A DPP Mwafulumila Kulira Shafie Hassan

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 19 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 53

  • @RoseThindwa
    @RoseThindwa День тому +3

    Za Zii Ngati mwatumidwa Malawi's sitikufuna machine wo

  • @MulowokaBlessings
    @MulowokaBlessings День тому +1

    Ukunena zoona big DPP alibe nzeru nkhalamba zilibe nzeru 😂😂😂 DPP akuyiopa game yakulila

  • @Twayaibrahim
    @Twayaibrahim День тому

    Ayakhula bwno abambo awa crias koma bvuto akuoposition mangot munthu walandra ndalama Malo mobvetsera bwno bravo Mr

  • @HerbartKaphamthengo
    @HerbartKaphamthengo День тому

    More 🔥🔥🔥🔥🔥Shafie DPP ikudziwiratu Kuti sazawina ndiye pachifukwa cha Ichi akungofuna kupasa anthu mmalawi Muno chiganizo oti masankho abeledwa pamene akudziwa Kuti zawo sizilibwino

  • @isaaczuze
    @isaaczuze День тому +3

    Mkulu uyu wandila ndalama ndipo ndi mbuzi yeniyeni ......chisilu cha munthu

  • @StanleyMunthali-s1d
    @StanleyMunthali-s1d День тому +1

    These guys are just blindfolding us . They forget 2025 is around the corner , Malawians panopa anasamba mokweza. Now they telling Malawians as if they are Angels now .They too should confess their past sins and be born again!

  • @isaaczuze
    @isaaczuze День тому +2

    Mkulu iwe ndi mbuzi Kodi chipani chinali ku press briefing anali a Dpp okha ....mbuzi iyi

  • @ChimwemweSimwela
    @ChimwemweSimwela День тому +1

    Anganga mwayankhula bwino

  • @MartinLondon-l4l
    @MartinLondon-l4l День тому +2

    Comrade nganga shaffi hassan ulemu wako mumatha kuyang'ana mbali zonse

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 День тому

      Ngati walandira ndiye kuti wachita bwino kuti aziphunzitse mbutuma kuti zizindikire kuti malamulo amapangidwa bwanji ndipo amapanga ndani? MP? KAPENA ATOLANKHANI?

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 День тому

      NGANGA NDAKUTAYIRANI KAMTENGO NDINU MUNTHU OZINDIKIRA NGATI SI ABOMA LIMODZI NDI ACHINA SALLO.AUZE NA AMENE ANALOWA MKALASI AMVA.MBUTUMA ZITSALA
      .

    • @GiftJulius-gx2kb
      @GiftJulius-gx2kb День тому

      Chisulu chadyera ichi

    • @GiftJulius-gx2kb
      @GiftJulius-gx2kb День тому

      Dyera galu uyu

  • @YamieManda
    @YamieManda 21 годину тому

    Macadet akufuna Jane Assah

  • @MulowokaBlessings
    @MulowokaBlessings День тому +1

    Taonani akungotukwana basi a DPP ndiye kutukwana mukutukwamako mwati muzaiona vote mmmmmm ndakayika chifukwa anthu inu ulemu milibe kuyambila magogo Anu aja opanda Manu mukamwa zochitanso chimozizi 😂😂😂 anthu simungalamulile ziko ndinu okanika komanso otembeleledwa MCP 2025 ikuwina whether you like or not

  • @HerbartKaphamthengo
    @HerbartKaphamthengo День тому

    DPP afford ndi UTM alira kale 😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 bwanji bosangonena Kuti a MCP apitilize Kuti ndalama zisaonongeke

  • @mayesojameskatete
    @mayesojameskatete День тому

    Atupele uja osazamuphwekesa UDF sitilola kukhala munkhwapa mwa MCP or DPP sitikuifuna tipita tokha kumasakho win or lose period ❤❤❤

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 День тому +1

    Malawi mayi ako iwe mapwala ako anamvomera ndani mapwala ako ndi kumangochi kwanuko andu osapita ku school akumangochi mwafikapo ndi umbuli wanuwo koma ine kumangochi bwanji kodi ayao awa

