PAC says, "Proverbs 27:5,6, Open rebuke is better than secret love.(A love that says and does nothing is not as valuable as an affection that rebukes.)vs 6.Faithful are the wounds of a friend;but the kisses of an enemy are deceitful.(A "friend" who will kindly tell you of your mistakes or faults is not destructive,but rather helpful [faithful].Conversely,one who flatters and kisses proclaiming everything to be wonderful and well,when in reality,it is not,is said by God to be "deceitful" and therefore ,an "enemy. ")
RATING YA MALAWI WA LERO MALINGANA NDI IZO TAKUMANA NAZO [MUZOBVUTA & ZABWINO ] 🇲🇼✍️TILI PA 82 % VIVA MALAWI.. Mmmm UKIMI NDI BUSINESS... OSANKHALA DZAKAKA/ UDZAKWAYE / ALENSI... TIYENI TIKHALE TONSE NDI CHIDWI CHITUKULA MA BANJA ATHU NDI DZIKO LATHU.. mosasudala NEEF: AIP!: ZAMANJA LENDE... AYI !! Just work extra harder in our Fields k o m n s o KUKONDA WOTILAMULURA POPEZA ENA CHITUKUKO Chao Mmmm MCHAPAKAMWA... KOMA Mgosatha pa Ground 😅🗣️ PRAYERS 🎉🖐️👉👍🇲🇼
komatu siyense angatsekule pakamwa motsutsa or kuzuzula boma kut ndi cadet cuz at the end of all Malawi ngwatose so ndale zili apo tose tili ndi udindo kumpanga Malawi okoma
💺🙏A PAC AMATIYIMIRIRA TONSE AMALAWI !! A PRESIDENT DR LAZARUS M CHAKWERA VIVA AMAYIMIRIRA AMALAWI TONSE MONGA PRESIDENT WA DZIKOLI 👍🇲🇼ZOBVUTA IZO TAKUMANA NAZO MDZIKO MUNO ZATIKHUDZA TONSE KUPHATIKIZA MKUZIPANI ZONSE . MABVUTO ENA TILINAWO MDZIKO MUNO MKUSAKHULUPIRIKA KWA ENA PAKATI PATHU Maka NGATI PAKUBVEKA ZA KATANGALE, KUSADZIKHUTHULA PA KAGWIRIDSE KA NTCHITO ZATHU, ULESI , KUBA, UMANJA LENDE, UNYOZA UTSOGOLERI MCHOLINGA CHOGWERSA CHUMA CHA DZIKO LINO. PAMENE A PAC ATENGA MADANDU ATHU KUPEREKA KWA A PRESIDENT MKOYENERA IWO A PRESIDENT ATAYESETSA KUKONZA ZINA MZINA KUTI ACHITE BWINO KUTI U PRESIDENT WA U MCP UPITILIRE. MONGA BWENZI , A PAC AKUTIWUNIKIRA KUTI TICHITE BWINO MDZIKO MUNO NDIYE KUTI PALI CHIBALE ! UMODZI POPEZA ZABWINO ZOBWERA, A MALAWI TONSE TIPINDULA. ✍️🎧,NDIPO UMPHAWI WA NJARA ; MAFUTA! MAGETSI! ULIMI! MISEU ! NJANJI ! CHITETENZO CHA MA ALLUBINOH ! UMODZI PAKATI PATHU ! KUTHETSA KATANGALE / KUBA ... ZONSENZI MKOYENERA KUCHITAPO MPHAMVU KUTI ULAMULIRO WA UTSOGOLERI WA A PRESIDENT DR LAZARUS M CHAKWERA 💞 UPITILIRE KUPANGA ZAKUPYSA ZOPINDULIRA BOMA LONSE IFE TONSE . POPENZA AZATHU AMATI * WAKUTSINA KHUTU NDI MNANSI .. !! * NDIPO AZIPANI ZOTSUTSA MGOSAYENERA KUSANGALALA NDI MA > SAKOLINE! ZINKHONDO ZA KU RUSSA/ UKRAINE!! KU MOZAMBIQUE!! KU ISRAEL/ MA PALATINA! KUPHEDWA KWA MA ALLUBINOH!! KUSOWA KWA FOREX !! NDI ZINA ZOTERO !! TIYENI TIYAMIKANE PAMENE BDIKOLI LILINKUYENDA BWINO!!. NB UKAKHALA WA NKHAZA PA UCHIPANI ! MDZIKO ZIMADZIWIKA... !! TIYENERA KUMAKONDANA NDI KUMAPEPHERERA DZIKO LATHU KUTI TONSEFE MULUNGU APITILIZE AKUTIKONDERA . PRAYERS 👍🙏
