MR BURA- DPP NDI YOMWE IKUTUMA BON KALINDO NDI ANTHU ENA KUTI AZINYOZA MCP

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 17 тра 2024
  • #malawipolitics #news #numeroyapastorntambabazi0788554028 #31march #funny #capetownmag #march2019 #zambia #live
  • Розваги

КОМЕНТАРІ • 160

  • @ChiyembekezoPhiri-sv8nw
    @ChiyembekezoPhiri-sv8nw 22 дні тому +2

    Mr bula musiyeni kalindo, inunso ndiye kuti MCP yakutumani mufuna nditumize zithunzi muli ndi chitchyola Banda eti! Mundisamale

  • @ShukuSh-vi1hk
    @ShukuSh-vi1hk 21 день тому +2

    Iwe ine ndikusaka mpaka ndikpeza iwe chisiru iwe ukukamba zatchuga osakamba bwanji zakikwera kwa fetreza kapena chimanga ukango bwera k cape tuwn kuno watha pamtumbo pako uribe mfundo

  • @user-hm9nc7lz6e
    @user-hm9nc7lz6e 22 дні тому +2

    Ndiwe opusa kwambiri ndiye amene asali mdzika yamalawi ndi ndani udzikawaudza amai ako ndi ana ako

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 21 день тому +1

    Ndi umbuli wakowo uyerekeza sugar wopangidwa ku south africa ndi sugar wopangidwa ku Malawi ......ndalama ndi imozi mbuzi iwe

  • @JamesMalango
    @JamesMalango 22 дні тому

    Inunso ndy ndindani opanda dzina

  • @MajotiMpandasoni
    @MajotiMpandasoni 21 день тому +1

    Kodi inu a mcp simasusa ntambo ndi akalindo nda anzawo awononga malawi ndindani Dpp ili paliponse osati kumwera bula

  • @fiskanmvula9367
    @fiskanmvula9367 21 день тому +1

    Iwe waboza bwanji MCP ukuyikira kumboyo bon kalindo amadzudzula chipani chilichonse galu iwe

  • @user-rl8xs2kf1o
    @user-rl8xs2kf1o 22 дні тому

    Kumalawi kulibe ntchito ,komwe muliko ntchito zambiri inutu mulungu akulangeni

  • @GospelSoldiers-sr7np
    @GospelSoldiers-sr7np 22 дні тому

    Kupanda mzeru osangokhala chete bwanji

  • @usherjamson174
    @usherjamson174 22 дні тому

    Chitsilu ndiwe ulakhulayo galu

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 22 дні тому

    Ukuona ngati chakwera akupasa mdalama eti

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x 21 день тому +1

    Bula bula mbuzi atonga kwanu ndi jelas bas olo kuno ku kep town mwachuka ndi jelas mbuzi inu ndiye bwanji mukulepela kumugwila waboza iwe

  • @KwestalanjesAjangale
    @KwestalanjesAjangale 22 дні тому +1

    Iweyo yakutumanso ndi mcp tinene chomcho bwa?

  • @JuniorHala-vf9ov
    @JuniorHala-vf9ov 22 дні тому +1

    Muluwali uyu wafumaso nkhuni chalo chanangika nadi

  • @KwestalanjesAjangale
    @KwestalanjesAjangale 22 дні тому +1

    Chibanzi chimenecho. Iwe tiziti dziko lili bwino ili ?

  • @ElvisKanyenda
    @ElvisKanyenda 22 дні тому

    Bundle yanga yathera pazopusa ine😢

  • @user-qv3bc4rv7q
    @user-qv3bc4rv7q 22 дні тому

    Machendeako galu iwe

  • @user-el8to1te3l
    @user-el8to1te3l 20 днів тому

    MCP ikamupanga sapot mtambo bwanj

  • @anodinjoya967
    @anodinjoya967 22 дні тому +1

    Mbuli yaikulu ndiweyo

  • @CaptainKaputeni
    @CaptainKaputeni 22 дні тому

    Panyapako

  • @user-mo1rs8qj6x
    @user-mo1rs8qj6x 22 дні тому

    Iwe bula pamtumbo pako ungayelekeze RSA ndi mw

  • @user-pl2lj6mh1z
    @user-pl2lj6mh1z 22 дні тому +1

    Choka iwe galu namachende iweyo chitsilu

  • @BlessingShabalala-py7fl
    @BlessingShabalala-py7fl 22 дні тому

    Ulindimatha galu iwe

  • @thokoJames-gp8mk
    @thokoJames-gp8mk 22 дні тому

    Komatu kutulukwa kwa adad anthu akusausika muntima 😅😅😅😅😅😅😅😅😅anthu kusowa ntendere

  • @Littlefair7
    @Littlefair7 22 дні тому

    Ngati DPP ikutuma Bon Kalindo ndiye ndi strategy yawo, a MCP paja ateategy inali kugula ma member a DPP, iwo atadandaula tinawauza kuti nanunso muzigula ma member a MCP, nanunso a MCP pezani anthu muziwatuma ndipo muli nawo kale achina Longwe.

