MCP Ikufuna Imuzimise Petar Muthalika Kuti Asapikisane 😭😭😭

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 31 січ 2025

КОМЕНТАРІ • 53

  • @StephanoIssah
    @StephanoIssah Годину тому +3

    Mayz oro atatenga chileso ife wathu ndi adadi bs kkk

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  Годину тому

      @@StephanoIssah 💙💙💙💙

  • @CharlesMotloung-w3n
    @CharlesMotloung-w3n Годину тому +1

    Whether there's no Peter or Peter, but dpp will make it, win win❤

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  Годину тому

      @@CharlesMotloung-w3n until forever 💙💙💙💙

  • @MonijaKataika
    @MonijaKataika 29 хвилин тому +1

    Malawians we are God fearing county..tikupempherera ife dzikoli president tikusintha ife.. Mulungu akuoneni amene mukuzunza anzanu inu

  • @harrymicah6140
    @harrymicah6140 Годину тому +1

    Ndipo ukunamatu iwe APM alowa alore alore akane akane

  • @Ruthgomonda
    @Ruthgomonda Годину тому +1

    Ukunama adady 2025 Boma😅

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 3 години тому +3

    Peter muthalika is a retired president he cannot stand whether u like or not

    • @EmmanuelJoseph-lj5eu
      @EmmanuelJoseph-lj5eu Годину тому +1

      Who told you that he is a retired president?

    • @RosinaPatel
      @RosinaPatel Годину тому +2

      Who told you he's retired?

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  Годину тому

      @@EmmanuelJoseph-lj5eu ask him my brother

  • @RosinaPatel
    @RosinaPatel Годину тому +1

    Mukumuopa APM..mulungu sakulola

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  Годину тому

      @@RosinaPatel ndiponso sangalile

  • @fannyzimba149
    @fannyzimba149 2 години тому +1

    Agalu a MCP MWATIKWANA musatinyasepo kazingopakilani ulendo chaka ichi

  • @MarySinjirani
    @MarySinjirani 59 хвилин тому

    APM kaya wina afune olo asafune akutenga Bomaaaa chakwela kodi bwanji kuwakaka milila a Malawi tatitu sitikuyifuna watizunza kokwanila kafike bwino

  • @JamesYusufu-l6d
    @JamesYusufu-l6d 2 години тому +1

    inu. chakwela zikoli silake. zimuvuta yekha. koma pano sakuwinaso. zamuvita zimolino silske komaso kuno sikurwanda. kuno ndikumalawi.

  • @CharlesMoffat-u1i
    @CharlesMoffat-u1i 3 години тому +1

    That is no sense papa PM his has to stand as a president of Dpp and Malawi 2025 to 2035 🎉🎉🎉❤❤

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@CharlesMoffat-u1i 💙💙💙💙💙💙💙💙

  • @ElestinaMwanza
    @ElestinaMwanza 2 години тому +1

    Panyapanu amcp

  • @DavisSiyanidivis
    @DavisSiyanidivis 27 хвилин тому

    Zimene akuganiza a mcp ndi zopenga ,chifukwa President Peter Mutalika sakaimila ku nyumba ya munthu akuimilira amalawi. Ngati atumidwa ku satanic azikapha abale awo,zonunkha amalawi sakufuna anthu sakukufunani mukuwakakamira bwanji? Zopusa ife sitikufuna amalawi, Peter Mutalika ndiye amene ali chiyembekezo cha amalawi.

  • @FrancisMkwate
    @FrancisMkwate 2 години тому +2

    Trump

  • @DavisSiyanidivis
    @DavisSiyanidivis 23 хвилини тому

    Zikoli silanu musatitengele kuntoso mwamva a mcp ndi President wanuyo siife anthu anu ayi akutumani zolakwika satanayo chiseko chikupanani simunati

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 48 хвилин тому

    Age Limit tinathana nayo.Kungotu nfti zikuteri angofuna chisokonezo m,Dziko muno.Abale Atsogoleri mulibe Chisoni Kodi m,ene AMalawi tikuvutukila?

  • @EdwardChapola
    @EdwardChapola 2 години тому +1

    Koma ndiye ziliko

  • @HannahBambala
    @HannahBambala 2 години тому +1

    Akunama ameneyo tikulephela kudya ife aziona

  • @RahamahIbrahim-s3x
    @RahamahIbrahim-s3x 3 години тому +1

    Moyo wa munthu uli mmanja mwamulungu ambuye kumwambako amutetezela apm

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 2 години тому +1

    Bola tadziwa tizaona poyambira pake ,mwatchukatu koma

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 3 години тому +1

    Ambuye akuwateteza adad mulungu ndi wa dongosolo palibe chida chosula chimene chigwire ntchito pa APM mu dzina la yesu mwazi ukumphimba wa yesu

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@GraceLimani-zw7dx mulungu awakonde add💙💙💙💙💙💙

  • @EmmanuelChaluka
    @EmmanuelChaluka 3 години тому +2

    Tatopanaye chakwera

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@EmmanuelChaluka komanso sitikumufuna

  • @InnocentHassan-m3r
    @InnocentHassan-m3r 2 години тому +1

    Munya manyi nose

  • @LuciusScott-q7o
    @LuciusScott-q7o 2 години тому +1

    Pamsanapanu munya muona aima

  • @NdaonaMsowoya
    @NdaonaMsowoya 3 години тому +1

    Ziwasata okha mcp amufuse mble wake gagame ngati asamunyonge ndi mwayi wakw

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@NdaonaMsowoya komanso AWA angozinamuza💙💙💙

  • @BrightonMkandawire
    @BrightonMkandawire 3 години тому +1

    Mapwaka wa mcp

  • @EmmanuelGodfreynkhoma
    @EmmanuelGodfreynkhoma 3 години тому +2

    Sizingatheke mudzina la yesu

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@EmmanuelGodfreynkhoma ndipo zoona zake ❤️😘❤️

  • @FrancisMkwate
    @FrancisMkwate 2 години тому +1

    Jesus christ

  • @YassenYasin-v6o
    @YassenYasin-v6o 4 години тому +2

    Chikangawa akuchoka avuneaza fune

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@YassenYasin-v6o ndipo alibe thawi

  • @MosesTangwe-q8o
    @MosesTangwe-q8o 3 години тому +1

    Mulungu simunthu ndipo sangayang'anire mfiti kuzunza anthu ake

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @MosesTangwe-q8o 💙💙💙💙

  • @AlinafeJackson-d6v
    @AlinafeJackson-d6v 29 хвилин тому

    Adad omweo

  • @TinasheKamanga-p9c
    @TinasheKamanga-p9c 3 години тому +2

    Sizitheka ndinthuuu

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      @@TinasheKamanga-p9c komanso Ife sitilola

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti 4 години тому +2

    Koma sizitheza, munalanda Boma, muona nyekhwe simunati Mr Chikangawa, Viva Malawi 🇲🇼 ♥ ❤ Malawi 🇲🇼 🇲🇼 🇲🇼 🇲🇼

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому +2

      @@eunicesaiti ndipo anya.manyi ameneyo

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 3 години тому +1

    Mulungu alipo

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  3 години тому

      Ndipo awatetezera adadi

  • @AvicckyBanda
    @AvicckyBanda 2 години тому +1

    Alomwe mukulongolola kwambiri

    • @ShillaShamil-v2y
      @ShillaShamil-v2y 2 години тому +1

      Tiyenera kulongolora iwe umati

    • @N-PULSE-MW
      @N-PULSE-MW  Годину тому

      @@ShillaShamil-v2y ndifusileni Kwa ameneyo