KWAYAKA MOTO KU MALAWI! ANTHU AWA APEKELEKA MASIKU 14 KWA CHAKWERA ~~ NGATI SAPANGA IZI IWO ATELE
Вставка
- Опубліковано 19 вер 2024
- KWAYAKA MOTO KU MALAWI! ANTHU AWA APEKELEKA MASIKU 14 KWA CHAKWERA ~~ NGATI SAPANGA IZI IWO ATELE
Welcome to our channel, where we dive deep into the intricate and evolving world of Malawi’s politics. From the rise of powerful political parties like the Democratic Progressive Party (DPP) and Malawi Congress Party (MCP) to the powerful impact of the UTM Party, we bring you insightful analysis on the key players shaping the nation. Explore the journeys of leaders like Lazarus Chakwera, Saulos Chilima, and the influential activist Bon Kalindo as they navigate the challenges of governance, power struggles, and the quest for a better future.
Our channel is dedicated to unraveling the complexities of Malawi’s political landscape, offering you detailed breakdowns of alliances, rivalries, and the significant events that continue to define the country’s destiny. Whether you're interested in historical perspectives or current political dynamics, we provide in-depth coverage and engaging content that keeps you informed and inspired.
Subscribe to stay updated on the latest developments, and join us as we explore the fascinating stories that shape Malawi’s political narrative.
#MalawiPolitics #PoliticalAnalysis #DPP #MCP #UTM #LazarusChakwera #SaulosChilima #BonKalindo #AfricaPolitics #PoliticalActivism #petermutharika
Namiwa ndi Office yanu pitilizani kupanga chilungamo mupaka Mulungu ationese chimene chinapha azibale athu zikomo kwambiri
Chakwera ndi azinzake a MCP akutitora kwambiri ngati dziko
Amenewo ndiye mau mr namiwa timakunyadilani
Chakwara achoka chikangawa
Rip SKC
Powerful massage
Chilungamo chiyende ngati madzi❤ from cape town
bon kalindo please join hands with nsmiwa and lead malawian kuoanga ma demonstratiin atule pansi udindo
Zoona tidakalira Abale athu ife
Ma demonstration akhale oti asiye pasi udindo.
That's good well done
Gear 2 ipondeni fader Mr Namiwa ❤❤
Loud and clear!!!!!
Well done Mr namiwa,, keep it up
Namiwa ,born kalindo ,mtanyiwa JB ,bakili muluzi TV ose ndi alomwe ,akumenyera kampeni mulomwe nzawo peter muntharika,koma adziwe kuti Malawi sikumuntha kwa muntharika
powerful 💪 Mr Namiwa
Pamenepo mwadza ndithu
Mr namiwa tikukudalulani pamozi ndigululanu mukamayangula zamakape amewa
Great job Mr Nam
Mr M Namiwa mmmmh Ambuye akutetedzeni ndithu mumatiimilira ulemu wanu 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🙍
Good point
Mr Namiwa mulungu akhale Nanu kulikonse mungapite, pitilizan kutumikira amalawi .
Ulemu wanu namiwa ❤
Tiyeni Tiyeni asatizolowere Bambo otembereledwa chikangawa yi
🎉🎉 nkhanii niyoona
Big up Namiwa
Makamaka kugwirana manja ndi kalondo
Yes ayankhe ndithu
Mademo omweo ❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Thank u umakwana
❤❤ umakwana malume
Ai chakwela asiye pasi udindo kuti afufuzidwe bwinobwo za ifa imeneyi
Paja Chakwera akuti sawopsyezedwa iye sanva za anthu
Ine ndili okwiya kwambiri ndi chipani Cha Mr chikangawa ndi m c p nkhondotu iyi akuyiyambayi😢😢😢
Big up 🔥🔥
Behind you !!
Ukunena zoona. Ndikudabwa kuti tikungokhala! Chakwera akudziwapo kanthu.
Uramurilo uwu ndiwa 1940 wachakwera
Çhikangawa achke
100% chilungamo tikuchifuna ife tatopa ndi ulamuliro wa chikangawa that is the point
Ndipo zithunzi za skc tili nazo ndipo chinawavula zovala ndi tayi munthu kusala ali mbulanda tichidziwe chifukwa taona ndege zikugwa koma si ya skc aaaa chikangawa wakupha
Naniwa adaika kale mutu pa njanji samaopa kufa ndiolimba mtima go ahead namiwa.
Kd chilima unafadi km zimanivutabe kuvetsa ishiiii😢😢
km aah pure awaaa mulungu awaone 😭😭😭😭
Zoona bwana
Ndipo so masiku 14 achuluka kumafunika kupanda mademo Ali kuunga asabweleso
Mukunena zoonadi za mademo ndi zochedwa.
❤❤❤❤
Zoona
Wamurder by phalombe muzik
Born kanindo please join them
Ifwanthamureni fada!!!!!!!
Rip skc mmmmm chakwera uyankhe ife tikulira mpaka pano sitimavetsa
Namiwa osafoka
Please work on you background music
Komanso akubanja asakhale chete please
Koma ndipodi akuma banja akhala chete kwambiri. Akuwugwira bwanji mtima akuma banja. Akudekha kwambiri akuma banja oferedwawa.
