 2025 to 2030

  • @ChrispinKashosha
    @ChrispinKashosha 9 днів тому +2

    Sianthu akudowa bodza velani koyambirilako anthuwo achita kusintha voice

  • @FelixKChisale
    @FelixKChisale 8 днів тому

    Musatinamizile ife kuno olo zitavutanwanji sitingavotele dpp

  • @HildaMbizi
    @HildaMbizi 9 днів тому +1

    UTM my vote

  • @ConsPempho
    @ConsPempho 8 днів тому

    Dpp boma basi izi ayi ndinthu

  • @SamuelKhumbiwa
    @SamuelKhumbiwa 9 днів тому +1

    Kumwela akusangalala ,bodza achewa mukutimphimba maso,ulamuliro uwu unthelamo popanda chochitika kuno,akt kuli Neef,tikungomva kt anthu akulandila ,kuli fetelizer wamakopon kuli ziii chimanga chikumasula pano kma ndi chofiila kusowa fertilizer,chitukuko china chilichonse kulibe,zonsezo zikuchitika komweko chigawo chapakati mau mbomi tili nao,apatu musat akapanda kusmala agwa,kd asamala chani nthawi yao yantha kale ,awat agwa kale kwatsala nditsikulo kt likwanilisidwe bas.,Achakwela akwela mumtengo akuona ngt pansiipa palibe mame

  • @ElizabethKazambwe
    @ElizabethKazambwe 9 днів тому +1

    Ndiye mwati government ngati boma?

  • @WelingsLongwe
    @WelingsLongwe 9 днів тому +1

    Mungoti ku dowa wisachula dera limene akuchokera zabodza mumasowa zokamba

  • @ErickCPatrick
    @ErickCPatrick 9 днів тому +2

    ,mcp,ngakhale,asemphane,zochita,samayambitsa,,,,,chipani,china,km,kum,mwelako,mpaka,zikwana,,10,zipani,mcp,ilikomwekoso,,,tionetsane,chaka,chakachino,

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 9 днів тому +1

    BOMA la MCP lagwa bwasi Chakwela anamudyesa buluzi amangolamulilidwa ndi Chimwendo mpaka kugwesa MCP

  • @alfredpatel3984
    @alfredpatel3984 8 днів тому

    Wise man Chimwendo yo?? Ngati kuli munthu wa MCP yemwe akupusitsa Chakwera ndi Chimwendo.
    Munkati boma ndilomweli lero mwagwila chiphwisi ku Dowa. Ndale za MCP zauchitsilu basi.

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 9 днів тому +1

    Malawian Cameras❤❤❤❤

  • @AbdulJohn-t7l
    @AbdulJohn-t7l 9 днів тому +1

    Achewa ndi ozikondadi nonse poti mumangofela kuti uyu mngwatu😂

  • @PatrickMalenga-h5m
    @PatrickMalenga-h5m 9 днів тому +1

    Inu musavere ameneyo kadet wa dpp dowa singavotere dpp mchewa sangasithe muwone koti mukapangire kampeni inu mukuchedwa

  • @owenmoses9434
    @owenmoses9434 9 днів тому +1

    Zilibwino kwambiri kuti izizi akuyankhulawa ndiachaeniake a MCp komaso ku base ya mcp-yomweyo😢 uyu atiphauyu iiii

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 9 днів тому +1

    Malawian Camera anali pomwepo koma anthuwo samamuona Malawian Camera ndi twinie brother wa Mose uja wa Baibulo znse zikhale poyera

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 9 днів тому

    Blues basi chakwera akagwele

  • @TamUs-u2h
    @TamUs-u2h 7 днів тому

    Mwakochana ma cadets nokha nokha apa, zopusa

  • @FytonRichard-t3w
    @FytonRichard-t3w 9 днів тому +5

    I like Malawi camera 🤳😂😂😂😂

  • @OviidMakumbi
    @OviidMakumbi 8 днів тому

    Government ngati Boma

  • @RoseMchenga
    @RoseMchenga 9 днів тому +1

    Ku mmwera kwake kuti anthu akusangalala? Ifenso kuno ayi

  • @AmosiChauluka
    @AmosiChauluka 9 днів тому +1

    Kuma amalawi tisazaerekezeso ku vote vinyau

  • @WilliousNyirongo
    @WilliousNyirongo 9 днів тому

    Kkkkkk mukamapanga zinthu muziyiwerenga kut anthu adziwe kut sizoopanga

  • @lewisdicksonmlozi130
    @lewisdicksonmlozi130 9 днів тому

    MCP iwinira kubwera not kuti zama voti..anthu amenewo akupanga ma plan obera

  • @DamsonSamson
    @DamsonSamson 5 днів тому

    Adadii oyeee 2025 akutenga boma basi mufune musafune koma simuthawa??

