Mulungu akutetezebe bro.Ntanyiwa,koma kungoziwa kokha sikuthandiza kanthu bwanji mupange njila ya action molumikizana ndi ma activities oima pa chilungamo,,mophatikizana ndi zipani zosusa,Namiwa Mulungu akuone
Mbuzi ndi amalawi.....everybody knows which gang killed chilima.... Commision of enquiry kungowabela amalawi taking chances for ignorant malawians....... After election anthu azakhapana yazikwanje live...coz mbavazi sizikulora kutuluka m'boma by fire by force
Amalawi simukudziwa mphamvu ya lilime tachuluka Onena zonyoza and yet tikuti tikufuna ntendere I don't think so tisamale kwambiri ndipo tisamalise kuti tikolore zabwino chifukwa tikuzala zonyasa kunene chilungamo, chakwera ndi woyipa koma ifeyo ma citizen ndife woyipisisa makhalidwe
Ameneyo ndye ntanyiwa 😅 kuswakuswa bas palibe kunyengerera iweyo unabwera kuzakhala 🙌 God continue keeping you safe in Christ Jesus Name
Akufuna atipusiyse nao commission of enquiry imeneyi,ndpo,more 🔥 🔥 Comrade
We are following
Koma aaaaa ayi
Ambuye akuonaa
Big up achalume
Matanyiwa God bless you keep it up
Ambuye azikutetezanibe ❤
Ulemu wanu Comrade Ntanyiwa. Timadziwa zooonadi kuchokera kwa inu.Inu ndiye maso athu a ife amalawi osaukafe. Ambuye azikutetezani nthawi zonse.Anthu awa omwe asakhidwa kuti achite kafukufuku wandege ife amalawi sitikukhutitsidwa nawo akungofuna kutipusitsa ife amalawi. Antanyiwa chonde ngati muli ndikuthekera kotenga black box yandegeyo teroni ndithu.Kuti akanyimbi amenewa ayaluke
mmaso mwanga ndikuona nkhondo Ku Malawi 😭😭😭😭😭
nkhondoi akubweresa ndi a MCP
mark my words
MAY YOU MTANYIWA BE BLESSED AND PROTECTED UNTILL EVER
Only radio we trust Limpopo fm
Comrade ntanyiwa kuno ku mulanje bale,amfumu achikandwe aonjeza chinyengo.kodi ndizoona subsidy azigawana anthu Zina limozi?
Chilungamo sichipezeka apooo mtanyiwa ❤❤❤❤ mumatiyimilila
Uhmmmmuu... Dziko lapansi.. womukhulupilira ndi Mulungu bsi... Even Limpopo akanaisankha.. bali chisintha
Koma ndikurakwa Ife tikulirabe koma sizitheka mulungu alipo kumwamba awulura chisisi😢
Ineso namiwa akundikaikisa
Mulungu akutetezebe bro.Ntanyiwa,koma kungoziwa kokha sikuthandiza kanthu bwanji mupange njila ya action molumikizana ndi ma activities oima pa chilungamo,,mophatikizana ndi zipani zosusa,Namiwa Mulungu akuone
Aikemo Bon kalindo kut tikhulupilire,namiwa wadya Banz
A Thawale omwe ali mu inquiry ndia mudzi umodzi ndi Avelentino Phiri,,, onse ndiakumchinji
Thanks comrade ❤❤❤❤❤❤
Amuchotse ameneyo akupanga zachibwana tikufuna chilungamo ife osati zoti atinamize ife ai 😮😮😮
is there to cover up criminals, let's hope koma ngati zili choncho tisayembekezere eligible results
Thanks Comrade ❤❤❤❤
We trust comrade m'ntanyiwa
Big up mtanyiwa
Komanso
In our culture
We need to
Consult a kumbumba then awoo pambuyo
Komanso aku mbumba a
Vomeleze
Then we can say we are agreed
Mmakwana bro
ntanyiwa umakwana more fire
Koma Comrade aaaa tiuzenizoona
Mbuzi ndi amalawi.....everybody knows which gang killed chilima....
Commision of enquiry kungowabela amalawi taking chances for ignorant malawians.......
