These guys are just blindfolding us . They forget 2025 is around the corner , Malawians panopa anasamba mokweza. Now they telling Malawians as if they are Angels now .They too should confess their past sins and be born again!
Taonani akungotukwana basi a DPP ndiye kutukwana mukutukwamako mwati muzaiona vote mmmmmm ndakayika chifukwa anthu inu ulemu milibe kuyambila magogo Anu aja opanda Manu mukamwa zochitanso chimozizi 😂😂😂 anthu simungalamulile ziko ndinu okanika komanso otembeleledwa MCP 2025 ikuwina whether you like or not
Malawi mayi ako iwe mapwala ako anamvomera ndani mapwala ako ndi kumangochi kwanuko andu osapita ku school akumangochi mwafikapo ndi umbuli wanuwo koma ine kumangochi bwanji kodi ayao awa
Zoona zoti kuli opposition suzimaziwika ali nziiii kuopa kuti angayalusidwenso nawonso ali ndi Magazi mmanja mwawo ndiye nkivuta kudzuzula Malawi anainongeka basi
mkuluyi akunena Zowona koma poti ma supporters a DPP adazolowera kutukwana apa mutukwanaso, MCP ikungokudodani ili pheee, ndiye musadatitu mulimbe kutukwanaku mpaka 2030 woooo.
Garu iwe kape weni weni waiona ndi DPP basi zakokhalira basi pamtumbo pako chsru chidebe chamunthu osamakadya ndalam zo uko bwanji nyani palukundu penipo mpikene mwedyo anambwa
Kulirako kukufunika panopa Chifukwa zisankhozo is around the corner Kodi Achakwera adalowela machine Achakwera sadalowere ma vote Achakwera adalowera ma demo Tingopanga ma demo basi kuti atuluke boma
Atupeletu mdi OPHUNZIRA NDIPONSO NDI OZINDIKIRA. KUNGOTI VUTO NDI ANTHU AMATSOGOLERAWO. A BAKILI ANANENA KALE ZOKHUDZA OTSATIRA CHIPANI CHA UDF NDISACHITE KUBWEREZA PANO ANAZIMVERA OKHA
Chili kwa anzanu chaipa mbuzi iwe. Sudziwa ntchito yoitanira atola nkhan kut ndikufuna uthenga ufike palipose... Am not member of dpp but if I lose my data listening stupit story from MCP members.... Mmmmm I feel bored... Therefore I just say had I know before I couldn't open it
Za Zii Ngati mwatumidwa Malawi's sitikufuna machine wo
Ukunena zoona big DPP alibe nzeru nkhalamba zilibe nzeru 😂😂😂 DPP akuyiopa game yakulila
Ayakhula bwno abambo awa crias koma bvuto akuoposition mangot munthu walandra ndalama Malo mobvetsera bwno bravo Mr
More 🔥🔥🔥🔥🔥Shafie DPP ikudziwiratu Kuti sazawina ndiye pachifukwa cha Ichi akungofuna kupasa anthu mmalawi Muno chiganizo oti masankho abeledwa pamene akudziwa Kuti zawo sizilibwino
Mkulu uyu wandila ndalama ndipo ndi mbuzi yeniyeni ......chisilu cha munthu
Mkulu uyu ndiozindikila kwambiri
These guys are just blindfolding us . They forget 2025 is around the corner , Malawians panopa anasamba mokweza. Now they telling Malawians as if they are Angels now .They too should confess their past sins and be born again!
Mkulu iwe ndi mbuzi Kodi chipani chinali ku press briefing anali a Dpp okha ....mbuzi iyi
Anganga mwayankhula bwino
Comrade nganga shaffi hassan ulemu wako mumatha kuyang'ana mbali zonse
Ngati walandira ndiye kuti wachita bwino kuti aziphunzitse mbutuma kuti zizindikire kuti malamulo amapangidwa bwanji ndipo amapanga ndani? MP? KAPENA ATOLANKHANI?
NGANGA NDAKUTAYIRANI KAMTENGO NDINU MUNTHU OZINDIKIRA NGATI SI ABOMA LIMODZI NDI ACHINA SALLO.AUZE NA AMENE ANALOWA MKALASI AMVA.MBUTUMA ZITSALA
.
Chisulu chadyera ichi
Dyera galu uyu
Macadet akufuna Jane Assah
Taonani akungotukwana basi a DPP ndiye kutukwana mukutukwamako mwati muzaiona vote mmmmmm ndakayika chifukwa anthu inu ulemu milibe kuyambila magogo Anu aja opanda Manu mukamwa zochitanso chimozizi 😂😂😂 anthu simungalamulile ziko ndinu okanika komanso otembeleledwa MCP 2025 ikuwina whether you like or not
DPP afford ndi UTM alira kale 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 bwanji bosangonena Kuti a MCP apitilize Kuti ndalama zisaonongeke
Atupele uja osazamuphwekesa UDF sitilola kukhala munkhwapa mwa MCP or DPP sitikuifuna tipita tokha kumasakho win or lose period ❤❤❤
Wazxiwa het? 😂
Malawi mayi ako iwe mapwala ako anamvomera ndani mapwala ako ndi kumangochi kwanuko andu osapita ku school akumangochi mwafikapo ndi umbuli wanuwo koma ine kumangochi bwanji kodi ayao awa
Zoona zoti kuli opposition suzimaziwika ali nziiii kuopa kuti angayalusidwenso nawonso ali ndi Magazi mmanja mwawo ndiye nkivuta kudzuzula Malawi anainongeka basi
Kulakhula mwazeru nganga
Okay chabwino koma ifeee chakwera sitifuna aiiiiiiiii
Wawo pe olo ryawo soni mmwee ilipyala mkawecheta soni yepyala yenuyo nambo soni Naga tummanye timtoche mmangochi muno
Mau ndithu
Iwe sia DPP okha galu iwe uzinva,,,, 😂😂😂😂
Pansete.... Pako... nganga. ku... mangochi ko..... wamva
Awa a DPP game akuiopa aona kuti palibe chawo 2025
Inunso muli ndi bodza muli mbali iti kweni kweni dpp 2025 boma
Nanunso.. angaang. . mumalitenga..... mbali.... ya. Mcp.... Osaganiza ... Zidzukulu .. zako. . bwanji ........
