Ambuye akudalitseni ndithu izizi ndizoona amalawi fe tikuyenela kudzuka ndi kuthandizana nao chifukwa sintchito yophweka iyi we have to help them ❤❤❤❤❤
Abd and funso lina ndi lakuti a president antiuza kuti akupita ku Mozambique ndi zimbabwe koma anapitilira kukafika italy ndi jermany bwanji atolankhani sanafunseko zokhudza mayiko awiriwa kuti tidziwe chimene amakachita
We need such checks on these people they are running the gvt as if its their own bussiness entity. Chimwendo banda is more powerful in mcp than chakwera
Mai wa Amalemu sanakwele nawo popeza kuti anali atangofika kumene pa ulendo wautali waku South Korea komwe iwo pamodzi ndi Malemu anakayimila ziko latu. Ngakhale malemuyu anali be chikumbokumbo potengela kuti iyenso anali otopa, koma kuti mwinamwake anakakamizidwa kuti akawonekele mwalo mwa Boma potengela kuti a president amati anali ndi ulendo waku Bahamasi. Koma nkhani Zake.. 😪🙆
more fire chilungamo chiziwike cdedi god may continue kukudalitsan pa moyo wanu watsiku ndi tsiku🙏🙏🙏🙏🙏🙏
MCP, Chimwendo zimuvuta heavy.
Anthu a mcp akutiyesa ngati makape awo sakudziwa kuti tikulilira mmimba,ndiye tsiku lozatulutsa mau kudzkhala ngozi
Koma guys omwe timanyozafe muziganiza anakakhala bare wanu. Kt simunakafuna chilungamo. Onse anja si abare anga koma anafa imfa yowawa .
Ndipo amwene😢
Amalawi enatu nzelu alibe
Anthu akupita kumaka tamandira munthu okupha mopanda manyazi ngati opanda mizimu
Anamiwa mulibwino ine ndilinanu ❤❤❤
Osawanyengelela ma gangster a MCP Mr Namiwa more 🔥🔥 🔥.
Chimwendo anenebwino komaso Mr mwayamba bwino zomwe timasowa kunva ife ndizo izi musalore chonde kuti paloweso chinyengo mulungu azakulipilani moyo wautali plz
Watching from France
Bravo 👏 to the cided 🔥🔥
More fire namiwa azajaira
More Fire 🔥 Mr Namiwa.
Proud of you Sir..
Keep it up CIDED
Thanks very much atsogoleri athu proud of you,,
Akulu nkhani mukuyitenga bwino kwambili ndipo osabwelela kumbuyo plz plz bwana namiwa
Tikudikira ma yankho anyoooooo!!!!
angomangidwa basi onse kukuyu chakwera varentino phiri onse apite kundende basi akolowe basi zoonadi osachedwa ma comrade
You are the real person
Atolankhani kumangofunsa zopepera basi 😂😂😂 CDedi more fire
Koma tidziyang,ana kochoka 2020 kufikila pano asdiki miya anafela ndale chilima anapita ndiathu ena 8 popandapo wina aliyese wa mcp zinatheka bwanji kapena panali line yanji a mery chilima amaenda ndiamuna awo thawi zose anawalesa ndani komaso chimwendo anawalesa ndani kuti asapite oooooooo palikathu mcp ititha tose
Pamenepo ndipomwe amalawi tiziwe kuti achakwera anapha chilima😭😭😭💔
Komad nhimomwemo Anene bwinod
Ipondeni fadah tikuziwa kt ikubwera gear 3
Ndipo sitizamvesa mpaka kale atiuze basi😭😭😭
Ajayila anthu amenewa
Chilungamo chiziyenda ngati madzi akulu akulu
Bwana namiwa tili nanu limodzi tikufuna kumva zoona zokha zokha pa nkhani iyi
Anangopakilamo a UTM okhaokha ndikukawataya kuchikangawa.
Maudindo anawakomela a MCP afika opera anthu
Agwadila iweyo,,,Iweyo mene ukuvekera lilime lakolo unayamba wavoteloko chakwera cibadwileni akutuma adpp
Zikuoneka ngati zocheza koma tsiku lophilika chithupsya likakwana tizachotsa mutu . Palibe ntsogoleli amene anabadwila kusanjika timachita kukuikakoni kukuchotsaniso ndikwaife 7 days ikwana tigwetsa babulo
Usi usanyere bwana❤
Zimenezi mudzimuwuza Billy malata ndi mzake Bennie Longwe ndi Redson Mulo kapena agape khombe ndi mbuli za ant
MCP ikuwona ngati ndi nthawi yakale yongopha anthu mwachisawawa ndi galu wanuyo
Namiwa moto kut bbbbuuuuu
chakwerayo akumpatsa phavu zompusa nyusi wamozambiki wakupha akuchezerana akupha athamangitsidwe chakwera kumalawi
Pitirizani big
Chakwela Ndi chimwendo banda ndi azakewose akwezedwe boti mukawataye pakati panyanja tiwone ngati angapulumuke agalu amenewo amphedwe
Agalu akupha mcp ma devils okha okha ndi useless chakwera
Ambuye akudalitseni ndithu izizi ndizoona amalawi fe tikuyenela kudzuka ndi kuthandizana nao chifukwa sintchito yophweka iyi we have to help them ❤❤❤❤❤
Abd and funso lina ndi lakuti a president antiuza kuti akupita ku Mozambique ndi zimbabwe koma anapitilira kukafika italy ndi jermany bwanji atolankhani sanafunseko zokhudza mayiko awiriwa kuti tidziwe chimene amakachita
Tinachotsa Dpp ndi mademo then iwoso adzachokamo ndimademo ngati 😅😅😅
Mafunso bwana simukumayankha mukuchulukitsa kulankhula zolankhula zizibwera after mwayankha
Congrants mr NAMIWA
Mbuli iyi kupanda kutero sakadya kunyumba or dzina lakero ndi LA milandu basi
We need such checks on these people they are running the gvt as if its their own bussiness entity.
