Mary Chilima wadandaula ndi kuchedwa kwa Commission of Inquiry; Chakwera wasolora K1.5 trillion

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 30 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 557

  • @mustazahra8398
    @mustazahra8398 2 дні тому +86

    Kwa ife amene timslowa pa UA-cam just to check if bakili muluzi tv has posted let's gather here

  • @rabisonpias5131
    @rabisonpias5131 2 дні тому +95

    Musamasowe koma a Braz, UA-cam is boring without kumvera BAKILI MULUZI TV.

  • @ganizankabango
    @ganizankabango 2 дні тому +36

    BAKILI MULUZ TV FANS LET'S GATHER HERE ❤

  • @ElatonGwaza-k4h
    @ElatonGwaza-k4h 2 дні тому +25

    Kupanda chilima agalu awa sitikanawa votera

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 2 дні тому +15

    Chakwera ngakhale atatumbwa motani adzafa basi ...or atamuonjezera zaka 1000000 adzaduduluzidwa pakhosi ...satana wachabechabe

  • @BeckhamDavid-v6c
    @BeckhamDavid-v6c День тому +11

    Brother musamasowe chonchi tikudalila inu kutidziwitsa zomwe dziko lanthu likuyendera respect boss❤❤❤❤❤

  • @HoskiesCharley
    @HoskiesCharley 2 дні тому +42

    Bakili Muluzi tv fans lets gather here

  • @frankjolijo
    @frankjolijo 2 дні тому +16

    aaa Malawi tinapusa kwambili 🤦🙆🤦🙆🤣🤣🤣🤣🔥

  • @MafavukeJere
    @MafavukeJere День тому +13

    Amene timati chakwera mchikangawa let's gather her

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 День тому +8

    Muno masanje ayi ndipo likoma sitikugulitsa,, gulitsani central region mukapeze kokhala

  • @veronicamalisero2671
    @veronicamalisero2671 День тому +5

    Koma awawa kuyankhula kot akafika pamalo minimum ndi 31years guilty conscious sikuwagwila komwe aliko?zimachita kuoneswlatu kut Biyeni samawafuna kuyankhula ngat mawa kulibe...sine wa ndale koma MCP ikudzipanga decompaign yokha..the economy is bad no wonder mayiko ena ukamacheza nawo anthu Ake amangoti Ku Malawi kosauka..shameeee dziko longokhalila ngongole silingatukuke zilingati mamuna okonda katapila

  • @WalterkinnelyPhiri-ey2yy
    @WalterkinnelyPhiri-ey2yy 2 дні тому +11

    kamajekete salephera kumutchula umva ka ma jeket 😅😅😅😅😅

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 День тому +4

    Chakwela ndamene adapha Chilima amalawi osapusitsika kumaona momwe palili pa ground, Chakwela ankamuzuza Chilima uja and ankati sakuimaso 2025.
    Osafusaso umboni wina
    Chakwela aimbidwe mlandu wa murder anapha chilima.

  • @temwekamlenje4358
    @temwekamlenje4358 День тому +7

    Ndimaona ngati Gotani Hara ali ndi nzeru koma ndi chibekete chodontha ngati a china kamajekete

  • @ShorishKenneth
    @ShorishKenneth 2 дні тому +13

    ❤❤❤❤first comment here gather all as l love BAKILI TV

  • @StevenGeoffrey-bf5io
    @StevenGeoffrey-bf5io День тому +5

    Ndipo live bigy tinakusowani ❤

  • @SHABILUKAZEMBE
    @SHABILUKAZEMBE День тому +4

    Amalawi ndi anthu abwino osangomuwombela bwanji chakwelayu

  • @JamesMasanje
    @JamesMasanje День тому +4

    Kom chikangawa forest

  • @AhmedHchipelesa-zm8oe
    @AhmedHchipelesa-zm8oe 2 дні тому +3

    As malawi we always appreciate u bro u have open all the hidden things in Malawi

  • @MbwanaAckren-hw5fy
    @MbwanaAckren-hw5fy 2 дні тому +4

    Inuyo ndi big bwana! Ulemu wanu!

  • @SaidiBaneti
    @SaidiBaneti 2 дні тому +4

    umakwan bakili muluzi tv 📺 ❤❤❤❤

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg День тому +3

    Akulu akulu Mary Chilima and all malawians of good will deserves better. Inuyo tangoganizani:
    1 Ndege yopanda blackbox kumukweza VP wa dziko.
    2.Ndege yopanda recorder, no any communication koma yanyamula Vp.
    3.Ndege yokugwa 10am kusaka kukayamba 5pm, zoona izi??
    4.VP sanapezeke, koma kukaimisa kusakidwa kwake zoona??
    Kodi zomwe zinachitikazi olo ali Chakwerayo olo mwana wake, akanakhutisudwa nd report ya German ija?????