  • @HevenChiwaya
    @HevenChiwaya 21 годину тому

    Zoona zoti kuli opposition suzimaziwika ali nziiii kuopa kuti angayalusidwenso nawonso ali ndi Magazi mmanja mwawo ndiye nkivuta kudzuzula Malawi anainongeka basi

  • @AssanMwapi
    @AssanMwapi День тому

    Kulakhula mwazeru nganga

  • @MaxonKambazithe
    @MaxonKambazithe День тому

    Okay chabwino koma ifeee chakwera sitifuna aiiiiiiiii

  • @HusseinBinali-z1s
    @HusseinBinali-z1s 19 годин тому

    Wawo pe olo ryawo soni mmwee ilipyala mkawecheta soni yepyala yenuyo nambo soni Naga tummanye timtoche mmangochi muno

  • @christopherchikankhen
    @christopherchikankhen День тому

    Mau ndithu

  • @chifundocharles2348
    @chifundocharles2348 День тому

    Iwe sia DPP okha galu iwe uzinva,,,, 😂😂😂😂

  • @SandraBanda-hd1li
    @SandraBanda-hd1li 23 години тому

    Pansete.... Pako... nganga. ku... mangochi ko..... wamva

  • @FranksonKennethChipande
    @FranksonKennethChipande День тому

    Awa a DPP game akuiopa aona kuti palibe chawo 2025

  • @MiddayDeleza
    @MiddayDeleza День тому

    Inunso muli ndi bodza muli mbali iti kweni kweni dpp 2025 boma

  • @SandraBanda-hd1li
    @SandraBanda-hd1li День тому

    Nanunso.. angaang. . mumalitenga..... mbali.... ya. Mcp.... Osaganiza ... Zidzukulu .. zako. . bwanji ........

  • @isaaczuze
    @isaaczuze День тому

    Anthu opusa omwecamalandila ndalama .... Zopusa zenizeni ......iweyo ukuona ngati ku dpp kuli mbuli eti ....akulu inu ndi mbuli yeniyeni ndipo simukuziwa zomwe zikuchitika

  • @DerickChudza
    @DerickChudza День тому

    Sakunama anthu aku dpp akuganiza ngati Ana, achina chaponda anakalamba musaiwale munthu akakula zelu zimabwelela a maganiza ngati mwana wazaka ziwili

  • @MosesDzonzi-em5px
    @MosesDzonzi-em5px День тому

    mkuluyi akunena Zowona koma poti ma supporters a DPP adazolowera kutukwana apa mutukwanaso, MCP ikungokudodani ili pheee, ndiye musadatitu mulimbe kutukwanaku mpaka 2030 woooo.

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani День тому

    Garu iwe kape weni weni waiona ndi DPP basi zakokhalira basi pamtumbo pako chsru chidebe chamunthu osamakadya ndalam zo uko bwanji nyani palukundu penipo mpikene mwedyo anambwa

  • @AbdulsharifulKalipinde-m6u
    @AbdulsharifulKalipinde-m6u День тому

    Kulirako kukufunika panopa
    Chifukwa zisankhozo is around the corner
    Kodi Achakwera adalowela machine
    Achakwera sadalowere ma vote Achakwera adalowera ma demo
    Tingopanga ma demo basi kuti atuluke boma

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl День тому

    Iwe namachede ngati watumidwa pwala lako ife machine awa sitikuwafuna manya pako iwe hassan

  • @ISMAELNKWATULANKWATULA
    @ISMAELNKWATULANKWATULA День тому

    Kape akungobwelenza kulakhula kopusa komanso kunali zipani zingapo ukungochula DPP chifukwa chiyani? akuti zikomo kwambiri muchomeyi kkkkkkk dzoba iwe

