Chipani Cha DPP Si Munda Wa Munthu - Nicholas Dausi
Вставка
- Опубліковано 27 сер 2024
- DPP Spokesperson Hon. Nicholas Dausi says the DPP is not someone's personal estate. It is a party of the people and the people are free to elect a leader based on the party's constitution.
Mneneri wa DPP Hon. Nicholas Dausi wati DPP si munda wa munthu. Ndi chipani cha anthu ndipo anthu ali ndi ufulu wosankha mtsogoleri potengera malamulo a chipanichi.
#malawi
Adad omweo
Whether you had a meeting or not, we need Arthur Peter Mutharika. Iweyo uzamvotere Nankhumwayo.
basi nkhalamba....anthu mulibe pothawira pena eeeti
Adausi munalidi mchipani cha dpp inuyo? 2020 dpp siinaluze masankho Koma anthu okhala ndi mtima ngati wa inuyo ndiamene a Nakonza chiwembu chomulanda boma mwaupando kuzera mumakhoti athu
aaa inu nde Sitingakuveleni Mabodza anuwa Dad bas ap
A Dad number 1 apa basi osati zanuzi a Dausi a Malawi sitidzakhulupilaso Munthu wamba kulamulilaso dziko IA Malawi
Who started DPP Party was Dawus or who? I've one question to you Dausi in Malawian parliament, is there any opposition leader?
Namkhumwa ngat akulephela kuyendesa paliament monga munthu wosusa ndiye angayendese dziko molongosoka. A daus sakudziwa chomwe akwelacho kut ndi chan
Kkkkkk nankhumwa zikumuvuta ku parliament angovomera zilizonse ndiye u President azautha bwinotu anthunu musagulitsepo chipani apa anthufe tikufuna Peter yemweyo basi
Ngti mukuona kuti adad saima mwalimba madzi daudi wankhala mcp kamudzu alipo ndy mukuona ngti muthu angamvere zainu palimbe mongopola moto adad2 akuimaso tinasiya kunkhulupilira adakhwi dziko lamalawi linapenya pano.
Uyuyu simunthu wamba
Honourable dausi talking exactly
Komabe we need adad omwewo
True speaking mr Dausi
Awa akufuna zosangalatsa thupi lawo
Sunati ulirad kuyendesa dzikotu sikuyendesa banja zimafunika anthu adzeru iziih sukuvesa mpati bankha iwe kkkkkkkkkk adad akuwinabetu ufune usafune
Muthalika never inspired me 😮 need new face in dpp
Mr Dausi alakhula zoona zake Ali ndikhutu amve
Pamtumbo pano dausi ndi amene akuombela manjawo
Adausi awa ndye akalamba ndi nzeru zomwe,, hule uyu
Iwee dausi tadzingodya nawo za mbava chakwera ukakhala usatanic ndi wake mudzikangomwa nawo magazi boma lokupha lokuba loipitsitsa
A Dausi zisiyeni...ngati mwatopa ...pitani ku MCP komweko....koma DPP adzsimira Mutharika.
Choka iwe dausi wadyera iwe
Choka galu iwe bakhalani ku MCP komweko wathedwa nzeru komanso dollar 💵 inakutherani pano mukufunafuna podyera
Inunso a MCP mukulubwalubwa Kodi chakwera ku MCP anavotedwa ni ndani? Kuchoka pa a tembo kufika chakwera atembo anakapikisana ni a chakwera? Agalu inu zaunyau basi za michira lendeéee
Iweyo Dausi ndiye umaganiza kuti DPP ndi munda wako? a DPP anakutola ndikukusambitsa iweyo ndi sopo wamakaka ndiye wayamba kuinyoza. Iweyo unali ndani Kamuzu atamwalira. Ngati simumadziwa DPP inachokela ku UDF. Iweyo unazolowera kupha ndi John Tembo umaganiza ngati kuti ineyo sindimakudziwa? Ndiye ndikuuze upite ku CI Ku Montfort Parish olo Bishop House ukafunse za ine . Unali ndani iweyo apa sindingakukumbe iweyo.. waiwala iweyo nthawi imeneyo
Koma chilungamo APM azaluzitsa chipani Kodi munthu wina kuchipaniko kulibe? Ngati kulibe basi 2025 iwalani Za DPP kuzalowa muboma mupakana muzapeze munthu wina not APM plz
Awa ndaakatundu
Koma 2025 dziko lonse likufuna adad iwe zitha mau
iwe dausi wadyela upeze Malo amodzi oti uzikhala ukungoti uku wapita Koma bwanji kukalamba dzelu kapena zantha
Choka iwe nkhope ngati manyi opondedwa nditayala ya trakita kodi anthu nonsenu mukufuna chani mukufuna ife anthu cholinga muzitidyesabe mayianuwo muona kuti azakuvoteleni ndindani
kkkk mukumva anyani inu a Mzomera ngwira ndi Magogo Gondwe ndi Jappi mhango
😅😅puwa person who are you,pls thank before you talk,sanje basi ,polanimoto abrother ,muzafandi bipi malume, kulankhula zopanda kumanga chipani ,akupasanindalama Kuti mukalankhule zopanda pache ,nkhondo siyimanga muzi polanimoto, APM ayimaso basi,
Kungoti kuyipa moyo komweko agalu inu ndi amene mwatiyika pa moto lelo malawi akuvutika chifukwa cha astana inu bwanji osapanga chipani chanu
Wina ayi adadi omwewo Nakhumwa ayi bolanso tupere
Mwati sagwirana ma jurrata😂
Dzimitu Dzanu 😏
Mbolo yako dausi