NAMIWA WAMUNG’ALURA CHAKWERA ZA FUEL NGAKHALEBE AMUIKA MU COMMISSION OF INQUIRY YA IMFA YA CHILIMA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 27 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 389

  • @thulanimpphiri6873
    @thulanimpphiri6873 День тому +31

    Amene amafunika mu inquiry. Pastor chumba .enock chihana .bon kalindo. Namiwa bakili TV tanyiwa akubanja mubusa wa ccap uja anamangidwa .mutumiki yasini gama. Mafumu ayi ose ndi adyera pamaunikaso jb abiti maness mery navisha suleman anthu amewa ndi amene amafunika mu commission of inquiry

    • @BrightZionga
      @BrightZionga День тому +1

      Ndipo live

    • @ancientnkhata1137
      @ancientnkhata1137 День тому

      Iwe khala chete

    • @FrankMsiska-i9j
      @FrankMsiska-i9j День тому +1

      Samasankha mbuli,,, achina ntanyiwa nde ndani ??

    • @thulanimpphiri6873
      @thulanimpphiri6873 День тому +4

      @@FrankMsiska-i9j mbuli ndi izi zimamena kuti ndege inafika kuno ku mzuzu ndipo anayibweza mdipo inagwera kutali ndi muzi komaso inazaza kaya inazaza ndindani zimagula fertilizer kubucha zinapereka ndalama ku foundation bridge zimezi ndizo mbuli zazikulu kuno kumalawi

    • @FrancisNyayi
      @FrancisNyayi День тому

      Wapatower

  • @alexsumani6823
    @alexsumani6823 День тому +16

    Bravo Sylvester Namiwa ,mawu amphanvu,God bless you

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf День тому +3

    Micah stood alone against 400 prophets and so was Elijah. See that you are Elijah of our time. All eyes are on you . Keep yourself holy and be blessed ✝️🕊️

  • @HondaFredzoG
    @HondaFredzoG День тому +4

    Zoti muli pakati pa mikango simukudziwa anamiwa nfusen chilima ku gwilizano anapanga ndi mcp uja

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani День тому +11

    Zoona timamva pa Bakili Muluzi TV ndlam idyani kwa Mulungu kulibe chibazi guyz

  • @SajeedYunus
    @SajeedYunus День тому +6

    I trust you namiwa God be with you in this journey

  • @AlexMofolo
    @AlexMofolo День тому +12

    Mr namiwa mukayelekeza kukalandir ndalama kt mutseke pakamwa mizimu ya athu idxakwiya kms 🇲🇼 sadzakhulupirira no chinyengo ulendo uno tidxiwe zoona mulungu akuonat

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole День тому +3

    Anthu anakukayikirani km powerful speech Mr namiwa ❤❤

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu День тому +2

    100%×100. Wow! Mr. Namiwa takunyadilani kwambiri. Eish! Thank you so much, keep it up.

  • @bysongeorge3243
    @bysongeorge3243 День тому +6

    We are giving you benefit of the doubt, Namiwa. You are outnumbered. The rest of the team has MCP DNA.

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c День тому +1

    Amen mulungu akutsogolelen paulendo wanu panokha simukwanitsa chilungamo chimamasula

  • @MastineChitsulo
    @MastineChitsulo День тому +4

    Mr Namiwa please kagwireni ntchito yachilungamo, amalawi amakhulupilira bungwe la Cdedi limeneri. So Anamiwa mukakhumudwitsa amalawi Cdedi idzathera pompo chifukwa amalawi adzasiya kukukhulupilirani

  • @dinchisale
    @dinchisale День тому +12

    Even if you will be in there Mr. Namiwa you cannot influence the Team to stop manipulating because you will not be a Leader

  • @dysonfysonchifundo2284
    @dysonfysonchifundo2284 День тому +1

    For this special speech Mr Namiwa God be with you and help you in all battle ❣️

    • @NEBRA-lm7ji
      @NEBRA-lm7ji День тому

      Mr Namiwa u the last chance of Malawians plz try ur best ambir ife zutiwawabe😢

  • @GeorgeKalima-e3m
    @GeorgeKalima-e3m День тому +2

    Poika Namiwa mu commission of inquiry kunali kulelesa mademo
    Amawona ngati achenjera Koma apapa nde azipalasila makala amoto 😂😂😂😂
    Pitani mukaike chilungamo pambalambanda Mr Namiwa our only hope in the entire inquiry
    Osaopa! Osatopa! Osafooka!,💪💪💪

