Politics yo dyetsana Manyi.. .We ready to die for this flag Zachimizi .Lilongwe sewage kwacha down youth struggling...and you want to bring fear to my head...No ! This is not 1993
Ndi plan yachikangawa imeneyo ndiyemwe wamuona Kut atha kumupasa bizy thaw ya kampeni ino.amanga bwanji Muthu opanda milandu, zake izo Ife nde boma tikusitha Patt!!?
Anthu a MCP ma plan awo amakhala olephera nthawi zonse adapanga plan ya Chilima anthu adawatulukiranso mwachangu lero apangaso izi anthu awatulukiranso nonse a MCP mulibe m'zeru ndale zanu ndi za anadi nokhanokha
Iyiyi ndi move akufuna asakayime nawo pa President adziyenda ndi Bello mu thumba... 🙆♀️🙆♀️🙆♀️
Eeeh Koma! There is just too much evil happening in this country. May the Almighty God come to our rescue.
Ine Joseph Mkuziwaduka Osadanda masten Sweet for sweat keep it up
Koma ife nde zatizunga mutu msaname ,zungokhala ngati za ma aged person ndithu kuti mwina akula anthuwa abwelera ku wumwana aaaaah 😊
Never give up pk
BomA la MCP ,,, mwatasa kwambili... Kufuna kubisa imafa ya SKC
History is best teacher koma kusanva anthu
Iyi ndi pulani kuti asaime pa koveshoni ndi Michael usi wagwirizana ndi chikangawa
Zoona akutiopa
Good make it truth on one life
Komatu utsi sufuka opanda moto dziko lonseli sangangoma Mayi Kaliyati! Akulu anati kang'oma kolilitsa sikachedwa kung'ambika osangoti poti ndimzimayi koma ngati alakwa afunika akumane m'chigamulo osamangonyoza boma.
Amawonjeza kma kupanga ndale sanyozana mayi uyu akhale nd displin
Politics yo dyetsana Manyi..
.We ready to die for this flag
Zachimizi
.Lilongwe sewage kwacha down youth struggling...and you want to bring fear to my head...No ! This is not 1993
But why mukumayika zithuzi nkhope yamagazi ngati munthuyo wakhapi propaganda
From Cape Town mitchells plain town centre. Chakwela ukufuna chiyani. Iweyo manganya ndimbuzi yamuthu kwambili ukuziwa kt upule sungatenge ndichingangawa wakoyo
Manganya ameneyo,,mafuta kulibe kummanga munthu wa utm akulira maliro achirima
Mayi ameneyu nayeso ndiosokoneza achita bwno kumutapa mesa ndi amene anathandiza bomali kt likhale pa pando eya uliziwe ziko zomwevlimapanga mwina uleka
Ndi plan yachikangawa imeneyo ndiyemwe wamuona Kut atha kumupasa bizy thaw ya kampeni ino.amanga bwanji Muthu opanda milandu, zake izo Ife nde boma tikusitha Patt!!?
Bwana Chakwera zomwe akupangazi adzafa ngati mwana ndipo sikale chifukwa pano anthu atopa nazo. Inu muzigona ndithu
Boma ili ndiloyipa kwambili don't warry amalawi tiligwesa popanopopano Muthu sumaluma Chala chimene chimakudyesa phala
Kalindo adanena kale izi ,sizodabwitsa
Kalindo ndi Katundu he never disappoints
Politics in Malawi is cleartivity that dazzles
Our country now is more 𝕎𝕠𝕣𝕤𝕖 𝕥𝕙𝕒𝕟 𝕓𝕖𝕗𝕠𝕣𝕖
Perekani chifukwa chomangira ...kungoti felony...timve zifukwa... felony sichifukwa..mukutisokoneza...
Mulungu si James pemphero mulungu amutetezere mai a kweni ndipo mzimu wa chilima uwakanthe anthuwo
Mulandu apalamula liti nanga masiku onsewa amadikila chani poti tava kuti anapalamula Mulandu ndiye masiku onsewa munalikiti
Mukamabweretsa nkhani zanuzo timaona ngati mwafufuza nkupeza chimene wamangidwira koma inunso muli mbuli pankhaniyiii moti mkumakasaka mma comments aanthu
Eti eti
ILI NDIBODZA KOMA ZOWONA ZAKE MCP IKUFUNA KUSOKONEZA UTM KOMATU MANGANYA NDI CHAKWERA NDIWO WAPANGA IZI MANGANYA
God deliver our beloved country whr r we going
Chakwera chitukuko ndichimenocho? failed president ever
Muja Paulos amanzunzira osatira Yesu ndi pamene Chikhristu chinafalikira kwambiri.Mungoonjejera mkwiyo wa pa 29 ndi 30 OCTOBER.