  • @user-gx5ht9gm3z
    @user-gx5ht9gm3z 22 дні тому

    NO PAIN NO GAIN BURA NDIZINA LAMNTHU KUDWANGWA KUNO NDIZINA LANGOMBE 10:19 YOSABELEK CHISILU CHACHIKUL NDIWEO BURA

  • @LamseyLazarous-dl5qd
    @LamseyLazarous-dl5qd 21 день тому

    😂😂😂 koma ichi man

  • @user-od3fs3nm8d
    @user-od3fs3nm8d 22 дні тому

    Iziz ndy zotherana bundle izii plz osamangoponyaa zilizose pilizi abale aaaaa

  • @user-el8to1te3l
    @user-el8to1te3l 20 днів тому

    Aaaaaa iwe ulibe nzeru kwabas tiye tikumane ntown ndikukwapule ine ndili Maitland muno ndikuchose mano

  • @JMilanzie
    @JMilanzie 22 дні тому

    Muyendenso mutiuze ma salary akumeneko

    • @clubjunta
      @clubjunta  22 дні тому

      Ndiye ukuona ngati salary yomwe akulandila kunoyo ikugwila ndi kudula Kwa zinthu ??
      Akulu tikukhalilanso kupilila kuno zinthu zikudula kuno

  • @KingjwaYao
    @KingjwaYao 22 дні тому

    Walandila ndalama ku MCP iwe usalimbane ndi the DC wamva uzingokhala ku cap town kwakoko mbuzi iwe

  • @paulpaseli6310
    @paulpaseli6310 22 дні тому

    Iwe mbalame kobas

  • @adamusaidih8570
    @adamusaidih8570 21 день тому

    Malume pathumbo pano ndi cabinet yose boni calindo ndi bakili ndiathu okamba zonveka osati iweyo malume muchite manyazi😂😂😂

  • @user-wr1km2gh4g
    @user-wr1km2gh4g 21 день тому

    Kodi lero ndalama ya South Africa R1 ku Malawi ndi makwacha angati,mukudziwa izi,ndi pamene muzibwera pa social media ndikumayankhula zanuzo

  • @JameMirward-vm4dm
    @JameMirward-vm4dm 20 днів тому

    Ndekut iweo ukufn mcp ikupase ndalama ,, chitsilu kwambir iweo

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q 21 день тому

    IWE NDI GALU, NKHUMBA KOMANSO MBUZI😂😮😅

  • @user-hr2cg3ku1l
    @user-hr2cg3ku1l 22 дні тому

    Ifeso tili konkuno ku South Africa usatinamize mbuzi

  • @charleslimbani8590
    @charleslimbani8590 22 дні тому

    Kkkkk koma ndimanena nthawi zonse kuti ngati Dpp sizawinaaaa 2025 ku zomba mental kukaxaza kwambiri.....onse omwe timasapota Dpp tizapenga......😂😂😂😂

  • @user-lz6lr8bv9t
    @user-lz6lr8bv9t 21 день тому

    Zaziii mbuzi

  • @patrickndojime1632
    @patrickndojime1632 22 дні тому

    Iwe ndendaninso wachokera kuti akutuma galu nkokhapanyo chisilu chamunthu ichi

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 21 день тому

    Ku south Africa ukupangako chiyani mbuli ngati chisilu

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 22 дні тому

    Inu ndichitsiru kwambili ndipo NDIWE wajeraso ukalimbanat ndi born kalindo utha kufa osadwara mwina sikudziwa umfuse Ife tikumudziwa Atha kukusitha iwe kukhala wamkaz kumaliseche kwakoko wamva usamale kwambili ,ukhale ochenjera tapitatu uzikalakhulira kumalawiko uwopako chani? Mapazi azikang,awo wamva MKAMWA mosephanamo galu iwe Mwana wahure

