Ine Ndimalimbana Ndi Area 30 - Bon Kalindo
Вставка
- Опубліковано 4 жов 2024
- On Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo, would like to comment on fake news and other issue including charcoal burning and the scuffle at MUA involcing MDF personnel.
Pa Nyasa VoiceBox, Bon Kalindo, akufuna kuyankhapo ndemanga pa nkhani zabodza ndi zina monga kuwotcha makala komanso chipwirikiti cha MUA chokhudza ogwira ntchito ku MDF.
#malawi
Ife a Malawi tizavotela bon kalindo ku sogoloko umbon ku bokina faso❤❤❤
I'm with you mr president bon kalindo
Bon kalindo umatiimilira keep it up
Your only our representative the Dc
The DC and Bakili Muluzi Tv our freedom fighters❤
Umskwans
Proud of you always our own president, president for us the poor Malawians, may God bless and continue to protect you, the Dddddd Cccccc!!!!
Booooooni Kalindo.... The DC
Kalindo best ever
Booooooooon kalindo 🙏
I like Mr kalindo
Ulemu wanu Mr President
Mulungu azimutetezela boni kalindo
God ahead u bon
Good luck bon
More fire Kalindo❤❤❤
kkkkkk kma Born kalindo nd 1 and he speaks the truth mmmm
God bless you Bon.Kalindo ❤❤❤
Asilikali amalawi olo atapita kukamenya nkhondo ku drc even pamozambik pompaapa, azikangophaphalisidwa/amangogwesedwa ngati ziwala, mbewa, iwo koma kutukwana ndikumenya amalawi anzawo nde Number one
❤
Ngati inu mwabisa ine ndimutchule bwaaa😂😂🎉
Bon kalindo ❤❤❤❤
Ben Longwe Ndiamene Amaba Magalimoto Ku South Africa Olo musamutchule Dzina Aliyense Akumudziwa Kuno Ku South Africa
Bon azatiyimilila upule ndithu mulungu azikudalitsa ndi lutha kut mwina make Malawi ixasitha
Tikanakonda kti 2025 tizavote ngakhale tili ku Johannesburg
Dc volume🎉
Mwana oopsa kwambiri olimbana ndi state house
Akakhala amene anathawa ku sasafilikawo musamudandaule, anafwifwa kalekale ameneyo ndipo zake zinada basi kkkkkkkkkkk, ndimwana opusa kwambiri
Ndipo tinalipila kaye Ku escom mpaka lelo atitizapatsa ndalama Kaye ...escom simasewela
Makala akalanda amapita nawo kt
Kodo a kalindo wa amangwira ntchito yotani tsiku ndi tsiku amadya amavala amasamba enafe tikuvutika kuti tidye iyeyu mwina ndi wa businesses kapena amalandila ndi kulakhula ku
DC🎉🎉🎉
Athombo thombo a billy malata mbuzi ya munthu yadya 6 million
Inu ndi anthu anthu sitigakusiyen mwapwiya dc
😂😂😂🎉 ziliko ziliko 😊
ulemu wanu KALINDO
The Dc
Chakwera sakuona zosez
Awa fodya amampweteka