THE DC IS THE ONE WHO TELLING PEOPLE THE TRUTH TO ANDSTAND EFFECT ON THAT'S ALL THE WAY I'M IN THE SAUTH AFRICA ESTAN CAP THANK YOU MR BON KALINDO MY ALLAH BLESS YOU ALWAYS HAVE A GREAT DAY ORROWYESS
Thanks Bon. I deeply feel that any priest asking for citizens' silence on the Chikangawa plane accident must first silence him/herself in the Spirit. Any gracious priest must flee from the tricky temptation of deliberately misinterpreting related scriptire like Romans 13:1-7). O LORD, save the integrity of our priesthood for a godly Malawi.❤❤❤
Mangochi ndi district yodzuka yosagona sitimaopa ife Ayao amanyi mutimva a MCP ,ife nganganga! Pambuyo pa president wanthu the DC mwana oopsa kwambiri. Ndiponso simukwanitsa kumupha tadzuka , munantola Chilima kuchikangawa pano tonse tadzuka pa ifa ya Chilima ndipo tipanga za ku Kenya very soon.
He feels pain of all poor Malawians Bon Kalindo mwana owopsa kwambiri the DC even angel akukuwombela mmanja good work reveals the truth while the evil hides inside the money
Tikufuna Chakwera adzayankhe milandu yonse,yosakaza chuma cha boma komanso imfa ya anthu asanu ndi atatu omwe anafa ku Chikangawa ndi ena onse ngati Zikhale Ngoma,Mkaka,Chimwendo Banda mkulu wa apolisi,mkulu wa nkhondo ndi ena onse mkazi wa Chakwera komansotu mwana wake Nick
A keyala anakanika kuipeza ndege yawoyawo 24hrs ndiye pano ati akuti akufufuza chomwe chinagwesa ndege kodi achipeza? Kkkkkkkk 24hrs failed to trace ndege by using technology search ndiye achipeza chomwe chinagwesa ndege?
Number Bon kalindo munthu osaopa kotse mulungu azikupatsani moyo wautali 👏👏🔥🔥🔥🔥🔥🔥
The DC mwana oopsa kwambiri from Njedza vg😅😅 love you more
THE DC IS THE ONE WHO TELLING PEOPLE THE TRUTH TO ANDSTAND EFFECT ON THAT'S ALL THE WAY I'M IN THE SAUTH AFRICA ESTAN CAP THANK YOU MR BON KALINDO MY ALLAH BLESS YOU ALWAYS HAVE A GREAT DAY ORROWYESS
CONGRATULATIONS TO YOUR MY BROTHER FRIEND FROM MALAWI I'M OLOSO FROM MALAWI ASHANKWELA HIS MUST LEE SINE PEOPLES OF COUNTRY 👌
The DC fire fire 🔥 your speak true papa don't be afraid, God i will protect you all the time
Watching from pmb south Africa number 1 God first❤
Thanks Bon.
I deeply feel that any priest asking for citizens' silence on the Chikangawa plane accident must first silence him/herself in the Spirit. Any gracious priest must flee from the tricky temptation of deliberately misinterpreting related scriptire like Romans 13:1-7).
O LORD, save the integrity of our priesthood for a godly Malawi.❤❤❤
Bonnnnnnnn kalindooooooooo the DC 🔥fire
Mangochi ndi district yodzuka yosagona sitimaopa ife Ayao amanyi mutimva a MCP ,ife nganganga! Pambuyo pa president wanthu the DC mwana oopsa kwambiri. Ndiponso simukwanitsa kumupha tadzuka , munantola Chilima kuchikangawa pano tonse tadzuka pa ifa ya Chilima ndipo tipanga za ku Kenya very soon.
Fire fire
We silute you the DC. May the almighty God continue protect you wherever uou will go♥️♥️♥️♥️
😂😂😂😂😂😂your expensive mwana woopsa kwambiri eish koma Bon the DC!
Warankhura bwino kwambili kalindo ❤
😂😂😂😂😂😂😂 azunguze anthu okubawa Boooon Kalindooo💪💪
Thanks so 🎉🎉🎉🎉🎉
Thanks for all you doing Mr kalidoo
The DC ! !!! MWANA WOOOOOOPSYA !!! Kwambiri , Nyama muzidya inde !; koma movutika kwambiri !
The DC keep the fire burning.
Thank you very much the DC for your work on behalf of poor Malawian
He feels pain of all poor Malawians Bon Kalindo mwana owopsa kwambiri the DC even angel akukuwombela mmanja good work reveals the truth while the evil hides inside the money
Watching from zimbabwe DC
😂😂😂😂amasulidwe basi Ana akubawa atikwanaaah
😂😂😂😂 kma bon kalindo chipongwe eee kkkkkk the Dccccccccccc
😂😂😂😂😂😂 Iputeni milandu inayo ife tiri ku msana kwanu😂😂😂😂😂 mantha njeee
Ndimawona ngati alankhula zanzeru awa tinvomereze kuti mukufunika kubwerela ku uphuzitsi kuja mukapange upgrade chifukwa chomwe mumapanga ndikunyoza koma osabweretsa solution.aaaaah
And Kodi mukufuna ife tizitengeka Nanu kenaka mudzatipusitse Pamawa mwayiwala kuti munanena nokhat zakuti Malawi siomufera? Ndiye musatikwanepo apa
The DC 🔥🔥🔥
The Dc mr bon kalindo you are talking true. M C P Must go Out we don't want m c p any more.Mr bon kalindo more
God always protect you, Chilungamo chako Mulungu akuziwa kufunika kwako kwa ife
Akuti osampha mwanako bwanji!😂😂😂😂 Koma kalindo.. kkkkkkkkk
This nation needs causal factors that lead to the plane crash not autopsy reports.