  • @CharlesfisheFrank
    @CharlesfisheFrank 2 дні тому +2

    Indotah yami ubuyile manje🎉 ngiyabonga sakuazah buthih😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😅😅😅😅

  • @Moses51
    @Moses51 День тому +3

    Mai malemu chilima mmmm waondatu amalawi let be together with mai mery chilima

  • @augustMag
    @augustMag День тому +2

    All the time best Bakili Muluzi TV Boma lopanda Chilungamo ngati limeneli silinaonekepo aluza kale chisankho achoke

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti День тому +3

    Welcome back bwana, timakunyadilani.

  • @giftelesoni
    @giftelesoni 2 дні тому +2

    You are talented guy no matter now you're attacking politics and attack them bro truth shall never perish

  • @EnerstManess
    @EnerstManess 2 дні тому +2

    Malawi kungonkgala ngat atidyesa mankhwala atulo abale satana akuyendela chakwera ndiwaphavu kwambili

  • @KarimTapyMshanga-kd1vz
    @KarimTapyMshanga-kd1vz 2 дні тому +2

    God's watchmen Bakili Muluzi Tv

  • @mollymasangano473
    @mollymasangano473 18 годин тому +1

    Mang'anyanso nde Kaya akuti Mulungu wadalitsa iiìiiiii. Koma abale 😅😅😅😅😅 Manganje kugudika nawo Amalawi musatengeke.

  • @GanizanMillias
    @GanizanMillias День тому +2

    kung'alura osaopa iyayi,ife pambuyo pano

  • @LovemoreSambuke
    @LovemoreSambuke День тому +2

    M'dima ungakule bwanji kumacha

  • @Razarusmbavachakwera
    @Razarusmbavachakwera 2 дні тому +1

    Bakili muluzi tv is here ndipo zisakho zikawandikilamo chonde bwanawathu pofunika ma software otse ndima computer 🖥 azakhale m'manjamwanu muzizatiwuza mene zizizakhalira

  • @alicdante
    @alicdante 2 дні тому +1

    Adolo awawa or atayamba campening kutasala one day yovotera. Titha kukuvoterani tose tikuonera this channel ❤❤

  • @HamzahMiles
    @HamzahMiles День тому +1

    Am sure kuti plan ya ndege ija anthu ambiri a mcp amaziwa 😢but what I like mulungu anati every soul shall test dieth 😭 no matter what

  • @FortyoneHarwa
    @FortyoneHarwa 2 дні тому +1

    Tinanzipha tokha ku votera. M. C. P. Tiyeni mifuti nafenso tikaphe akulu akulu a. M. M. P

  • @paulnyondo7572
    @paulnyondo7572 2 дні тому +1

    Chipani chakupha cha mcp .kupha anthu 9 simasewela bakili muluzi ananena kale kuti ndichipani chagazi .amalawi gotani hara ananena kale kuti mcp yikuyenera kupitiriza kukhesa mwazi kuti yipitilire mpaka 2030.si uyu chilima wapelekedwa nsembe pamodzi ndi anthu 9.ofunika amalawi tisamale ndi mcp chipani chakupha chagazi

  • @kubengovender6996
    @kubengovender6996 2 дні тому +1

    Bakili muluzi UA-cam channel is back to basic let's gather together!!

  • @AyandaPhungula-bg9ql
    @AyandaPhungula-bg9ql День тому +1

    Ndale sikumphana kodi a MSP mudakhala bwanji kungongala ndi ntima wakumpha basi eish 😢😢😢😢

  • @LuciusMakupe
    @LuciusMakupe 2 дні тому +1

    Kma anthu awawa samachilapa bwanji everytime misampha Yao ikungoulurika kma ndithu anthu opanda manyazi osasintha kti mwina nkutinamiza ndi tizitukuko kma eeee Mulungu tiomboleni nanga mafuta aja anakalandira ku Nsanje aja iii

  • @VincentMatola-s8g
    @VincentMatola-s8g 2 дні тому +1

    Kkkk chibwana chimalanda mulungu anavomeleza zofuna za akumalawi posankha MCP anthu ngati sasamala ndikuthawila kwa mulengi wawo akhala m,mavuto oposa amenewa

