Oyimba onse amanyoza Bushiriwa, nkhani,yake ndi umphawi. Iwowo amafuna kukhala oweruza?ine si fan wa Bushiri and i've never been. Koma sindingamamuweruze.
Thanks for your true report about the Prophet Shepherd Bushiri and his beloved wife (Prophetess... As well as the Malawian musicians who composed their music despising, criticize, or contempt the Prophet Shepherd Bushiri!!! Anyway... Only God knows... HE'S THE RIGHTEOUS GUDGE IN HEAVEN AND AND ON EARTH.
Chimandisangalasa ndichoti bushiri utsogoleri ali nao sapsa ayii. Anthu ndie amathoka zaiye siku ndi siku. Koma mumpeza Alii pee . Iye bola ubale wake ndi mulungu uli bwino
This is true 💯💯💯💯 There is no way to like him this is Deval stan blood money God will fire him 🤞🤞🤞🤞🤞 he must repent en come back to Islam the truth he knows en Islam is straight way to go pradise plz plz bushir come back to Islam before judgement
Ananyozedwa yesu Christ bushiri ndi ndani oti asanyozedwe??? Chomwe muziwe zonse ndi zosala ndalama kuimba bwino kutchuka kulemela koma ngati zonsez tikupanga yesu mkati mwathu mulibe mmmmm tiyeni tigwile yesu molimbika basi ,,
Bushiri is man of God why God created us on his image don't judge. Just saying is not man of God 1. Ur selfish 2.wachokapo pamaso pamulungu Only God will justify us let love one another don't trust a man trust in God.
Zikomo poonera, chonde Ngat simunachite subscribe.. kumbukiran kutero ... Muchite like ...video iyi .... Zikomo
Akupanga sanjechabe
👍
1qq
@@starlonjamusHy Hy hyhy
😊😊😊😊😊😊😊
Oyimba onse amanyoza Bushiriwa, nkhani,yake ndi umphawi. Iwowo amafuna kukhala oweruza?ine si fan wa Bushiri and i've never been. Koma sindingamamuweruze.
True bro
Mbuzi iwe umanama......usiye kupanga za anthu
Kodi bwanji mumazimva kuzindikira bigy kungofuna basi kulimbana ndi oyimbawa muungofuna kuwalakwitsa aaaaaàh
Very much Best bro please ceep it up good job bro
I will try my best
Piksy didn't liar he only says the truth moreover that song of him it's my favorite song....akutithera mtundu m'malawi ameneyo...#MartseKeepRip😥
Pakut tilibe mphavu zopangila judge km mmmmmm
Thanks for your true report about the Prophet Shepherd Bushiri and his beloved wife (Prophetess... As well as the Malawian musicians who composed their music despising, criticize, or contempt the Prophet Shepherd Bushiri!!! Anyway... Only God knows... HE'S THE RIGHTEOUS GUDGE IN HEAVEN AND AND ON EARTH.
Proudly you my brother " nd nkhan ngat zmenez 🤟
Love it
That’s true, blood money. Magician full time.
Pastor David Kalirani Amayenera kukhala pa number 1
zofotokoza zanu zili bwino,ndizosakolana zachindunji bwino bwino.mulipo awiri ndi big mani enake samazitchula dzina lake .
Mkulu wa bakili Muluzi tv
A Malawi ife tilibe ulemu Mr Bushiri zawo dzidayela khale chofunika ndi ulemu basi monga ine ndikuti ulemu wanu mr Bushiri .kodi A Malawi tinakhala bwanji munthu aliyitse akalemela.ali ndi vuto
That’s true, Bushiri is a magician and I can’t understand how people are so brainwashed.