yeah koma tizitelo for the better future as a country not mmene zukhalilamu , tinene zoona Malawi sakuyenda mosonyeza tsogolo labwino nde Pena ndibwino wena akamatsutsa or kuzuzula kumanvera otherwise boma ndilomwelidi koma ntsogoleri nde anthu adzasintha
PAC says, "Proverbs 27:5,6, Open rebuke is better than secret love.(A love that says and does nothing is not as valuable as an affection that rebukes.)vs 6.Faithful are the wounds of a friend;but the kisses of an enemy are deceitful.(A "friend" who will kindly tell you of your mistakes or faults is not destructive,but rather helpful [faithful].Conversely,one who flatters and kisses proclaiming everything to be wonderful and well,when in reality,it is not,is said by God to be "deceitful" and therefore ,an "enemy. ")
Sitikusintha❤❤❤
Ndi omwewa afiti opemphela anatiika m'mavuto azawoneni, zaka 4 zonsezi amati Chakwera akuyendesa dziko bwino, ife a Malawi tikuvutika.
Boma ndilomweri la Malawi koma utsogoreri tisintha
Apule Koma chidodo pochita zinthu ziwapangitsa Kuti September ziwavute motsakaikitsa. Akonda anthu akuba mu BOMA kusiya kukonda ife anthu wobvutika
Leah umakwana
Honestly speaking, their intervening has come at an extra time that is almost towards the end of the game.
Leah you're such a talented journalists, recieve your flowers🎉
Inuyo a pac mykupindereza mamember ena Kuti atenge mipando yanuyo kuleperera kupanga convetion cholinga muzingokhalabe inuyo nde mphanvu zodzudzula azanu mukuzitenga Kuti aneneri onyenga inu
RATING YA MALAWI WA LERO MALINGANA NDI IZO TAKUMANA NAZO [MUZOBVUTA & ZABWINO ] 🇲🇼✍️TILI PA 82 % VIVA MALAWI.. Mmmm UKIMI NDI BUSINESS... OSANKHALA DZAKAKA/ UDZAKWAYE / ALENSI... TIYENI TIKHALE TONSE NDI CHIDWI CHITUKULA MA BANJA ATHU NDI DZIKO LATHU.. mosasudala NEEF: AIP!: ZAMANJA LENDE... AYI !! Just work extra harder in our Fields k o m n s o KUKONDA WOTILAMULURA POPEZA ENA CHITUKUKO Chao Mmmm MCHAPAKAMWA... KOMA Mgosatha pa Ground 😅🗣️ PRAYERS 🎉🖐️👉👍🇲🇼
Pac yopoyira komaso yokondera
Vuto mukusitama koma mafuso mukumakana kuyankha pac inatha imamufuna Peter
Kumwela palibe chimanga cholandila Ife timaona ngati kwaoko ndekomwe akupeleka mwakathiti
akugawa chimanga kumwela koha pakati sakugawa mchifukwaxchake aluzire kmaso kuchedwa kuthandiza
Akubwela tikuyandkila Ku vota bwanj akanangokhala chete bas ndpo Boma Lina likalowa azakhaleso chete bas
A pac atutumuka akuwona kuti zindu zitha kuwavuta ku sogolo kuno chifukwa akhala akubeleka bomali ndiye pali awasina khutu kuti achenjele chochi😅
😂😂😂😂😂😂 cadet walila
komatu siyense angatsekule pakamwa motsutsa or kuzuzula boma kut ndi cadet cuz at the end of all Malawi ngwatose so ndale zili apo tose tili ndi udindo kumpanga Malawi okoma
Awa amatengeka ndi mphepo,akaona anthu akutukwana boma nawonso amapita konko,pamene boma lachitako amayamikira koma mopanda nako chilimbikitso,saona m'mene zinthu zikuye dera pa dziko lonse lapansi ndikuyelekeza kwao kuno,komano kwakulu amaona zoipa Basi.
