MWANO OMWE APANGA A UTM__26 January 2025

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 4 лют 2025

КОМЕНТАРІ •

  • @Edward-y3v
    @Edward-y3v 8 днів тому

    Most welcome

  • @JamesALLi-m8i
    @JamesALLi-m8i 8 днів тому +1

    Yes Apm is coming soon to be president of this country Malawi 🇲🇼 🙌

  • @JoelTchuma-g3s
    @JoelTchuma-g3s 8 днів тому +1

    Mwaona ino Dr HKabambe kudzikweza kwanu!Awakubwerera kwao ku DPP.

  • @BashiruAdamus-l2b
    @BashiruAdamus-l2b 8 днів тому +2

    Kubwerera kwamakolo sikulakwisa ayi ndipo mwalandilidwa kwambiri

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 8 днів тому

    More 🔥🔥🔥 adadi tikukufunanidi tatopa ndi mavuto

  • @BakhePaliso-h8h
    @BakhePaliso-h8h 8 днів тому

    My vote 💙 my vote 💙

  • @JoelTchuma-g3s
    @JoelTchuma-g3s 8 днів тому

    A Henry,akoloko nonsenu yesetsani ,aYonamu nonse bwerani inu kuChikwawa bwererani APM Musamnyoze Iye ,Mulungu ali patsogolo pake.Mose ndi Yoswa walero.Pakati,kumpoto ndi kumwera onse afuna APM abwerere.

  • @chrischigoma5854
    @chrischigoma5854 4 дні тому

    Anthu adyela awa, zipitani ife tikhalabe chonchi komanso mudziwe tikuvutikila limodzi bcz nde mukuoneka opelewedwa ngati ine ndemwe

  • @lifayohbenson1994
    @lifayohbenson1994 9 днів тому +3

    Zikusiyana zomwe mwalemba
    Tidzasiya kutsata page yanu

    • @chrischigoma5854
      @chrischigoma5854 4 дні тому

      Ndipo zoputsa zomwe akumachita this days akumalemba Mutu osiyana ndinkhani cholinga munthu ungotsegula basi

  • @MarthaChigonero
    @MarthaChigonero 9 днів тому +2

    Zokongola

  • @Wyson-bo3sp
    @Wyson-bo3sp 8 днів тому

    Monga mulungu adatuma yona kukalalikila ku niniv iye nkuzemba koma chinsomba chitatumeza chidakamulabvulila mbali mwa mzinda omwe iye Yehova adamuuza kuti akalalikile, mulungu sathawika, chomwechonso nonse mudathawila ku zipani Zina dziwani kuti kubwelela kwanu ku DPP sinu ini ayi koma mulungu afuna kuti nonse pamodzi muthandizane kupulumutsa malawi yemwe lelo lino wagwidwa mu ukapolo wazaoneni.

  • @FatsaniDissi
    @FatsaniDissi 3 дні тому

    Guys mutu sukusiyan akutanthauza kt kucoka a UTM ku cipani cawo kupita ku DPP ndy mwanowo inu simukumvetsa Pati

  • @Maxielyies
    @Maxielyies 8 днів тому

    Powerful

  • @OwenJambo-g4m
    @OwenJambo-g4m 8 днів тому

    Kkkk

  • @LysonMkomadzinja
    @LysonMkomadzinja 8 днів тому

    Mukamati dpp singabweleleso m'boma mukutanthauza chani NGATI inuyo anthu oyipa a Mcp mwabwelelaso nde what more DPP? Koma ine ndiwa utm ndimangofuna kukozapo

  • @GiftHaward
    @GiftHaward 8 днів тому +1

    Tatoos ndi MCP we'll come a dad

  • @JoelTchuma-g3s
    @JoelTchuma-g3s 8 днів тому

    Mulanje wa khala wa moyo tsopano.Inu aku MULANJE WACHITA BWINO KUPEPESA.

