COMRADE NTANYIWA CHAKWERA WAPELEKA 1 BILLION NDI CHOLINGA CHOFUNA KUTHANA NDI PETER MU PARLIAMENT

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 59

  • @chrispinchirwa9563
    @chrispinchirwa9563 20 годин тому +7

    Tionera pamenepa ngat tili ndi ma MP wokonda dziko kapena ndalama. Mbuzi za athu aphese a malawi a galu

  • @HassanMawila-h5f
    @HassanMawila-h5f 19 годин тому +6

    Chakwera chiseko chammpana😂😂😂😂😂

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi 20 годин тому +4

    President wamtima oyipa Chakwera

  • @Michealangabi
    @Michealangabi 19 годин тому +4

    Ntiponyeleni nambala yanu amtanyiwa pali nkhani pa namwera turn-off ku zomba malosa

  • @PatricaTchuwa
    @PatricaTchuwa 19 годин тому +5

    Mfiti chakwera chimuthu cha kumidima

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 12 годин тому +1

    Apm akumuopatu ......😂😂😂😂😂 Adad more fire ife tili ndiinu ...boma la chikangawa ratikwana

  • @AminahMussah
    @AminahMussah 19 годин тому +3

    ine nde chakwela wafika ponditopetsa nsaname aaah

  • @ALLIEDAUDI-w6t
    @ALLIEDAUDI-w6t 20 годин тому +1

    The first mn to view this groglam now

  • @LilianKachala-yz2xf
    @LilianKachala-yz2xf 10 годин тому

    Koma ma MP amenewo tilinao ntchito.ife ndalama zaozo adye ife sizikukhud,a wathu ndi APM basi.akuimatu Peter basi. Go konko.

  • @LameckDanken-tm4rt
    @LameckDanken-tm4rt 20 годин тому +7

    Tonse amalawi tiyeni ku paliament

  • @StalnLossan
    @StalnLossan 4 години тому

    Mmmmm km achakwera e wandikwana

  • @DalitsoMatope
    @DalitsoMatope 19 годин тому +3

    Chakwera nyelo ya mako

  • @bellsnampanda
    @bellsnampanda 11 годин тому

    Chaza.mdiyani Chakwera mulungu amukhulukire

  • @mussakapalamula1990
    @mussakapalamula1990 14 годин тому +1

    Mulungu ndiye ndi yankho lathu a Malawife tikuvutika kwambiri sizinaoneke.

  • @EUGINEMWADALA
    @EUGINEMWADALA 6 годин тому

    Or APM atapanda kuimila, MCA ikutulukabe m'boma Basi enough is enough

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 13 годин тому

    MCP nkhaniyi sayimalizayi ndipo ayaluka zedi ziwavuta sure

  • @AndrewChilambo
    @AndrewChilambo 8 годин тому

    Kodi apm mkumuwopa chani kulephela kwanu sivuto la piter mthalika

  • @ElizabethKachipeso-rl8fi
    @ElizabethKachipeso-rl8fi 19 годин тому +8

    Ai mwachedwa nayo tiyeni mwaumuthu tikaonane kovota gt muli ndiathu gt athu amakukondani mukuopa chani likondeni dziko amalawi tikulila 😭😭😭😭😭😭

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 12 годин тому

    Munthalika simumukwanksa...machepa Achikangawa party

  • @AndrewChilambo
    @AndrewChilambo 8 годин тому

    Inu ndinu mfiti zakupha mlibe manyazi ziwani mkango ndi mkango mcp ndiyakupha

  • @augustinechibbalazi8897
    @augustinechibbalazi8897 13 годин тому

    Malawians with me inclusive, are going to polls this 16 Sept.How are we thinking? Going to polls in a country of
    wrangles instead of first bringing Unity and Freedom in Malawi. Thereafter, free and fair tripartite Voting.

  • @alfred-i5p
    @alfred-i5p 14 годин тому

    Chakwera akulimbana ndi machine, APM ndiye vote ya aMalawi

  • @RiteRoderick
    @RiteRoderick 13 годин тому

    Amalawi osalorayi zopusa tipite ku parliament zibwana ai dziko ndilathu ili ndipo parliament ndiyaife not ma MP

  • @McDonaldbeketeNkhata-n4l
    @McDonaldbeketeNkhata-n4l 6 годин тому

    Chakwera watha zeru palibe chimene akuchita sizitheka

  • @Hannif-o2z
    @Hannif-o2z 10 годин тому

    Chakwela akunama afune asafune peter aimaso

  • @JamesMaduka-wk8xi
    @JamesMaduka-wk8xi 7 годин тому

    Kukula 😂kwa Peter mcp sizikwakhudza iwowo apangezachipanizawo sizugwilizana ndikunyumbayamalamulo ukokuphelawanthuufulu dpp iwonayokhazoti a qpm akula osatiiwowo iwowo apangezawo

