BRIAN BANDA KUPHAPHALITSA ZIMAFUSO -🤔🤔🙌🙌21 July 2024

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 14 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 55

  • @JumaGadaff
    @JumaGadaff 2 місяці тому +15

    Akayamba choncho dziwani kuti mulungu wamakamu ayamba kuwakantha inu mulungu awavula zovala onse akuimila MCP ife chete ndi umasiye wanthu amen 🙏🙏

    • @moosasinoya3307
      @moosasinoya3307 2 місяці тому

      May Soul Rest In Peace SKC😭🔥💪

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 2 місяці тому +1

    Mtsukuluzi simunampatse mpata kwambiri ngati mmene munachitira ndi Ndebvu za mwayi. Muzipanga balance a Brian Banda. Mwaonetsa tsankho

  • @MervinMwambinga
    @MervinMwambinga 2 місяці тому +1

    He can be a youth, well educated, good passions and visions but our constitution does not give power to Vp to decide and implement ideas. We have evidence, our lovely late VP SKC. He was our only hope for this country and no one else. Tiye tizinamizana chonchi basi.

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 2 місяці тому +4

    Skeffa chimoto wathadi eti mpaka afika apa kkkkk

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 2 місяці тому

    Big up brother man!!

  • @WilliamBandaWili
    @WilliamBandaWili 2 місяці тому +7

    Mcp ndiyakupha

  • @NelsonMarley-m6p
    @NelsonMarley-m6p 2 місяці тому

    Zimayi opusa chinkhope ngati mtengo wamulambe mxiew

  • @AisherKhaalid
    @AisherKhaalid 2 місяці тому +1

    Mayi Chikata my neba from Mzuzu

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d 2 місяці тому +3

    Satana amayenda ndi asatana azake amalawi wosazindikila kumasapota anthu akumpha amcp

  • @chitanibenito1109
    @chitanibenito1109 2 місяці тому

    AAAAAAAAA nthawi Yotani monse muja??? Mumba ndi chakwera amabera limodzi agalu amenewa shupitiiiii

  • @HarrietMtenje
    @HarrietMtenje 2 місяці тому

    Dzitukuko dzompha anthudzo alamulira inuyo

  • @macmsiska2937
    @macmsiska2937 2 місяці тому +3

    Mbava yayikulu iyo yikamayankhula m'maso muli gwaa

  • @PriscillaKhumbanyiwa-i1d
    @PriscillaKhumbanyiwa-i1d 2 місяці тому +1

    Anthu andale makonda kumuchula mulungu pafupipafupi mulungu akukantheni bava za mcp

  • @JaneMoyo-ws2di
    @JaneMoyo-ws2di 2 місяці тому +1

    Botolo la madzi okumwa muziliika kusogolo kwanu a Brian osati ku mbuyo or ku mohepete kwanu muziliona or mulibuzy

  • @LloydMkula
    @LloydMkula 2 місяці тому

    Akufuna kutumikila a chakwera not a Malawi ma delegates mazimvelatu

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza 2 місяці тому

    Ziyezekanani ku mcpkp uyaaa

  • @joeljere4385
    @joeljere4385 2 місяці тому

    Onse aku North okhaokha

  • @UseniMailosi
    @UseniMailosi 2 місяці тому +3

    Koma siteniwe muganise bwino sachakwela muiwale

  • @EnerstManess
    @EnerstManess 2 місяці тому +2

    N'gona zen zen

  • @CrispineBetha
    @CrispineBetha 2 місяці тому

    Akunama amayiwotu 2025 mcp mulibepo😂

  • @GiboTakondwa
    @GiboTakondwa 2 місяці тому

    Mwamvatu nokha akuti eyeyu akufuna azizatimikila achakwela osati amalawi

  • @kingsleymsampha2260
    @kingsleymsampha2260 2 місяці тому +1

    Mukupikisana kwambiri because you are in government now,, fact osati zinazo aaaaaah. We have also heads to reason.

