Samuel Lwara Is Just A Noise Maker - Comrade D Phiri

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 6 лют 2025
  • On Nyasa VoiceBox, Comrade D. Phiri says that people should disregard Samuel Lwara’s comment on APM’s age because Samuel Lwara is nothing but a noise maker.
    Pa Nyasa VoiceBox, Comrade D. Phiri akuti anthu anyalanyaze ndemanga ya Samuel Lwara pa zaka za APM chifukwa Samuel Lwara si kanthu koma wongopanga phokoso.
    #malawi

КОМЕНТАРІ • 26

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 20 годин тому +2

    Ndipo zowona alwala masiku ano akunyoza kwambiri inenso ndawatuluka akusokoneza kwambiri

  • @Ayanali-cr4vy
    @Ayanali-cr4vy 20 годин тому +1

    LWARA ndi member wa UTM
    Nde tizikumbukira kuti chipani cha UTM ndi Chipani cha anthu akatangale akamwa,okonda kunyozana azawo
    Koma Kabambe sitsogoleri wabwino komanso sakuyenera kukhala vice president

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole День тому +1

    Lwara ndimamukonda kmno adayamba mbwerera ,mwayankhula bwino comrade.

  • @MastonWatson-g7g
    @MastonWatson-g7g День тому +1

    Ndipo zolankhula zake ndi za ziiiiiiiii zopanda mchere.

  • @MarySinjirani
    @MarySinjirani 13 годин тому

    Lwara ndipo ndi kuti ndi chitsiru cha mzibambo chopanda nzeru ndi chadyera kodi lwara amazitenga ngati ndani chitsiru ameneyi nzeru zopusa zake asake kopangira osakhala kuno ku Malawi zikuvuta usowa kokajiya wanya

  • @tingamasi106
    @tingamasi106 22 години тому

    Chilungamo chimawawa. Let all parties stand paokha, peter wakalamba and thats the reality. Zodabwitsa mzakuti amene mukusapota pitala ndi achinyamata kodi ndekuti achinyamata muzingoonbera manja nkhalamba? Aaaaah hate Lwara the more you can komano zoti pita wakalamba ndizoona. Do you want to tell malawians kuti amene angalamule ndi nkhalamba basi? Ndipo Lwara wayankhula bwino kukalambatu sitchimo ndi mdalitso ochokera kwamulungu. Retirement age m'boma ndi 60 yrs and peter is heading to 90 years amalawi tikufuna chani? Utm singaberekedwe ndi mkhalamba.

  • @MariamAdamNassah
    @MariamAdamNassah 22 години тому

    Komansotu iyeyo akupita kumweko kugogoko
    Kodi iwe Samuel mesa umamulangisa kabwira thawi imeneija atanyoza apm ndipo unapeleka chisanzo chomcheka bwino

  • @Dan44-x5b
    @Dan44-x5b 23 години тому

    I can see more from your accent but what Lwara says is right. We needed to find a younger candidate

  • @tingamasi106
    @tingamasi106 22 години тому

    Ife a utm tikagwirizana ndi sam lwara amene mwakwiya ndinu a dpp ndipo musova. Mkhalamba ayi period. Lwara keep the fire burning. Lwara sanatukwane wayankhula zoona zokhazokha

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 23 години тому

    Lwara ndi munthu wopusa kwambili ineyo ndinasiya kumvera ma audio ake

  • @CathrineRamseyJafaal
    @CathrineRamseyJafaal 20 годин тому

    Sam anathawa ku mcp ndiye akufuna asokoneze kabambe chimene mungaziwe kabambe sangawine pa yekha

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 23 години тому

    A lwara ndi munthu woti zoyankhula zake saziwika kuti Ali mbali iti ......a lwara siyani kuyankhula za dpp

  • @AlickMDayi
    @AlickMDayi 19 годин тому

    Samuel Lwara ndi wanganyu wa D Kabambe ojiya anamuthamangitsa ku MCP

  • @JackMvura
    @JackMvura 21 годину тому

    Lwaala akunena zoona bridge yakutha ayi ingagwetse wanthu pitala ayi akapume

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 20 годин тому

    Kabambe ayenela asogole ngati pangakhale mugwilizano kuti athandize malawi osati kuthqndiza zipani akunena apayu ndi mbuli yothelatu

  • @NaphiChiwaya
    @NaphiChiwaya День тому

    Zikomo pomuyankhu ameneyu amaonjeza ine ndinasiya kumvera ma odiyo ake

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 20 годин тому

    Samuel akunena zoona osanama peter sangathandize amalawi analephela kale komaso panopa wakalambisisa bwanji ku dpp asankhe achina suleman ayendese malawi osati kuyendesa dpp.koma vuto amalawi timangosapota zilizonse vuto umbuli

  • @Eddakachere
    @Eddakachere 22 години тому

    He is just a noise maker and nobody

  • @JoyceMasuso
    @JoyceMasuso 22 години тому

    Wadya fodya wakupoto ameneyo ndiopusa

  • @edsonnyasulu5394
    @edsonnyasulu5394 20 годин тому

    Panopa tikufuna musogoleli woti akhoza kuyendesa dziko osati chipani ndiye dpp achina chisale azatipweteka kutibelaso ndalama tatopa nawo a dpp mbava

  • @GeshoMwakitwile
    @GeshoMwakitwile 22 години тому

    Pita muthanyula ndiokalamba

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 День тому +1

    Ndipo comrade D Phiri mwamuyankhula bwino nkulu ameneyu wayankhula mosefukira kwambiri, kutheka kuti anadya Fodya

  • @MariamAdamNassah
    @MariamAdamNassah 22 години тому

    Samuel lwara ndi kabwira amaganiza modotha

    • @QochiweNkhoma
      @QochiweNkhoma 16 годин тому

      Mwinanso Lwala ndi Kàbwira amapakulana 😂😂😂