Nicholas Dausi at MCP, facing President Lazarus Chakwera

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 25 січ 2024
  • Honourable Nicholas Dausi speaking at the Mwanza development rally where the president of Malawi, Dr Lazarus Chakwera was present

КОМЕНТАРІ • 361

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata6933 5 місяців тому +24

    Anthu akuononga malawi ndi amenewa

    • @user-kp6ng8bc2f
      @user-kp6ng8bc2f 5 місяців тому

      Day wa one kuzachimanga Kaye chikachapike mutu ku maulako

  • @innocentissah2636
    @innocentissah2636 5 місяців тому +18

    Anthu adyera amakhala ndi mbalume ndikuonera chitsiru chimenechi chotchedwa Nicholas Dausi

    • @innocentchapotera7416
      @innocentchapotera7416 5 місяців тому

      adzafa imfa yowawa kwambiri

    • @petereliezer3795
      @petereliezer3795 5 місяців тому

      Osapsa mtima ndale za ku malawi ndi part of entertainment 😂

    • @patrickmasa7145
      @patrickmasa7145 5 місяців тому

      Uziwa et zongovela izi dausi macheza awa ahaaa kuwatengela upusa adha​@@petereliezer3795

  • @KennedyTchauya-fl5yk
    @KennedyTchauya-fl5yk 5 місяців тому +3

    The king is back🌋🌋 welcome Mr Dausi , home is best

  • @DokotalaPhungu-lk4kn
    @DokotalaPhungu-lk4kn 5 місяців тому +7

    Dausi kujiya kumeneko. Limbikira akupasa u minister. Udyeretu. This is your last term.

  • @EmmanuelMbilu
    @EmmanuelMbilu 5 місяців тому +17

    Ill never stop following him or atasitha chipani🔥💯...... He's just a vibe person 😂

    • @jacobjerome6538
      @jacobjerome6538 5 місяців тому +1

      😂😂😂😂😂😂 munthu osokoneza ngati uyu ine sindimamuonepo ayi,kuchenjela kwake koopya heavy

    • @MacDonaldkachala-cm5gc
      @MacDonaldkachala-cm5gc 5 місяців тому +1

      Dausi greatest of all times, good vibes😁😁😁

    • @towerankhoma1380
      @towerankhoma1380 5 місяців тому

      Ndipo inenso sindidzasiya kumukonda 😂😂😂

    • @user-jq1gy5ds9n
      @user-jq1gy5ds9n 5 місяців тому

      Kwambiri kumalowa chipani chabwino osati chipani chamunthu

    • @DickLinje
      @DickLinje 5 місяців тому

      ❤😮 of😢😢
      ​@@jacobjerome6538😅😅🎉😢😅😅🎉

  • @InnocentKapesi-gx7yf
    @InnocentKapesi-gx7yf 5 місяців тому +9

    Awa ndi achitsiru kwabasi

  • @user-oh5vs1gl4n
    @user-oh5vs1gl4n 5 місяців тому +12

    chisilu chimenechi ife pambuyo pa adadi

    • @NgomaRaheem
      @NgomaRaheem 5 місяців тому

      Ako nde wasiya kut nawe bwampini

  • @HarveyMhango
    @HarveyMhango 5 місяців тому +1

    ❤❤❤❤ Ambwana umatha

  • @carlossadimba595
    @carlossadimba595 5 місяців тому +1

    That's great move Mr president and braval to Mr Dausi you are taking a good choice .....