Ambuye mutetedzereni bon kalindo ndi munthu yemwe akutitthonza pa mavuto athu
A Bon kalindo inuyo mulungu adzikudalitsani ndine Luciano kuchokera ku Mozambique
DC woyeeeeeee katundu womanga ndi mawaya
Stand to honest Mr kalindo
Inu ndi 1 Bon Kalindo 😂❤❤❤❤❤❤❤❤❤
,,ngakhale tili Mayiko akhunja tizabwela tizaku votelan Mr bon karindo
Kkkkkkkkkk if you try to catch my people I will catch you 😅😅😅😅😅😅😅
Watching you from Zambia ❤❤❤❤❤❤❤
😂😂😂 aidya nyama koma azidya akulila kkkkkkk
You are becoming bakili muluzi TV 😂❤❤❤
😂😂,😂😂the diiiisiiiiii
Ndimakunyadilan the DC tilinanu
Chilima anaphedwa ndi Chakwera. Aliyense akudziwa zimenezo ndipo ndikudikira mwachidwa kuti atiuze chomwe chinamupha Saulos Klaus Chilima
Tifufuza mbuziyi ikatuluka mboma...ndipo chikaferatu kundende chimfiti chimenechi.......mbuzi😮😮😮😮😮
Ati tikusendani😂😂😂😂
The DC more fire anthu admarc bwana akuvutika kooopsa bwana president wa osauka
Asaaa koma winiko mpaka amako😂😂😂😂
My vote
😂😂😂😂 ati atamangidwe ndi amako😂😂
The DC ❤❤❤❤❤
😂😂😂Akakumanga bail ilipo
Kd nanga ma demo aja Mesa lero pa 10 tulukan munyumba am already outside
The Dc good Messnge Mr bon kalindo ❤
Tikufuna Chakwera adzayankhe milandu yonse,yosakaza chuma cha boma komanso imfa ya anthu asanu ndi atatu omwe anafa ku Chikangawa ndi ena onse ngati Zikhale Ngoma,Mkaka,Chimwendo Banda mkulu wa apolisi,mkulu wa nkhondo ndi ena onse mkazi wa Chakwera komansotu mwana wake Nick
We follow
Captain kalindo dolo kwambili
The DC😂😂😂😂😂❤❤❤❤
Moto booo Dc tililimozi ❤❤❤
A keyala anakanika kuipeza ndege yawoyawo 24hrs ndiye pano ati akuti akufufuza chomwe chinagwesa ndege kodi achipeza? Kkkkkkkk 24hrs failed to trace ndege by using technology search ndiye achipeza chomwe chinagwesa ndege?
Komaso Bon kalindo ndimangowona ngati tingopeza nafeso futi kujozi kuno timenyane ndiboma lachakwela ukuwona bwanji
Inenso ndikuona choncho
Tiwachotse agaluwa
Keep fire burning
Umakwana boma lautsiru kwabasi
Kkkk boma laluza milandu
😂😂😂😂😂😂😂😂😂 Born kalindo 🙏🙏🙏🙏🙏
D c wi love you 🎉
The DC Born
DC he is the voice of the voice less
Uthenga wamphavu kwambiri ife tili pambuyo
Mfana oophya kwambili
Unasala wekha bon anzako onse anadyesedwa ma banzi pano ali chete
Km ndodo iyandikile coz komwe tikupitak kulib kuchez
Antongwetongwe olalikira hahaha
Boni kalindo moto kuti buu umatiyimilila
❤❤
Watching from israel pa boma
Uyu ndi one😂
The DC njedza Villege TA MABUKA
Yomweyo DC😅
👌👌👌👌👌👌👌
Koma kumenekoo!!
Zikuyenera kutero, DC ndiwe President. Ukuyenera chitetezo chochuluka ndithu. Komanso achitetezowo awonjezere, azikwana 3000
Amve pain amenewo
Boni kalindo keep it up
👌
Enafe nde tinasiya kale kale kuonera Mbc tv
Thanks watching from Blantyre
Kodi za ma demonstration pa 10 July zili Pati?
nane ndufuna kuziwa.. zilipati zakuyenda pa nseu lero?
Chakwera sakumvesa za kulimba mtima kwako
Thanks bon kalindo
Moseliwa
Osaopa
Akalindo
Zoona bon kalindo mulungu alinawe
Koma sakuyamkhulapo za manganya ku mcp
kod mesa mmat lelo tikathamange kod ??
🎉🎉🎉🎉🎉
😅😊😊😊😮
❤❤❤
The dc
Moseliwa mapwiya......
The DC ❤❤❤❤❤❤
Mwana ooopsyaa kwambiri mulungu akudalitse
The DC mwana owopsa kwambiri
Lelo ? Wait for next
Chilungamo chi ma wawa chikamayakhulidwa