A pac ndiokondera inu
Leah umaitha
Zoona a PAC ndi okondera
Mkulu wa pAc wabwera mochedwa
Malikisio tipaleka tokha 0.7%
Chimenechi ndicho chilungamo chinenedwe
Atakhuta bwinotu kwambiri
💺🙏A PAC AMATIYIMIRIRA TONSE AMALAWI !! A PRESIDENT DR LAZARUS M CHAKWERA VIVA AMAYIMIRIRA AMALAWI TONSE MONGA PRESIDENT WA DZIKOLI 👍🇲🇼ZOBVUTA IZO TAKUMANA NAZO MDZIKO MUNO ZATIKHUDZA TONSE KUPHATIKIZA MKUZIPANI ZONSE . MABVUTO ENA TILINAWO MDZIKO MUNO MKUSAKHULUPIRIKA KWA ENA PAKATI PATHU Maka NGATI PAKUBVEKA ZA KATANGALE, KUSADZIKHUTHULA PA KAGWIRIDSE KA NTCHITO ZATHU, ULESI , KUBA, UMANJA LENDE, UNYOZA UTSOGOLERI MCHOLINGA CHOGWERSA CHUMA CHA DZIKO LINO. PAMENE A PAC ATENGA MADANDU ATHU KUPEREKA KWA A PRESIDENT MKOYENERA IWO A PRESIDENT ATAYESETSA KUKONZA ZINA MZINA KUTI ACHITE BWINO KUTI U PRESIDENT WA U MCP UPITILIRE. MONGA BWENZI , A PAC AKUTIWUNIKIRA KUTI TICHITE BWINO MDZIKO MUNO NDIYE KUTI PALI CHIBALE ! UMODZI POPEZA ZABWINO ZOBWERA, A MALAWI TONSE TIPINDULA. ✍️🎧,NDIPO UMPHAWI WA NJARA ; MAFUTA! MAGETSI! ULIMI! MISEU ! NJANJI ! CHITETENZO CHA MA ALLUBINOH ! UMODZI PAKATI PATHU ! KUTHETSA KATANGALE / KUBA ... ZONSENZI MKOYENERA KUCHITAPO MPHAMVU KUTI ULAMULIRO WA UTSOGOLERI WA A PRESIDENT DR LAZARUS M CHAKWERA 💞 UPITILIRE KUPANGA ZAKUPYSA ZOPINDULIRA BOMA LONSE IFE TONSE . POPENZA AZATHU AMATI * WAKUTSINA KHUTU NDI MNANSI .. !! * NDIPO AZIPANI ZOTSUTSA MGOSAYENERA KUSANGALALA NDI MA > SAKOLINE! ZINKHONDO ZA KU RUSSA/ UKRAINE!! KU MOZAMBIQUE!! KU ISRAEL/ MA PALATINA! KUPHEDWA KWA MA ALLUBINOH!! KUSOWA KWA FOREX !! NDI ZINA ZOTERO !! TIYENI TIYAMIKANE PAMENE BDIKOLI LILINKUYENDA BWINO!!. NB UKAKHALA WA NKHAZA PA UCHIPANI ! MDZIKO ZIMADZIWIKA... !! TIYENERA KUMAKONDANA NDI KUMAPEPHERERA DZIKO LATHU KUTI TONSEFE MULUNGU APITILIZE AKUTIKONDERA . PRAYERS 👍🙏
Kulira uku mutulukabe
Mwarembatu😅😅😅😅😅
Ndizoona boma ndilomweli tikumanena mobweleza bweleza kuti boma ndilomweli basi
yeah koma tizitelo for the better future as a country not mmene zukhalilamu , tinene zoona Malawi sakuyenda mosonyeza tsogolo labwino nde Pena ndibwino wena akamatsutsa or kuzuzula kumanvera otherwise boma ndilomwelidi koma ntsogoleri nde anthu adzasintha