  • @PETERPHIRI-v9e
    @PETERPHIRI-v9e 2 дні тому +1

    Ngati sindinavele bakili muluzi tv sindimava bwino chonde musamasowe❤

  • @KennedyKanyama-ce8lb
    @KennedyKanyama-ce8lb 2 дні тому +1

    Aaaa osamadabwa ngati akuchedwetsani dziwani kuti ochedwesayo ndiamene anapanga zimenezoyo

  • @FamousKitchen-r2o
    @FamousKitchen-r2o 2 дні тому +2

    History is best teacher ❤

  • @RAFICKRAHIMUMUSSAH
    @RAFICKRAHIMUMUSSAH 2 дні тому +1

    After longtime no lisen so am suffering toomuch. God bless you brother

  • @ibrahimalfred6539
    @ibrahimalfred6539 2 дні тому +1

    Popeza Amalawi sitichedwa kuiwala tikavotele mcp so kachiwiri

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 2 дні тому +5

    Gotani Hara Chimene munamanga ndi Chimenechotu. Munamanga Kuti muphe Chilima ndipo munaphadi .
    M H S R I E P ✝️ ✝️✝️
    VP SKC.
    Chakwera munthu Woyipa
    Chikangawa Party 👹⚒️🐊🐊🐊⚒️👹 Banja la mzako lili pa umasiye chifukwa cha Mtima wako wa Ng'ona.
    Unaphera CHILIMA Udindo.
    God will punish you Lazalo
    Well done Brother from BAKILI MULUZI TV
    Stay blessed 🙏
    Stay safe ✊✊
    Fight for the better Malawi ✊ ✊✊.
    God bless you Brother .
    Good work: Unforgettable moment : 10 June 2024
    CHIKANGAWA
    MZUZU

  • @maxwellmashon4897
    @maxwellmashon4897 2 дні тому +1

    Anthu oipa awa ndi amene anapha anthu ose aja anali mu ndege komanso anapha Mia

  • @MATTHEWSGPHIRI-ho7ud
    @MATTHEWSGPHIRI-ho7ud День тому +1

    Bwana munasowa 😢 musamasowe chonchi pilizi 😮

  • @JamaniNyirongo
    @JamaniNyirongo День тому +1

    Zaka 31 galu iwe kukamwa ngati konyera bakha

  • @AmanaHambalie
    @AmanaHambalie 2 дні тому +1

    Akutitu musamale akutelo kamasaya Billy malata

  • @EdwardGeorgeKasabola
    @EdwardGeorgeKasabola 2 дні тому +1

    Big man watulukira sopan

  • @EllenChimera
    @EllenChimera 2 дні тому +1

    😂😂😂😂😂MG 2 ndi blesser😂😂😂

  • @ChikumbutsoDzukwa
    @ChikumbutsoDzukwa 2 дні тому +1

    Ipondeni Fadah 💥🔥

  • @DouglasDazuKamwendo
    @DouglasDazuKamwendo 2 дні тому +1

    Mhunu vakashata but Mwari ariko.

  • @VajraBanda
    @VajraBanda 2 дні тому +1

    A zibabo🎉🎉🎉🎉🥰🥰🥰🥰

  • @PreciousChibwana-q8q
    @PreciousChibwana-q8q День тому +1

    Ulemu wanu bro❤❤

  • @PatrickMailos-j6u
    @PatrickMailos-j6u День тому +1

    Achimwene musamasowe

  • @Vincent-k4y
    @Vincent-k4y 2 дні тому +1

    MCP chipani chamagazi

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe День тому

    Mg2 yo kodi mmodzi yekha .!!? Vera kamtutukule.ndi Mary yolamu..kkkk kodìonicayo alibe nsanje ? Kumamudyera kudya kwake iyeyo ali pomwepo ? 😮😮😮😮😮

  • @JosephIsaac-s1c
    @JosephIsaac-s1c День тому

    Brother Bakili Muluzi tv and Comrade ntanyiwa may almighty God continue to bless and protect you wherever you are ❤❤❤❤❤❤

  • @augustMag
    @augustMag День тому

    2025 ikuchedwa kiufika kuti tichose Boma lopanda Chilungamo ndi chifundo Bakili Muluzi TV 🔥🔥

  • @KhachimiluShaffie
    @KhachimiluShaffie 2 дні тому

    Brother wa Bakili muluzi TV. ifetu timakukondani kwambiri kotero ife tinali tikudandaula nditu ... Mulungu akudalidzeni nditu kwambiri..❤❤❤ the best history.