Chikangawa wapita ku us
Zinthu izidzi Chakwera ndi agalu azinzakewa atipedzelera kwambiri sinanga chinanga sakuopa chilichonse wayambira mabungwe, zipani zotsutsa amipingo ndi zipembedzo a Malawi Eni akewo nde nyanyi chifukwa angoyang'anidwa akamapanga zoputsa zakezo
Coz tamupatsa mphamvu zonse watansa malamulo nde angowasintha Ngati am'nyumba mwake
Koma tonse tikagwirana ndikumanga chimodzi Kanyimbi ameneyu idzakha mbiri Kuti adalipo pharaoh
Serious
Kenako athamanga ndi chithumba cha ndalama kenako munva ziwonetsero zija sitipanganso
guys nkhani ndimeneyi atsogoleri amalawi dzikoli alitola kwambili pasakhaleso kusekerera anthu opusawa
Timenyeren nkhondo mr namiwa
Koma nkhani ya 14 days 21 days inayambapo ndi kale. Koma palibe chomwe chikuchitika.
Khalani anthu ochita osati olankhula okha.
Akakuphani ndi bread zonsezo musiya kulankhula, nanga amzathuwa ndalama yaboma siiyi ikuthera kugulira anthuyi.
bwana aNamiwa pangani zomwezo ife amalawi tikulila
Awuzeni chilungamo awuzeni chilungamo chidutse muchilungamo
Namiwa ukumanyako ku chikangawa? Dege yikawa ya chakwera? Lindilani Germany namwe ,
Niwopenga awa akuwa namiza ninkhala ya dpp ija
Va ziii ivo
Rest in peace bhiyeni ngt bodza eeeesh
Chilungamo chiyende ngati madzi, mcp njakupha ndani sakudziwa? Mcp imapha
Ndipo live chomwe akuziwa kuyenda yenda kuba ndarara kumapitira maiko akuja athu akudya chitedzi
Esh Anamiwa mukundilankulila bwino bwanji
14 dyz yachuluka kwambiri mr Namiwa chikangawa must goooo
MCP ndi chipani Cha kupha ndikale
Kulila talila..Pano tidziwe choona
Kodi 7 days yomwe munamupatsa chimwendo Banda uja zili pati?
Lilo dziko Lina sindikukayika konse awa pochoka ku UNGA anangofikira ku court dziko akulamulira asilikali, koma poti ku Malawi kumangodzivetsa chisoni. Komatu kunena chilungamo mafunso akufunsidwa ndioveka ndipo onse okhudzidwa akazivera sindikukayika amatuluka mamina ndithu
Apa palibe zobisa anatiphera chilima achakwera.chipani cha mcp ndichowophya chamagazi .
Ndipo 1983 kunalibe anthu ambili wophunzilanso anali wochepa ndiye matamawo akuyambira pati
Musasiyile pomwepa bwana😢
Zoona zoona
Akumveka ngat wa Bakili muluzi TV 😂😂😂
Koma I support you Mr.Namiwa
Nvuto amalawi fe Mantha too much 😅😅😅😅
Ndipo zoonadi ngati sakuyakha chomwe anamuphela chilima ifeso timupha tidulakhoso komaso uyu Richard chimwendo tidula khosi
Ma deadline sakuopaso
Dzikapangani ma demo ife tilibe nazo ntchito chifukwa sikut adzadzukaso ayi wapita ameneyo
Nanga anamuvula zovala Chilima ndi ndani mpakana lamba?nanga emwe analoleza kuti Ndege iwuluke kuli nyengo yosakhala bwino ndani? Nanga munthu anamuletsa Richard Chimwendo kuti asakwere nawo ndani? Nanga emwe anamuuza president yo ndi ndani kuti Ndege inafika ku Mzuzu
Ife sitidikiratu 2025 kuti akathyaliwa achoke m'boma, mcp dziwani ichi Malawi siopusa palibeso ndale apa nkhani ndi mwazi wa anthu apa.
Zoona anene bwino
Osaopa. 😅😅
Ndipo ndizoona chakwela akudziwapo kathu za imfa ya chilima satana chakwela
Zikomo kwambiri bambo namiwa chenjani giya2 tiri pambuyo panu wawa.
ummmm uyu ndiwa opposition ndamuona tsopano
Ndye????😏😏😏
Bon kalindo NDIwa opposition nsooo mmmm ife tifuna chilungamo
Umafuna azisekerera zoipazi
Nde umafuna afufuze ndani poti opposition nde angapange
Wa opposition kuti chani...why are you hating the truth.....be there for the truth not for favours..... these guys are standing for the truth so whats wrong with that
Komadi pangan zomwezo kuthamanga bas
Auzen amalaw timulowele fasting ya estere ameneyi adwale khate
Mulungu akutsogolele big chilungamo chofunika akutizolowela achakwela kwambili kutiwa kokhalila kutulukila kukamwa
Cided ilibe mphamvu payokha, ichite mgwirizano ndi mabungwe akukulu.
Kom bvuto LA anamiwa MA press briefing anu nsitinaonepo itabala zipatso
Choti mudziwe anamiwa ndi mutharika pangani ndinuyo kafukufukuyo osati ena paja ndinu madolo aza ndenge nde ife tikuvera or mupitenawo ku mzuzu muka pangireko kampeni agogo anuwo paja nde alomwe anzanu
Komaso adawuxandani kuti athu wose anali mundegemo afa anadxiwa bwanji?
Mubweletse zoti inuyo mwafufuza otsati zawukalizo ngati kuli akukutumani sizipindula izi. tiyamba kukutsikani muli be fundo zothandidza amalawi
Uyuyu ndi dolo