  • @LysonMkomadzinja
    @LysonMkomadzinja 8 днів тому

    Komano tingokozapo kuti awowo sanali a UTM awo anali a Manganya ndepaja anathamangitsidwa chifukwa anali a Mcp amaona NGATI UTM angaipusitse

  • @Paul-q2p
    @Paul-q2p 8 днів тому

    Mutu WA nkhani mulembenge makola please

  • @laurentbutao4084
    @laurentbutao4084 8 днів тому

    Komatu mwalakwitsa Heading ife timatsatila UTM osati zomwe tikuonazi

  • @HildaMbizi
    @HildaMbizi 8 днів тому

    Vauchindere naleka kujula page yinu muli wazereza mwalemba utm uku VA dpp mwagongowesa namufumani

  • @FayazNhlema
    @FayazNhlema 9 днів тому +1

    Page iyi pang'onondipang'ono anthu asiya kuyipanga follow...aka ndi koyamba ndikomaliza ndasiya kutsitira page imeney.

  • @isaihmagani5697
    @isaihmagani5697 8 днів тому

    Kusonyeza kuti UTM ya Kabambe sizinthu alibe chikoka bwenzi tulandira alendo ochokera ku DPP komwe adaliko iyeyo

  • @CharlesMlenga-k4m
    @CharlesMlenga-k4m 8 днів тому

    MCP ilipheeee ikudziwa zochita inu batekesani

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 9 днів тому

    Mwano=kusiya UTM atasankhidwa ku convention. Koma panopa inu a DPP mulimbanne ndi SMARTMATIC yomwe inavotera kale Chakwera.

  • @Eqrah-hj2nu
    @Eqrah-hj2nu 9 днів тому

    Ok

  • @PreciousVungani-c8x
    @PreciousVungani-c8x 8 днів тому

    Mazila ako galu iwe zmenezi ndye zichani

  • @DimplesDumplingHouse
    @DimplesDumplingHouse 8 днів тому

    HOT 265 be careful

  • @Enock-gu5ff
    @Enock-gu5ff 8 днів тому

    Tiyeni tizinena zoona iyi ndi proof kuti arowadi ku dpp carakwika ndi cani komaso ambiri akubwerabe nde mutani

  • @YusufMoyo
    @YusufMoyo 8 днів тому

    😂😂😂😂😂 Anayika pusi nyumba

  • @ChilekeniNguluwe
    @ChilekeniNguluwe 8 днів тому

    😂😂😂😂😂 ndale zakumalawi ndi choncho.

  • @CharlesMlenga-k4m
    @CharlesMlenga-k4m 8 днів тому +1

    Koma alendo ake osasamba kkkkkkk or muphatikizane simumaka mcp ndi machine

    • @HopeLiwonde
      @HopeLiwonde 8 днів тому

      You will regret

    • @Stevekatiwa-tp3oq
      @Stevekatiwa-tp3oq 8 днів тому

      Machende ako uwonaso tili Malawi momuno tonse

    • @GrayManyeka-h7c
      @GrayManyeka-h7c 8 днів тому

      Mwanapiye wabwelera mmapiko amche

    • @HamitonFrank
      @HamitonFrank 8 днів тому

      Pamtumbo pakuda ngati tambala wakuda Chikangawa zithupsa

  • @RaphealKwelani
    @RaphealKwelani 8 днів тому

    Apa angochokelatu mbusa uja bas

  • @KennethChama-bc7ge
    @KennethChama-bc7ge 9 днів тому

    Koma anthuwa sanalembese sazavota

  • @RICHMONDGOON
    @RICHMONDGOON 9 днів тому

    ❤❤❤❤

  • @WilliamGama-w8m
    @WilliamGama-w8m 8 днів тому

    Why MCP is ruling again? don't cheat your self let us wait and see

  • @CharlesMlenga-k4m
    @CharlesMlenga-k4m 8 днів тому

    Agogo team kkkkkk dpp will never win again MCP pachiwongolelo

  • @WanangwaMfune
    @WanangwaMfune 8 днів тому

    Page yopanda nfundo kkkkkkk

  • @JohnfosterNkusengwa
    @JohnfosterNkusengwa 9 днів тому

    We are not here to sheck never what you need to know is that this is political manner oky we need food for our loved ones not party

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 9 днів тому

    Kwachema

  • @giftsululu4274
    @giftsululu4274 8 днів тому

    Diedly party
    Inu nda modzi agalu inu
    Boma ndilomweri

  • @kingkhudze7937
    @kingkhudze7937 9 днів тому

    chisankho chabwino

  • @BERNARDSIKWESE
    @BERNARDSIKWESE 9 днів тому

    DPP will never rule again