  • @joeljere4385
    @joeljere4385 5 місяців тому +3

    Chakwera ❤ Dausi❤

  • @GeorgeFwanthaphiri-ov4bt
    @GeorgeFwanthaphiri-ov4bt 5 місяців тому +2

    ❤❤❤❤❤

  • @StevenPongolani-pp9by
    @StevenPongolani-pp9by 5 місяців тому +5

    Politics is the game of thrones

  • @smokeestery1101
    @smokeestery1101 5 місяців тому +5

    Ukalande mcp,, DDp waikanika, sungaithe dpp ase wachepa

  • @user-qh5jo5qh3b
    @user-qh5jo5qh3b 5 місяців тому +2

    Apm my vote

  • @WilfredMathews-yl6ij
    @WilfredMathews-yl6ij 5 місяців тому +4

    Politics is the game of Numbers 😂😂❤

  • @rodglae6657
    @rodglae6657 5 місяців тому +1

  • @user-uc1pd1tc2x
    @user-uc1pd1tc2x 5 місяців тому +12

    Mbalame yokuba iyi achita Manyazi APM akulowa boma❤❤❤

  • @Johnfrank-gi5uc
    @Johnfrank-gi5uc 5 місяців тому +4

    Imeneyo ndiyo Democracy aliyense ali ndi ufulu wopita komwe akufuna ineso ndiponso ku UDF don't blame it's my rights to do so, thanks

    • @khaleedsaidi6232
      @khaleedsaidi6232 5 місяців тому

      Democracytu taionatu ife ndipo ndakulupilila kuti anthu a dpp analidi ademocracy ndipo anthu aja asakhala ademocracy. Nthawi ya dpp akaitana amcp kuti akhale pamonsi amakana lelo Iwo aliboma akawaitana a dpp akumabwela semene zikuoneselatu kuti dpp ndi imene imaziwa democracy ndiime phopo bwanji

  • @DanielJuly-dj2ji
    @DanielJuly-dj2ji 5 місяців тому +1

    Dausi is too clever. Eish ! 🤐🙌

  • @patrickmpinganjira3099
    @patrickmpinganjira3099 5 місяців тому +1

    My man Hon. Nicholas Harry Dausi

  • @noelcheonga8247
    @noelcheonga8247 5 місяців тому +1

    Dausi I like this politician whether he changes side to MCP I like his character

  • @evancenasoro922
    @evancenasoro922 5 місяців тому +8

    Ukatelo afuna malo ukoooo😂😂😂😂 ichiiiiii

  • @MatthewsPhiri-jh7zl
    @MatthewsPhiri-jh7zl 5 місяців тому

    Welcome back

  • @IbrahimWezely-qd4vj
    @IbrahimWezely-qd4vj 5 місяців тому +3

    Feel free this is your original party, takulanfirani madala

  • @mcbethmbewe5421
    @mcbethmbewe5421 5 місяців тому +1

    A rolling stone gathers no moss...

  • @lazaruschitsamba8394
    @lazaruschitsamba8394 5 місяців тому +2

    no this is politics

  • @issahabdullah7186
    @issahabdullah7186 5 місяців тому +1

    These Greedy politicians doesn't care for the Needy

  • @user-qq3ip1od6i
    @user-qq3ip1od6i 5 місяців тому +4

    Munthu oipaaaaa,, wadyela.. Osakonda dziko

    • @luciuschigoga2607
      @luciuschigoga2607 5 місяців тому

      And when he left MCP for dpp he did well neh?
      Wise up

  • @user-nj3pv2wc1n
    @user-nj3pv2wc1n 5 місяців тому +1

    Zoona boss

  • @kha6068
    @kha6068 5 місяців тому +4

    Abambowa ndi achitsilu chonchi kani

  • @baziliobwanali4753
    @baziliobwanali4753 5 місяців тому +1

    Keep going Dausi

  • @GladysGwaza
    @GladysGwaza 5 місяців тому

    The servant of the people ( do service to the people)

  • @josephngoliwa
    @josephngoliwa 5 місяців тому +1

    Hon. Dausi thank you simunanyoze Dpp and APM.. Zikomo.

  • @HenzelPat-vd8cz
    @HenzelPat-vd8cz 5 місяців тому

    🔥🔥🔥🔥

  • @user-oo5bx1rl3j
    @user-oo5bx1rl3j 5 місяців тому +2

    Iweyo Dausi ukuganiza kuti anthu angadye stadium. Ndikupempha inuyo a MCP don't trust Dausi olo anthu akwào samàmukonda ai monga ndanenela kale kuti he is a sweet talker

    • @luciuschigoga2607
      @luciuschigoga2607 5 місяців тому

      Inu mmafuna anene kuti chani chomwe bomali siikudziwacho?