After election anthu azakhapana yazikwanje live...coz mbavazi sizikulora kutuluka m'boma by fire by force
NGAKHARE MUTAGULA ANTHU WOSEWO DZIWANI KUTI A BANJA LA CHILIMA SAKUSIYANI AYI NDITHU NKHANI IYI SIYIDZATHA
Kuphulitsakuphulitsa
Ine ndine mmodzi mwa amene sindimagwirizana ndi boma ili, koma sindimagwirizana ndizimene Ntanyiwa amakamba, inayo ndi jealous, dolo ndi BM TV
Nkhala choncho ife tikumunkhulupilila
Ndie bwanji osamangolimbana ndi BM TV yako yomweyo bwanji
Kuyesesa bro umayesesa koma anthu ife kusamva
Amalawi simukudziwa mphamvu ya lilime tachuluka Onena zonyoza and yet tikuti tikufuna ntendere I don't think so tisamale kwambiri ndipo tisamalise kuti tikolore zabwino chifukwa tikuzala zonyasa kunene chilungamo, chakwera ndi woyipa koma ifeyo ma citizen ndife woyipisisa makhalidwe
Game on Mtanyiii
Namiwa ndanena kale kuti ngati anamiwa akupitira amalawi apite kaye kwa mutumiki wa Mulungu yasini gama akamulumbirise kuti apitira chilungamo ku inquiry apo bii ngati akukana namiwayo nayeso ndi mibulu yebiyeni. Koma namiwa ngati wadya ndalama Mulungu wamoyo akutemberera moyo wako wose uzaziwa kuti kumwamba kuli Mulungu. Chakwera sakuziwa kuti minyama yose ikuchitika ku Malawi ndi mukwiyo wa Mulungu koma sakufuna kulapa
Akudziwa Koma sakufuna kuvomeleza ndkugonja pamaso pa Mulungu
Kupusa kwa ife a Malawi tinapeleka mphanvu zose kwa mtsogoleri ngati Mulungu ndiyetu ndizimenezi akutidoda
A Malawi tilimbe mtima mabzi ataika saoleleka palibe chimene angayankhule wapha keliyara kupotsa opalatsa njinga😂😂😂😂
Namiwa dzimachende dzako kapusise amako😢😢😢 panya pako
Ndnkaona ngati Namiwa ndi munthu wabwino osadziwa kuti ndi satana weni weni
Ndipo press briefing yomwe apanga zana ija kkkkkkk aaah Ali kutali ndi chilungamo
komano commission of inquiries amayenela awayimise ntchìto anthu onse omwe akukhuzidwa ku chikena ku police mpaka order above
Abusa a Nyirenda zoona ndi inuyodi????
In poli-tricks they say that everyone has a price
Koma limpopo FM ndiya DPP.TSONO mukwanitsa kodi?
Mtsnyiwa💥
Namiwa mmmmmm
Ndizoona palibe chophindula olo chimodzi olo akuti pusisa kwambili
Auze comrade
Abusa a Nyirenda zoona ndi inuyodi??????
Boma Ia mcp ayi zikomo 😢😢😢😢
Tipemphe president WA seventh day Adventist church asalowe NAWO ntchito yobisa mwazi okhetsedwa CHOONDE Yehova akwiya nanu
Muuzedi ameneyu
Achenjeledi
Chimfine chavutanso atanyiwa
Ponyani messages koma kutethatu 😂😂😂 zovutatu.....
Iyetu kufuna kubisa chilungamo
Asiyeni adzikalumbira Mulungu yekha ndamene akudziwa zonse, pangatalike zidzawululika
Ikwayale imeneyo ilepheleke chifukwa athuo ndi osokoneza okhaokha
Ntanyiwa ndiiiwe Kape nawe umangozfuna ndalamazo at first ndinkakukhulupilira kma ndiiwe Zoba Shasha ndi Bakili Muluzi TV Inu ndiyopanda kalikonse mapwala anunso
Abusa a Nyirenda zoona inuyoo?????
