CHACHITIKA NDI CHANI NDI BAKILI MULUZI TV PA FACEBOOK NKHANI YONSE ZAKHALA BWANJI KODI

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 4 лют 2025

КОМЕНТАРІ • 219

  • @ImranWyson-e9o
    @ImranWyson-e9o 3 дні тому +15

    Akung'alula ndithu😂😂😂 Best TV ever

  • @MandalaChaona
    @MandalaChaona 2 години тому

    🤣🤣🤣🤣🤣 Koma Ziliko liko komabe Utsogoleri usinthidwa.
    Anyway I love BAKILI MULUZI TV, History is the best teacher ✍️✍️

  • @DantonKaipa-v8i
    @DantonKaipa-v8i 2 дні тому +4

    Kutheka ndi yemweyu, pajatu chilungamo chimasakanikilana ndi mwana.l always proud with bmtv he is real the best teacher, now and forever.

  • @YusufAjida-t8r
    @YusufAjida-t8r 3 дні тому +9

    Zachamba izi akufuna kuononga Zina la bakili muluzi TV koma akunama kwambili Ana achepa timamukonda ❤❤❤❤ kwambili bakili muluzi TV

    • @PromiseSaidi
      @PromiseSaidi 6 годин тому

      Mn akupanga post ekha bakili muluzi tv km chifukwa chachikulu ndichoti bakili muluzi tv amakonda DPP ndie dalitso kabambe wakana kupanga alliance ndi chipani cha DPP

    • @msatisi.reangfordphiri
      @msatisi.reangfordphiri 4 години тому

      ​@@PromiseSaidinde moti a Kabambewo akuti ali nayo 50+1 yotchaira Chimwendo?

    • @LeonardEnock-e1t
      @LeonardEnock-e1t 4 години тому

      Bakili muluzi tv anayamba nkale kumung'alura chilima anangosiya apa atamwaliramu koma ndiyemweyu ndinthu BMT 😅😂

    • @SulaimanIssa-b2h
      @SulaimanIssa-b2h 3 години тому

      Ea ndima haka amene aja ineso ndavera nawo muli zofooka zambili zimene zikusonyeza kut siwa bakili muluz tv

  • @yusufu-g6e
    @yusufu-g6e 3 дні тому +11

    iyi Nd bakli muluz TV yaa mcp

  • @HOMEAWAY-h7t
    @HOMEAWAY-h7t 3 дні тому +2

    The ever best tv in mw we still love the people who are manengng this ❤❤❤

  • @LinlyMathewe
    @LinlyMathewe 7 годин тому +2

    Kaya ndi yemweyu Kaya zopeka but never give up UTM my vote ❤❤❤

    • @SulaimanIssa-b2h
      @SulaimanIssa-b2h 3 години тому

      Ayi sibakili muluz TV ndi mahaka amene aja. Muivele bhobho ndi fake voice. Page imene ija yapangidwa haki ndi athu a boma ndiofina kuononga chipani cha utm. Ndiye choyamba akuyenera kuipisa mbili ya chilima. N mu audio imene ija muli zofooka zambili zimene zikupeleka chikhulupililo kut siwa bakili muluz TV

  • @denndavie6041
    @denndavie6041 3 дні тому +12

    Ndipo ineyo chilima sindingamu bakile. He was indeed a bad guy with Lucius Banda.

  • @ThokoMsonkho-hy4uc
    @ThokoMsonkho-hy4uc 3 дні тому +5

    Pamene page yomweyo ikawulutsa nkhani ya maliro a Chilima mumati ndiyabwino chifukwa akangofuna kukuthandizani kuti a UTM mumuziwe CHAKWERA pazomwe amapanga Chilima kufikira imfa yake.
    Koma kunena chilungamo inenso ndinamuona kuti Chilima uja anali wamwano ndiponso anali chitsilu pa ndale. Kuzichotsa yekha kwa PETER kenako kudzalumikizana ndi Chakwera pamene paja anapusa pa ndale potengera mbiri ya MCP mbuyomu. Munthu amapanga mistake koma pokhapa ndimamukonda kuti ndiwadyera komanso ndiwamwano ndinso alibe nzeru zautsogoleri.
    Mmene amamulankhulira BAKILI MULUZI purezideti wapuma uja ndinamuwona kuti tsogolo panalibepo mwa iye. Anali wa mwano kwa akuluakulu amayenera kumwalira basi

  • @Ayanali-cr4vy
    @Ayanali-cr4vy 2 дні тому +2

    UTM sichipani chomasapota
    Atupele Muluzi my Vote

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 дні тому +4

    Kunena zoona, Bakili Muluzi tv alibe mbali, amayamikila pamene pali bwino, komanso amadzudzula polakwikapo.

