My genuine advice to UTM: Don't make alliance with any party unless you are taking the leading role (presidential position) in that alliance. Otherwise, kaloweni nokha kuzisankho, and when you lose accept it and move ahead, you will win in 2030 with landslide because i don't see any leader who can change zinthu apart from leaders in UTM
Pali kusiyana kwambiri pakati pa munthu wa xool ndi un educated. Enawo adanena ndithu kuti,one sindidziwa kanthu. Power mtumbuka akunenetsa Pano kuti Ali ndi upangiri wosiyanasiyana pa nkhani ya chitukuko
He sounds like VP not President But Goodluck Mtumbuka ife a DPP tisankhileni munthu oti tagwile naye ntchito muchaka cha 2025 ADADI akazatenga usogoleri Plz ma delegeti a UTM munthu ndiameneyu
Atsogolreli a chipani cha UTM mutachita kuti kutenga A Mtumbuka ndi A Bambe onse kukhala kuyendesa U T M ndipo a Mayi athu okondedwa ndiposo olimba mtima a Kaliyati akhale pompo as SG ndipo musalowe mu alliance. Dzikoli lizaphulidwa.
Me waiting the results after the Convention in November. Koma chomwe mudziwe Mtumbuka and Kabambe is more less than WIPON OF MASS DISTRACTION. Fredokiss will be the Minister of youth in the first place, but hope is there to be President in future. UTM ikadzangotenga boma ikubwera kudzakhala 🔥🔥🔥🔥 zinazi tayesa komanso zinazi tazibweleza koma manyaka okhaokha 🤮 a Malawi tikapusa ndithu dzikoli sitidzalinva kukoma mpaka Yesu adzabwera. Unless there is another Malawi after this life kumene mwina SKC anapita kukatikonzera 😭😭😭😭 REST WELL BIYENI 😭😭
A stitch intime indeed serves nine ,Utm as a problem of kuyang'anira zinthu ( kulekelera even the late SKC had a same problem so izizi we re not sure bwana ,,,,,, cos u have never been there before nde this time around Malawians wants anthu odziwa zintchito osati Ya class ,atleast "Kabambe , Atupele, Chihana and APM
You are right its high time we should try the northerner and its my belief will do better as will be from minority may work for all regions to get the second term.....if we miss this opportunity mmmm kaya ..zakwathuzi sizikuthandiza chitukuko chadziko.....
Mfundo ndiye zikuveka koma Poti a Malawi amadziwa kulonjeza koma kukwanilitsa kumavuta, akangowina amalephela kukwanilitsa zomwe amalonje ,chimene chimakula ndi kudzikundikila kusava zofuna zawanthu komanso kulephela Ku tsegula misika ya a dmaric , koma ngati mukunena zowona vote yanga ndiyanu
Koma ine ndikufuna Kuti akabambe ndi mtumbuka modzi mwa inu kuluza modzi akhale Vice President zikhala bwino
Pk mwamutaya?
One ndikuganiza kuti akabambe atsogole Mtumbuka akhale vice
Ndipo ndizomwe ndimafuna ,even me
My genuine advice to UTM: Don't make alliance with any party unless you are taking the leading role (presidential position) in that alliance. Otherwise, kaloweni nokha kuzisankho, and when you lose accept it and move ahead, you will win in 2030 with landslide because i don't see any leader who can change zinthu apart from leaders in UTM
Exactly my thoughts
Zoona mwanenazi. 👏🏻👏🏻👏🏻👏🏻
Combination of Mathews mtumbuka and kabambe can take this nation to another level, Akweni pa mpando wa u SG ndiokwanila
I think so too
Koma guys achinyamatafe tikanagwirizana kuvotera UTM. Kuli ma candidate abwino kwambiri. Chakwera is a waste of time
zoona
Kwanu konko, congress ikunyenyani ndthu
@@justinchabwera5380yakuphayo😂
@@johnbullyohanittokasikizim7127tiyavoterabe Congress
My vote 4 mathews Mtumbuka ,a leader of gud vision ,osati kwinaku
Akulankhula Chichewa koma zamnzeru zokhazokha. You're very wise.