    • @AidaGremu
      @AidaGremu 16 годин тому

      Ndipozoona zake

  • @JacobMsukwa-q6v
    @JacobMsukwa-q6v 14 годин тому

    May the good Lord continue blessing you aseh😢😢we lost our comrades indeed en still more our hearts remained blocken😢😢

  • @ManMen-kp2ze
    @ManMen-kp2ze День тому +1

    Bravo Namiwa, be strong, my home boy, fear God and He will bless you, I like ur saying " I wii expose who ever tries to bribe me,"

  • @HolmanDazah
    @HolmanDazah 16 годин тому

    Am the one to believe and trust Mr Anamiwa to handle this issue by fearing God, make it transparency and accoutable. Ndipo make sure kuti the inquiry must be on the heath.

  • @MatthewsJanuary
    @MatthewsJanuary День тому +10

    Ngati mukufuna kuti anthu akukhulupireni, tengani andale alowepo, achibale oferedwa alowemo

  • @noahgaleta4193
    @noahgaleta4193 День тому +2

    I'm worried for you Mr Namiwa , we can't lose you again? What if they have a plan to kill you, please almighty God be with Mr Namiwa and protect him

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 День тому +1

    On that list, i trusted you mr namiwa please do this for us,as a Malawian 💪💪🙏🙏

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 День тому

    Zikharedi live......tizizamva.....ndinthu. Takuldalirani..mr Namiwa...,. osaopa

  • @BerthiaChikopa
    @BerthiaChikopa 10 годин тому

    Its my pray anamiwa mulungu akuchotsereni mantha in Jesus name

  • @JailosIsaac
    @JailosIsaac День тому +8

    Mr Namiwa can you please 🙏 just exclude yourself from this crew

  • @DalitsoPhiri-sq5nl
    @DalitsoPhiri-sq5nl День тому +2

    Coach is in the field of play endeed, let's support the Namiwa the great go bring the truth of Our late vice president SKC mlungu akusogoleleni

    • @harrymicah6140
      @harrymicah6140 День тому

      Bora nawe namiwa ukapange zachilungamo kumeneko

  • @oscarbalakiya3138
    @oscarbalakiya3138 6 годин тому +1

    Lero bwez ali Timoteyo Mitambo😅😅

  • @FabianoJohn-t9o
    @FabianoJohn-t9o День тому +3

    Anamiwa ife takukhulupilani koma mukhale wachibale was anthu ofeledwawo akhalemo

  • @NoluvuyoMatutu
    @NoluvuyoMatutu День тому +1

    Mr Namiwa uli olimba ntima wandikumbutsa Julius Malema ❤❤ big up

  • @dalitson3558
    @dalitson3558 День тому +3

    I don’t trust this Namiwa guy, but he needs to be very careful with this sensitive issue

  • @AbdullahSaeed-tg1cm
    @AbdullahSaeed-tg1cm День тому +1

    Namiwa...the only Hope of Malawians now....❤

    • @youmad9087
      @youmad9087 23 години тому

      Chifukwa ndi mlomwe?

  • @munyenyembe
    @munyenyembe День тому +1

    Tikudalira inu a namiwa pliz, we love you so much

  • @RedsonMakaka
    @RedsonMakaka 14 годин тому

    Indeed time is the best judge

  • @RuthJopilo
    @RuthJopilo 16 годин тому

    Point Mr Namiwa❤

  • @geofreykandabongomani4715
    @geofreykandabongomani4715 День тому +1

    Mr namiwa i don't trust this issue i think best way u have to go their with mr bone kalindo the DC mwana wowopya kwambili

    • @SteveNdhlovu-r2x
      @SteveNdhlovu-r2x 19 годин тому

      U r right it can be a plot take care Mr namiwa u r going to work with crocodiles

  • @papelariareis.e.
    @papelariareis.e. 20 годин тому

    Musavutike kupita kutali even akaliati atengedwa koma umboni is very safe respect to Mr boooooon kalindooo the DC anamiwa even outside the country ma audio mmmmm pray for Malawi guys

  • @HassanJimmy-r1n
    @HassanJimmy-r1n День тому +3

    Inuyotu Mr Namiwa timakukondan komano ifeyo a Malawi tikukuwopelan inuyo MCP ndiyakupha inuyo nonkanonka kumeneko mukuwona kut mulisefu(Namiwa)? Ndi m'mene inuyo umaiziwila MCP ndinu otetezeka?

