Mary Chilima ndi mkazi wa masiye musiyeni allele ana ake, kodi mulibe chisoni??? Mukufuna kuti Mary awasiye ana ake pa dzuwa?? Mary usapange ndale ino ndi nthawi yolira mwamuna wako komaso kulera ako osati kupanga ndale chonde chonde Mary usayambe Ndale
Anthuwa akubelatu chifukwa akuziwa Kuti kusogoloku chawo kulibe akapanda kuba pano kumagula manyumba kunja kumanga ma Hotel ndima lodge ku malawi asiyeni basi,nawo a UTM alole mary chilima akhale president wa chipani osati manga kaya kwinako mumati chani
Malawians let’s wake up!!! This is straight forward issue President is supposed to do something on the matter basic on report but he is quite busy traveling, thats why we are suspect him to be involved on the issue.
The DC, business as usual imeneyi ikukhudza ambiri, ogwira ntchito ma department a Boma, ma Ambulance ambiri sakuyenda nkhani yake negligence ma bwana. Otsutsa Boma nawo Tulo , negligence, kudikira 2025 anthu azawavotere ..moti agwilizane alipane Boma la MCP to resign and form an interim government and change constitution. Azipani zotsutsa nao ndi okulilana mitima koma asazinamize kuti without coalition angatenge Boma pa okha.
Gentlemen, let’s think like the new generation. What makes Mary Chilima a good leader? You can’t put Mary at the forefront of this battle. Politics is serious business; don’t joke about it. Why are you choosing her over all the men available? You’re confusing the followers. We don’t understand what you’re aiming for. Are you being bribed? Are you suggesting that Mary is more courageous and brave than Kabambe, Kasambala, or Mtumbuka? Be realistic, guys. Corruption is everywhere. You must be corrupt to campaign for her. Do you want to harm her the same way you harmed her husband? What do you mean by saying Mary Chilima can turn things around? Please elaborate.
The DC , go and meet her in person, the country needs her and she is the only person who can truthfully investigate what happened on 10 June 2024 to his husband and 8 others. Please Mary , take the mantle . It will be a compensation from God for the loss.
The DC, I'm your fan. Mumatiimilira ndipo umanena zoona zokhazokha. Keep the fire burning.
Tiyeni....Amalawi tigwilane maja ....tigwese Bomali tipage Chimozi.... Amalawi plz... Mcp yakwanatu
Mr. Bon kalindo mumalankhula bwino kwambiri Marry is a good leader
bodza Mary ndiwe mwana
Mary Chilima ndi mkazi wa masiye musiyeni allele ana ake, kodi mulibe chisoni??? Mukufuna kuti Mary awasiye ana ake pa dzuwa?? Mary usapange ndale ino ndi nthawi yolira mwamuna wako komaso kulera ako osati kupanga ndale chonde chonde Mary usayambe Ndale
Kuti MCP ichoke pakufunika opposition yonse ipange alliance bas
AMALAWI IFE KUGONA KWAMBIRI CHILUNGAMO NDICHOTI AMALAWI SITIMAKONDANA NDIFE AMANTHA
Nkhani iyi akalindo ife abthu wamba sitingamufikile presidentiyo anthu ofunika kutero ndi ma mp kumufunsa presidentiyo mu parliamentimo ngati julongosora kwake ndi kumeneko angomuwuza kuti turapasi udindo immediately
Anthuwa akubelatu chifukwa akuziwa Kuti kusogoloku chawo kulibe akapanda kuba pano kumagula manyumba kunja kumanga ma Hotel ndima lodge ku malawi asiyeni basi,nawo a UTM alole mary chilima akhale president wa chipani osati manga kaya kwinako mumati chani
❤inde we need our mum Mary to be strong and agree to take UTM please we beg you mama Inthe name of Jesus
Malawians let’s wake up!!! This is straight forward issue President is supposed to do something on the matter basic on report but he is quite busy traveling, thats why we are suspect him to be involved on the issue.
More 🔥 the DC Booooooni Kalindo!! Mary Chilima ndi number one kuichotsa mcp ng'ona party no more in Malawi 2025.