  • @petertengani
    @petertengani 8 годин тому

    Zatembenuka, ng'ombe zayang'ana ku joko.
    Yomweyo...
    😆😆🤦🏽‍♂️❤️.

  • @AlfredGanizani-v9f
    @AlfredGanizani-v9f 5 годин тому

    😅😅 tingodikira kut give zambili my vote to my chakwera is number one

  • @WilsonNedi-s6t
    @WilsonNedi-s6t 3 дні тому +4

    Siwa bakili muluzi ameneyo anthunu musakhulupilire

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 3 дні тому +7

    Amene waja ndichi machine 😂🎉

  • @wisdomlimbe9483
    @wisdomlimbe9483 3 дні тому +2

    Olo zitakhala zoona, who cares about DK's private life? All I know he can run the economy way better than the current situation. Malawi is not looking for munthu yemwe sananyengepo. Tikufuna munthu woti atsogolere kukonza chumachi kuti wolimbikira azidya thukuta lake. Enafe we don't care kaya akhala Chakwera yemweyi, kaya Enock Chihana, kaya APM, kaya Atupele kaya DK, kaya wa Bakili Muluzi

  • @GeoffreyMarko-v3s
    @GeoffreyMarko-v3s 3 дні тому +4

    Chilima anasocheresa dzikoli😢😢😢😢😢

  • @HenryNanthuwa
    @HenryNanthuwa 3 дні тому +2

    Nosense get lost bakili muluz zoputsatu izi

  • @NenaniMoyenda
    @NenaniMoyenda 3 дні тому +1

    Ma pulopaganda a MCP awa ndipo BMT akangotukila musambulidwa🤣

  • @harrisbanda5891
    @harrisbanda5891 3 дні тому +3

    Akubweletsa nkhanizi siwa bakili muluzi tv, ndiena mwa afisi achikangawa kufuna kuipisa ndikuononga mbili ya utm , komabe tinene mosapsyatila pano , chilima ndamene anationongesela malawi wathuyu , after all anangoti duuuuu ngati akumetedwa osafuna kususa nkhanza zomwe zilimdziko , nayenso chikangawa kukapha mzake pambuyo poti amabela limodzi y?, y dd u do dat chikangawa?

  • @MorrisDzonzi
    @MorrisDzonzi 4 години тому

    Zazii kumudetserela Kabambe akumuopa awa,,Zonse nchabe koma Chakwera walephera achoke basi

  • @EmmanuelkpPraise
    @EmmanuelkpPraise 3 дні тому +6

    Aaa zazii uyu si wabakili muluxu tv

    • @SulaimanIssa-b2h
      @SulaimanIssa-b2h 3 години тому

      Ea ndima haka amene aja. Akayambileso. A mcp amaonatu ngat amalawi ngogona kwabasi kkkk

  • @WilliamNhlane-fd9hi
    @WilliamNhlane-fd9hi 3 дні тому +2

    I don't think this is bakili muluzi , awa ndi mcp akufuna tisalankhule imfa yachilima .