    • @BeatriceNkhoswe
      @BeatriceNkhoswe День тому

      Ineso ndili ndi nkhawa kwambiri munthu akaphedwa uku ndi mcp

    • @MussaSubeli-bh3ge
      @MussaSubeli-bh3ge 2 години тому

      Tiwayikize mapephelo Anamiwa😱😱😱😱

  • @RaphaelWinford-t7u
    @RaphaelWinford-t7u День тому

    Zoonadi amalawi ambili sitimakhulupirila munthu , komano chonde, Anamiwa tiwakhulupirile sikuti munthuyu sanalandile ndalama ai , tiyeni timukhulupirile.... Be blessed Mr Namiwa....❤

  • @BrightonChirwa-b5c
    @BrightonChirwa-b5c День тому

    😊God bless u mr namiwa, ndipo takukhupirani,

  • @JonaSato-j8e
    @JonaSato-j8e 17 годин тому

    God be with you ❤❤❤

  • @CatherineChidothe-x2k
    @CatherineChidothe-x2k День тому

    I like the speech of u brother Namiwa keep the fire burning

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 17 годин тому

    We also expected people like Kalindo, Kamlepo Kaluwa or his son Penjani and Enock Chihana

  • @Mwaiphiri-v3d
    @Mwaiphiri-v3d День тому

    Is that commission of enquiry an independent or chakwera commission of enquiry?

  • @lungisanishezi1023
    @lungisanishezi1023 День тому +1

    In Namiwa we trust

  • @christopherZulu-q5s
    @christopherZulu-q5s День тому +1

    You are saying the truth and please am Zambian but I have been following this issue since June 10 ,chilima was killed so please stand for the Malawian s so that the truth must come to an end otherwise it was a plan move for chakwera why he changed his mind to stand 2025

  • @HaroldMasanga
    @HaroldMasanga День тому

    Anyway Mr. Namiwa wishing you all the best and may God guide you.

  • @MarryNyilongo-s5x
    @MarryNyilongo-s5x День тому +1

    God bless you always

  • @joegibsonzulu2599
    @joegibsonzulu2599 День тому +2

    Commission of Enquiry imeneyi ( maka maka its composition) sikundipatsa chikhulupililo olo pang'ono. Kwangodzadza ma delegate aKhongelesi basi. Don't expect any justice from these party loyalists. Namiwa, extricate yourself from this pantomime.

  • @BlessingsMakalani
    @BlessingsMakalani День тому +1

    I like you Mr Namiwa what you said l'm under whith you

  • @ChristinaMdeza
    @ChristinaMdeza 16 годин тому

    Comrade anamiwa chonde chonde maso athu kudziko lathuli lilipa innu chonde ima pa chilungamo musadye nawo ndalama izi za magazi cha chakwera inuyu please we love you ❤❤❤😅

  • @LawrenceLidaraPhiri
    @LawrenceLidaraPhiri День тому

    Thanks Mr. Namiwa but my aim went want UTM and the family we lost the people to be together for equirely

  • @MillieMalakam
    @MillieMalakam 16 годин тому

    God ahead u my brother

  • @ShakiraJackson-x8w
    @ShakiraJackson-x8w День тому

    All we need family members to be involved radios and tv have to inform us live accept MBC radio and TV we don't trust them go well mr nawiwa All the best

  • @LouiseBukani
    @LouiseBukani День тому +1

    Raw deal indeed !

  • @Kenmoney-xp7tz
    @Kenmoney-xp7tz День тому +3

    Nanga akumabanja bwanji mulibemo inu a namiwa banji simunawauze aikemo? Why is it almost only namiwa included? Why not opposition and media? Madya mabanz inu nyari sanafike ma band akubwera trust me

  • @THOSI-d1l
    @THOSI-d1l День тому

    Power full speech Namiwa

  • @RajabAssan
    @RajabAssan День тому

    Powerful speech

  • @TimeAbilu
    @TimeAbilu День тому

    Pakufunika kuonjezera like Bon Kalindo DC, relationship for die pple thats good to additional Namiwa

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr 19 годин тому

    Komanso zikayendani mosamala, Tisakuluzeni Mr Namiwa.