Mu nyengo yong'alura
Dr chikangawa
Vuto amalawife tinapusa chifukwa amakhala ngati Maiko ena Maliro Achilima sanakaikidwa kufikira atafufu kuti chinachitika ndi chani Apo AI osaika Maliro mpaka Chakwera ature pansi udindo ndithu izi zinakatheka
Born kalindo the DC mwan oopsa kwambiri ng'alulani paliponse the DC 🔥🔥🔥🔥🔥
You're the one voice of the justice speech 🔥🔥🔥🔥 the DC Boooon Kalindo never give up
Mr DC our president ❤❤❤❤❤❤
Wapenga kaleeee
Pa Mary ndiye ayi
Zoona.. Mpaka. Mary!!! Amalawi. Musamangolankhulapo. Kumawonanso. Kutsogolo.... Olo. Uja. Akumuti. Mtumbuka. Uja. Mmmm. Ndi. Zero!!!
Kom thawi ya Peter kunali mademo ayooooo paka kuchoka kom apa kuliziiiiii
Dangerous Child a.k.a DC Boooooon Kalindooooooooooo🔥🔥🔥🔥🔥🔥💪
Bon kalindo ndi wa malawi keep up my president we love you
Mulimbitseni mtima Mary Chilima The DC tikuonamo kuthekera.
Maliro aja ndi akulu kudziko laMalawi, sizingakhale zoona kuti mkazi Chilima pompanopompano apitirire kupanga zandale, timakuvetsani bwana DC and mumatiimira koma zankazi Chilima musiyeni kaye abaphwa misozi😢
The Diiiiiii ciiiiii
Am going back to Malawi if Mary agreed to stand as a president of utm you have my vote
bofza
The Dc Bon kalindo good message
Our own DC
The DC💪
The DC, business as usual imeneyi ikukhudza ambiri, ogwira ntchito ma department a Boma, ma Ambulance ambiri sakuyenda nkhani yake negligence ma bwana. Otsutsa Boma nawo Tulo , negligence, kudikira 2025 anthu azawavotere ..moti agwilizane alipane Boma la MCP to resign and form an interim government and change constitution. Azipani zotsutsa nao ndi okulilana mitima koma asazinamize kuti without coalition angatenge Boma pa okha.
😂😂😂 Kodi Mesa akuti ndegeyi inanyamulmra maliro akasamphara Ulendo ku mzuzu nthawi imene imanyamura maliroyi zinthu Zimenezo munalibemo kapena zinachoka nthawi imene ikamanyamura vp
The DC ❤❤❤❤❤
This president must step down😢
Mary my vote
The DC president waife amphawi
More respect big man!!
Malawi yaonongeka umphawi watipweteka tasiya kufwila ntchito timangolandila ziphuphu ngakhale azibutsa alowerera kusiya chilungamo bola alandila ndalama tikuyendera ndalama osati malamulo adziko
Asirikali ndi apolice akumalawi ndi mbuzi za anthu...they only protect few thieves
The DC HEAD OF SPEECH
Chitini zopanda madzi ndiye kalindo kod nthawi batile linatha nthawi yanji ndiye lelo mkunyoza chakwela osaphatikiza wosewo bwa galu ndipo ndipo ndiwe kambwee chikalindo kuchikamwa ngati wadya nyasi
Iweso chikamwa chakocho ngt dzenje la chimbuzi chokumba , mwana wa pedegu
Chikangawa son, ngt mukudya nawo ndalama zamagazizo thawi ikubwela Mulungu aku kwapulani limodzi. Kumaoneka ngt mashasha mukama commenta zoduka mutu muziona Malawi Mulungu amaikonda satisiya tokha
Nice mbwiyanga
zosaveka anthu awa ndiwakumpha ndipo marawi sazatheka ndipo mukunena zowona from DC
Mary for life
Ngati malawi first , tiuzeni tsiku lama demostration , tisangokhala chete,
Sizingatheke kuti wina aliyense angozipangila payekha payekha
team the dc❤
Ayi. Mary chilima. Ndiye. Ayi. Aaaa. Amalawi. Mwatani. Kodi. Mumangotchulapo. Olo. Mtumbuka. Uja. Aaaa. Zero
More fire Bon Kalindo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️❤️
❤ bwana Born kalindo
DC 🔥🔥 amakwana
Lero ndiye ndakumva bwino wanena zinthu zogwira ntima
Mawu ❤❤
Chinga khale chi alliance cha mphavu bwanji ❤️🔥❤️🔥
Awo asaphatikizane ndi DpP adzaona mbwadza
Mfundo ya Marry Chilima ndi #1 kma andale kukonda mipanda sizingatheke
A born kalindo timakunyadilan nthawiwi zonse
Merry akukwanila
Gentlemen, let’s think like the new generation. What makes Mary Chilima a good leader? You can’t put Mary at the forefront of this battle. Politics is serious business; don’t joke about it. Why are you choosing her over all the men available? You’re confusing the followers. We don’t understand what you’re aiming for. Are you being bribed? Are you suggesting that Mary is more courageous and brave than Kabambe, Kasambala, or Mtumbuka? Be realistic, guys. Corruption is everywhere. You must be corrupt to campaign for her. Do you want to harm her the same way you harmed her husband? What do you mean by saying Mary Chilima can turn things around? Please elaborate.