  • @WysonAdamu
    @WysonAdamu 12 годин тому

    ine antanyiwa ndikufuna ndikufuseni Kuti Kodi chipani chayemcp anthu Ake amaganidza chifukwa Apapa mwachidziwikile Kuti sakugona Tulo ndiadadi

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 20 годин тому +2

    Ndiwe galu kwabasi chakwera wukufuna ife amalawi tizidya manyi Ako mbuzi musiyeni Peter jealous basi zisiru za MCP foseki

  • @JamesMaduka-wk8xi
    @JamesMaduka-wk8xi 7 годин тому

    Mcp yazindokilazoti mpatailibe

  • @DavidJackson-ox4xm
    @DavidJackson-ox4xm 13 годин тому

    Chakwera anya manyi this year

  • @MosesTangwe-q8o
    @MosesTangwe-q8o 11 годин тому

    Ndipo tisasekelere zopusa ai asatisankhire zochita ife stikukufuna takukana basi

  • @annuelkadyenji9457
    @annuelkadyenji9457 17 годин тому

    A comrade nkhani mukaiyamba muziimaliza chifukwa mumatisiya mmalere

  • @KondaniPhiri
    @KondaniPhiri 15 годин тому

    Tipite tonse amalawi komwe tikasokhane nawo popanga zaozo akaziweso kut nafe takwiya. Dziko sila chakwela ndila ifeyo amalawi. Osati anthu akunyumba ya malamulo. So tiyeni komweko. Bas

  • @MariaMponda-n6p
    @MariaMponda-n6p 16 годин тому

    Mumakwana komaso mumandipeza

  • @RuthChimangeni
    @RuthChimangeni 14 годин тому

    🤣🤣🤣🤣🤣 MCP yachepa ndipo samukwanitsa muntharika

    • @RiteRoderick
      @RiteRoderick 14 годин тому

      Ana achepa a MCP 😂😂😂😂😂

    • @RuthChimangeni
      @RuthChimangeni 13 годин тому

      @RiteRoderick akusowa kosewera

  • @MerryMolitchi
    @MerryMolitchi 15 годин тому

    Zobisa zidzaululika lero siizi

  • @ThomasMlowoka
    @ThomasMlowoka 18 годин тому

    Chiseko champana ameneyu

  • @Alliechamolie
    @Alliechamolie 12 годин тому

    Amalawi tapusa kwambili ziko ladyela

  • @GiftBello-v1i
    @GiftBello-v1i 17 годин тому

    Muthalika sakuimila MCP asaiwale kuti ndi wa DPP , malamulo awowo akhle Ku MCP konko

  • @TechZaketa
    @TechZaketa 16 годин тому

    Anyamata zakanika kuyendetsa dzikoli aaaaa

  • @DetterYasin
    @DetterYasin 16 годин тому

    Yeheva atithandize

  • @GiftBello-v1i
    @GiftBello-v1i 18 годин тому

    Like it or not no more Mcp , ndalama landilani mudye ndi mana amenewo koma mukavote mwah nzeru

  • @ChomboNgosi
    @ChomboNgosi 16 годин тому

    Chakwera mulungu akuone ndithu

  • @MerryMolitchi
    @MerryMolitchi 15 годин тому

    Kuthatha ndi moyo

  • @SusanPilingu
    @SusanPilingu 17 годин тому

    Kodi Ambuye mwatikwiila ife Ana anu tikhululukileni tikubvutika ife dzikoli POTI osauka alibe mau ndalama zikalankhula chilungamo chimakhala chete

  • @MercyChiwaya-um6us
    @MercyChiwaya-um6us 16 годин тому

    tionana ku September

  • @LesterManyengo
    @LesterManyengo 18 годин тому

    Wamulakwira chiyan?ambuye kumwambako paja oyenda ndi kupanga,lake lowelo limusakaze, pharaoh walimba mtima,ambuye athere mmadzi pharaoh ameneu

  • @JohnBamusi-o8l
    @JohnBamusi-o8l 20 годин тому +1

    Eeeeee😂

  • @AishaMuhammad-v8m
    @AishaMuhammad-v8m 18 годин тому

    Mulungu atichitile chifundo ndithu

  • @SmartMailos
    @SmartMailos 18 годин тому

    Akuopa a,mcp

  • @EmilyKanyika
    @EmilyKanyika 18 годин тому

    Achina chikangwa mcp machimo