Nice one brood good work
Ndi zoona bro
Mwaitha bro muzibwelabwela
Best one bos
That's very gorgeous
Major one is Great
Koma Mthuzi ija simaseweratu 😂🙌
Anaswa
True chilugamo akuchiziwa iye urendo wa kumwamba ndi one one so let God be God
Keep it up
proud to him man of God...enawa yakula ndi nsanje...m'nyamata ali ndi mphatso ya utumiki uyu congratulations to major 1
Ndazkonda❤
Kodi ndindan amene samaziwa zot namadingo ndi bushir amadana
Muzibwezerabwera ndi nkhani ngat izi
Wasatanic uyu, ngozi mmene zikuchitikira ku malawi mukuyesa ndi chani, ngozi zoopsya zikuchitikazi chibwerere bushiri kumalawi, magazi akuwukha mwakathithi anthu akufa moopsya and tinanena bushiri atangobwera ku malawi, kuzichitika ngozi zoopsya munthu Wasatanic ameneyi akabwera.
True that brother
Yes was satanic uyo too since Ali ku Malawi everyday I hear accident why her please bro don't defense him hey,but follow Jesus Christ not men
I've ukutiuza za bushir KT titaninaye
Moyo ndikamozi ndagwirana ndinamdingo
Atapempha ndalama ndikuwakaniza amangotukwana. Moses makawa anavomera kuti ndi mfiti pa radio.
I like him, he has a humanitarian motivation, big up Shepherd Bushiri. Ngati zintchito ndizonyasa kuseli let God do His of Judging
Km mwatzindkilisa zambili man sam
Nanga iwe ukt bwanji
Ine ai akuziwa ndi Yahweh
TNM super rige malawi
Mukasowa chati usamalimbane ndi man of god
Fire up otsogoleri
Ndimamukonda Bushiri chifukwa samanyoza munthu sayakhula mau opusa kwa munthu. Inu muli Holly lnu mukumaimba nyimbo atsikana atavula ndee oipisisa lnu mwawalimbikisa athu kut God will bless them kapena mwawatengerathu kwasatana
Timakunyadilan bro nkhan zkumveka bwn kwambiri✊👏
Piksy ndi mfauna oziwika ndi bouma😂
Tnx for the good report
Enewa ndi zanje
Tose tapachalu chapasi ndise wakuchimwa Bushiri nayo wali ngat lwee pala wamanya lchi suzapanga zamuthu uzamukonda kwa mbiri. God bless Bushiri so that forex yisamasowe lfeso tikapulumusike
Machitidwe awo abushiri ndi amene tikuti samapemhphera mlungu ndipo ine sindizawakhulupirirapo ata
Alandililatu pasipano ameneyo kumwamba kulibe mark my words
Ineso chimodzimodzi alikuti Gracy Chinga cz of him ulemuumene mukuunenawo ndiyekuti mphotoyake
Ndayikonda so much keep up agood work
Nambululuka, mwaiwala kuti amambululuka koma alibemapikp .
keep it up .though am late to comment
Thanks so much
Nyimbo ya namadingo ya wabwela muli uthenga wabwino kwambiri ndipo kwa munthu wawumunthu pamenepo Palibe vuto lililonse 🤔🤔
Komatu bushir ngodekha akayankha ndiye kuti zavuta mmmmh
ATHU AMAMUNYOZA BUSHIRI CZ CHUMA CHAKE CHOCHOKERADI KWAMULUNGU (ziwan kuti Dziko lapasi limadana ndizochokera kwayehova}
Ndizoonadi anamunyoza prophet shepherd bushiri
Iweso uyambe kumunyozako
aMalawi timakodwa wina akamavutika
Nde kuuluka mwamba ndiphamvu yaumulungu ndiyesu yekha adapang zimenezija aise plibeso akuenera kupang paziko lapasi
Chimandisangalasa ndichoti bushiri utsogoleri ali nao sapsa ayii. Anthu ndie amathoka zaiye siku ndi siku. Koma mumpeza Alii pee . Iye bola ubale wake ndi mulungu uli bwino
Mulungu wake utii nanu kutengeka ndi zili zonse
@@mastersubiri7934 Mwandifusilako boss!!