Amene azasankhidwe pa udindo wa u president arumbire kuti nkhope ya chirima asazachose paripose pamene yiri osati kungotenga ndikuchosa zose ayi
DR:KABAMBE :AZAWINA KOMANSO DR MTUMBUKA AZAKHALA VICE PRESDENT
Kabambe to vice opanfansi zokqmbilana
God bless you Matthews Mtumbuka. You're the next president.
Mmmm. O mwa. Hundred. Mtumbuka😂
a mr.mtumbuka tiri pambuyopanu mulunga akusogorereni ❤
Mtumbuka yu ndendende Peter. ❤❤❤ Chichewa chovuta kma zipatso zautsogoleli zooneka
Indeeeeeee awa ndi Nyamata uyu Bola azakhale President or VP oyeeee UTM Moto🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥
Mfundo full more 🔥🔥🔥 mtumbuka
Mtumbuka
president, vice Kabambe. I can't wait to vote!
Komatu anzanuso ankatero asanatenge boma, kungotenga ali buzy kumakakwera njinga ku Germany ife tikufa ndi njala, ntchito 1 million lija lasanduka kosaka chiteze kutchire 😢😢, Ambuye muoneni pomwe wafika Malawi tsopano, tisankhireni tsogoleri yemwe achose misonzi yathu, musalole tizisankhire tokha tsogoleri, Koma inuyo mutisankhire
😂😂😂😂kabaza
Pali kusiyana kwambiri pakati pa munthu wa xool ndi un educated. Enawo adanena ndithu kuti,one sindidziwa kanthu. Power mtumbuka akunenetsa Pano kuti Ali ndi upangiri wosiyanasiyana pa nkhani ya chitukuko
He sounds like VP not President
But Goodluck Mtumbuka ife a DPP tisankhileni munthu oti tagwile naye ntchito muchaka cha 2025 ADADI akazatenga usogoleri
Plz ma delegeti a UTM munthu ndiameneyu
UTM oyeeh🥳🥳 waluka Continue waluta🔥🔥🔥
I'm proud to have a youthful democracy in leadership in Malawi
Zikumveka bwino koma vuto mumalonjeza tikavota simumatikumbukila ai ndye chonde mukunenazo zikhale zoona
Mr mtumbuka ur president of Malawi ❤ UTM my vote
Mmmmm hmmm Ambuye atithandizee
Atsogolreli a chipani cha UTM mutachita kuti kutenga A Mtumbuka ndi A Bambe onse kukhala kuyendesa U T M ndipo a Mayi athu okondedwa ndiposo olimba mtima a Kaliyati akhale pompo as SG ndipo musalowe mu alliance.
Dzikoli lizaphulidwa.
Akukhala ngat akuwelenga nkhani pa mbc, ngat Hassan Goba, eg, akumukuntha kwambiri mbomalooooo😂😂😂
Dr kabambe akhare president inu vaic
Never make alliance with other parties for utm to be successful
My vote
Ine sinima vota chifukwa snikhulupilira anthu andale koma uyu afuna aniyambise akanitenga bwino
Welcome Mathews Mtumbuka. This is the rebirth of new Chilimas. Let's fulfill Chilimas ideas and beyond.
Lets go!!!! Lets go!!!!
Contesting doesn't mean division. Let the people's choice win.
Utm ingotaya nthawi , kulibe wanzelu kumeneku ai . Utm inatha 2021
Maganizo abwino big koma musalonjeze zambiri pakamodzi zingalowe bodza😮
Thandizen Mtumbuka zake Ku Mpotokoo😊
Me waiting the results after the Convention in November. Koma chomwe mudziwe Mtumbuka and Kabambe is more less than WIPON OF MASS DISTRACTION. Fredokiss will be the Minister of youth in the first place, but hope is there to be President in future. UTM ikadzangotenga boma ikubwera kudzakhala 🔥🔥🔥🔥 zinazi tayesa komanso zinazi tazibweleza koma manyaka okhaokha 🤮 a Malawi tikapusa ndithu dzikoli sitidzalinva kukoma mpaka Yesu adzabwera. Unless there is another Malawi after this life kumene mwina SKC anapita kukatikonzera 😭😭😭😭
REST WELL BIYENI 😭😭
Kodi nd za m'maboma? Kkkkk zikundivuta kunvetsetsa ine😅
Encouraging speech. Let's support him. Let's not look at his age but his ability to deliver. But should be careful not to promise people the moon.