  • @Paulo-f5d
    @Paulo-f5d День тому

    Adala inuyo musadzafe mudzango kusowa,eeh koma awonekela poyela chakwela, fiti yamuthu kubisa brack box ,mkumapatsa ndalama woumba,alibe zelu ,local Mozambique

  • @Dean-l5d
    @Dean-l5d День тому

    If I buys bundle..it's bcz I love this channel...God protect you Bakili TV

  • @STEVENMPONDA-o6r
    @STEVENMPONDA-o6r День тому

    CHAKWELA nd muthuu wakuphaa anamuphaa CHILIMAH ndpo anamuphera u dindo CHAKWELA ngwaa kuphaa ndthuu

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe День тому

    Kkk monicachakwera alipo mankhwala akuti kumeneko kwakoko kozizirako kuzikoma..ukafunse azimai a kuchiradzulu distruct ndi thyolo ndi zomba district and mulanje and phalimbe districts and machinga and mangochi districts . akugulitsa ndipo a chikangawa wo sadzapitanso kwa Vera kantukule ndi mai yolamu..kenakio ungomupusitsa chikangawayo akhale bambo " Nanyo " kuti asamaphensi anzake kkkk uchitatu sieti mònica

  • @Moses51
    @Moses51 День тому

    The best TV only we have in Malawi BAKILI MULUZI TV keep up updated osawopa until chikangawa chibwele poyela

  • @ThivadoartistDyson
    @ThivadoartistDyson День тому

    Vuto ndife amalawi, timavela anthu omwe ali kudyelera dzikoli anthu ochepa okha omwe ali pafupi ndi president, iwe akudya money, akukhuta ,akumwa tea ,komanso akuyendela magalimoto apamwamba, koma ife osauka ,ovutika ,osowa ,anjala, ausiwa ndipo ndife ma millions ya anthu tikuvutika palibe chomwe boma mkutibela tikamalira ,boma likubweleka ndalama zochuluka mmaiko akunja mmalo mothandiza dziko ndi anthu omwe tikuvutika ndipomwe iwo akugawana okhaokha ife mkumapitilira kuvutika, koma tili buzy kumavelabe iwowo, zachisoni kwambiri pano akubwela ndi plan yobela zisankho mkumati tiyeselele kkkķkkkmk amalawi ndife ovetsadi chisoni, zomwe tikupangazi ndichimomodz bambo ndioledzela akagwila ganyu amaiwala kuti pakhomo pali njala yonse amakamwela mowa ,mai akagwila kut akagule ekha chakudya akupatsanso bamboyo kut akamwele mowa mkumalilabe pomwe tikuchita mwadala, kuvotelanso mcp . Ndipo kudzaliranso mtawina mcp palibwino adzangootcha dzikoli chifukwa tilibe mzelu, tikuvela chimwendo banda, tikuvela kunkuyu, tikuvela zikhale ng'oma anthu ochepa zoona akufuna tiwapatsebe mwai omatizuza chonchi.

  • @johnmussa7461
    @johnmussa7461 День тому

    Awa ndiakutundu ....kulankhula ma live okha okha ....check n arrest but no where to be seen ....still releasing the fame.

  • @lingsonmitunda293
    @lingsonmitunda293 День тому

    Thank you BMTV
    Chipani cha MCP tikuchithetsa mdziko muno ndipo akanganya onse awa alowa ku ndende.
    Keep this screenshot.

  • @davidkadyakapita8836
    @davidkadyakapita8836 2 дні тому

    Ulemu wanu Big man.Manganya ndi Iscariot kumene.Adagulitsa ndi kupereka Chilima ndi Kasambala komanso miyoyo 8 ina ija.

  • @FywellDjali
    @FywellDjali День тому

    Our history teacher, Mr Bakili Muluzi TV we always appreciate you for teaching us and always stand for your people Malawi big up Bakili Tv.

  • @RuthChilobwe
    @RuthChilobwe День тому

    Kapena kukoma kunatha..amangozizira .amai nonica chakwerawo kkkk.ndiye bola kufa .nanga ena azikudyera kudya kwako iweyo uli pomwepo...kumeneko.

  • @stanleychipyela5275
    @stanleychipyela5275 День тому

    Koma siboza ai president chakwera akuziwapo katu pa infa ya chilima ndine wakuzambia siboza ai yehovah mulungu wamakamu akuona tidikile kaya bwanji

  • @rodrickmphamba3847
    @rodrickmphamba3847 День тому

    You always gather real facts before talking that's why am always trusting your source man. Keep up the good work

  • @macrozajailos8548
    @macrozajailos8548 День тому

    May God forgive us....our willingness for change costed us what we couldn't afforr to lose.