  • @GiftPhiri-n8r
    @GiftPhiri-n8r День тому

    God bless you Mr namiwa

  • @quoniemagalasi9123
    @quoniemagalasi9123 День тому

    Truth is truth whether one person or 2 but i will see 18 people fearing one true man.

  • @FabianoMalitino-cz8wz
    @FabianoMalitino-cz8wz День тому +1

    Mwayankhura bwino we are waiting for the results

  • @ShekiriBanda
    @ShekiriBanda 2 години тому

    Akupatsani Bazi inu Mark my words born kalindo alikut umu

  • @SandraChibaka
    @SandraChibaka День тому +2

    This commission is fake

  • @PriscaMussah
    @PriscaMussah День тому

    Namiwa ,God first plis

  • @samsonchibambo7977
    @samsonchibambo7977 День тому

    1) Funso langa ndilakuti kodi mukudziwa anthu amene mudzikawafunsa mafuso - mwina ngati aku army, a president, anthu a kumudzi kufupi ndikumene kunagwa ndege, anthu a ku Mzuzu ndi ku Lilongwe airports ndi ena onse amatumiza ma nkhani zakusowa kwa ndege?
    2) Kodi ndi zowona kuti anthu ena amafuna kekwera nawo ndege koma ena anaudzidwa kuti mundege munalibe malo. Kodi nkhani yimeneyi ndizoona?

  • @FracksonMadani
    @FracksonMadani День тому +1

    Namiwa iwe, ukhale ochenjera ngati njoka ndioona mtima ngati nkhunda, mau ako asathere m'mazira, adzalira ndithu

  • @LydiaMsazurwa
    @LydiaMsazurwa 2 години тому

    Alright, Koma musazatinamize Kuti anthu Aja ,anangochitidwa Ngozi chabe chifukwa,ndegeyo inagwa,ndikuwomba mtengo osagwaso mtengowo,zimenezo ayi ,zichepe.
    Koma mutiwuze Kuti mwawapeza , chifukwa Chilima anaphedwa ndi zigawenga,mopelekedwa ,ndi President wa ziko la Malawi Chakwela.
    Mukazaloza Kuti President ndi amene ,anatumiza anthu aja,ndikugwilizananso ndi aUsi

  • @MartinMartin-d3g
    @MartinMartin-d3g День тому

    Mr namiwa mulungu kusogoleleni koma osakaiwala mafutso awa
    1 ndindani anati ndege inatdzaza
    2 ndani anatenga black box
    3 ndindani anamuudza president kuti ndege inafika ku mzuzu
    4 ndindani analoledza ndege kuuluka yopanda zoyenelela
    chifukwa chani chimwendo anakane kukwela ndege ndindani

  • @ChristianMalingamoyo
    @ChristianMalingamoyo День тому +2

    Mr namiwa we can't trust you anymore

  • @MagadaleneManjengwa
    @MagadaleneManjengwa День тому

    Kod simunganditenge kukhala nawo ku commission Inquiry pliz

  • @FredrickChizwa
    @FredrickChizwa 17 годин тому

    Ndiye mukamati wang'alura Chakwera ndimawu ATI ong'alura apapa😂😂 km anthu umbuli ukupwetekani ndithu

  • @LumbaniPolowani
    @LumbaniPolowani День тому

    Ine I which mukamayamba commitional of inquiries tizimvera nawo azakhale live koma nkulu winayo amuikayo mmm ka Ty??

  • @HolmanDazah
    @HolmanDazah 16 годин тому

    Am saying namiwaa titumikileni musamvere anthu opanda mzeruwo. Am saliute you!

  • @FranceKaloposha
    @FranceKaloposha День тому

    Which Malawi do you save?

  • @CharlesMunyado
    @CharlesMunyado Годину тому

    Namiwa iwe nchitsiru kotheratu ngati akusankha ukadakana iwe ndiwotembeleredwa kotheratu paja unazanama Kuti akuba pamapeto Poti anakutapira ndalama ine ndikungoti namiwa iwe ndigaru Kodi akubanja alipo Kodi mafumu alipo ambungwe omwe so aboma alipo namiwa mbuzi

  • @Laurent-h9u
    @Laurent-h9u День тому +1

    The truth must prevail 😢😢😢

  • @WendyPhiri-h5t
    @WendyPhiri-h5t День тому +1

    Sitikufuna tizamve kuti mwalandilako billion

    • @joegibsonzulu2599
      @joegibsonzulu2599 День тому

      Inenso maganizo anga ndi omwewa. Zayamba kukayikitsa kwambiri.

