let's all take part in whatever is happening in our country that can develop our country and don't waste time and point fingers at the Government us as Malawians have the ability to develop or put Malawi on the map let's try to find a way to solve our daily problems together we can.
I stand with Ellen the hand over of government from one party to another has been ignored each every party one to implement there own programs throughout the old one how can we go ahead with this spirit
Ndagwilizana ndi fundo yakuti ndarama zimene zikuperekedwa zantukura pakhom ziziperekedwa kamba kakuwapasa athu tcito yakukoza misewu ndizinazotero cz zovuta ndizambili kom ngati mukuwapasa athu ndaram zaurero who is going to fixed our problem please let's think about it
Izizi zinandiphonya ..the first question was "what was wrong with this country kuti zinthu zisamayende bwino?" The answer is simple ...our economy is not stable ,why, the who panel of the cabinet and the president himself don't know nothing about economy azutsogoleri anthu alibe upangiri odziwa kayendetsedwe ka chuma Malawi muno akukanika kuika ndondomeko zoti kodi dzikoli katundu akhale stable asamangikwera every month titani nanga kuti anthu zakudya zipezeke titani
The lady in yellow killed it, very confident and straight
Good conversation
It has to rotate in whole country, so that many views can be heard and build one nation with strong pillar
Fredokis this is great initiative, let the youths come together mobilize resources and have more of this conversations
Had time to watch eeeh this is What we all need Fredo you're a true leader Ntchana, let's change our Country 🔥🔥
Malawians youths and mum let's gather here ❤❤
I wish zinthuzi zitapitilira ngati mademo aja ankati this week Lilongwe the other week Zomba. Nde kaya bwana Fredo mtitelo kaya.🎉🎉
I am beauty James from Dedza malawi but am watching this program in south Africa and l really like your program my brother fredokiss continues this
Nice 👍 fredokiss keep it up of the good work
Thats good development mr Fredo keep it up biggy
Great brother fredo keep moving on that vision l hope you will build great Malawi 🇲🇼 am kenneth following in South african
As Malawian we need leader like him ❤❤❤
This is very greatly needed in all cites ndithu 🔥🔥🔥
Big Up Fredokiss
PHYZIX HAS SAID A POWERFUL STATEMENT
Good conversation, Fredo wandituma💥📷
This is beautiful, I like the way it has been given
Honestly Fred has a big vision in Malawi wishing you a big best, keep it up
let's all take part in whatever is happening in our country that can develop our country and don't waste time and point fingers at
the Government us as Malawians have the ability to develop or put Malawi on the map let's try to find a way to solve our daily problems together we can.
Very good initiave
Your flowers 🎉🎉 Fredo
It's my wish kuti utapanga this program in every district kuti enafenso tithe kuika nzeru zanthu I really wish that Fredokiss
Congratulations pidokis i love this conversation ❤❤
Good move will be waiting for you in mzuzu bwana fredo❤
One time fizoo🎉🎉🎉
I like this program.... come to Lilongwe Fredo
This is an important activity, yomwe tikufunika kupanga view as Malawian ,,
waiting for it in lilongwe
Ambuye ana anu nde ali ndi ukali ndizochitika ku dziko la malawi kuno eeh🙌🏿
Step by step we get they united.big up🔥🔥🔥🔥
Great conversation
Bwana Fredo ulemu wanu. You're a great influence. Tchwe mwana thchwe Jr.
This is great development.
Interesting.. .keep it up
A step in the right direction. 🔥
What a way to go......
Thank you. Win or loose these discussions are important. Power to the people. ✊🏾
Ntchana fredo umayesesa big up you really love your country ntchana
This discussion is very important as Malawian let's change our mindset Malawian
Change is here
Powerful 🔥
One time my man 💪
Good conversation from fred
This is a good initiative. Nthaw inachepa koma kkkk
Fredo my Vote 🔥
I stand with Ellen the hand over of government from one party to another has been ignored each every party one to implement there own programs throughout the old one how can we go ahead with this spirit
Bravo Sir Fredokis!
Malawi yimafunika asogoleri ngat Fredo umakwana
The conversation that matters
This should continue so that Malawians maso anthu atsegule.Tidziwona komwe tikupita
🔥🔥🔥🔥🔥🔥
And l have questions what can I do to join this program cz am interested with it
Good development❤
Ndagwilizana ndi fundo yakuti ndarama zimene zikuperekedwa zantukura pakhom ziziperekedwa kamba kakuwapasa athu tcito yakukoza misewu ndizinazotero cz zovuta ndizambili kom ngati mukuwapasa athu ndaram zaurero who is going to fixed our problem please let's think about it
Ntchana 🔥
💥💥💥
Tchana🔥🔥🔥🔥
Achina Mwayuta , power
I believe Fredoh will think about Mangochi, Dzatiyendelen nafe tidzamasuke
Kunali boiz yachamba 🎉🎉🎉
Adha a jonzie aja osawatola 🔥
When next will I join you
Vuto ndi Andale basi katangale wanyanya, Malawi alingati nyumba yopanda fandeshoni remember muluzi anagulitsa makapane aboma.omwe amathandiza kulimba ntchito anthu ambiri two madzi kuno amangoziyendala basi Malo mowagwiretsa ntchito zaulimi zimafunika kwambiri koma ndalama akungoba basi.malawi kuti zithu ziyende ndi zithu zitatu basi zaulemi misewo yabwino makhwala zipatala apezeke.
Km a host eeeeee
Phyzo🔥
Mwayiyambayi ndi more....
Mutibweretserenso pajoz pano
Kodi basi zithera Ku Blantyre?? Ma city enawa zifikeso
Kugawana nzeru mwa nzeru
mayi a yellowa anakonzekatu
hahahahaha koma wandiwaza ndi mdala wamtukula pakhomo,masamu ake anaphunzila kuti?hahahahaha koma conversation inali nyatwa
That's my country kuwenge ku tk tok thena Pali ma comments especially ma video yakuvula
Izizi zinandiphonya ..the first question was "what was wrong with this country kuti zinthu zisamayende bwino?" The answer is simple ...our economy is not stable ,why, the who panel of the cabinet and the president himself don't know nothing about economy azutsogoleri anthu alibe upangiri odziwa kayendetsedwe ka chuma Malawi muno akukanika kuika ndondomeko zoti kodi dzikoli katundu akhale stable asamangikwera every month titani nanga kuti anthu zakudya zipezeke titani
Clement Kachisi 54:14
Campeni
Kungopepherela kuti zipitilile ndizithu zabwino kwambili
Initiative yabwino kwambiri Taphunzilapo zambiri
vuto lalikulu ku Malawi kuno ndi problem......
Kulilongwe mubwela liti??
😂😂chibwe pipo
Fredokiss umakwana
Following comments😂
Time out tonse liar's🤣🤣🤣🤣 2025 mulila kt mfooooooooowooo!!!
Malawi ananukha uyu
Ngini yabho
kodi health bwanji palibe amakamba zachipatala
zoonadi inenso ndinalipira mkw500000 koma passport ya ma page 35 komanso kuidikila zaka ziwiri
Same things being talked over and over again.
Ntchana 🔥