I don't know why Malawi has never recognize Chitsitsimutso choir in a special way.I have known this choir since I was in Primary school.Respect to this choir❤❤❤❤❤The best choir in Malawi.
Great ❤❤job well done guys mwaimba momveka bwino ndipo movetsa chisoni how l wish malawians could recognise you.may the soul of SKC continue resting in peace taluza great man you will remain in our hearts forever bwana 😢
I don't know why Malawi has never recognize Chitsitsimutso choir in a special way.I have known this choir since I was in Primary school.Respect to this choir❤❤❤❤❤The best choir in Malawi.
🙏🙏🙏 you have been following us........ much respect
Inde kuli azinyongo nthawi imeneyo
@@viennasamuel2976 till date alipobe 💥💥💥
Analakwisa kwambili inakakhala kuti ndingozi athuwa sanakamwalila ayi mwina anakangovulala Koma siku Lina mulungu azaonesa zose
Achakwera ngati simulapa ndithudi magazi aanthu awa adzakhala pamutu panu mpaka tsiku lodzayamkha mulandu kumwamba chifunga chikunenedwa apa ndinu😢😢😢 akuti tsiku lina dzuwa lidzawala chifunga chidzachoka meaning tsiku ina inuso mudzakhala nyembo 😭😭😭😭😭 imfa ya chilima pafupifupi aliyese akuloza chala inu mwachita kutani inuyo lapani mudakali ndi nthawi 😭😭😭😭😭
Great ❤❤job well done guys mwaimba momveka bwino ndipo movetsa chisoni how l wish malawians could recognise you.may the soul of SKC continue resting in peace taluza great man you will remain in our hearts forever bwana 😢
You're really our heroes keep on going, may living God continue blessing you guys
Uzakungunukatu siku lina amalawi azaziwa zonsezo coming soon kuti tiziwe chilungamo mr chifunga uzakungunuka siku lija likubwela ukungunuka zuwa la yehova likazawalamo
Very very brilliant song guyz mumatha kupanga compose nyimbo mwaliladi mosanyengelera ayi may his soul rest enternal piece
Well done guys chifunga ndi chakwera yah yah
Ngozi anayipanga yinatheka Koma kutuma anthu opanga chisoni kukamaliza chifunga chakwera mmmmn ndalama unabwereranji athu ataya chipangano Mai ine mmm😊maso gwaaa
Iwe chifunga😢😢😢
Chifunga tsikulina chidzakungunukadi nyimbo yokhudza
Chifunga
What a song..chifunga chinatiphweteka..tikudikira dzuwa layehova❤😢
Legends in music at the same time RIP Dr. Chilima
Continue Resting in Peace SKC. You were our hope for a better Malawi. All in all, we Praise God Almighty in everything 💔
Lukas Kaphereni and others RIP
Great work
😢😢😢😢😢😢mmmmmmmmmmmm chifunga cikungunuke pompano
Chisisimutso imatha kuimba hvy ❤❤
Zosamvesetseka Koma God is good
This choir is number one in malawi
Mcp paulendo basi
One hell of talent here❤❤❤❤
Dzuwa la Mulungu likubwera iwe chifunga
What a touching song ,RIP SKC😢
Zoona iwe chifunga chakwera kupha anthu osalakwa
Rest in peace doctor chilima
Great
Ikufunika aitane ku nyumba ya pre akaimbe nyimbo yabwino
😭😭😭😭😭
😭😭😭😭😭😭😭💔💔💔💔💔
Uzakungunuka
RIP SKC
Zoona imfa ya chilima ndi anthu ena ndi yovetsa chisoni
Chitsitsimuso choir is the best
Rip chilima 😢
RIP SKC😢
Ameni
😢
Chifunga
Mm mm God why
Literature
Please taponyani nyimbo zambiri za chitsitsimutso
Check out another one
❤❤❤ you guys