Розмір відео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показувати елементи керування програвачем
Автоматичне відтворення
Автоповтор
Atupele umaona patali brother vuto amalawi kusanva mmmm lelo ndizi chigoba chamadeya 4500 kkkkkk
Muthalika ndimachini big up bakili muluzi tv📺
The only our last hope of Malawi
Powerful speech, the only hope for malawians
Prophet speech..Apm my vote
Kusamva A Malawi Lero chakwera wagwetsa bus wánthu a vulala
Kma Atupele ni munthu amalosera kma vuto ni anthufe timati azapanga zimene anapanga abambo ake kma sizili choncho onani peter mene anayendetsera dziko kuposa bingu zinthu zimasintha
Koma ndiye ankanena zowonaditu amalawi tinalakwitsa kumpatsa lenala
APM my vote ❤❤❤❤❤❤❤
Naa Chakwera nde bola Atupele
Even Mutharika Atupele ali ndi experience to think fast
@@MahometAli-e8w Zoonad kwambiri ndithu brother
@@MahometAli-e8w Zoonad kwambiri eishiiii Chakwera mfitiyi mm
That's fact
Prophetic
Aliyese awona tiwonaso 2025inshall allah tupere ulamulire
Zooona😊
Uku ndiye kuyankhula kogwila mtima, kuyankhula kwachikoka kwa usogoleli sizina.mmmmm koma kugula mafumu ma venda.heeee waiona yekhweeee
Big up brother man!!
Nkhalamba ndi nkhalamba basi singasinthe kukhala mnyamata, ndi chimodzimodzi ndi MCP
Koma nawo angoyankhula.. politicians are just the same
Adali ndi fundo ndi bambo awo awazonena alibeso athawira ku dpp
Kkkķkkk zoyonadi ❤❤
Amanena zoona ndithu
Dzimachende dzanu achawa, chomwe mmadzi ndikuchapa kumatako
Ndkuonamo tsogolo mwaiwe atupele,ndpo chikhulupililo chathu amalaw chomaliza taika mwaiwe.ndie usazatikhumudwitse mfundo zako zogwila mtma zed
Uyuyu koma samandiwaza wakhala chete malawi ikuvutika nde lero ukutulukano.. atupere ekha nde ai
Mudakali mukulira mpaka 2035 woo chakwera akulamulira zanu izo zi fit inu
Cholinga ukufuna pitala ankadzawina uzabwerepo ndimwe ndi yellow yako
Tsono yemwe sanali lenala ndiye anamuchotseranji anthu?😅😅😅😅
Umbuli wa anthuwo dyera ndi nkhwidzi... Lero siizi Chakwera angowowozedwa ngati chitsiru
MCP inaberekedwa ndi Akhothi..
Tipaseni update ya South Africa ICJ ndi Israel
😮L
mcp singasinthe or zitavuta maka nkhanza zoyamwira APM ndikaswiri pa utsogoleri
How to be an experienced person, m'mesa umayamba ndi ulenalawo,iwe atupele,Malawi is not ur father's Farm,of course ur was the president of Malawi, ndiye iwe ukufunaso upresident, Malawians have opened their maso ndi makutu,Malawi isn't ur farm
mcp ndi chipani choipa
Anatiwonongela ufumu wanthu WA Kwa chikulamayembe
🎉🎉🎉🎉
🎉
😂😂😂😂 eee zamuvutati
Muluzi anapatsa Bingu lenala
Apm boma
Zandale izi anthu awa sungawakhulupirire
Ndipo zowonadi
Mbambande bwana
Cadet Yako ija uchira
Utachile ndiweyo mbuzi yako ingowowozedwa ikamayenda😂😂😂
Zoonad
Best TV🔥🎮
Za manyi
Atupele umaona patali brother vuto amalawi kusanva mmmm lelo ndizi chigoba chamadeya 4500 kkkkkk
Muthalika ndimachini big up bakili muluzi tv📺
The only our last hope of Malawi
Powerful speech, the only hope for malawians
Prophet speech..
Apm my vote
Kusamva A Malawi Lero chakwera wagwetsa bus wánthu a vulala
Kma Atupele ni munthu amalosera kma vuto ni anthufe timati azapanga zimene anapanga abambo ake kma sizili choncho onani peter mene anayendetsera dziko kuposa bingu zinthu zimasintha
Koma ndiye ankanena zowonaditu amalawi tinalakwitsa kumpatsa lenala
APM my vote ❤❤❤❤❤❤❤
Naa Chakwera nde bola Atupele
Even Mutharika Atupele ali ndi experience to think fast
@@MahometAli-e8w Zoonad kwambiri ndithu brother
@@MahometAli-e8w Zoonad kwambiri eishiiii Chakwera mfitiyi mm
That's fact
Prophetic
Aliyese awona tiwonaso 2025inshall allah tupere ulamulire
Zooona😊
Uku ndiye kuyankhula kogwila mtima, kuyankhula kwachikoka kwa usogoleli sizina.mmmmm koma kugula mafumu ma venda.heeee waiona yekhweeee
Big up brother man!!
Nkhalamba ndi nkhalamba basi singasinthe kukhala mnyamata, ndi chimodzimodzi ndi MCP
Koma nawo angoyankhula.. politicians are just the same
Adali ndi fundo ndi bambo awo awazonena alibeso athawira ku dpp
Kkkķkkk zoyonadi ❤❤
Amanena zoona ndithu
Dzimachende dzanu achawa, chomwe mmadzi ndikuchapa kumatako
Ndkuonamo tsogolo mwaiwe atupele,ndpo chikhulupililo chathu amalaw chomaliza taika mwaiwe.ndie usazatikhumudwitse mfundo zako zogwila mtma zed
Uyuyu koma samandiwaza wakhala chete malawi ikuvutika nde lero ukutulukano.. atupere ekha nde ai
Mudakali mukulira mpaka 2035 woo chakwera akulamulira zanu izo zi fit inu
Cholinga ukufuna pitala ankadzawina uzabwerepo ndimwe ndi yellow yako
Tsono yemwe sanali lenala ndiye anamuchotseranji anthu?😅😅😅😅
Umbuli wa anthuwo dyera ndi nkhwidzi... Lero siizi Chakwera angowowozedwa ngati chitsiru
MCP inaberekedwa ndi Akhothi..
Tipaseni update ya South Africa ICJ ndi Israel
😮L
mcp singasinthe or zitavuta maka nkhanza zoyamwira APM ndikaswiri pa utsogoleri
How to be an experienced person, m'mesa umayamba ndi ulenalawo,iwe atupele,Malawi is not ur father's Farm,of course ur was the president of Malawi, ndiye iwe ukufunaso upresident, Malawians have opened their maso ndi makutu,Malawi isn't ur farm
mcp ndi chipani choipa
Anatiwonongela ufumu wanthu WA Kwa chikulamayembe
🎉🎉🎉🎉
🎉
😂😂😂😂 eee zamuvutati
Muluzi anapatsa Bingu lenala
Apm boma
Zandale izi anthu awa sungawakhulupirire
Ndipo zowonadi
Mbambande bwana
Cadet Yako ija uchira
Utachile ndiweyo mbuzi yako ingowowozedwa ikamayenda😂😂😂
Zoonad
Best TV🔥🎮
Za manyi
Nkhalamba ndi nkhalamba basi singasinthe kukhala mnyamata, ndi chimodzimodzi ndi MCP