Chimwendo banda is more powerful in mcp than chakwera
We independent investigation about Chilimas plane clash
Chikangawa chikangawa
Opposition kukanakhala anthu angapo ngat nkulu ameneyu bwez zinthu zilibwino
Funso ngati sayankha mupanga chani,
Mukapana yumozi or awiri azaulura chisisi
Hmmmmmmm may those who perished in that tragic accident restwell till the truth comes out for the nation to be at rest
Atiwuze chilungamo
Namiwa akufunika asilikali phwamwamwa. Atetezedwe. Anthu achilungamo ngati awawa amasowa
Anamiwa Moto tili limodzi tiyeni Malawi akufunika anthu ngati inu big up
Ndipo ng'ombe zija ndizawo anakayendela Achakwerazo ife monga aku banja takana ng'ombe sizanthu
Kwayaka.moto kkkkk 😂💪💪💪🔥🔥🔥🔥🔥
Iweyo gwapewe uyende sinanga magogo aja akunyemera ,,apule mtima phee!!!
Mulungu ndi woopsa zoona zeni zeni pa nkhaniyi ziziwika no secret under the sun
🔥🔥🔥
Truth
Zambiri zidziwika za imfa ya Biyeni
Namiwa✊
Chakwera a anaphadi Chilima
Chakwera anapa chilima
The truth must be reviewed
Thilimozi basi❤
💪💪💪💪💪🔥🔥🔥🔥🇲🇼
tithandizeni pankhan imeneyi
Munalibe olo modzi wa mcp Mundege
Tiyeni naone agalu awa
Ndiye kuti mu ndengemo munali anthu 10 kale okwereratu amene andunawo akuwadziwa
Zaziii mukungochedwa nazo zopanda pake inuyo ngati mukuwona palichinqchake chinachitika inuyo bwanji osapeza anthu ena oti akuthandizeni tiziwe chowonadi osati kupita uku kupita uku bwanji nanuso pezani yankho lanu timve
Zaziii . Funk you
Anthu akuyankhula
Iweyo ukuyankhula bwano
Kodi iweyo akutuma kuti maliro ayiniake upangire kampeni magogo aja
Pathako pako iwe cholinga akuveni ndani or mutatani simdzakhala oramura
Zoona zake
Zikusowani zolankhura inu kodi kufa kwamoyo wamunthu mulindibuku la mumalawi wina aliyense yonse munthu azafa inuyo pangani nzeru kuti mupeze lipoti lenileni mukunena zang.ombe inuso ngati ndi kampeni yikuvutani ndithu pano dairy nkhani zopanda pake uposichoni wanu ikuvutani ndithu
😢😢😢truth chilungamo
Dziko ndi lanthu ili asatiopseze
Chimwendo us you can see the truth is coming out
Tiyeni tili pa mbuyo pAnu
Zabwino zonse anamiwa komaso mayi wa malemuwa akueneleka kufusidwa ndi chifukwa Chan sanakwele ndege?
Mai wa Amalemu sanakwele nawo popeza kuti anali atangofika kumene pa ulendo wautali waku South Korea komwe iwo pamodzi ndi Malemu anakayimila ziko latu.
Ngakhale malemuyu anali be chikumbokumbo potengela kuti iyenso anali otopa, koma kuti mwinamwake anakakamizidwa kuti akawonekele mwalo mwa Boma potengela kuti a president amati anali ndi ulendo waku Bahamasi. Koma nkhani Zake.. 😪🙆
Mkaka is playing the card.,
Km big awa amadziwa kukamba nkhani
Inu report simunawerenge
Bwanji osakawafunsa a times kuti nkhani iyi iwo adayitenga kuti nkhani?
Zoona
Chimwendo banda!!! 😂😂😂😂😂
Namiwa machine
We need atsogoleli ngat Namiwa
ndi zigawenga koma anapanga mwa umbuli chuwuluka chimatera kuchenjera ndi kupusa zinawandikana
👍
Tili limodzi guys we want the truth through commission of enquiry
Tiyeni nawoni agaluwa
😂😂😢 truth
zigawenga za M C P
Kamufukuleni chilimayo ngati anali mulungu wanu ndi ngozi imeneija basi ngati chimwendo anapulumuka ndi mulungu yemwe bwanji nanga mary chilima nayeso anasintha ulendowo nthawi yathayitha inu ndi mbuli bwanji anapita basi kenako ndinu mwamva
Chika iwe khala chete
@@MaulanaBanda-r5o kkkkkkkk
Agalu mcp aku gahenna awa
Tiyen
Tien nayo mkhan mpaka tidziwe zoona zen zen
Tikumvera nawo basi
Namiwa ndi zibwezi zake ziwili akaliza akazi phwale
Satana iwe
khaniyi anamiwa ife tilinanu pamozi ndizona ziko si lilibwino pakhani ya ndege komaso athu 9 tiziwe chilungamo chenicheni chifukwa a ndizonyasa izi tikuziona apa nda mcp abwele ayakhule komwe anazitenga khanizo chifukwa akunena zoti ife amalawi tikulephela kutengapo mtu