  • @ErickCPatrick
    @ErickCPatrick 9 днів тому +2

    ,bodza,ilo,mwapangana,nokhanokha,musanamizile,anthi,akudowa,muwaonetse,taone,,,akulankhulao,akutumaniwo,akuphwetekesa,mcp,singatekeseke,ndizopusazo,komweko,kuno,ayi,zagalu,zanuzo,

  • @ChristopherManase-s1f
    @ChristopherManase-s1f 9 днів тому

    Kkkk koma mcp simugona nayo tulo. Mwagula wanthu kuti azinyoza mcp. Kkkkkk koma

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 9 днів тому

    Apm boma 💙💙💙💙🙌💙

  • @vinceynyone6693
    @vinceynyone6693 8 днів тому

    UTM pa16 Sept chongii ✅

  • @DysonTummiesSajiwa
    @DysonTummiesSajiwa 9 днів тому +2

    Mukunamizana Dowa yake itiyo inuyo ingodikilani September basi

    • @symoldicky
      @symoldicky 9 днів тому +1

      iwe uliko wekha kusowa Kuno ukat dowa yake just bcoz iwe udya nawo achimwendowo ife tifele zimenezo?

  • @stevenbanda6665
    @stevenbanda6665 9 днів тому +1

    Wawa😅😅😅

  • @BashiruAdamus-l2b
    @BashiruAdamus-l2b 9 днів тому +1

    Boma ili palibe chomwe anganene achita azipita anthu okuba ndi kupha basi

  • @BerthaChisoni2
    @BerthaChisoni2 9 днів тому +2

    Zinthi suzuyenda...

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs 9 днів тому

    Kodi wina amatepa iwo asakudziwa kapena zochita ukoza 😂😂😂😂 chifukwatu nde adadekha

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 9 днів тому +3

    Tachita bwino anthu aku Dowa mulape

  • @alfredfunani5641
    @alfredfunani5641 9 днів тому

    Malawian cameras 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @HalisonSolomon
    @HalisonSolomon 9 днів тому +1

    Abu bweretsa fatireza 😅😅😅 nchewa ANAKONZA BOMA ili ndi logwaigwa osati inachita chibwana yagwakale iyi

  • @TameeraInglis
    @TameeraInglis 9 днів тому

    Mukuiwala mbava zina izi Howa nkaka, kamajekete zikhale ng'oma n

  • @FelixMayeso
    @FelixMayeso 6 днів тому

    Dowa wake uti?

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 9 днів тому +1

    Koditu pafika malawipa kudzavotera mcp ndikupanda nzeru

  • @RossanaMitha-tl9in
    @RossanaMitha-tl9in 9 днів тому +1

    Siluyenda bwino ataaa

  • @AlfredManjawira
    @AlfredManjawira 8 днів тому

    Aaaaaaaa kķkkkk ndakatulo kapena drama

  • @SamuelNandolo-s5w
    @SamuelNandolo-s5w 8 днів тому

    Mumtumizire chimwendo

  • @AnnahKachidza-e8y
    @AnnahKachidza-e8y 8 днів тому

    Achitsiru Inu mwasowa zotumiza eti

  • @WarriorKB-l3i
    @WarriorKB-l3i 9 днів тому

    Ife tikamanena mumati tikun
    ama apapa mwamva nokha DC ananenso kuti ku dowa anthu akumvutika mumaona ngati akunama, mwacidule mcp palibe ciliconse yacita kwa a malawi 0% .apapa basi yagwa chifukwa alibe nthawi yokoza dzinthu alephela zaka nde angakoze dzinthu menzi 4? Panopa adzingopakila APM akubwela.Takunyadilani anthu a ku dowa kumene chikangawa amati mkwawo mwachita bwino kudzimasula nyau zimenezi.