Tsiku lomwe Ntanyiwa azapatsidwe ntchito ndi Boma anthu azanenanso kuti wadya ndalama...analipo achina mavuto Bamusi, Ben longwe pano mukuti namiwa wadya ndalama chifukwa sanakusankheni...Amalawi ndiovetsa chisoni coz amankhulupilira anthu omwe amawapusitsa...
athela kuwili ose samachedwa kufaa
Bola namiwa timamuona ndi maso koma iwe umangokamba koma osaoneka
Tsono nanga mukufuna chani amalawi.mesa munkati mukufuna achakwera akhazikitse commission of inquiry?tsono chalakwika ndichani kodi anthu inu.mukufuna chani?mukufuna moyo wa Achakwera kapena.
Ndipotu izizi ndiye zoona zokhazokha ndi ntanyiwa timupase ulemu
Ndimaona ngati tidikile Kaye ndicholinga choti tizaone zimene angazatulutse after kafuku fuku wa comission of inquiry yasankhidwai ,
Ndicholinga choti mafunso omwe tilinawo ngati amalawi azayankhidwa mu lipoti lomwe azatulutselo .
Ngati m'malawi wina aliyense akuzafuna kudziwa yemwe anamuletsa Richard chimwendo banda kuti asakwele ndege ponenakuti inadzadza , pomwe ndegeyo inali yokwela anthu 18 , koma panthawiyo inali itanyamula anthu 9 okha ,
Komanso tikufuna kudziwa chifukwa chomwe Chakwela analetsela anthu kuti asapitilize kufufuza ndege pachifukwa choti kunada itasowa ??
Komanso amalawi akufuna kidziwa chifukwa chomwe anampasila Chilima kuti akwele ndege yomwe inali yosakwanila zipangizo ngati black box ??
Komanso kayalidwe kankhani kakusiyana ponenakuti ndege inafika ku mzuzu ndikubwezedwa , pomwe wina akuti ndegeyo siinafike ku mzuzu , ndiye tikufuna chilungamo chiyende ngati madzi .
Zoona. Kuononga ndalama kwa anthu ogulidwa.
Popanda Limpopo amaliwife tingakhale ntulo kwambili
A a a a a chan? Oh😮😮
Sorry abraz ife timamuvera ameneyu
Koma chikangawa ai zicomo
Ndiwe wopusa kwambiri chifukwa mumaumiliza kuti ichitike ndiye aipanso.
Anamiwa ndimapasa ulemu koma zoti angafuse zoti achakwela anauza kt ndenge anaibweza kuzuzu ndan
Mwayambakotu kkkkk
Boma la Mcp ayi Zikomo😢😢😢
Namiwa ndi wa mcp sangatithandize muthu oyipa
Big up
Kuswakudwa😅😅😅😅😅😅
Uzinamiza mbuzi zizako garu iwe
Komaso inu aboma nose odzungulila Mitu inu mayi kaliyati thawi yoseyi ankhala ndimalemu chilima lelo mukwapekela Kuti akufuna kumpha chakwela Kodi inu mwadzungulila Mitu nose mukonena Kuti tikuwamanga chifukwa UTM ija mukuziwa Kuti mayi kungowuna chani palibe chadzelu mwachiona Kuti tiwanamidzile Kuti akufuna kumpha chakwela inu dzimenedzo mukuudza ana Koma samalani thawi ndikachisilu
Pena akuluwaa amanamaaa
Iwe tanena zako zoonazo chikangawa iwe
Ndiyetitani amalawi nkothekakutiathuwakuwaimisa ndikusakilamo ena
Ife pa mbuyo pa ntanyiwa basi
Ndipo ndizoonadi zili choncho kumene ndipo zinadziwika kt zitero
Palibe chimene tingaembekezere
Ntanyiwa ndi moto...
Wabodza uyu musamamvele amachita kutumidwa, naye amapezelapo mchere wake don't trust enewani guys
Namiwaso ndi kape
Zomvesa chisoni kwambili
Koma kulimba mtima kumalumbira osaopa Mulungu
Iweyo umaopa mulungu koma chigololo ndi ufiti sumasiya bwanji
Umakwanaa boss ❤❤❤❤
Chokaaaa iweee mbuli ya munthu
Bmuli ndiyinuyo machende ako
Kodi ukudwala matenda anji
Sukunama aise ndi mbulidi ya ku Limbuli imeneyi, udzingomva chizungu
Big up ntanyiwa