Розмір відео: 1280 X 720853 X 480640 X 360
Показувати елементи керування програвачем
Автоматичне відтворення
Автоповтор
Akawina usi tonse tikupita ku dpp ndi afford cz udf idatha mcp ikatipha😢
Akufuna kuba chipani uyu usi i don't trust him
AKupanga zonyanyalitsa anthu osalakwa kuti okhao a mcp azakhale ndi mphamvu yolawila kuzaponya voti 😢
Annabel akudalila Chan Kodi Mesa adachita kusakhidwa zothekanso kumuchosapo kuikapo ena
Musalore ndiye chakwela achokela madem
Ndili ndi maganizo ena oti tizapange lisanafike tsiku loponya voti ,Ndaonazoti pakufuna pachitike zibwana zofuna kutipusisa ngati ndife masaizi awo .Ndiye tidikile kaye
Koma mcp why koma a opposition please musalore zimene kapena kugonjela amcp please musalore 🧎🧎🧎please please guy's amec apasidwa ndalama musalore. Chuma chamalawi sichikuyenda bwino athu kudya kopelewela. No economics mcp wy.
Musadandaule ai ndili momuno ndibulitsa mec yo ine akunama amenewo ,tangotini ziii.
Osaopa osafooka osatopa chilungamo chioneke sitikufuna Smartmatic ayi
Nrb ikulemba amcp okhawokhakodi mantha bwanji anthu inu
Malawi is now hell on earth
Kodi palibe anthu ena Ndiye tisankhe anthu ena ogwira ntchito Chifukwa ndalama zimene akagwile ntchitozo ndi za Malawi
Anamalomba palibe kudekhanso apa nde kulibwino dziko alitenge asilikali tisazakhalenso ndi president ochoka ku ma parties
.mwambo not mambo
Apapa pakufunika ma dhemo iyiyi osatekhe because ambili tilibe ma id
Dpp utm afod bomah
Komatu wonani zomwe zikuchitika ku Mozambique light now
ADAKAIMIKIDWA KAYE .not adainikidwa
Kom uyu akufuna kutula udindo ndimademo kom kusanvaku ndalama kapena chan
Kalemberayu.adakainikidwa kaye.chifukwa andale zonse sakubvomereza .ndipo dzikoli.ndilatonse osati mcp yokha
Kodi mukufuna kuti uza kuti mcp nde ndiyomwe ili ndiphamvu kuposa ife a malawi
Pakufunika ma dhemo apapa because mcp ikutionatu kupusa
Mai anabel bambo wake anali wankhanza nayenso walozera zomwezo
Ndipo ali kugahena
Usi ndiwe garu
Akawina usi tonse tikupita ku dpp ndi afford cz udf idatha mcp ikatipha😢
Akufuna kuba chipani uyu usi i don't trust him
AKupanga zonyanyalitsa anthu osalakwa kuti okhao a mcp azakhale ndi mphamvu yolawila kuzaponya voti 😢
Annabel akudalila Chan Kodi Mesa adachita kusakhidwa zothekanso kumuchosapo kuikapo ena
Musalore ndiye chakwela achokela madem
Ndili ndi maganizo ena oti tizapange lisanafike tsiku loponya voti ,
Ndaonazoti pakufuna pachitike zibwana zofuna kutipusisa ngati ndife masaizi awo .
Ndiye tidikile kaye
Koma mcp why koma a opposition please musalore zimene kapena kugonjela amcp please musalore 🧎🧎🧎please please guy's amec apasidwa ndalama musalore. Chuma chamalawi sichikuyenda bwino athu kudya kopelewela. No economics mcp wy.
Musadandaule ai ndili momuno ndibulitsa mec yo ine akunama amenewo ,tangotini ziii.
Osaopa osafooka osatopa chilungamo chioneke sitikufuna Smartmatic ayi
Nrb ikulemba amcp okhawokhakodi mantha bwanji anthu inu
Malawi is now hell on earth
Kodi palibe anthu ena
Ndiye tisankhe anthu ena ogwira ntchito
Chifukwa ndalama zimene akagwile ntchitozo ndi za Malawi
Anamalomba palibe kudekhanso apa nde kulibwino dziko alitenge asilikali tisazakhalenso ndi president ochoka ku ma parties
.mwambo not mambo
Apapa pakufunika ma dhemo iyiyi osatekhe because ambili tilibe ma id
Dpp utm afod bomah
Komatu wonani zomwe zikuchitika ku Mozambique light now
ADAKAIMIKIDWA KAYE .not adainikidwa
Kom uyu akufuna kutula udindo ndimademo kom kusanvaku ndalama kapena chan
Kalemberayu.adakainikidwa kaye.chifukwa andale zonse sakubvomereza .ndipo dzikoli.ndilatonse osati mcp yokha
Kodi mukufuna kuti uza kuti mcp nde ndiyomwe ili ndiphamvu kuposa ife a malawi
Pakufunika ma dhemo apapa because mcp ikutionatu kupusa
Mai anabel bambo wake anali wankhanza nayenso walozera zomwezo
Ndipo ali kugahena
Usi ndiwe garu