Izo ndindare manganya ndichikangawa afuna kuzunza azawo mmalo mosakha njira zotesera mavuto mmalawi muli bize kukorezer mukwiyo amalawi
Basi manyodza dpp ameneyo lelo adziwona okha kuti boma ndi dpp chipani cha ulemu
As MCP tries to kill UTM and entire opposition using Kape manganya,, shame
Ku Malawi timayankhula Chichewa,chitumbuka atinthandauzire mlandu wake timve bwino bwino
Ndingoziwa nawwo kuti azukako bwanji amai lero kuchitokolosi,ndadzuka ndi matha zedi😢😢😢,so God help us
Angofuna kuti kweni asapedze ku convention it's like government want to finish U T M. But God is watching.
MCP yikuopa chisankho ndichifukwa ayamba musokoneza mwapha chilima mwayamba kaliati nikufuna kusokoneza UTM afiti imwe a satanic imwe ba MCP agalu inu from Zambia 🇿🇲
Tru,,God z watching,,Mulungu awamenyera Mai kaliati nkhondo Ali cete
This is what we expected from Mcp with it's president too bad
MCP become scared of Kaliyati
Iri si boma ayi akufuna kuti kumbutsa nthawi ya kamuzu banda from mocambique
Inka Malawian politics very few women speak out. Kaliati is a voice for women.
mulandu wanji wosachulidwa
Malawi wawola chikangawa ukuwononga ziko lathu uzinka kwanu satana iwe
Michael Usi amadziwa kuti sangakhale president, Akweni for President,we are praying for you Akweni and our country Malawi
JESUS JESUS INTERVINE IN THIS SITUATION 😢😢
Ausi ndi munthu oyipa kodi. Usi iwe kayin. Umapemphera chani
Masiku atha kale awa tionana this coming year, kutha nzeru kwa Boma uku😢😢😢😢
Nde mukanangokhala chete osabwera ndi nkhani zossmveka spa mudziyamba mwafufuza kuti anthu adziwe chenicheni
Leave her alone this government bin Laden are at Malawi
Nde bwanji mlandu woo sakuwutchula, iziituu khaza akupanga ,kod zonsezi akuchitachi akufuna chani kwenikweni
Anthu a MCP ma plan awo amakhala olephera nthawi zonse adapanga plan ya Chilima anthu adawatulukiranso mwachangu lero apangaso izi anthu awatulukiranso nonse a MCP mulibe m'zeru ndale zanu ndi za anadi nokhanokha
Boma limeneli ndi loipa kwambili tionetsana 2025
Manganya akudziwa za kumangidwaku, Mulungu akuona, opposition be careful about
Koma ndi chani makamaka, God have mercy on us
Nkhani yonseyi ndi manganya ndipo khulupirirani kut manganya akudziwapo kanthu koma mulungu ndiwabwino Patricia kaliati atuluka mudzina layesu chikangawa koma umaziwa kut ku police skwabwino
Ana ambuzi inu mumangophatikiza zinkhani Tive ziti zopusa zimenezo mukufuna anthu akalakwa asamamangidwe dzitsiru zaanthu
Mcp mukunama uyuyu amupanga realise mukuona ngat tiopa anthu opusa inu chakwera ulibe nzeru
Koma APA titamangisane basi amalawi
Zopusa basi.Mulibe umboni weniweni chotipangila tag ndichani.
Awamanga chifukwa Choti anawakana chibwenzi apule,zoona mungamalimbane ndi mzimai mukufuna muzikhala busy kumugwilira kumeneko
Angofuna kupeza mpata osokoneza nsonkhano waukulu wa UTM pa 17 Nov. 2024
Channel cha bakili muluzi tv chija musazachipwekese iyewuja amaziwa chinachilichotse ndipo
Or utakhala ndiphamvu motani km zimatha or udindo umantha km asiyeni apange chimene akufunacho km siku lina malawi uzabwereraso muchimake
Kod tamakambani ndi PK apalamula mulandu waukulu mlandu wake uti felony simulandutu tanenani Mulandu wake
CHAKWERA NDI MBULI AMADANA NDI ANTHU AZERU
Azimai boza osayenda maliseche muzangoyaluka musiyen ngat mukuona mavuto gulu lake ndilomweli lomwe linalimhlbikisa zisokonezo nthaw ya pita
Akudziwana awa ndi momwe amadyera. Anthu a ndale zawo ndi zimodzi.