  • @JessieNgwira
    @JessieNgwira День тому

    Namiwa you have our trust please don't let Malawian regret

  • @EsetaGerate
    @EsetaGerate День тому

    Namiwa ❤❤❤ndipo ukapange zakupsa kumeneko akusankha Dara kut anthufe tizanene lnuyo

  • @Wilsonmalata
    @Wilsonmalata День тому

    Powerful namiwa

  • @SamuelAntone-mz6nq
    @SamuelAntone-mz6nq 6 годин тому

    Auuzen zoon amalawi adziwe chilungamo 🙏🙏🙏🙏💪💪💪💪

  • @abgi.doctor.august
    @abgi.doctor.august День тому

    Zikomo kuti mukhala nao pa ulendo umeneu tidalira inuyo mukafukufuku ameneyu tipemphe Ambuye apitilize kukutetezani kukudalisani ndi kukuchinjirizani pa ntchito imene muyiyambeyi🙏🙏

  • @MascotAnderson
    @MascotAnderson День тому

    Ndakukhulupira namiwa kagwire ntchito moopa yehova

  • @SteveMwélérø
    @SteveMwélérø День тому

    We trust you more after you bring the truth not your speech today 😢

  • @georgekamanyuzi108
    @georgekamanyuzi108 День тому

    ❤❤❤❤ great

  • @DumisanPhiri
    @DumisanPhiri День тому

    Go on mr

  • @RoseChimbwefu
    @RoseChimbwefu День тому

    Mr Namiwa chonde mafuso anthu a Malawi ali manja mwanu chonde ayankhidwe pa commission of enquiry iyi

  • @samdiverson9733
    @samdiverson9733 День тому

    Iwe namiwa take care Koma

  • @MALUMBOMNELEMBA-kf1vq
    @MALUMBOMNELEMBA-kf1vq День тому

    Dr chilima anali wa ndale koma bwanji sinayikepo azipani ?

  • @IreenMwachande
    @IreenMwachande День тому

    Mukadya banzi tikudziwani kusitha mayakhulidwe koma muchite mene mukyankhulira apa ai ambuye akutsongoleleri koma muli azibusa Ena muzikawawonesesa ndi azibusa okonda ndalama tikudziwa komanso mafumuyo ndiokonda ndalama muzikawawonesa muzolakhula zawo zinazo ndi njoka

  • @AbdulIbrahim-b6v
    @AbdulIbrahim-b6v День тому

    Pandale you can say that you can not accept enybig position but if it happens then a namiwa mulungu azapanga bugwe lanu kugwa pansi but for me people from my home khonjeni TA kapichi sanama we trust you please

  • @GodfreyKamphiripiri
    @GodfreyKamphiripiri 17 годин тому

    ❤❤❤❤❤❤Nimiwa fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee fireeeeeeeeee

  • @AdamJames-x7x
    @AdamJames-x7x День тому

    Mr Namiwa inquiry yoyamba mukapenge chakwera chifukwa mission yonse anayambisa ndi iyeyo kuti chilima afe, chilungamo chonse chili ndi chakwera pasapezeke bwamtasa wina omamubisa chakwera ameneyu ,

  • @SteveNdhlovu-r2x
    @SteveNdhlovu-r2x 19 годин тому

    Mr chakwera you made a big mistake for not including just one of the deceased 9 people in the commission of inquiry

  • @JudithMaida-ug4oi
    @JudithMaida-ug4oi День тому

    All the best mr Namiwa chomwe mungadziwe kut if u made a mistake kuzadzuka Namiwa wina inuyo muku Seva ndende ya chikumbumtima

  • @chippakaribafox2865
    @chippakaribafox2865 День тому

    Nuff respect comrade namiwa!...aluta continua!

  • @JeanBanda-zy6wu
    @JeanBanda-zy6wu День тому +1

    Anthu 18 olo a Namiwa mutachita chilungamo atha kumakupinda kumakuzemba
    Any way let's wait and see

  • @SamukLungu
    @SamukLungu День тому +1

    Iwe ngati warandira kare ndarama kabweze panga choti akubanja akharepo iwe upitangati ndani

  • @Randy-er2xo
    @Randy-er2xo День тому +2

    Bola osatinamiza

  • @THOSI-d1l
    @THOSI-d1l День тому

    Amalawi akukhululupilira wekha Namiwa