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 13 годин тому

    Mukapeza wa MCP aliyense mupheni ndipo palibe mirandu iliyonse.

  • @MiracleDamiano
    @MiracleDamiano День тому

    AMBUYE tichitiren chifundo dziko lathu 🙏😭😭😭😭😭

  • @PaisonUmali
    @PaisonUmali День тому

    chilima adandimema kut votele chilombo aas😭😭😭😭😭 ndikadadziwa sakadayiona yang vot Koma mulungu yekha amuonetsa

  • @IdrisahChuma
    @IdrisahChuma День тому

    Koma zobela zisankho 2025 nde muiwale ndipo ife sitingalole zachibwanazo munya muona anyapapi

  • @AnussaKaupa
    @AnussaKaupa 8 годин тому

    Timakunyadiran mupitirize kumatipasa zosiyana siyana tiziziwa zochitika zamayiko azathuwa kuti kurinj

  • @AnussaKaupa
    @AnussaKaupa 8 годин тому

    Timakunyadiran mupitirize kumatipasa zosiyana siyana tiziziwa zochitika zamayiko azathuwa kuti kurinj

  • @victormbewe7462
    @victormbewe7462 День тому

    Osamangoyankhula pa social media pano ngati ndife mbuli krausi chilima convinced us to get this manyaka and now it's our own time to change the goals of our children 💪💪💪💪

  • @JesseKanjanga
    @JesseKanjanga День тому

    Kwathu ndikulira kuilira mizimu yonse ija9,Ambuye aulura zobisikazo

  • @AbdulrazaqHussain
    @AbdulrazaqHussain День тому

    Ladies have a heart, don't just utter your words b4 you think, remember time changes everything, fear the time mama

  • @Homeofpeace321
    @Homeofpeace321 День тому

    Manganya anamupeleka Chilima kuti aphedwe, anaulula kuti they were about to end aliance ku MCP then zinapangitsa kuti kasambala aphedwe ili trap yopha Chilima. Izizi ndili ndi umboni koma kuti ndiwasumile andimanga popeza ali m boma

  • @MarkChunda-i2m
    @MarkChunda-i2m День тому

    Mtendere sitiupeza chifukwa ana aja sanali anthu wamba😢😢😢😢😢😢😢😢

  • @AndrewjemesJemes
    @AndrewjemesJemes День тому

    Achilima ngwilizano unawaphetsa koma nthawi mkachitsiru chilungamo chizawoneka

  • @BatumeyoChikopa
    @BatumeyoChikopa День тому

    But why chilima😭😭😭adalakwanji mhsrip but God knows 😢😢

  • @LoydMcheleka-uq3ix
    @LoydMcheleka-uq3ix 2 дні тому

    Tiyeni tingopanga za azanthu ku Kenya ,tiyambile pompano pa social media kupanga mademo keneko tikathele pamusewu , osakatengaso chilolezo

  • @OssmanAbubaker-w3x
    @OssmanAbubaker-w3x День тому

    Zoonadi brother these are useless Government and they are criminals MCP ndi chipani chasatana

  • @eunicesaiti
    @eunicesaiti День тому

    Pamalo 31 years, Really? Malawi is a democracy country, get it!!!!

  • @webstermbewe8395
    @webstermbewe8395 День тому

    Thanks for the update we have been waiting for this continue to give us the best analysis of what is happening around the world

  • @SkeffaKaifa123
    @SkeffaKaifa123 2 дні тому

    Best TV bakili muluzi my Brother congratulations ❤

  • @rashidsaid2232
    @rashidsaid2232 2 дні тому

    This people they must get under arrested in 2025 they made Malawians poorest than any country

  • @Joe-h9v
    @Joe-h9v 2 дні тому

    Dziko ndilawathu dzaka 31 dzambwiyu 2025 mukuchoka mwatikwana agalu inu tikufuna umboni wa chilima

  • @aubreykamwendo4315
    @aubreykamwendo4315 2 дні тому

    Ine chomwe akfuna anthu awawa sikuchiziwa 😢kodi ndlama zonse zomwe abazi akadyela kut God have in this country

  • @WatsonValeta
    @WatsonValeta День тому

    Chakwera it's very useless poyerekeza ndi mtengo wa mlombwa

  • @LysonKumwenda-v1m
    @LysonKumwenda-v1m День тому

    Iwe kukhara mobisara mpaka liti wa bakili iwe chifukwa MCP m boma sichoka ase becare 😂😂😂😂😂