Thanks so much Dr we respect you from the past 80s and 90s. I hope these idiots has forgotten these because they are young. Keep it up to let us know the trueth
Akuti a boma mwaba 3 trillion ndipo mukubisa m'ma bank osiyana'siyana, mukumangira nyumba zibwenzi, zina mwasunga ku Cuba....koma mukupangiranji izi pomwe a lot of Malawians akuvutika ndi umphawi? Muzionatu
If a boat were sinking on Lake Malawi today , do you think they could have any capacity to go and rescue people quickly as , for example, ZAMBIAN soldiers can do? If they can't, what is the point of having two barracks?
Hands of to Kamlepo and his son. Anthu inu Malawi siwanu,it's for the people who were born in Malawi. A president mukuchitisa manyazi mulungu,azisogoleri anzanu mumipingo, Assemblies of God,pamozi ndi ine Deacon,mukumangosainila nkhanza zina zilizonse,nyansi zokhazoka pangani chilungamo . A president pangani reconciliation ndi mulungu,resign from politics.Mulibe mtendere inu ngakhale mukudya bwino,mwaonda nazo mkati mwa mtima. Apolosi ovutika anzathu siyani kuzunza ife Malawi anzanu,you are just the bread winners like us. Akakutumani siku Lina simkabwerera, people will overcome your power. Umaliro wake wazakumubondani na misi,nthonga ,umaliro wake lakusizgika ni banja linu. Amalawi wavuka imwe atopa Chakwera resign Kuli Moto kumwamba. Zokoma zazikoli zakutengerani koyipa . Ana ang,ono,akupweteketsani Bwerani Kwa Yesu a president. Yesu akudandaula pantanda. Mwazunza amalawi osauka,anthu opunduka,amasiye,amayi Ali pa uchokolo,ma compasation anamfedwa ndi zambili. Misozi ya Yesu Khristu yagwera pa inu Soka😢😢
But Why Salima have two baracks?? ..ndalama angoyenda nazo mmisika kusokoneza akut maganizo a a Malawi..kutiona kuvutika kwambir koma Mulungu awaone mwa padeladela
NDIYE MULENGEZE KUTI TIZIPHANA CHIFUKWA MWATIONJEZA CHAKWERA SUNGANDIVUTE INE NDI SIKU LIMODZI INE ALILA AKWANU IWEYO ZIKHALI N'GOMA IWEYO NDIYE NDI MAMINISI KUPHWESA INE MIMBAYO WAVA TIMAKUPASA I ULEMU KOMA NDINU MAVI ONUKHA KWAMBILI PANYO PANO CHAKWERA IWEYO USAMALE CHIKANGAWA SIPANAPITE NTHAWI KUTI MWINA ANTHU AIWALE KOMA IWE ULI BUSY KUCHOSA MOYO WA MUNTHU MBOLO YAKO CHAKWERA NIPHANYA CHIMUTU CHAKOCHO WAVA MAVI PONYELA PAMATAKO PAKOPO
You won't die prematurely in Jesus name.don't worry God is protecting you. Chilungamo chikuyenda ngati madzi apa dzikoli talisambira mmanja kuti Mulungu wathu achite nalo basitu.
@@Stevekatiwa-tp3oq eeh eeh man mpaka opusaaa? Ochenjelanu mulibho. Ulemu wanu 🙏. Ine ndimawafunsa awo akuti mowa Tizimwa size or today kumasuta MWA limit
Mr kamlepo don't worry nthawi yaanthu mukuwadandaulao yatsala yochepa misonzi mukugwetsayo owo adzagwetsa x7
Thanks so much Dr we respect you from the past 80s and 90s. I hope these idiots has forgotten these because they are young. Keep it up to let us know the trueth
A honorable Foniyo msayivomele, akungopasani ndalama mkagule yina nokha
Kamplepo kukhala maiko ena bwenzi akupasibwa ulemu chifukwa adagwila ntchito yaikulu kuno ku malawi
May God protect you and your family,daily prayer is the key,have your lawyers get your phone,you are a great Malawian treasure.🙏🏾
Dziko ndi anthu Ake ndi conco mulungu akupulumutse iwe kamlepo ufike tchaka CA mawaci bass God protects kamlepo kaluwa and other family
This Kamlepo Kaluwa is a real Malawian let's respect him and let our money return
Unuyo osawopa anthu awa atikwana ndipo tiwaponda aziwe sopano kuti tatopanaqo agalu amwnewa Mr chikangawa
Amenewo asiyeni Akaluwa
Akuti a boma mwaba 3 trillion ndipo mukubisa m'ma bank osiyana'siyana, mukumangira nyumba zibwenzi, zina mwasunga ku Cuba....koma mukupangiranji izi pomwe a lot of Malawians akuvutika ndi umphawi? Muzionatu
They hate him because he spill beans which is good for poor Malawians
Keep going mr KK we're really following you and all you are speaking out is all true thise stupid people they taking Malawi like they own it
Apolisi analowanso gulu la zigawenga lotchedwa MCP 🐊 zam'mabango
Why background music
Ayi bwana phone musalandile anthu awa ndimamafiya tiwonana chaka chama I hope to remove this nyasi
May God continue protecting you fadah
Don't worry father kamlepo Mulungu afungatila Satana ndi olephela bas
You don’t know why Salima have two barracks 😂
⁉️😂
If a boat were sinking on Lake Malawi today , do you think they could have any capacity to go and rescue people quickly as , for example, ZAMBIAN soldiers can do? If they can't, what is the point of having two barracks?