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 дні тому +2

    This is the best station

  • @RinosChilumpha-y2d
    @RinosChilumpha-y2d 3 години тому

    Zimachitika koma bakili muluzi TV sayimila mbali ai palipose amang'alula bass

  • @TaniaMphalumo
    @TaniaMphalumo 2 дні тому +1

    Ayi.izi akupanga ndi mayiko usi ngati simukuziwatu ndi manganya akupanga zosezi😊

  • @AlexanderTraffick
    @AlexanderTraffick 3 дні тому +1

    Nkhani izi zokomera Kwa Anthu atambara wakuda.mcp

  • @ChrispineMuzungu-l8h
    @ChrispineMuzungu-l8h 2 дні тому

    History is the best teacher 🎉🎉

  • @harrymicah6140
    @harrymicah6140 3 дні тому +2

    😂😂😂😂 uyu nde ndakayika kut ndi Bakaili muludzi ukadusa wez history is the best teacher aa tabwali uyu

  • @SkevaMustapher
    @SkevaMustapher 3 дні тому +3

    Amene uja si bakili muluz tv tikumudziwa ife ayi akusiyanilatu kwambili

  • @MuhammadAlie-b7v
    @MuhammadAlie-b7v 4 години тому

    Uyu si bakili muluzi tv

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi 6 годин тому

    Who said ahhhh Like me here when listening

  • @PreciousBenes
    @PreciousBenes 2 дні тому

    Dk my vote

  • @GoodluckVithumbiko
    @GoodluckVithumbiko 3 дні тому +2

    Anthu woputsa inu asatana kupusa anachikangawa kufuna kutiwonongera utm yathu makape inu kupusa ndawononga bandle yanga panyo pani

  • @ShoryenNgumuya
    @ShoryenNgumuya 3 дні тому +5

    Km yaaa ziliko kumalawi

  • @abdulsalammkwepu3321
    @abdulsalammkwepu3321 3 дні тому +1

    History is the best teacher

  • @SaimonBanda-ez6km
    @SaimonBanda-ez6km 14 годин тому

    Komano saknama bakili tvi 🎉❤

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 дні тому +1

    Uyuyu ndi munthu ong'alura basi
    Sayendela kuti uyu ndi ndani

  • @marryphili5419
    @marryphili5419 3 дні тому +1

    Ndiwe galu kwabasi sindiwe bakili muluzi TV mungofuna kungowononga mbiri zazipani zisiru inu

  • @LeyvanSamuel-pe5tc
    @LeyvanSamuel-pe5tc 3 дні тому +1

    I like to listening BMTV 🔥

  • @bridgetmajor3646
    @bridgetmajor3646 3 дні тому +1

    Uyu siwa Bakili tv...zaboza izii mwayitani.....Bm tv za chamba basi

  • @AngolaChinga
    @AngolaChinga 3 дні тому +2

    😂😂😂😂😂😂😂 wakhaula uyu si wabakili muludzi tv

    • @SulaimanIssa-b2h
      @SulaimanIssa-b2h 3 години тому

      Kkķkkkk nane ndaivela so muli zofooka zambili

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg 3 дні тому +1

    Agalu a MCP awa

  • @HamdanMaleta
    @HamdanMaleta 3 дні тому +2

    Chilima anali opoila kwambiri

  • @ElizabethMulinde
    @ElizabethMulinde 3 дні тому +3

    Uyu sibakili muluzi tv

  • @lastonmasoatenganji-bs5gf
    @lastonmasoatenganji-bs5gf 3 дні тому +2

    Si wa Bakili Muluzi uyu mpang'ono pomwe. Olo mdani atakuchimwira chotani ndipo kwa nthawinso yoyamba, ungayankhulirenji zonsezi ngati kulibe mawa?

  • @LaynaAdam
    @LaynaAdam 3 дні тому +3

    Mmmmmmmmm siwa bakili tv ameneyo ndi munthu wina

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 дні тому +1

    Akabambe akuchepa kwambiri kuyelekedza ndi Bakili Muluzi tv

  • @uzaleuzale8603
    @uzaleuzale8603 3 дні тому +2

    Chimashini chija chayamba kugwira ntchito mukatero😂

  • @StephanoMussa-q6d
    @StephanoMussa-q6d 3 дні тому +2

    Bakili muluzi guys wagudwa Inu simukudabwa ma videos ake for the past two weeks mmene akumvekela? Guys wake up everybody has price

  • @SydneyMwale-u9w
    @SydneyMwale-u9w 3 дні тому +3

    Fake news

  • @Hdsagdf-t1n
    @Hdsagdf-t1n 3 дні тому +2

    Munamiza ana kodi kkkk mwanya

  • @GabrielMuziDlamini
    @GabrielMuziDlamini 3 дні тому +2

    Komabe sikudwisa big kuti ngati sanamuhaki😢

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u 2 дні тому +1

    Let's gathering here
    Iyiyi ndiye yeni yeni TV

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 дні тому +2

    Chilima anawononganawo dziko la Malawi, kupupuluma Chilima, that's why anamupha.

