Dr Michael Biziwick Usi VP has two hearts from the whole of last two weeks in Blantyre, Mulanje and. Thyolo he was preaching to the youths not to praise politicians and the youths and women should not be used as dancing objects but should be busy making money and now he who said those words is allowing the same to happen on his road side rallies.
Ena sakusangalalawo sanadye
Ai zikomo muzaziona
Mr vip phalombe is suffered district all passed government migowi to Nambazo no good road mr minganjira pass our massage to our president mr chakwera
Ovina ake ndiye mwalipila ochepatu bwanji, change chinatha?
Ndpo
Mmalo movala makaka a mcp akugwiritsa ntchito za UTM zamanyazi
Wichita kugulidwa awa kkkkk😅😢😂
Achewa aliyese ndi yoweyooo munakhala bwanji ndi manganya wa MCP kumuvinila
Kuchititsa manyazi anthu anga, mphamvu zodukulirazo mukuzitenga kuti? Kukondwako kusonyeza kuti zinachitika ku chikangawa zija inu munaiwala? Anthu omvesa chisoni inu 😢, rest in peace SKC😭😭😭😭😭😭
Dr Michael Biziwick Usi VP has two hearts from the whole of last two weeks in Blantyre, Mulanje and. Thyolo he was preaching to the youths not to praise politicians and the youths and women should not be used as dancing objects but should be busy making money and now he who said those words is allowing the same to happen on his road side rallies.
Manganya ukulakwitsa kugwiritsabe UTM yet unachokako, man , use MCP or odya zake alibe mulandu.
Azimayi mukamalza kuvinako muzikagona ndi njala,wat a shame
Komano ndi chifukwa chani akuyankhurira ali mu galimoto? Mantha kapena kunyada
Aphalombe amzanga mutichitisa manyazitu😊
Bumphawi sizinthu
Azionela okha
Ndale nd bzns apa manganya ali kokawoda mavote 😢😢
Mr. Ussi please stop wasting taxpayers money. It is as if you are celebrating your boss's loss of life. Time will judge you mapwiya wanga.
Ndichifukwa chianti vice president akuyenda yekha? Kapena alibe mkazi?
Kundichititsa manyadzi
Uphawi sizithu
Anthu aku phalombe muli ndimanyazi koma
Idyani ndalamazo ndi zathu...osakavotera MCP mwamva😅
Koma galu uyu akuti chani makamaka? Zinazi umangoti waziyambadala manganya the spirits of nine people are waiting for you and chikangawa.