  • @harryphiri849
    @harryphiri849 9 днів тому

    Mabodzaamenewo mcp yiwinaso yinua dpp mukumasowazokamba ndinumakape mukunya bomandilomweli sitikusitha

  • @HyTy-r3m
    @HyTy-r3m 9 днів тому

    Pepani ife kummwera kuno sitikusangalala tikuzunzika osati masewera so ife timati bola anzathu kumeneko poti ndikwawo

  • @AminaMdala-q8k
    @AminaMdala-q8k 9 днів тому

    Meangless I'm from Thyolo but I'm not a Dpp Supporter, so kukhala waku Dowa sizitanthauza kuti ndi wa Mcp

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 9 днів тому

    APM 💙💙💙

  • @geraldtuwaga-iz6ll
    @geraldtuwaga-iz6ll 9 днів тому

    Dowa kuchipinda kwa chikangawa party

  • @ErickCPatrick
    @ErickCPatrick 9 днів тому +1

    mukamachita,ndala,musamachulutse,bodza,kunamizila,anzanu,zoipa,dziko,lidapenya,,,,kuwanamizila,anthu,akudowa,kapena,kuwaona,kupusa,athu,akudowa

  • @collennyadile8179
    @collennyadile8179 9 днів тому

    anthu amene amamwa ma ARVS basi zinthu zativuta chifukwa America yasiya kaye thandizo lake kodi apanga bwanji chakwera pamene kwawo ndikuba basi

  • @Mirriumkamwendo
    @Mirriumkamwendo 9 днів тому

    Moses kumkuyu mukumuiwala ndi zikhale ng'oma

  • @BraveBanda-p2j
    @BraveBanda-p2j 9 днів тому

    APM MY VOTE DPP WUY😅😅

  • @JaneBanda-ht4ve
    @JaneBanda-ht4ve 9 днів тому

    CHAKWERA mukumva naye kuwawatu, olo mulembe ganyu achewa opepela nkumalankhula zopepelazo mungozinamiza. CHAKWERA awina ndi landslide ndipo mudzapita ku court simudzawina mulandu chifukwa MCP idzawina mwachilingamo osati Tippex wanu uja ai

    • @tingamasi106
      @tingamasi106 9 днів тому

      Ndiwe mbuzi

    • @HaroonSaidi-jv3ek
      @HaroonSaidi-jv3ek 9 днів тому

      ULENDO UNO KULIBE ZA CHIZOLOWEZI

    • @JaneBanda-ht4ve
      @JaneBanda-ht4ve 9 днів тому

      @@tingamasi106 Lucifer iwe, ngati Mai ako anabelekapo mbuzi ndi kwanu komweko.
      Anthu ongodziwa kutukwana pa social media phindu lake ndi chani kutuwa muli mbuuu

    • @JaneBanda-ht4ve
      @JaneBanda-ht4ve 9 днів тому

      @@HaroonSaidi-jv3ek ubwino wake September 16 kwatsala miezi yochepa, omuvotela Chakwera akuchulukilabe🇲🇼✅🔥🔥🔥🔥🔥

  • @AndrewMatiki-i5z
    @AndrewMatiki-i5z 9 днів тому

    Government ngati Boma yemweyo
    Likugwaa

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 9 днів тому

    Dowa yayankhulatu.

  • @ThomasJohn-j8x
    @ThomasJohn-j8x 9 днів тому

    Chimwendo akuzitenga ngati ndi yesu

  • @PatriciaAlomwe-oz8wc
    @PatriciaAlomwe-oz8wc 9 днів тому

    Azanu zikoli amaliyendesa bwino kma inuyo yakwiya ndi mizimu ya kuchikangawa

  • @WilliamBelvin-fq4ky
    @WilliamBelvin-fq4ky 9 днів тому

    Bodza Ili 😂😂😂

  • @PatrishaMwale
    @PatrishaMwale 9 днів тому +1

    Koma simukunama

  • @UmaliMmussa
    @UmaliMmussa 9 днів тому

    Boma ili silikusamara za kampen iyi ikupakuliratu ikagwa iwowo alibe khawa zawo zizakhara zatheka

  • @MemoryWanda
    @MemoryWanda 9 днів тому

    Kulibeso chakwera kuwina

  • @GeraldChilundu-e3v
    @GeraldChilundu-e3v 9 днів тому

    Anthu awa a MCP awononga dziko asawapatsa vote

  • @TamUs-u2h
    @TamUs-u2h 7 днів тому

    Zopusa zeni zeni your playing drama

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 9 днів тому

    🔥🔥🔥🔥

  • @drbanda6105
    @drbanda6105 9 днів тому +1

    KKKKKKKKKKKK.MCP..😂