Umakwana sam
I like him he has a humanitarian
pamenepo zoyamikila zake ndi ziti
Namadingo sanalengezepo kuti wasiya kuyimba nyimbo zauzimu
Watch my next video
Am still love bushiri
😂😂😂 kodi zotelo
Ose oyimba sangakhare obonza koma ndi zen zen izi
Fact👍
Number one bushili
Za zii kumangolimbana ndi anthu, that's sighn of poverty 😢
Great
Simungapezemo ndalama
Bushili ndinthu wabwino kwambiri
Haji❤
Lelo apiksy omweo kulandila ndalama Za yemweo akafuna kupepha kumangopepha Osama lankhula zopusa amafo nde awo nawo Ali khwekhwere konko
God will judge am just a mere person and our lord said let millet grow together with glass separation shall be done at the end
Ngati ndi wasitaniki mulung ndiye adzamuweluza, osati ine kapena iwe, chotsa chitsotso chili mmanso mwako, uwona bwanji chitsotso chili mmanso mwamzako, chako usanachotse.
Ayizikomo
Mmmmmmh mmmmh ndizapamwambadi well explained
Thax for information❤
Muchedwa nazo limbikirani ntchito
😂😂😂😂😂 chilungamo chimawawadi anthu a bushili akuwoneka olusa tuu samala aise
Zikomo kwambili sam malvitha zaveka bwino
zikomo mupitize kusokola nkhani zotele nizofunika koposa
Nice video
Proud of u
Anthu timakhulupilila ma prophet omwe anamwalila koma munthu yemwe timamuona zimakhala zovuta kukhulupilila komabe Pali mau Oti munthu sachuka Dela la kwao anthu azakhulupilila kuti bushiri analidi munthu wamulungu atamwalila ambili omwe Amati bushili simunthu WA mulungu sawelenga malembo oyela ngati ndioipa mulungu ndiyemwe angaone kuti akuchita choipa osati inu AI
Athu ena samakodwera akamachita zabwino padziko rapasi mzawo.
BUSHILI NDI MUNTHU WABWINO KWA MBIKI OK
God have mercy on you
Adha pasanapako ndwe galu kwambili Kod kusowa nthito ndkomwe kukuchititsa eti
Adzabwera ngati akhristu koma kuti adzanyenge ochuluka.Mawu awa ali mu bible koma anthu eti kakakakaka
This is true 💯💯💯💯
There is no way to like him this is Deval stan blood money God will fire him 🤞🤞🤞🤞🤞 he must repent en come back to Islam the truth he knows en Islam is straight way to go pradise plz plz bushir come back to Islam before judgement
Koma ndiye
Osamanyoza atumiki amulungu
Pwedo
Ananyozedwa yesu Christ bushiri ndi ndani oti asanyozedwe??? Chomwe muziwe zonse ndi zosala ndalama kuimba bwino kutchuka kulemela koma ngati zonsez tikupanga yesu mkati mwathu mulibe mmmmm tiyeni tigwile yesu molimbika basi ,,
Bushiri is man of God why God created us on his image don't judge. Just saying is not man of God 1. Ur selfish
2.wachokapo pamaso
pamulungu
Only God will justify us let love one another don't trust a man trust in God.
Love it
Be careful with a word of God and don't make a mistake to follow wrong things that you will know that this is a wrong. read jobs 13 verse 14
Like
Ina ija amati musamamange nhumba kwapongozi
Moses Makawa anavomereza kuti amatamba pa radio. Pamenepo wasatanic ndi ndani? Bushiri sindimamutsata koma Bushiri sananene kuti iyeyo ndi otamba.
So nice
Only God knows
Sanamunyoze koma chilungamo
Vuto anthu amafuna azikhala mbali ya olemelayo which is totally wrong
I have no respect for the magicians. I can’t understand how people are so brainwashed. God help us.
me too .
Sure
Bushiri Salimbana ndi mafana opanda vision
Ndiwe chisiru iwe chikukukhuza ndichani, or ine ndithanso kuimba zomwezo chifukwa iwo apulofeti anuwo ndiaboza
😂🤣😂
Tikufuna Ena ngat mbiri ya bushiri