Kodi Ku DPP Vuto Lanu Ndi Chani Kukakamila Munthu Wamkulu - Samuel Lwara

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лют 2025
  • Today on Nyasa VoiceBox, Samuel Lwara is question why the Democratic Progressive Party is so adamant in keeping Professor Peter Mutharika s its candidate despite his advance age.
    Lero pa Nyasa Voice Box, a Samuel Lwara akufunsa chifukwa chomwe chipani cha Democratic Progressive Party chikuwumirira kuti mtsogoleri wa Prof Peter Mutharika asamuyimire ngakhale kuti wakula.
    #malawi

КОМЕНТАРІ • 28

  • @LizSemu-y6v
    @LizSemu-y6v 17 годин тому +1

    Apm my vote

  • @AndileZondi-b1u
    @AndileZondi-b1u День тому +1

  • @WilliamChi-c6p
    @WilliamChi-c6p 18 годин тому

    Nzeru ulibe ndipo malangizo ako kutsogoloku adzakubwerera pafupike patalike ngati wasowa zolakkula ingosiya ndipo uyambe kupemphera dziwa kuti mulungu wasunga mau ako

  • @Ayanali-cr4vy
    @Ayanali-cr4vy 23 години тому

    Kabambe sitsogoleri wabwino
    Kuvotera Kabambe kuli ngati osakavota
    Atupele Muluzi my Vote

  • @GeoffreyMarko-v3s
    @GeoffreyMarko-v3s День тому

    APM it's my vote omuwopa mukuchuluka APM Boma 💙💙💙💙💙💙💙💙💙 ☝️☝️☝️☝️☝️☝️

  • @Ayanali-cr4vy
    @Ayanali-cr4vy 23 години тому

    Atupele Muluzi my Vote

  • @MariamMwalabu
    @MariamMwalabu День тому

    APM my vote

  • @WilliamChi-c6p
    @WilliamChi-c6p 18 годин тому

    Unkaoneka ngati woganiza koma ndiwe kape otheratu page yakoyi wainonga ndi audio imeneyi .koma uli agogo ako iweyo .kwanu kulibe okalamba ?iweyo ndiwe munthu omvetsa chisoni ndipo mulungu akukhululukire .sunga mau awa

  • @MikeWallace-e7l
    @MikeWallace-e7l 19 годин тому

    Ndimakuona ngati wa nzeru poyamba koma ndiwe chitsiru cheni cheni

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 19 годин тому

    Ndipo iwe lwala upenga misala ife ndivoter Apm mufune musafune Apm akulowa😂😂😂😂😂munya in

  • @LeyvanSamuel-pe5tc
    @LeyvanSamuel-pe5tc 23 години тому

    Ndipo ndkukavotera APM 😅

  • @KingsleyKunneno
    @KingsleyKunneno День тому +1

    Okanika ndi aMalawi .Koma Boma ndilomweli ..Mcp sitikusintha .wa 90 years akagwere uko .

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani 22 години тому

      Ndpo modzi mwao ndineyo okanika aise ndpo Peter or atakhal ndi zaka 400 koma vote yanga kwathu komse Peter tkachonga or akuyendera wheel chair or drip ii pamkono koma hahahahaha Peter basiiuiiiiiiiii or atakhala ali bokosi

  • @Jafari-s3c
    @Jafari-s3c День тому

    Iwe lwara ndiwe opusa kwambiri, komaso iweyo siwe wa utm, ndiwe wa mcp timadziwa, umazitenga ngati ndiwe wanzeru kwambiri kuposa onse

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 22 години тому

    Age is just number but we need experience how to run government so keep quite

  • @WarriorKB-l3i
    @WarriorKB-l3i 15 годин тому

    Aaaah za ziii ukawafunse Ambwiyako fotseki tamufuna APM ndife osati iwe dont talk nonses.

  • @MalizeniOliviaBridan
    @MalizeniOliviaBridan 21 годину тому

    Luwala panga chako chipani uwauze amalawi akakuvotere

  • @HaltonChanza
    @HaltonChanza 17 годин тому

    Chifukwa nyamata ndi chitsiru nthawi zonse monga uja analonjeza koma osakwanirisa

  • @BlessingsNambera-d6d
    @BlessingsNambera-d6d 23 години тому

    Iyeyo ndichifukwa chani Ali ndi makolo ake akulu osawapha bwanji

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani 22 години тому

    Ndpo iweyo ukunama Peter or akanakhala zaka 400 komabe ndi votee yanga kwanu ngt kulibe nkhalamba zili kwanu komweko

  • @LaynaAdam
    @LaynaAdam День тому

    Tikuonamu ubwino mwankhalambamo akulu musatiuze zochita ovota ndife

  • @JoiceNkhoma-s1m
    @JoiceNkhoma-s1m 20 годин тому

    Are encouraging de parties not to have alliance??? den u jst pretend coz u knw our president kabambe payenkha sangawine no doubt abt dat

  • @ZaiduAbudurazack
    @ZaiduAbudurazack День тому

    Nawe wasowa zochita

  • @OdreckNdemanje
    @OdreckNdemanje 19 годин тому

    Wamkuluyo siMunthu??

  • @ClifordBwwanali
    @ClifordBwwanali 21 годину тому

    Chitsiru chamunthu

  • @MariamAdamNassah
    @MariamAdamNassah 22 години тому

    Wamwa mtonjani iwe