  • @christophergibson72
    @christophergibson72 21 день тому

    Perfect said

  • @CharlesmakveliNyirenda
    @CharlesmakveliNyirenda 22 дні тому

    Chitsilu iwe ndalama ya Malawi ungafanitse ndi South Africa or American
    Mbuni ya mu2 iwe panya pa mayi ako

  • @JackMvura-ik2td
    @JackMvura-ik2td 22 дні тому

    Zoona man auzeni akuona Ngati awina kale DPP inatha akupha malubino sitikuwafuna kumalawi ndichifukwa chake chipani chanu chitha Ngati makatani zisanaoneke magazi alubino sadzachoka painu oipa DPP ya pitala

  • @user-kv8rk4ms5q
    @user-kv8rk4ms5q 22 дні тому

    Mtambo anali wamabugwe wa MCP koma anali omenyela ufulu ndi amene MCP inagwilitsa nde iwe ndiwe mu Chewa ulibe ufundo

  • @actuarialscience2283
    @actuarialscience2283 15 днів тому

    Mc Hende anu. Mapwala anu. Bon Kalindo sakulankhulira DPP.

  • @GIFTTONY-sw5qh
    @GIFTTONY-sw5qh 22 дні тому

    Inu ndy kuganiza kukuvutani ... Ufulu umamenyeredwa pamene waphwanyidwa osati pamene sunaphwanyidwe,,, palibe chanzeru chimene mwayankhupo coz anzanuo amapeleka umboni ogwirika nanga inu umboni wanu ulikut?????

  • @eliffagondewe8214
    @eliffagondewe8214 21 день тому

    Iwe. Ndi wamisala ndinthu, kodi @Bakili tv amanena zonama??? Iwe ingodya ndalama zomwe akupatsazo imbwaaa. 💔💔💔

  • @alexandermwale4669
    @alexandermwale4669 22 дні тому

    Ndengati ulipo ndiwe ndani iwe wapangapo chani kumalawi kambwi iwe

  • @paulmanyamba5437
    @paulmanyamba5437 22 дні тому

    Takunvani komano mokupemphani mukunveka kununkha mkamwa kwambili ndipotso palibe chomwe ukudziwa chokhuza dziko kuti limayenda bwanji ukunveka kuti umavala kamano ndiwe kape kwambili

  • @user-rk4ch1ly3z
    @user-rk4ch1ly3z 21 день тому

    Kodi iweyo ukufuna utamika,ukuwona ngati athu angamvele zomwe ukunenazo,iweyo walemvedwa ganyo ndi mcp wopoyila iwe eti,usamangogwila maganyu ako bwanji?

  • @ThomasStephan-tg6ng
    @ThomasStephan-tg6ng 22 дні тому

    Panyapako ok did we opusa kwambili

  • @mustafailanga2585
    @mustafailanga2585 21 день тому

    Iweyo ndigalu ukumana wina amene ali ku Philip mbudzi yamunthu

  • @GraceLimani-zw7dx
    @GraceLimani-zw7dx 22 дні тому

    Inu munkatuma mtambo, chilima ku panga ma demo amakuletsani ndani kodi

  • @user-rt4uv1mz1d
    @user-rt4uv1mz1d 22 дні тому

    Inu ndi achisilu kwambiri voice opusa kwambir

  • @ChaibishuSwadck
    @ChaibishuSwadck 22 дні тому

    Mk4,500 R 25 ikufanana galu iwe mbuzi yamunthu
    ikusiyana motani R25 to mk 4,500 iweyo ndikusaka paka ndikupeza ndipo ndikupha ndili cape town momuno galu iwe

  • @LemanKawala
    @LemanKawala 22 дні тому

    Ndipo akanati tidzivota sitigavutere ameneyo ukuti ndi president

  • @user-oy1yk3hg9k
    @user-oy1yk3hg9k 21 день тому

    Ukhale ukunen za mzeru aliyese angakutukwana kkkkk peza zina zochita kkkk

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 22 дні тому

    Dpp iwina ndipo Malo akowo usazapereke chifukwa pazakhala Manda Ako osati office ya DPP , Kodi Peter Mutharika samatukwanidwa ? Ndinu achisiru chilungamo mukuchikana chakwera wakoyo wapanga chani? Mwapasidwa ndalama inu uphawi wakumvutani inu

  • @user-vm7iz6oz6r
    @user-vm7iz6oz6r 21 день тому

    Ndiwe galu kwabasi ,zomwe akuyakhura athu ndizaboza? Aaa zaziiii

  • @EvanceMponda
    @EvanceMponda 18 днів тому

    Ukanakhala Dolo bwenzi uliku Malawi kuno nde unathawa kuno Malawi chifukwa chani? Ungafananise chuma Cha Malawi ndi south Africa ndie umbuliwo umenewo

