Kom mavote awawa ngt sangayendeso bwino ndekut mau tilibe ife anthu osauka cz akusangalala ndiandale okha bc kom Malawi ikubwera munthawi ya Tsamunda😭😭😭😢❤🙏
Nde HE Dr Joyce Banda zikumukhuza pati munthu wachipani china aaaah koma this is cheap propaganda.nde WhatsApp call imakhala nde end to end encryption nde inuyo yagwela kwa inuyo how???
Koditu limpopo fm si ya mcp ndi anthu amalawi akuvutika ndiye inu a Congress musamabwere ndi ma coment amanyi mungotuluka we support nthanyiwa no matter what wamva iwe.
Zambiri mwa nkhani izi zilibe umboni zimafunika kuti muziwonesanso proof kuti audio ndi iyi other wise it's just a propaganda nkhani zopanda umboni, we must our brain sometimes to think about these things
Zekariya 11 15 Pamenepo Yehova anayankhula nane kuti, “Tenganso zida za mʼbusa wopusa. 16 Pakuti ndidzawutsa mʼbusa mʼdzikomo amene sadzasamalira zotayika, kapena kufunafuna zazingʼono, kapena zovulala, kapena kudyetsa nkhosa zabwino, koma iye adzadya nyama ya nkhosa zonenepa, nʼkumakukuta ndi ziboda zomwe. 17 “Tsoka kwa mʼbusa wopandapake, amene amasiya nkhosa! Lupanga limukanthe pa mkono wake ndi pa diso lake lakumanja! Mkono wake ufote kotheratu, diso lake lamanja lisaonenso.” ipite kwa apule
Kodi mukamati dzikoli akuliva kuwawa ndi Anthu akumpoto ndi akumwela apakati Fe sugar tikugula 200 kwacha thumba lachimanga tikugula 5000 nanga feteleza tikugula 20000 tamdimasulilani ine chifukwa kunena zoona aliyese akuvutika chifukwa cha Boma ili ndiye mwina tili ndi zigawo zapakati ziwili pa malawi. Pano koma naa dela lakwathu palibe akuva kukoma
Nde mfuti kuphela anthu kumalawi mesa Malawi ndiziko kamtendele😢😮😮 zimenez zosathek ife tikamuteteza President wathu Bonkalindo❤🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Ndipo mulungu akuone iwe chakwera ife tizimva kuwawa iwe uzinjoya zoona mulungu ndi mulungu
Am not sure if MEC will do good for all malawians
Olo atazabela tizavotanso zomwe anawapanga anzawo a dpp nawonso azaziwona zomwezo mark my words
Tithokoze ntchito yabwn a Comrade Ntanyiwa ...km pena zikumaoneka ngt propaganda mukamanena cfkwa simukumatipatsa umboni ogwirika Mr Ntanyiwa mwachitsanzo what's group mukunenayi pakanakhala voice yotsimikizira zimenezi wosangonena ndi pakamwa panu ai km pena muzitipatsa umboni wogwirika ngt mmene amachitira wa Bakili Muluzi.
All plans will cancelled in Jesus name amen
Ayelekeze kuzaomba chipolopolo, pa 8 pano apeza polekera. Tili pa sewu pa 8 pano ngati amapha akape pa 8 pano.
@@SifatiMoses 0
Amen
Amuphe Bon Kalindo awone momwe Malawi 🇲🇼 iyalukira kuzakhala nkhondo ya mipaliro
Angayambitse nkhondo ndani?
Following from south africa
With respect Mr Ntanyuwa, no one will reward u only God knows how much to reward u my brother
Mayi uyu ndiwoyipadi mtima eti Yoo 🙌🙌🙌
But why can't you play the audio of their conversation timakusatilan koma zinazi timagona ngat mukakhala mwakhuta chabe
yes ndakunyadira sweet
I love Limpopo fm, Com Mtanyiwa, we love Bon the DC ng'alulisation K. Kalua i love Malawi's keep going God always flights for his children.
❤❤ antanyiwa pitilizanj ntchito yanu god bless you please amalawi let's fight for our country palibe angatimenyele dziko lathu please
Koma ntchito ilipo ndithu koma komaaaaa komaaa
anthu amisara mukuchuluka, komaso bwanji mukukhara alone nokhanokha? Ndiyet dpp sitivotera coz mukuonetsa kt dpp alone mumadya bwino eti?
Comr Ntanyiwa please keep the fire burning, Malawians deserves to know the real truth about SKC ,.the DC Bon Kalindo #MALAWI FIRST #LIMPOPO FM.