Ndale zaku Malawi
amalawi sisamapange chochi zosezi wapanga ndi usi pofuna kumulepere kuti asamenyere ufulu wa malawi basi tiwuzeni chomwe a mcp mukufuna chencheni
Uku ndi kuwonjezela nkwiyo wa chikangawa airport.
Kunzuza azimayi ndi mavuto akulu kwambili kaliati amatukwana bakili muluzi koma sanammange boma la chakwela ndi lolephela atetezeni azimayi onse nzdiko muno kusaziwa ndale ndi matenda
Boma loyendesedwa ndi zigawenga komanso mbava chonchi tikavotere anthu okuti akumanga anthu popanda zifukwa zenizeni
Akanango chepetsa mwano azipanga ndale bwinobwino ngati anzake
Akufuna manganya kuti atenge chipani kuti chibwerere ku mcp a kunama tu manganya anthu savoteratu
kulakwa uku asamutelo muthu
Kodi akufuna kumpha athu angati chifukwa chani m dima umadana ndikuujika bas tikufunabe commission of equrery
Mulungu salakwitsa kalikose akuwoneni pokuyikani nose wokhudxidwa pa ifa ya chilima
mcp mantha ayambika ndi chipan chomwe chinawayika pa mpando
Kod ufulu wa Azimai uja uli kuti Achakwela sizona mwachitazo
Boma koma lachakwera peter Samatha upulezident
Waikeso bambo ako aja akhale president wanva mbuzi iwee
Koma chakwera zikusata zomwe kuchita tikumana 2025
kenaka mumva kuti winwa atenga injuction yolepheretsa convetion,so that rumour is true,shame we are becoming a lawless nation
NDNAKAKONDA MANGANYA KUKOVESHONI ASAMULOLA AI NDI ANENE WAPANGITSA KUTI MAIWA AMANGIDWA AKU NDIKUPANIKIZA ANTHU ADZIKO MUNO PAKUFUNIKA PHAMVU MCP NDI CHAKWERA NDI ANTHU AKE WALITENGA DZIKOLI NGATI MUNDA WAMASIYE
Ukundiye kumulakwira kale lonse lija bwanji osamupha iiiii Koma ndale zakumalawi inu akangopezeka Kuti Wafa ndithu munditsimikiza Kuti khondo iyamba ndithu
Tisamakhale ngati malawi siyophunzila
Manganya panga manyazi ulibe umunthu Chocho kumati muzakhale president
Munamutenga nokha Lazalo ku chipiku kuti akhale president wanu lero akumangansoni mukhaula naye Chikangawayo
Koma apolice amene mikugwirisidwa ntchito achipan tizaona boma likadzasintha ntchito za mcp ndizimenezo chipani chakupha iweso jezebelo ziwa kt paudindo umenewo uzachokapo
Mulandu waukulu oponsa wakugwa kwa ndege ?
Ukayenda usasiye mlomo amayiwa amazitenga ngati adzao alibe pakamwa
That's indeed
Ndipo zikuonesadi kuti ndichina manganya inu aboma mukulemhera kukongola zakuchikanga nanuso muzamqngidwa
Michael usi ndiamene akupanga zonsezi
Kufunatu kukwiisa azimai uku aaaa anthu Ali mu mkwiyo kale mukufuna Malawi atani?
Dzulo tamva nkhani yonyoza yokhuza Malatavkodi mwamupanga chani?mwamusiya kamba ndinzanu?Kodi bwanji a Mcp simukupanga manyazi ndizomwe mukupanga manyazi? Dziwani ichiiiiii mukamapanga zinthu musamayangane pansies koma muziyangana kumwamba chifukwa mwini wa zonse alikumwamba.Timuope mulungu tisagwilise ntchito nzeru zathu chifukwa tizayankha patsogolo.Mulungu simunthu okondedwa.kubwenzera mkwayehova...........
She got problem I don't trust her the way I saw briefing with other party talking MEC and MCP and she can make big crime
YAA NDIZOWONA CHAKWERA MANGANYA NDI PLAN YOCHITA KUKOZA MISANA YANU MBUZI WHY OSAMANGA AMENE ANAPHA CHILIMA MUKUMANGA ANTHU OSALAKWA OSACHITA MANYAZI KUNKUYU ANAPHA MUNTHU BWANJI SIMUKUMANGA APOLICE IZI MUKUCHITAZI MADZAYIVA KUWAWA
Strong we stand,free up PK
Sizowona zimene zikuchitika ngakhale atapanga zimenezi ifeyo sitikubwerela buyo boma lokupha zotumidwa
Chikangawa political party has failed to run malawi gvt
ndiye bwino kupllice kumangopita aphawi