Tell us why
Zomati ndizaulula ndizaulula zii, ife sizmati sangalasa ai lelo si mawa ai ndibwino kuulula lelo a malawi tizziwa
Hands of to Kamlepo and his son.
Anthu inu Malawi siwanu,it's for the people who were born in Malawi.
A president mukuchitisa manyazi mulungu,azisogoleri anzanu mumipingo, Assemblies of God,pamozi ndi ine Deacon,mukumangosainila nkhanza zina zilizonse,nyansi zokhazoka pangani chilungamo .
A president pangani reconciliation ndi mulungu,resign from politics.Mulibe mtendere inu ngakhale mukudya bwino,mwaonda nazo mkati mwa mtima.
Apolosi ovutika anzathu siyani kuzunza ife Malawi anzanu,you are just the bread winners like us.
Akakutumani siku Lina simkabwerera, people will overcome your power.
Umaliro wake wazakumubondani na misi,nthonga ,umaliro wake lakusizgika ni banja linu.
Amalawi wavuka imwe atopa
Chakwera resign Kuli Moto kumwamba.
Zokoma zazikoli zakutengerani koyipa .
Ana ang,ono,akupweteketsani
Bwerani Kwa Yesu a president.
Yesu akudandaula pantanda.
Mwazunza amalawi osauka,anthu opunduka,amasiye,amayi Ali pa uchokolo,ma compasation anamfedwa ndi zambili.
Misozi ya Yesu Khristu yagwera pa inu
Soka😢😢
Mr kamulepo ulemu wanu , gulani phone ina iyo itayeni atenge chikangawayo
😂😂😂😂😂😂 chikangawa kkkk
Keep it up
Kom back ground track takozani ikumasokosa
Wosadanda bambo anayamba kudana ni Yesu
The big man
Kudandaula yayi adada ka mulepo Kaluŵa, Chiuta nimukuru awo wamubilani foni ndarama walije, Chiuta wawezgerepo foni iyo, awo walikumupokani foni Chiuta wawalange wose
Amalawi akuvutika kusowa makwala mu hospital ndalama zogulila makwala mwazigawana ayi amuye atengepo gawo
Ndi a kuba ayikoda phone
It's matter's of time one will take off this cruel government
Kkkkkk akulephela kugula phone kkkkk apolisi ndichanikoma
Kkkkkkk
Awuzeni achikangawa fogs amenewa malume 😂😂😂, they're too young for politics
Iyooooo 😮
Mcp 2025 0vote kunoko ku Ntcheu khulupirini
Ndi mene amadyela agaluwa
I love u mr kamulepo
KODI MAYI YOLAMU CHAKWERA ZIKHALI MKAKA USI KOD CHILIMA UJA SANAKUKWANENI NDI ANTHU 8 AJA
Waku Nkhatabay yo ndiye eeeee eeeeee eeeee 😂😂😂😂
😂😂😂
My father mungule 4 ni yina basi
😂😂😂😂koma kamlepo😅
But Why Salima have two baracks?? ..ndalama angoyenda nazo mmisika kusokoneza akut maganizo a a Malawi..kutiona kuvutika kwambir koma Mulungu awaone mwa padeladela
Amuputa dala uyu anati ziii ngati kunalibe
Nsambi kwambili chakwera satana yehova akuona
NDIYE MULENGEZE KUTI TIZIPHANA CHIFUKWA MWATIONJEZA CHAKWERA SUNGANDIVUTE INE NDI SIKU LIMODZI INE ALILA AKWANU IWEYO ZIKHALI N'GOMA IWEYO NDIYE NDI MAMINISI KUPHWESA INE MIMBAYO WAVA TIMAKUPASA I ULEMU KOMA NDINU MAVI ONUKHA KWAMBILI PANYO PANO CHAKWERA IWEYO USAMALE CHIKANGAWA SIPANAPITE NTHAWI KUTI MWINA ANTHU AIWALE KOMA IWE ULI BUSY KUCHOSA MOYO WA MUNTHU MBOLO YAKO CHAKWERA NIPHANYA CHIMUTU CHAKOCHO WAVA MAVI PONYELA PAMATAKO PAKOPO