  • @user-hm1bf6cw8t
    @user-hm1bf6cw8t 5 місяців тому +1

    Dausi ndi machine ayiseye 🔥

  • @franciscazuwawo3426
    @franciscazuwawo3426 5 місяців тому +4

    Dausi ndikatundu 😂😂😂🙌🙌🙌

  • @TrimaMpima
    @TrimaMpima 5 місяців тому

    Yee

  • @mijerimasiye7310
    @mijerimasiye7310 5 місяців тому +1

    Malawi walero womvetsa chisoni zedi nkhalamba zingotipusitsa zili pheeeee

  • @user-dv7ht6vn9s
    @user-dv7ht6vn9s 5 місяців тому +1

    Ku Mwanza samufuna uyu.... Kubisa mawanga mbuzi iyi... Fisi wachabechabe.... Sadzawinanso ku Mwanza

  • @MacDonaldkachala-cm5gc
    @MacDonaldkachala-cm5gc 5 місяців тому +4

    Dausi , leaving DPP, knowing that it's worn out and no direction, it just moving like a dragon fly, Martha😂😂😂😂

    • @AnnoyedCaptainHat-ol4dj
      @AnnoyedCaptainHat-ol4dj 5 місяців тому +1

      Koma Dausi ndi mbuzz eti

    • @backfordrowanlwazi7892
      @backfordrowanlwazi7892 4 місяці тому

      Mukunama mufunseni Dr Joyce Banda mpaka kuthawa mudziko muno

    • @backfordrowanlwazi7892
      @backfordrowanlwazi7892 4 місяці тому

      Late Nelson Chikalamba Khonje anali waku Khondowe Nkhata-Bay north anakana mai ake omubereka

    • @MacDonaldkachala-cm5gc
      @MacDonaldkachala-cm5gc 4 місяці тому

      You can't join your mother, it's not a choice It's by nature, you can join the party 'coz it's a choice, just because DPP it's not a party, it's Mutharikas family business that's why things are going this way, I understand it's not a problem for jobseekers, the yes bwanas 😂😂😂

  • @user-kz3ps1je1n
    @user-kz3ps1je1n 5 місяців тому +3

    Sadziwa chomwe amafuna uyu

  • @InnocentNkhonyo-rs9lq
    @InnocentNkhonyo-rs9lq 5 місяців тому +2

    Malawian politics

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg 5 місяців тому +2

    Dausi, Dausi, Dausi..........ayi zikomo Ambuye akuone ndithuuu.

  • @user-gk6bf7xe9g
    @user-gk6bf7xe9g 5 місяців тому

    🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️🙋‍♂️

  • @MaryTchapo-py4hh
    @MaryTchapo-py4hh 5 місяців тому +2

    Atha bac

  • @user-ir5xk2sw3k
    @user-ir5xk2sw3k 5 місяців тому +1

    Uyu ndi swiswili uyu Dausi!

  • @HelvBen-sc1zu
    @HelvBen-sc1zu 4 місяці тому +1

    Ichi nd chitsiruuuuu

  • @user-ie5pc4ox8i
    @user-ie5pc4ox8i 5 місяців тому +1

    Olo chakwera sakumutorela kuyankhula ichichi aaaaahhh

  • @robertrichman9376
    @robertrichman9376 5 місяців тому +2

    Mbuzi iyi

  • @yamikanijames6915
    @yamikanijames6915 4 місяці тому

    Welcome to MCP Mr dausi

  • @moseskavalo3304
    @moseskavalo3304 5 місяців тому

    Kkkkk tizilpa koma, we are sinners, too much lies and hypocrisy

  • @TamandaniMwale-sr8vd
    @TamandaniMwale-sr8vd 5 місяців тому

    Shaaaaa Kalulu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl 5 місяців тому +5

    Ndausi ndi opusa kwambili

  • @BlessingsButao-cm8sx
    @BlessingsButao-cm8sx 5 місяців тому

    All the best

  • @TimbaTv001
    @TimbaTv001 5 місяців тому +1

    Nkhope kunyasa ngati manyi

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 5 місяців тому

    Nonsense!!

