Zomwe Apanga A UTM Kuchoka Ku Tonse Alliance Zandisangalatsa - Manza Wa Kwa Chinsapo

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 11 лип 2024
  • On Nyasa VoiceBox, a Malawian named Manze from Chisanpo in Lilongwe shares his thoughts on UTM's decision to exit from the Tonse Alliance.
    Pa Nyasa Voicebox, M'Malawi wina dzina lake Manze wa ku Chisanpo ku Lilongwe akufotokoza maganizo ake pa ganizo la UTM lotuluka mu Tonse Alliance.

КОМЕНТАРІ • 20

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 26 днів тому +5

    Kumuikapo manganya chifukwa manganya ndiyemwe anapeteka chilima mmanja mwa cakwera kuti amuphe ndimkona anamuika pampando at avice president akunama manganya wangoona kutenga sambi chabe

  • @Hamzamabvuto
    @Hamzamabvuto 26 днів тому +4

    I'm the first person to comment here I love UTM but I'm not the member of UTM

  • @MerryWayson
    @MerryWayson 26 днів тому +3

    Achita bwino kuthesa ❤❤

  • @JairoseManuel-p5p
    @JairoseManuel-p5p 26 днів тому +3

    Sanalakwise kuchoka

  • @SHEREEFKanthochi-ft3dm
    @SHEREEFKanthochi-ft3dm 26 днів тому +3

    inenso ndikunva kukoma zedi

  • @DannielOnions-fy3dc
    @DannielOnions-fy3dc 26 днів тому

    Nice one thanks U.T.M MORE

  • @susantembo2076
    @susantembo2076 26 днів тому +1

    UTM please forge ahead. Don’t listen to any other distractive noises

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 26 днів тому +1

    Mumakwana inuyo more fire 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @raffickaffick
    @raffickaffick 26 днів тому +1

    Bravo fada

  • @AugustineTheu-of6nv
    @AugustineTheu-of6nv 25 днів тому +1

    Zikomo kwambiri nkulu wanga kwa mawu ako ogwira mtima. Inenso m'bale ndikanakhala mwana wa chilima mbuzi imene ija Chakwera ndikanamuthamangitsa pa maliro kuti asowepo. Amene uja si president ayi

  • @VeronicaChirwa-ct4os
    @VeronicaChirwa-ct4os 25 днів тому +1

    Manze ndagwirizana nawe kwambiri pa zomwe wanenazi. Inenso Chilima akanakhala m'mbale wanga sindikanalora kuti abwere pa maliro a Chilima. Ndipo ndikanachita zoti amalawi sanaziwonepo. Kaya ndikufa nanenso ndikanafera pompo. Chakwera ndi munthu oyipa kwambiri.

  • @stevenfrancism3638
    @stevenfrancism3638 26 днів тому

    ❤❤❤❤❤❤

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 25 днів тому

    Ineyo ndinakakhala m'bale wanga ndinakati Maliro sikuika tiyeni tikamutulire chakwera akadye sured pakanavuta komanso sinakalora wina aliyense wachipani cha MCP kupedzeke pa Maliro ndithu kunakachema

  • @Felista-m4q
    @Felista-m4q 25 днів тому

    Inenso ndanyadira kwambiri

  • @ErnestChansa
    @ErnestChansa 25 днів тому

    Mwalakhula fundo zabwino big chakwela ndi galu yambuzi fiti

  • @MacleanKwacha
    @MacleanKwacha 25 днів тому

    Ndipo ine ndizafunisisa anthu amenewa asazaikidwe,tizadyere nsima

  • @user-ui4ux5kc8d
    @user-ui4ux5kc8d 25 днів тому

    Ngakhale kufa kwake kwachakwera anthu tidzavina kusangalala ndipo kaya imfa imeneyi kwaiyeyu ikuchedwa patii munthu oipa uyuu akanafa koma ndithu ambuye timenyereni mkhondo afee ndithu presedent ameneyi

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 26 днів тому

    Kuga mwacakwera anthu tidzakondwa komanso kuvina kuti chokupha chija chafa

  • @gracemkandawire8769
    @gracemkandawire8769 25 днів тому

    Tiyeni tizavotele UTM. Kuti mzimu wachilima uzause mu mtendele