We're with you boss
Following from south africa tienazo comrade ntanyiwa
Kom mavote awawa ngt sangayendeso bwino ndekut mau tilibe ife anthu osauka cz akusangalala ndiandale okha bc kom Malawi ikubwera munthawi ya Tsamunda😭😭😭😢❤🙏
Ndipo ineyo ndimalira ndikupemphera, Malawi ngat bodza ichichi cha pasi pa nyanjachi chaisandusa Malawi kukhala dziko la umphawi komaso lopatsa mantha
@@cynthiakananji1608 end panop dziko lathu muli nkhondo yachinsisi imene akupanga galu ameney Dairy kupha anthu😰😰😰
Matishit ayambile komwekuno am here at cape town DC samukwanitsa asake wina
Ludo NDI UTI ndizachindemo
No more secret on ground nowadays 😂😂😂
Osaopa ,osatopa ,osafooka Mademo tichita mosogozedwa ndi Mulungu osaiwala ku vala Mask ku ziteteza komanso kuvala zovala zofanana ku avutike pofunafuna munthu yemwe akumufuna kumuchita chipongwe moto kuti buuuuuuuu❤❤
No wonder Joyce Banda adakali ku Alliance akufuna azipanga zauchitsiluzi.
Mumtanyiwa gwirani ntchito yolemetsayi musatope mulungu akuthandize
Kwambli chifukwa mukasiya ndekut ife bc tathela pamenepo Mcp izakhalebe ndiulamulilo
Pitirizani big brother. Mukuchenjedza champhongo
Mmm
Vuto ndi amalawi tili ndi ufulu kukana chairperson wa mec koma tingovomeraza zili zonse
Ndipo Zoona amalawi tinachenjera moputsa aaa timangoziwa kutukwana
Ngt mukunama inuyo vuto ndiimeney kya tinakhala bwanj kya
Mwachepa nazo mafana
akungo usowa zocita chakwera pomalimbana ndi BON KALINDO musiyeni
God bless Malawi 🇲🇼
Ine ndagwirapo ntchito mu 2004 ndipo chisankho kudziwa yemwe awina ndi simple as long as zowelengera pa poling stains zisasinthe
Mizimu ya yathu sizingatheke Kuti tisamaziwe zinsisizi Lero Mulungu waziuluranso
Mbambande big man ❤❤❤❤❤
😂😂😂😂😂😂😂 koma ndale za pa Malawi zabwerera chikale
Kmn zomwe akupanga apule aaaaaa gyz simunthu wabwino uyu km chomwe iye akufuna azingowaophweza anthu bs mutu owumawo 😊😂
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂koma maboza akhala apa ai ayi dzinanamizani anthu akumulanje tcholo phalombe ndi chilazulu amenewa ndamene amabvela zanuzi zaziiu
Komanso inu mumataya thawi bwanji kumamvela ngt akukukakamizani? Pezani Zina zochita ife tizimvela mpaka chikangawa achoke
Ayi,, lord almighty will reward you
Ukunena zoona opposition party si akuonesa chidwe ali gone azawo akuyenda mipingo kugura anthu. Koma Mulungu kumwamba wava kulira kwa amalawi
Proud of you
Mr chikangawa chakwera ndi a gwape azakowo mukunama zisankho simubera tikubwera ku Malawi komweko Joyce Banda ndi
Joice Banda joice banda ukuwaphwetekesa amalawi matako ako
Akunamatuuu😂😂😂😂 the DC amusiye
Adzinamiza amenewo .Teroni ndithu akatengedweko
😂😂😂😂😂😂 u are, the man eeeee
Mmmmmm koma abusawa bwanji? Samauopa mkwiyo wa yehova
Takulandirani Mr Ntanyiwa mutimvesa kukoma
🔥🔥🔥🔥🔥🔥👍👍👍
mulungu wanthu siokufa ndiwamoyo zizitheka zimenezo
Koomatu kuli zinthu...ndalama zija .,.mmhuu
Yeah 😅 zikufunikadi tidzichangamuka a Malawa osamawopa yeah
Mukuluza track tsopano ndi mabodza anuwo aaaaa ,munaphunzira mpaka pati,mmmmmmmm mupusatu
kanyereniko uko
Pliz Comrade release the audio
Chete ana a peter munthalika ndipo satibera ayi
It's a sign of umbuli kumavera zopanda mutu izi. Tipase umboni iwe. Osatipasa meeting yo bwanj tiione
Antanyiwa t shirt musamuphonye Lezala kumachinjiri kuno. Thanks
Ntanyiwa koma inu mulimbavinu kkkkk....anthueatu ndiwoyipa kwambili
Ndiye Ali busy mpaka watsup call
Anthuwatu sakugona tulo
Mulungu si munthu mark my word
Mulungu watuma inu kuti muliwombole dziko lamalawi eish popanda inu sindikudziwa kuti zikanakhala bwanji mmmm osatopa please 🙏 please kumenya nkhondo ngati ya family yako 7:20 ukumenya ya dziko .Mulungu sakusiya choncho ndithu
Timakunyadirani a comrade ntanyiwa chakwera ndi a gwape azakowo mukunama mavoti simubera
Aululeni,tikufuna president owina mwachilungamo, Mulungu alipo kumwamba and tipemphera atikwana anthu amenewa
Limpopo yayamba bodza inu Rudo ndimpongozi wa chakwera ndy atuma bwnj boyfriend wake kkkkkkkkkkk
Nde akakhala mpongozi sangakhale ndi chibwezi???