  • @ZionekaMember
    @ZionekaMember 19 днів тому

    Iwe chisiru kwambiri economy ya Malawi ungaifananize ndi Malawi chisiru chamunthu

  • @ShukuSh-vi1hk
    @ShukuSh-vi1hk 21 день тому

    Iweso ndie pamtumbo pako uribe fundo ulibe mzeru kwambili

  • @user-ti2ct8ts8d
    @user-ti2ct8ts8d 21 день тому

    Anthu akutukwana kale ,Koma ndiwe kape kwambiri,

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 21 день тому

    Bula lingalhale zina la munthu .
    ..zingochita kuonekelatu kuti munthuyi ndi chisilu

  • @adamu1287
    @adamu1287 22 дні тому

    Iweyo boliyako mbudzi yamunthu pamodzi ndi mcp

  • @RichardMatandala
    @RichardMatandala 22 дні тому

    Mapaz Ako ada

  • @mrsmoseskita9180
    @mrsmoseskita9180 19 днів тому

    Mutu ngati choswera malambe galu iwe pamodzi ndi mbuzi yanu chakwera

  • @user-ee6be5kl5o
    @user-ee6be5kl5o 19 днів тому

    Iweyo bura Mutu wako sugwila ndithu munthu angamatumidwe kukapanga zoyipa mmayesa ukakhala ndi munthu umakana ukuyetsa Kuti MCP ikupatsa ndalama eti ngoo walemba mmadzi ndipo osamawalora anthu opanda nzeru Ngati ndi mbuzi nzake chawezi kumayankhulira anthu musiyeni Mr DC azikamba zanzeru, bwanji osamadzudzula boma la chakwera likuba ndalama dzuwa likuomba sitikufuña kumakumveranso iwe ayi chitsiru cha munthu

  • @wisdomsadyalunda2001
    @wisdomsadyalunda2001 21 день тому

    Ulibe content...iwe osangosiya bwanji.

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 22 дні тому

    Uzaziwa chilungamo ndikazaponya voti .
    ..mbole ya amako galu usatinyase.......nchewa opanda nzelu
    ...uzafunse anzako achewa kuno akuvutikila

  • @IssakeMateyo
    @IssakeMateyo 20 днів тому

    Zoona zake zimenezo

  • @phindiswatshibo7101
    @phindiswatshibo7101 17 днів тому

    Ndikupeza ku houtbay konko galuiwe

  • @user-qe2yi5zc3n
    @user-qe2yi5zc3n 22 дні тому

    Kunama iwe galu kwabasi iwe simkuziwa kuti chakwera wanga zithu iwe zopusa kwabasi ndi mcp yakoyo

  • @Trancy-xt4py
    @Trancy-xt4py 22 дні тому

    Ndinu achisiru inuyo 100r Kuno mumagurapo zithu zingat¿ Panga compare ndikumalawi 100 kwacha ungagurepo mchugar , California yaumfiti iwe ukukhala jondolo ungawawudze anthu zeru ? Atumbuka INU mumaziwa chani? Chifukwa mumasalidwa mulibe zeru musatukwanise atumbuka abwino ndinu opusa zakwamerica upitako uziudza abale ako ukukhala jondolo umanyera backet umfiti wako

  • @yusuflifa2923
    @yusuflifa2923 22 дні тому

    Galu iwe, chamba chimene amakubimphira thupi lose chinakupengetsa.. ugayerekeze south African ndi Malawi .

  • @IssakeMateyo
    @IssakeMateyo 20 днів тому

    Kodi tu athuwa ndi oti sakudziwa chimene akunena athuwa kkkk

  • @EvanceMponda
    @EvanceMponda 18 днів тому

    Uchitsiru ukhale munthu ukanakhala Bura?