  • @stevemtambalika
    @stevemtambalika 2 місяці тому

    Chikangawayu watha basi kkkkk

  • @FaheemChipojola
    @FaheemChipojola 2 місяці тому

    Amai awa nzeru alibe ndithu

  • @NthambiInvestment
    @NthambiInvestment 2 місяці тому +1

    Ngati mukunamizana zowinaso muiwale,, vote ya 2025 tikavotela kuchikangawa ,, MCP Pachilani muzipita ,,,,,
    Nanunso a skeffa ndi a mlaka plz plz ziyalondolelani anthu koyenela pl

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 2 місяці тому +1

    😂😂😂 thiraspot paka 1 mita

  • @inessmsiyambiri8517
    @inessmsiyambiri8517 2 місяці тому +2

    Nyero yako mzimai iwe ndithu

  • @Betty-fe9ql
    @Betty-fe9ql 2 місяці тому +1

    Koma ma comment a Brian mpake pena amankhoma 😅

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 місяці тому

    A Brian ndi a ndevu apatu tikudabwatu leroli kwabookatu Ku MCP money kkkkkk.eeeeee koma abaleeeee.

  • @DavieMoyo-pe8vn
    @DavieMoyo-pe8vn 2 місяці тому

    😂😂😂😂 nyamata WA vinyo Ku MCP Malawi ngosangaratsa

  • @DanielZitande-y1d
    @DanielZitande-y1d 2 місяці тому

    Abambo idzoo za ku chipani kwanu siii zotandidza a Malawi

  • @EDGARMPIKAMEZO
    @EDGARMPIKAMEZO 2 місяці тому

    A Mumba is very controversial, kudzikundikira too much. Ubwino wako amaudziwa ndi ena. Zikuonetsa kuti atasemphana nawo mwayi uwu atha kuukira chipani . He is too confident. He is not bigger than the party.

  • @alomuddin8801
    @alomuddin8801 2 місяці тому

    Mcp ya khanza yabweletsa njala mu dziko la Malawi chilichonse chinakwera mtengo,

  • @EnerstManess
    @EnerstManess 2 місяці тому +2

    Mbava

  • @andrewBwanaisa
    @andrewBwanaisa 2 місяці тому

    Mwagwa nayo nonse a mcp

  • @lupakishomalangaelix6606
    @lupakishomalangaelix6606 2 місяці тому

    Usi sakaimila uku?

  • @jamesmsonkho4830
    @jamesmsonkho4830 2 місяці тому

    Kkkkkkkkkkkkkkk

  • @LowanMasiye
    @LowanMasiye 2 місяці тому +1

    Boma ndilomweli

  • @giftmakoyo1441
    @giftmakoyo1441 2 місяці тому

    Amayi inu mmmm😢

  • @kingnavitcha6243
    @kingnavitcha6243 2 місяці тому

    Angalephere kuchitsa chipani choti ndi chake

  • @DjshukulanGift
    @DjshukulanGift 2 місяці тому

    Kamat uku sizitha bwino uku mungot phee

  • @tisuhmakhwah7085
    @tisuhmakhwah7085 2 місяці тому

    Woiphonya ati akufuna kutumikila chakwela not malawians.

  • @mussamapira801
    @mussamapira801 2 місяці тому

    Akuba okha okha

  • @AleksaWilliams-qc6cn
    @AleksaWilliams-qc6cn 2 місяці тому

    Zaziii

  • @ChimwemweChiwawa-g5o
    @ChimwemweChiwawa-g5o 2 місяці тому

    Amayi opusa

  • @KondwaniLungu-x5l
    @KondwaniLungu-x5l 2 місяці тому

    Anthu akewa sizothandiza ziko

  • @samuelosman3215
    @samuelosman3215 2 місяці тому

    Aaaa simulaka uyu?

  • @hopembendela
    @hopembendela 2 місяці тому

    iwe wakhutatu kondole eti

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw 2 місяці тому +1

    paja iwe dxina lako ndani

  • @IssaJohn-cb8vn
    @IssaJohn-cb8vn 2 місяці тому +1

    Kkkkkkk oyimba akumalawi

  • @michaelzuze6516
    @michaelzuze6516 2 місяці тому +1

    I regret watching this shit

  • @MarriamBakalie
    @MarriamBakalie 2 місяці тому

    Ndiwe galu pamodzi ndi akwanu ose stupid guy gud man for nothing.