Dr Mtumbuka ndi mtumbuka. Aphunzira kulankhula pompano asiya kuyowoya
Vuto ndi wa ku mpoto.Ndale za mmalawi ndi za tsankho ndipo ndi za mzigawo.
Dziko linasintha chotsani kaganizidwe kameneko
100 percent perfect said
Kodi usi wadzima 🙄amajijilikila pakatipa 🙌
During Saulos iyeyi anali kuti and why saanamusankhe?
Pomwe pagona khani ndiposekula makapanipo boma lamalawi tikumvutika kamba kopanda makapan chifukwa tilindizambili zotiyenereza modzikoli dzikomo Dr Matthews
Tikadzaluza tidzavomereze zotsatirazo chifukwa sitikufuna kuti chipani chife.
mulibe utsogoleri umu, zikatha anona ndi aswiswiri dithu
Akulu awa ndithu zadzawina,mark my words
Pakati pa iwe ndi kabambe please ,mulungu atipase
Ine ndamukonda Mtumbuka
Kambalame koulukitsa kamaphonya chisa bwana mukuyenera kukhazika mtima pandi phuma lachuluka. Otherwise you’re a good leader 🎉
Zikomo bwana Bola nanunso mukazawina musazayambe kunena kuti (wakhwitu wakhwitu)
Mtumbuka ndi Kabambe ndiomwe agathandize dziko lino
Where were you Mr mtumbuka?UTM may God see you through
I love you Mr mtumbuka /
Zaziiii bas ina ankatelo
Bola izi sizokhalira kunja nsima misika mumuuze usi apite akajambule tikuferanji komwe akuja chiteze
Malawi is lacking good leadership but these two leaders Mtumbuka and kabambe they must lead us ViVa UTM tsogolo lowala.
Chepesani kusisa voice pa intro makosana
Mulungu alowelelepo plz🙏 all the best
Nthawi yonseyi adali kuti awa ndikudabwa kuti palibe akuluakulu ena palibe apa
Mtumbuka hoyeeee
Zaziii kungofuna kuzaba basi mungakhale prensident waziko inu kungofuna kuzawononga ziko basi bwanji panopa kulinjara osatuluka kuti kamene ulinako wapase anthu ovutika maboza basi
MCP Kuba kwambiri, tengani dzikoli a mtumbuka
Mudzaziwonanso m'mene adzazibere amenewa ndalama, these are politicians, nanji ma amateur
True
Kudzikonda chabe
Palibe zachilendo zikukambidwa apa
There's future
Atumbuka nawo ndiasakho amangofuna okhaokha maudindo wakhwituwakhwitu zanga eine mtumbbuka Bola kana be 😮😮😮
Find another reason. That one is outdated.
@@jonathanmwanja3994pita nazo kwina zimenezo ku UTM kulibe
Koma nanu pano sitikuyendera za ntundu koma yemwe awombole malawi
Tadzilankhulani mukamaiza mupumule tilindi ntchito zomwe tinaziwona kale ndi dpp tikufuna zimenezo zongotinamizazi zatikwana
Pa mbuyo panu inu ndi kambabe kammbilani mugwile limodzi
UTM for sale now
A stitch intime indeed serves nine ,Utm as a problem of kuyang'anira zinthu ( kulekelera even the late SKC had a same problem so izizi we re not sure bwana ,,,,,, cos u have never been there before nde this time around Malawians wants anthu odziwa zintchito osati Ya class ,atleast "Kabambe , Atupele, Chihana and APM
Tiyeni tiyese atumbuka mwina angatithandize
You are right its high time we should try the northerner and its my belief will do better as will be from minority may work for all regions to get the second term.....if we miss this opportunity mmmm kaya
..zakwathuzi sizikuthandiza chitukuko chadziko.....