  • @isaaczuze
    @isaaczuze День тому

    Kodi mkulu ameneyi mdiwakuti .....chisilu cha munthu ochi

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr День тому

    Zoti majority rules umayimvetsetsa koma, odambana mkamwa iwe? Mboliyako

  • @PrinceChapola
    @PrinceChapola 16 годин тому

    Kodi inu adpp munthu akakuzuzulani inu mukungoti wapasidwa ndrama Kodi inuyo bwanji mupite Nanu mukalandile ndramazo bwanji inu anthu opusa inu Kodi inu simumszuzulidwa panja ndinu anthu osakhululuka ngati nkhalamba yanu ija inuyo kutani Kodi?? Mumafunakuti zikoli muzingolamula inu nokha basi anthu osowa fundo inu dziko lidakukanikani anthu muwauza chani kuti akumveleni nkhani pa nsonkhano kumangotukwsna basi zaziiii

  • @EmmanuelGasiten-fo5dr
    @EmmanuelGasiten-fo5dr День тому

    Wakutuma Mtenje?

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 День тому

    PALI MWAMBI WAKUTI TUMIZANI MBAVA IKAGWIRE MBAVA. DPP NDI MBAVA POKHUDZA NKHANI YAZISANKHO. UMBONI ULIPO PITANI MUKAONE UMBONIWO KUKHOTHI KUTI ANABELA ZISANKHO.NDIYE CHIFUKWA CHAKE AKUOPA ANZAO APANGA ZOMWE ANABELA IWOWO.

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 День тому

    Ngangatu mukuoneka kuti ndinu munthu odziwa kuchita analyse zinthu. Nganga inuyo ofunika kuchoka ku Mangochi chifukwa ndinu munthu oyang"ana patali. Chifukwatu ku meneko anthu ambiri amangotsatira ziri zonse zomwe yakamba DPP. ONSE AKUKUTUKWANANI APA KUTI MWAFUFUZE MUPEZA AMBIRI NDI MBUTUMA MKALASI NDIYE KUTI ANATHERA MU STD

  • @yassinn5634
    @yassinn5634 День тому

    Atupeletu mdi OPHUNZIRA NDIPONSO NDI OZINDIKIRA. KUNGOTI VUTO NDI ANTHU AMATSOGOLERAWO. A BAKILI ANANENA KALE ZOKHUDZA OTSATIRA CHIPANI CHA UDF NDISACHITE KUBWEREZA PANO ANAZIMVERA OKHA

  • @ShamimuBisani
    @ShamimuBisani День тому

    Kodi iweyo ukunena zopusaz osaganizra ana ako otuwa aja adzakhal bwanji mwe alukundu pathako pako

    • @yassinn5634
      @yassinn5634 День тому

      A Shamimu za anthu OSAMBA IZI

    • @ShamimuBisani
      @ShamimuBisani День тому

      @@yassinn5634 amakobiri osati za anthu osauka ngt ine panopa eyetu zokomera andlama inu nanga kampopa ngolo mphawi otheratu okudya zotoleza ngt ine pano mkumatan dziko ndilanu ili znse mzanu zmwe

  • @JoelKacheche-x6i
    @JoelKacheche-x6i День тому

    Mwayankhula zoona lemi wanu anthu oganiza mwachilungamo ngati inu ndiwomwe tikuwafuna,dpp ndichipani chama propaganda komanso kusokoneza,sangakane makina ovotera komanso kumukana chairman wa electrol commission siku la lero,malamulo aziko lino anapereka kale mphamvu kwa chairman kugula makina amenewa,ntambo asakupusiseni nayenso ndiwosokonekera kwambiri

  • @PrinceBlessings-bv5bs
    @PrinceBlessings-bv5bs День тому +1

    Chili kwa anzanu chaipa mbuzi iwe. Sudziwa ntchito yoitanira atola nkhan kut ndikufuna uthenga ufike palipose...
    Am not member of dpp but if I lose my data listening stupit story from MCP members....
    Mmmmm I feel bored... Therefore I just say had I know before I couldn't open it

  • @eliasMwamba-q5f
    @eliasMwamba-q5f День тому

    Pansetepako nyapapi

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 День тому

    iwe mapwala ako iwe mbunzi yachabe chabe

  • @samanthamuller7643
    @samanthamuller7643 День тому

    Patumbo pako iwe ukuziwa chani iwe