  • @AbelShaba
    @AbelShaba День тому

    Mmmm kwesi koma B TV wadya chibanzi

  • @HarryMsudzula
    @HarryMsudzula 3 дні тому +2

    Bakili Muluzi tv is not God cancel him in your mind be careful ndiye sitikavota if it is that

  • @ShukuraniTonex
    @ShukuraniTonex 3 дні тому +2

    😂😂😂😂😂😂😂😂

  • @KnowxySainet
    @KnowxySainet 8 годин тому

    Uyuu c bakili TV weniweni anthu a mcp awa muone kumapeto kwake akukakamila mau oti history is best teacher nonsese

    • @ishaqyassin5001
      @ishaqyassin5001 7 годин тому

      Ubwino wake Chisale ndi wa kuba Kabambe mbava ya munthu

  • @ChavuksFrancois
    @ChavuksFrancois 3 дні тому +2

    Nkhani zonsezo a Malawi akudzidziwa, kaya chilimayo, kaya Kabambe a Malawi akuwadziwa. Nkhani za personal sizingasinthe chilichonse kwa a Malawi zotsatira UTM

  • @EmilyKanyika
    @EmilyKanyika 3 дні тому +3

    Machimo

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza 3 дні тому +2

    I don't think that this is Bakili Muluzi TV kaya mwina

  • @MosesMbale
    @MosesMbale 3 дні тому +1

    Bakili Muluzi ndi dolo ndamutayila kamtengo

  • @mbelengamavuto2517
    @mbelengamavuto2517 3 дні тому +2

    Zosamveka izi mukuyakhulazi

  • @ConsPempho
    @ConsPempho 8 годин тому

    Ai I hanger😂

  • @GeorgePhiri-ub2of
    @GeorgePhiri-ub2of 2 дні тому

    Mwakhaula Uyutu si mtanyiwa ai oti tsiku ndi tsiku odzingolimbana ndi chakwela ai

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 3 дні тому +4

    Koditu chilima sanali munthu wabwino ayi ngakhale chakwera anamupha

  • @Gwedeza-q3f
    @Gwedeza-q3f 2 дні тому +1

    Ndi bodza ili ndi propaganda ya mcp, uyu siwaBakili muluzi TV 😂😂😂😂😂 ndidzabodza ndi aganyu awa a mcp

  • @AustinAllan-lh5ij
    @AustinAllan-lh5ij 2 дні тому

    Ku Chikangawa uku guys 😅😅😅

  • @SmartMailos
    @SmartMailos 2 дні тому

    Sizona siiye

  • @tasiyanakasalu6228
    @tasiyanakasalu6228 3 дні тому +1

    Ndiyomweyo kungot akangana bax kkk

  • @CharlesKaujole
    @CharlesKaujole 3 дні тому +2

    Dars

  • @MimiKapito
    @MimiKapito 3 дні тому +2

    Zaboza uyu

  • @SolomonNjolomole
    @SolomonNjolomole 3 дні тому +1

    Doud Suleman ndi azizake kuyesera machine agula aja apa game mbola.

  • @AngolaChinga
    @AngolaChinga 3 дні тому +2

    Inu uyu si wabakili muludzi tv kapolo wa mcp uyu

  • @phillipchampoxychapola4165
    @phillipchampoxychapola4165 3 дні тому +1

    Kwamene akuvesesa sanganene kuti page yahakidwa koma vuto anthufe timafuna kuti munthu uja azikamba zambari imodzi

  • @ErickCPatrick
    @ErickCPatrick 2 дні тому

    kabambe,wakuba

  • @natashamathala8715
    @natashamathala8715 2 дні тому

    Yaaaaaah a mcp mwafika patali, koma mukunama naye wa bakiri muluzi simumukwanitsa ayi mwachepa dikilani akuyankhani nzanuyo akubwela ndithu chifukwa uyu si wathu wathu wa bakili muluzi ayi ine ndakana izi.