Aunt joy nawonso
Ma audio muzitumiza ngati ma umboni
Ponyelela pa president chakwela fiti mulungu azakulanga
Mademo alipo wa polisi aliyense amene akayambise zopusayo zikamuonekera be owned
Nonse amene mudamvotera M.C.P ndinu zisilu za wathu mukupha anthu, kuba,kuonong,a
Ndipo zoona lne ndinavota ndinali ndilikumalawi Koma pano ndilikuno kujoni
Koma pano ndilindimaganizo kwambiri Kut ndikanadziwa ndikanangosiya osavota chifukwa ndinavotera mufiti
Apolice amene ananyamula machine km akuzuzikaso ndimunthu uyu chakwera nonse mitumbo yanu apolice ndimunthuso ameneyu ot adzalamuleso dziko lidzafika pat mbolizanu
Kkkk koma palibe chinsisi pa dziko lapansi
😂😂guys anyamata awa ulemu wawo
Kkkkkkk muli bhoooo kwambiri munthu wakulu
Jesus the nazarene knows everything chakwera you will immediately face the consequences
Achita bwino kwambili ayambile iweyo kukupha 😅😅😅anthu omvetsa chisoni inu mufa mu zomwezo
ndpo maraw turo siizatheka
Nde HE Dr Joyce Banda zikumukhuza pati munthu wachipani china aaaah koma this is cheap propaganda.nde WhatsApp call imakhala nde end to end encryption nde inuyo yagwela kwa inuyo how???
Koditu limpopo fm si ya mcp ndi anthu amalawi akuvutika ndiye inu a Congress musamabwere ndi ma coment amanyi mungotuluka we support nthanyiwa no matter what wamva iwe.
😂😂😂ana achepa
Zambiri mwa nkhani izi zilibe umboni zimafunika kuti muziwonesanso proof kuti audio ndi iyi other wise it's just a propaganda nkhani zopanda umboni, we must our brain sometimes to think about these things
Zekariya 11
15 Pamenepo Yehova anayankhula nane kuti, “Tenganso zida za mʼbusa wopusa.
16 Pakuti ndidzawutsa mʼbusa mʼdzikomo amene sadzasamalira zotayika, kapena kufunafuna zazingʼono, kapena zovulala, kapena kudyetsa nkhosa zabwino, koma iye adzadya nyama ya nkhosa zonenepa, nʼkumakukuta ndi ziboda zomwe.
17 “Tsoka kwa mʼbusa wopandapake, amene amasiya nkhosa! Lupanga limukanthe pa mkono wake ndi pa diso lake lakumanja! Mkono wake ufote kotheratu, diso lake lamanja lisaonenso.” ipite kwa apule
Ndipo mpaka kuvulidwa zovala?mlungu aliko ndipo mlungu azayankha.
Nanga pa chilimwe mumati bwanji
Ok
Malawi wathu ali moto
Kuyankhula ndy mukuyankhula ,koma vuto ndatsogoleri athuwa sakudzuka,ativulalitsa
Timakunyadirani a Limpopo
Tiye. Nazo muthanyiwa
Zoona a opposition akugona kwambiri
Koma mfiti Chakwera mulungu akukanthe sure
Naiyi yokha antanyiwa mwatinamiza chifukwa ngati mumamcera olo inali WhatsApp call bwenzi mutapanga record kuti a Malawi tizimvela ndikuti anthuwa ayalukedi zenizeni. Mesa samakupezani? Ndebwenzi tsiku lina mutawaika pa air ife ndetingaturukedi mwaunyinji not like this sizikubebanso
awatu tithana nawo gen z sakuyiziwa ndipo sitizawapha Loma stroke😂
Ife chonde nafe tikufuna ma T Shirt ya MALAWI FIRST.
Koma anthu muli ndi bodza
Muthu ukuona kuti munthuu ndi wabodza osamataya thawi yako ndi muthu wabodzayo bola osamavela program yake
Kodi mukamati dzikoli akuliva kuwawa ndi Anthu akumpoto ndi akumwela apakati Fe sugar tikugula 200 kwacha thumba lachimanga tikugula 5000 nanga feteleza tikugula 20000 tamdimasulilani ine chifukwa kunena zoona aliyese akuvutika chifukwa cha Boma ili ndiye mwina tili ndi zigawo zapakati ziwili pa malawi. Pano koma naa dela lakwathu palibe akuva kukoma
Kkkkkk agwa nayo achakwera
Mulungu odziwa kuteteza azikutetezani a mtanyiwa
Joice banda upole moto panyini pako
Wapha chilima ndi anthu onse anali mu ndege ija ndi chakwera, Joyce nayenso ali mommo anthu a satanic Inu nonses
Hmmmm guys zinazizi mungofuna ma views eti??? Nanga ndi Boni yemwe kuchita kumusonkhanisila mfuti? Munthu wakufa kale uja inu?
Palibe kubera mavoti sitifuna Malawi akhale wa satanic zidzitheka