  • @chifundokumbali-nv7fz
    @chifundokumbali-nv7fz 5 місяців тому +1

    Awa ngadyera

  • @JamesSaidi
    @JamesSaidi 5 місяців тому +1

    ineso ndikumva sugar ndima comment dpp is winning this game

  • @Yamikie-yamikie
    @Yamikie-yamikie 5 місяців тому

    Ngamisala awa

  • @ChikondiChikwakwa-if7du
    @ChikondiChikwakwa-if7du 5 місяців тому +2

    Kkkkkk ndale zimampangisa munthu kukhala chitsiru ndithu

  • @user-bg3rt8dy8u
    @user-bg3rt8dy8u 4 місяці тому

    Nice

  • @user-cm5pv8dn7k
    @user-cm5pv8dn7k 5 місяців тому +4

    Machende ako chi nicholasi dausi omafuna udindo ku dpp mukuziwa kuti APM sakucheza ndi ana

  • @YusuffuDaud-cs7yu
    @YusuffuDaud-cs7yu 5 місяців тому +1

    Monica ndiye watchena ndipatse number yako

  • @StiveriaChikonga-rh3fi
    @StiveriaChikonga-rh3fi 4 місяці тому

    A chitsiru awah 😎 ndiye ukuwona ngati mene wa choka ku dpp ife tikukusowa umatipasa bzy saname buzi iwe

  • @merviselias6230
    @merviselias6230 5 місяців тому +3

    Tinakutulukani adausi ahule pa ndale,,😂😂😂😂

  • @timothylipenga8413
    @timothylipenga8413 5 місяців тому

    Chi Vibe 🎉🎉

  • @user-ft9ex5gy5c
    @user-ft9ex5gy5c 5 місяців тому

    Even president akuziwa Kuti ndi tambwali uyu.kuthwa pakamwa zaziiiiiii

  • @SACHAMAGIC
    @SACHAMAGIC 5 місяців тому +1

    Politricking at crimax

  • @Phill-nh8ru
    @Phill-nh8ru 5 місяців тому

    A president akukupusitsani ameneyu wadyela mndalama uyu. Koma palibe oposa DPP pa chitukuko olo kumwamba kukudziwa mulungu ndi mboni

  • @user-oe5vb2in3e
    @user-oe5vb2in3e 5 місяців тому +1

    Dausi abambo oputsa heavy

  • @wangachindeya8577
    @wangachindeya8577 5 місяців тому +2

    😂Ineyo sakomenteso 😂 ndikugonva kukoma ndi makoment ndawaonawa 😂😂😂zadziwika kut dpp ndi boma basi ❤
    Apm woyeeeeeeeeeee❤❤

    • @user-ee6be5kl5o
      @user-ee6be5kl5o 5 місяців тому

      wapanga bwino dausi kuchitaedwa ku chipani Cha dpp , akunama uyo afuna kukudyelani ndalama chenjerani nayeni ameneyo akukupusitsani ndinthila kuwili mumasokoneza kwambiri

    • @LenzoChilek
      @LenzoChilek 5 місяців тому

      Oyee!!!!!!!!

  • @user-kp6ng8bc2f
    @user-kp6ng8bc2f 5 місяців тому

    Ulibe mfundo Nicholas dausi. Iwe ndiwadyela basi palibe chimene unachita cha nzelu ku mtundu wa a Malawi. Ndiwe mbuzi ya munthu masikini weni weni

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi 3 дні тому

    Musavotere anthu woyenda ndi mphepo ngati amenewa

  • @NgomaRaheem
    @NgomaRaheem 5 місяців тому

    Iyi ndembuzi yeni yeni ndithu machende ako galu

    • @victorbanda9039
      @victorbanda9039 5 місяців тому

      Mpaka kutukwanatu wasiya machende abambo ako kutchula aazako

  • @user-vp8mr5ot7q
    @user-vp8mr5ot7q 5 місяців тому

    Mbava is shame to my motherland country, Guys we must know that we gonah be same like zim

  • @RonaldFunsani-ik1us
    @RonaldFunsani-ik1us 5 місяців тому +1

    Chisilu ichi chokuba chifuna chikwama ichi

  • @user-qe2lv3hs8q
    @user-qe2lv3hs8q 5 місяців тому

    typing....