Anthu opusa omwecamalandila ndalama .... Zopusa zenizeni ......iweyo ukuona ngati ku dpp kuli mbuli eti ....akulu inu ndi mbuli yeniyeni ndipo simukuziwa zomwe zikuchitika
Sakunama anthu aku dpp akuganiza ngati Ana, achina chaponda anakalamba musaiwale munthu akakula zelu zimabwelela a maganiza ngati mwana wazaka ziwili
mkuluyi akunena Zowona koma poti ma supporters a DPP adazolowera kutukwana apa mutukwanaso, MCP ikungokudodani ili pheee, ndiye musadatitu mulimbe kutukwanaku mpaka 2030 woooo.
Garu iwe kape weni weni waiona ndi DPP basi zakokhalira basi pamtumbo pako chsru chidebe chamunthu osamakadya ndalam zo uko bwanji nyani palukundu penipo mpikene mwedyo anambwa
Kulirako kukufunika panopa
Chifukwa zisankhozo is around the corner
Kodi Achakwera adalowela machine
Achakwera sadalowere ma vote Achakwera adalowera ma demo
Tingopanga ma demo basi kuti atuluke boma
Iwe namachede ngati watumidwa pwala lako ife machine awa sitikuwafuna manya pako iwe hassan
Kape akungobwelenza kulakhula kopusa komanso kunali zipani zingapo ukungochula DPP chifukwa chiyani? akuti zikomo kwambiri muchomeyi kkkkkkk dzoba iwe
Kodi mkulu ameneyi mdiwakuti .....chisilu cha munthu ochi
Akuti ku Mangochi
Zoti majority rules umayimvetsetsa koma, odambana mkamwa iwe? Mboliyako
Kodi inu adpp munthu akakuzuzulani inu mukungoti wapasidwa ndrama Kodi inuyo bwanji mupite Nanu mukalandile ndramazo bwanji inu anthu opusa inu Kodi inu simumszuzulidwa panja ndinu anthu osakhululuka ngati nkhalamba yanu ija inuyo kutani Kodi?? Mumafunakuti zikoli muzingolamula inu nokha basi anthu osowa fundo inu dziko lidakukanikani anthu muwauza chani kuti akumveleni nkhani pa nsonkhano kumangotukwsna basi zaziiii
Wakutuma Mtenje?
PALI MWAMBI WAKUTI TUMIZANI MBAVA IKAGWIRE MBAVA. DPP NDI MBAVA POKHUDZA NKHANI YAZISANKHO. UMBONI ULIPO PITANI MUKAONE UMBONIWO KUKHOTHI KUTI ANABELA ZISANKHO.NDIYE CHIFUKWA CHAKE AKUOPA ANZAO APANGA ZOMWE ANABELA IWOWO.
Ngangatu mukuoneka kuti ndinu munthu odziwa kuchita analyse zinthu. Nganga inuyo ofunika kuchoka ku Mangochi chifukwa ndinu munthu oyang"ana patali. Chifukwatu ku meneko anthu ambiri amangotsatira ziri zonse zomwe yakamba DPP. ONSE AKUKUTUKWANANI APA KUTI MWAFUFUZE MUPEZA AMBIRI NDI MBUTUMA MKALASI NDIYE KUTI ANATHERA MU STD
Atupeletu mdi OPHUNZIRA NDIPONSO NDI OZINDIKIRA. KUNGOTI VUTO NDI ANTHU AMATSOGOLERAWO. A BAKILI ANANENA KALE ZOKHUDZA OTSATIRA CHIPANI CHA UDF NDISACHITE KUBWEREZA PANO ANAZIMVERA OKHA
Kodi iweyo ukunena zopusaz osaganizra ana ako otuwa aja adzakhal bwanji mwe alukundu pathako pako
A Shamimu za anthu OSAMBA IZI
@@yassinn5634 amakobiri osati za anthu osauka ngt ine panopa eyetu zokomera andlama inu nanga kampopa ngolo mphawi otheratu okudya zotoleza ngt ine pano mkumatan dziko ndilanu ili znse mzanu zmwe
Mwayankhula zoona lemi wanu anthu oganiza mwachilungamo ngati inu ndiwomwe tikuwafuna,dpp ndichipani chama propaganda komanso kusokoneza,sangakane makina ovotera komanso kumukana chairman wa electrol commission siku la lero,malamulo aziko lino anapereka kale mphamvu kwa chairman kugula makina amenewa,ntambo asakupusiseni nayenso ndiwosokonekera kwambiri
Chili kwa anzanu chaipa mbuzi iwe. Sudziwa ntchito yoitanira atola nkhan kut ndikufuna uthenga ufike palipose...
Am not member of dpp but if I lose my data listening stupit story from MCP members....
Mmmmm I feel bored... Therefore I just say had I know before I couldn't open it
Pansetepako nyapapi
iwe mapwala ako iwe mbunzi yachabe chabe
Patumbo pako iwe ukuziwa chani iwe