It won't happen tilinanu madala
Aliense azafa,,,, mark that words zitsilu za mcp
Tangoing'alulani akulu
😅😅😅😅😅😅😂😂😂😂😂 is the eeeeee,eeeee,eeeee,for me😅😅😅😅😅😅😅
Vuto lake andale ena amuiwala kamlepo
lankhulani bwana kamlepo
Chiona ndi chipande powomola
Muzingodomola one by one basi malume 😂😂
Muwasumile amenewa ku bwalo lamilandu a galu amenewa
Ndazipeleka kukhala lawyer for free, kasumeni mulandu ndipo iwiri, okunamizilani plus phone yanu
Apolice akusunga phone yanu chifukwa cha chakwela ndiamene amatuma apolece kuti azimanga athu chifuwa alindimatha panyasi zimene akupanga enawo ngongotimidwa koma ambuye akuwona chifukwa akanakhala kuti iye sakuziwapo kathu phone yanu akanakupasani thawiyomweija koma alinayo cholinga kuziwa akuziwa chakwela kuti phone yanu andi apolece bwanji akukhalachete ndemawa azizati palibe chomwe akuziwa chimuthu choyipa kuyipa kwachinkhope ndintimawomwe kuyipa nkumati ndibusa busawake wakuti wakumidimatu ma bafomet amitu 6
You won't die prematurely in Jesus name.don't worry God is protecting you. Chilungamo chikuyenda ngati madzi apa dzikoli talisambira mmanja kuti Mulungu wathu achite nalo basitu.
Koma akamlepo kutha samatha choncho ndithu anthu ankakupasani ulemu koma mpakana apapa ayi ndithu.
Sim card yokha abweze... Wa police wationjeza
That's the kamplepo kalua i know, amatakasa madala wa,
Akamlepo nkhani yizktha kodi osapita kupolice koko bwanji ndinu munthu wamkulu
Mmmm this one is a real legend
Ayoswa kunotu yanu..
Ija mmati muimba phone ku police kuti mwana Wa Kamlepo amangidwe.
Ndipo pokhapo mneneri eee watenthedwa🤣🤣🤣
MCP sizasintha, kamuzu Banda anaonga chipani
Phone pelekani siyanu
Apolice akumalawi ndiotsauka akufuna kuti aziyendela 4n yanuyo vuto samalandila ndalama yoti athakugura 4n zakulandila apolice o
Eeeee guys 3 Trillion kwacha 😢😢😢
Ampase telephone yake chimene asakumpasila munthu ndi Chan kod
Osawopa tikudziwa ntchito zawo zokupha
Ndiwe wa mtopola iwe
Zosayendatu kwabasi
Ayaluka 2025 hold my words
Mowa Tizimwa mwa size or fodya kumasuta mwa limit
Wasuta fodya ndani
Wamwa mowa ndani?
Ndan iwe kod ukufusa zopusa iwe? Wamwa mowa ndan?????
@@Stevekatiwa-tp3oq eeh eeh man mpaka opusaaa? Ochenjelanu mulibho. Ulemu wanu 🙏. Ine ndimawafunsa awo akuti mowa Tizimwa size or today kumasuta MWA limit
Kamlepo osaopa pitilizani ntchito,
Auzenii
Afiti a MCPigs ndi ufiti. Pamtumbo panu a MCP.
Gulani Ina basi boma iyi mmmmm
😢😢😢😢
Za lero kapena za dzulo izi abale
Musamantchuluse sounds sizikumavekaaaaaa
Chonde chonde phoni yo musarandile Bambo. .. ... Anthu wa ali cholinga....kma inuyo ndi 1
4n Yao apaseni basi
😂😂😂😂😂
Tsono boma likumva pa u.tube.wasowa chochita galu uyu