  • @chrisschikozera7271
    @chrisschikozera7271 5 місяців тому

    😂😂😂😂.....my question is where is chilima since I don't see him wht going on 😅

  • @user-cb2cv9fz7m
    @user-cb2cv9fz7m 5 місяців тому +1

    Awa kkkkkkk maliro wo mulira ambili

  • @AkiduMustapha-vq2nt
    @AkiduMustapha-vq2nt 5 місяців тому +1

    Iziiii ndichifukwa dziko silikupita pasogolo Kuba omwewo amabawo akungodzungula ndimaudindo kumangosintha zipani

    • @madalitsoonale5338
      @madalitsoonale5338 5 місяців тому

      Ndipo kwambir awa akubwezeletsa chitukuko pambuyo

  • @geraldmtika7961
    @geraldmtika7961 4 місяці тому

    Kodi vice anajomba this day?

  • @user-dl8ng2zn1r
    @user-dl8ng2zn1r 5 місяців тому

    Daus

  • @user-nm8gp1du2m
    @user-nm8gp1du2m 5 місяців тому

    Awa ndiwosokonekera awa,,, zakuziwa chimene akufuna panoyo pa moyo wawo.. Akungosokoneza Malawi

  • @prestonkasito1815
    @prestonkasito1815 5 місяців тому

    Akuluwa

  • @madalitsoonale5338
    @madalitsoonale5338 5 місяців тому +1

    This man is stupid, with such kind of these people thus y Malawi is going nowhere

  • @tricknkhatah
    @tricknkhatah 5 місяців тому

    Dirty game 😅 interesting game.

  • @stevenfrancism3638
    @stevenfrancism3638 5 місяців тому

    Dousi Dousi Dousi, umafuna chani kwenikweni?

  • @user-xd2uz1bh3l
    @user-xd2uz1bh3l 5 місяців тому +1

    Dausi watha bas. Ndipo saoloka pa ndale ai😂😂😂😂

  • @user-wi9hz8fk8i
    @user-wi9hz8fk8i 5 місяців тому +1

    Wakulizani Dausi makape

  • @chikondipound5077
    @chikondipound5077 5 місяців тому +1

    Be careful with him he is a snake in the village not in the grass ,he did a lot of bad things during kumuzu

  • @user-ip9ei9ko9v
    @user-ip9ei9ko9v 5 місяців тому

    Zaziii

  • @user-js3ds5qz4r
    @user-js3ds5qz4r 5 місяців тому +4

    Kkkkkkk Koma dyela ndimatenda pakulira iwepo dausi mmmmhu

    • @user-pn7cj9hb3t
      @user-pn7cj9hb3t 5 місяців тому

      Eti eti kape weniweni

    • @user-cq1wv9nq4y
      @user-cq1wv9nq4y 5 місяців тому

      Zovetsa chisoni ndipo abambowa afika pa uchisiru ndithu

  • @user-sp3iu3rv1t
    @user-sp3iu3rv1t 5 місяців тому

    Dawusi usazaende Dela lakwathu ku zomba tizakugenda ngati kwanuko anakwanisa kumubera chakwera wakoyo carpert ifekuno tizagenda conivo

  • @user-cm7zw6pk6d
    @user-cm7zw6pk6d 5 місяців тому

    Amadyera mphotho bambo Nicolas Dausi .Amakometsa kumene kuli madyo .

  • @simonpaul6567
    @simonpaul6567 5 місяців тому +1

    Mbuzi yamunthu iyi

  • @petermsamariamapira8933
    @petermsamariamapira8933 5 місяців тому

    be careful Mr President anthu wa amayimbila ng,oma komwe kuli mpunga, cholinga azidyabe ,ovutika kumangofutuka ,Mulungu akuona

  • @wilsonali7890
    @wilsonali7890 5 місяців тому +1

    Zitsiru za anthu izi

  • @dicksoncassim1954
    @dicksoncassim1954 5 місяців тому +1

    Iwe ndi wa congress iwe wachita bwino kukuthothora ku mcp

  • @user-qp8kh2hj9o
    @user-qp8kh2hj9o 3 місяці тому

    Dziko la Malawi linatembeleredwa anthu opanda umunthu ngati awa ndi omwe akupangisa kuti anthu azivutika