😢tione zina
Mtumbuka wooooooyeeeeeeee
Mfundo ndiye zikuveka koma Poti a Malawi amadziwa kulonjeza koma kukwanilitsa kumavuta, akangowina amalephela kukwanilitsa zomwe amalonje ,chimene chimakula ndi kudzikundikila kusava zofuna zawanthu komanso kulephela Ku tsegula misika ya a dmaric , koma ngati mukunena zowona vote yanga ndiyanu
Lucky to you!
There is no doubt he is intelligent. Ku MCP kulibe olo wa JCE. Chakwera alibe JC;
Hahahaha
Eti eti ,ali ndi PHD tu uyu
Za school anathana nazo pano alipa school yapa ground
😂😂😂
Good bomaa
amanganya kapena kuti a V P mr usi bwanji sanathamangileko kokadya chitedze abale inu?
please mr. bon kalindo muuzeni mnzanu kuti akasye chitedze pomwe inu mr bon kalindo mukulankhulira anthu chilungamo our advocate amphawife
Ineyo ndikusapota inuyo nose awiri Dr mtumbuka ,komaso Dr D,kabambe inuyo awirinu amene alephele adzakhale wa chiwiri kapena nditi vice president, mpando wa secretary ndikanakonda wini wa mpando umenewu asachoke akhale pomwepo mayi p, kaliati, mayi kaliati chonde sikukunyozani ayi mpando wanu ndi secretary general ndiye wanu mwachoka nawo kutali ndipo umakhalani,chonde chonde mai kaliati.uyu kazitapeyu mumati ndi Michael usi ameneyu akhale owona za achinyamata kapena nditi wa yufi chigawo cha kumwela adzinamiza anyamata akumeneko kuti adzipeza nthawi yopanga madirama ake akumudikira bon kalindo, nginde,mai asikono komaso achisi ndi enaotelo.
Kkk koma ase
😂😂😂😂koma ada
Mwauyu ndikuonamo utsogoleri
English v Mathematics Devaluation v Dama
Kuyankhula kwa munthu oyembekezera kukhala mtsogoleri wa dziko koma kumeneku .
Kulibe mapokoso
mtumbuka mukunama.
Ali ndi befutu koma azalimba during campaign time😅
Fire
Utm forever
CHITSILU CHSKWRRA ANTHU AKUDYA ZOSADZIWIKA CHITSILU MUTU WAMAKO CHITSILU OSAGANIZA IWE CHAKWERA
Amtumbuka aku achita kuphedwa ndimabugwe ,,,zikakhala bwino chikanakhala chiganizochake ndekuti azakhala ngati achakwela sakuziwa chomwe akuchita asongoleni ngati awa aziza yendela maganizo anthu
Wandale aliyese amatero inu Mesa imakhala njira yofuna kupanga anthu kuti adziwe kuti ndiofunikira
Mfundo zabwino kwambiri komaso zogwira mtima koma ofunika anthu kuwachotsa maganizo akuti atumbuka amachita tsankho MMA office kuti azikhala okha okha pachibale Pao
Kkkkkk kusowa msogoleni ndiinu nomwe
Inu mukumunyozani pitanitu mukayimile muli phwii
Good speach.
Kulankhula ndikuchita ndi zinthu zosiyana..ndipo palibe chachilendo apa
Inutu mwinadi kuphula Malawi pa mavuto
Wooooooooo
Kuyakhul bho bho t Mr
Wandale amana muti athu andiphepha mmm izi ine ayi
Palibe mapokoso apa.
Manganya ndiamene wazi hitsa yekha
CHAKWERA AKUFUNIKA ADXAKHALE LIFE NDENDE MTSOGOLELI OYAMBA KUTI ENA ADZATENGEREPO PHUZILO
Kudzangomunyonga bwanji ?
Kamageni kaye Peter uja
🔥🔥🔥🔥🔥🔥