  • @amontchuwa6876
    @amontchuwa6876 16 днів тому

    Iwe sukuziwa kt ndrama yathu ndiyakugwa aaaa bwanji kd

  • @user-oy1yk3hg9k
    @user-oy1yk3hg9k 21 день тому

    Iwe ndy ndi kape uzuzika kma olo one tambala ya wandale suinukha aise bola uzingolimbikila yokolopayo kumeneko

  • @ernestphiri5507
    @ernestphiri5507 22 дні тому

    Tseka pa chimbuzi you have no point

  • @patriciacraiton-sf5vu
    @patriciacraiton-sf5vu 21 день тому

    😂😂😂 Galu Iwe kuzambia kuno sugar it's very cheap so what are you talking about

  • @WinessMatcthuwana
    @WinessMatcthuwana 16 днів тому

    akuluwa ndiachisiludi

  • @jackmambo2638
    @jackmambo2638 21 день тому

    Kodi makolo ako umakonda Ase ife sitifuna kutikwana

  • @mkupabanda-nd2vb
    @mkupabanda-nd2vb 17 днів тому

    Umawakonda abale ako koma man?...…. chakwela wako uja ndi usi okhowokha tu mutu Muja........mwina sunamve zoti wapangaso pinyolo nyanja yathu chaku karonga side uku😂😂😂

  • @user-si7po9sd5i
    @user-si7po9sd5i 22 дні тому

    Ndiwe opusa kwambiri,BuraBura ndiyekutichani? Ndine Mr Bura? Galu iwe eti,ukununkhaso nkamwa choka,usandichimwitse.

  • @LamseyLazarous-dl5qd
    @LamseyLazarous-dl5qd 21 день тому

    Mbombela sanamange ndichakwela iwe ndi mbalame

  • @user-nn7sv5yb8h
    @user-nn7sv5yb8h 22 дні тому

    Iwe ndi mbuzi suziwa kanthu wakutumayo akukunamiza chitsiru anthu akufa ndi njala sukudziwa anthu akuba mboma sukudziwa usadzinamize tonse tili kuno usamanene zopusa

  • @isaaczuze
    @isaaczuze 22 дні тому

    Galu iwe ili ndi malo iwe

  • @CrossmanLingaoChirwa-df3gf
    @CrossmanLingaoChirwa-df3gf 21 день тому +1

    Aaaa a Mbale zikanakhala bwino mukanasiya kuti onyozanawo amalize chifukwa inuso mukuwonjezera kunyozako ndinene kuti nanu mwatumidwa ndi M C P?
    Ngati pangakhalre kuyankhula kuti zinveke bwino chosani kunyozako
    Chinthu china osavutika kujambula Chackers,Spa,Kaya Shoprite
    Mbale ndalama ya South Africa ndi ya mphavu kuposa Malawi
    Malawi akudadaula pa Malawi level osati South Africa
    Anthu mukumalandila R6,ooo pa mwezi ndiye akulandila K6, OOO kuno ndani?
    So don't waste time converting Rand to Kwacha
    Ngati zili bwino ndi chifukwa chani muli kumeneko?
    Mukasintha Rand kupeza makwacha mophweka musapuse mani
    Bwerani mugobole mommuno kenako muzayankhulenso zimenezo
    Ngati mukufuna chilungamo osanyoza chifukwa simukusiyana ndi enawo mwaonetsaso mbali next time za samaleni malankhuludwe otherwise muli fundo zogwirika komano zaonongeka ndi kunyoza pozuzula onyoza!!!!!!mmmmmmm

    • @isaacchiwaula731
      @isaacchiwaula731 17 днів тому

      Muli ndi mbali man, ur comment it's nice but muli ndi mbaliso inuyo man kkkkk

  • @AustinChiyembekezo-cx4mz
    @AustinChiyembekezo-cx4mz 22 дні тому

    Zikhala ku Capetown yakoyo galu wamunthu iwe mboli Yamako

  • @MadalitsoGama
    @MadalitsoGama 21 день тому

    Nyapapi

  • @MustafaEdward-bp2ip
    @MustafaEdward-bp2ip 22 дні тому

    Iwe ndiye ndi chisilu bas

  • @AishaChipande
    @AishaChipande 21 день тому

    Aaaaaaaaa dwangwa yake itii yomwe ukunena umachiziwa chamba iwee

  • @shadreckchijere6772
    @shadreckchijere6772 19 днів тому

    Ukufuntha bro

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q 21 день тому

    NKHUMBA IWE

  • @user-nl5nk2wx1q
    @user-nl5nk2wx1q 21 день тому

    PANKHOLO PAKO MULUKHU IWE.
    ZOTI ANTU AKUVUTIKA KUNO KU MALAWI IWE SUZIWA NKHUMBA

  • @user-lz6lr8bv9t
    @user-lz6lr8bv9t 21 день тому

    Nanga iweso wachokakuti mbuzi

  • @ChristopherMartin-yr2xx
    @ChristopherMartin-yr2xx 21 день тому

    Galu iwe ulibe mnzeru kodi ukufuna kuononga zomwe sakuziwa kuti aziwe