  • @NoahPhiri-f7m
    @NoahPhiri-f7m 3 дні тому +2

    Sibakili tv ameney ndiwa mcp

  • @MikeLodzi
    @MikeLodzi 3 дні тому +1

    nkhani izizi siza bakili muluzi tv
    anjanjawidi angolowelelapo

  • @ChikondiMusaya-x6n
    @ChikondiMusaya-x6n 3 дні тому

    Sibakili muluz ameneyo

  • @NelesonchibwanaMandera
    @NelesonchibwanaMandera 2 години тому

    Bakili muludzi TV imanena zoona ine ndimankhulupililad amankhala kut waziwona kale sogolo lake

  • @AlexanderTraffick
    @AlexanderTraffick 3 дні тому +1

    Komatu TV imeneyi imakhwefura munthu kkkk achina kamajekete Ali ziiii

  • @EDSONMahamand-v2z
    @EDSONMahamand-v2z 3 дні тому +2

    Aise ulemu wako umalongosola moveka bwino zaveka bwino kwambili

  • @Mustapher-fb4qp
    @Mustapher-fb4qp 3 дні тому +2

    Chirima ineso sindingamuyikire kumbuyo

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h 3 дні тому +2

    Sibakili muluzi TV imeneyo ndi propaganda

  • @PatrickZinenanie
    @PatrickZinenanie 2 дні тому

    Si bakili muluzi ameneyo ndi zigawenga za chikangawa party mcp

  • @EvanceSungani-cv9jk
    @EvanceSungani-cv9jk 3 дні тому

    MCP paja yakunga chiwembu kwa bakili muluzi TV this is plan ,,,,,

  • @DonaldBanda-qi7yw
    @DonaldBanda-qi7yw 3 дні тому +2

    Ndale zaku Malawi ndi zosokoneza anthu

    • @DonaldBanda-qi7yw
      @DonaldBanda-qi7yw 3 дні тому +1

      Ndi kunena zoona Ana amasiku ano sakudziwa kuti Kodi Atsamunda amalamulira bwanji dziko lino. Chimene akudziwa ndi kulemba Nkhani ZOSOKONEZA A MALAWI pa SOCIAL MEDIA basi, komanso kuwapatsa Bomali popanda masankho sangathenso kulamulira dzikoli adzangokhala mavuto okhaokha basi.

  • @BrightLuciano
    @BrightLuciano 2 дні тому

    Zazi SI Bmtv uyu 😢😊

  • @greycianmbewe4573
    @greycianmbewe4573 3 дні тому +1

    Lankhulani koma timuvoterabe

  • @YounusWabullah
    @YounusWabullah 3 дні тому +2

    Ndi propaganda iyi zamkutu bas

  • @AlgentChilanga
    @AlgentChilanga 3 дні тому

    Soi ndiye uyu wa BM Tv😂😂

  • @KondwaniChaponga
    @KondwaniChaponga 3 дні тому +1

    Mkamalimbana ndi BMT mutha ngati makatani

  • @LusunguKalua
    @LusunguKalua 3 дні тому +2

    Mmm ayi sizoona izi

  • @AugrinNgunga
    @AugrinNgunga 3 дні тому +1

    Mayaz sibakili muluz tv uyu aaa timatha zimenezo kulemba pa page yamuthu

  • @johnlameck8366
    @johnlameck8366 3 дні тому +1

    Kkkkk koma bakili muluzi alipo

    • @UzeChongo
      @UzeChongo 3 дні тому

      Alipo tavera kale atulukira lero lino

    • @SulaimanIssa-b2h
      @SulaimanIssa-b2h 3 години тому

      Kulibe panopa. Wapangidwa haki

  • @IdressaMussa
    @IdressaMussa 3 дні тому

    Ameneyo sibakili muluxi TV

  • @MetuseSelai
    @MetuseSelai 3 дні тому +2

    Si wa Bmtv ameneyo

  • @Extratremendouszeus
    @Extratremendouszeus 3 дні тому +1

    But you have to check because there are many bakili muluzi TVs...else you bakili muluzi never does this