I caught the words Kaya ndikuso nkhondo
MR DC kulankhula ndiye mwalankhala koma anthuwa Samantha ali ngati mbuzi
❤❤❤
We need our mum Mary Chilima
Amalawi olimba mtima tilipo koma bvuto mabwana ngati achina non kalindo mumatsowa kuti tilumikidzane,timangobuula basi
Joker nd mery kod chikuvuta ndichan? Dpp Udf afrod utm nd ambewe please
THE DC ❤❤❤❤❤❤
Joker ndi Mary kumene❤️
how special is Mary kuti DPP, UDF, pp,asiye zawo ndiye azikapanga za Mary ways bwanj iyeyo kalindo mmatimirira kima apa pokha simunayankhula za nzeru
Pitilizani kutiyimilira....the DC🔥🔥🔥🔥🔥🔥
More 🔥
Big man
The DC , go and meet her in person, the country needs her and she is the only person who can truthfully investigate what happened on 10 June 2024 to his husband and 8 others. Please Mary , take the mantle . It will be a compensation from God for the loss.
akulu aku army ingonenani madeal omwe munauzidwa kuchita chifukwa zikukhalirani awa ngochenjera milandu ikhara mmanja mwamu
Musiyeni Mary chonde asapangeso zandale
100% love it.
I support you bwanawe someone must resign sure panafunika mademo anyooo
Minister of homeland security ndi mbuzi yamunthu...i wonder whats gonna happen to this thieves when their time is up
Morning
Mr boon kalindo the DC president wathu izi mukuyakhula mosabitsa Apatu amalawi mademo pamafunika ndithu
Live
Facts
Mary kungoimira atha kuwinilatu or osapanga alliance nd aliyense
Ndizooona chipani kuti chiyende ndindalama Sono Mai wo ndi jokadi mbali zonse komaso asakaike chitha kuwina kuzela pangwilizanowu
Rodriguez Elizabeth Davis Anthony Taylor Lisa
Kuswa kuswa
The DC umakwana
The DC 🎉🎉mary emweyooo ifee monga amaiii tili pambuyo pake
Nkhani ndi ya Mademo
Tinamufunakarekare ameneuja
The DC
Awa ndi akatundu ndimakunyadilani
Mary my vote 🎉🎉🎉
Kung'alura kung'alura the DC
yes nkhani ndiyomweyo ya mary basi nkhani ndiyomweyo akufuna kubisa nkhani zambiri zukani mayi chirima anthu akufuna inu osaopa osafooka osatopa ambuye ati tsogorera
Koma combination imeneyo ikhala yovutatu osati masewera
Matha malawi
Kd ngati munalibe zipangizo zolumikizana kuma airport nanga atanyamula maliro a kasambala amalumikizana bwanji? 15:03
Uthenga wamphamvu kwambiri ndizoona mai chilima alsongolere chipani
Osaopa panga comment bas the Dc
Kkkkkkkkkkk koma Dccccc umakwana
Mukufuna kumuphanso mariya
Komaso akazi achakwera anati olo aluze iwo adalemera kare adaya khulapo izi akucheza ndiadzawo zinayenda pashosho npopa tinanva
Ask them mr Dc
Zoonadi
Asiyeni anawo ayendepaokha UTM,AFORD ,UDF. ndiPDP
Bon Kalindo, you are the man. How can I meet you?