BAKILI MULUZI KUCHEZA NDI BRIAN BANDA 11/05/2024.

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 10 тра 2024

КОМЕНТАРІ • 97

  • @osmanmalinda939
    @osmanmalinda939 Місяць тому +9

    The first program kuonera ndikuseka nawo limodzi 😊 pamene enawa kumangokhala kulozana zala basi. What a great man

  • @TabiaNicks
    @TabiaNicks Місяць тому +5

    Long live our former president

  • @GhettohVibies-wn9zo
    @GhettohVibies-wn9zo Місяць тому +1

    Respect to you our X President Dr Bakili Muluzi🙏🙏🙏💕

  • @johnkatapeh7182
    @johnkatapeh7182 Місяць тому +8

    Long live Dr Bakili Muluzi❤❤❤❤❤❤

  • @user-cy7gd1go6y
    @user-cy7gd1go6y Місяць тому +3

    Pule amene anawafesa kukoma amalawi paka nthawi yochepa😢😢 mulungu akudaleseni mr muluz ndi wumoyo ndimakukondan❤❤❤❤❤

  • @waxyamidu5638
    @waxyamidu5638 Місяць тому +2

    Ulemu wanu bambo aife mwatilela zambiri talandila zaulele moti nyengo ya makolo athu samakwanisa kugura respect for you our father and thanks Brian potionesa atcheya

  • @luetec
    @luetec Місяць тому +2

    what a wonderful interview, ViVa a tcheya, the best well dressed president in Malawi

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому +3

    Atcheya tsopanoooo!!! timakunyadirani president wamsangala odziwa kuseka, osakhala zinazi aaaah

  • @JoshusMbewe
    @JoshusMbewe Місяць тому +1

    Long live Dr. Bakili Muluzi
    Abwanawa ndi munthu wabwino

  • @user-he7bu2tp8z
    @user-he7bu2tp8z Місяць тому +1

    Well spoken Dr Bakili Muluzi atsogoleri azitero tikufunilani moyo wautali pamodzi ndi family yanu Mulungu azikudalisani nthawi zonse

  • @user-qe2lz7mx7u
    @user-qe2lz7mx7u Місяць тому +1

    Bakili knows how to choose but bingu was the best ayao simuziwa economy

  • @AdamSteven-ne9hg
    @AdamSteven-ne9hg Місяць тому +1

    Nantahala ife muthawi yanu long life atcheya

  • @DonaldBanda-qi7yw
    @DonaldBanda-qi7yw 10 днів тому

    That's true His Excellence Dr Bakili Muluzi could stop just to give someone a lift in his Ministerial Car. For example is my Father (Late Stephen Eliya Banda) and myself, His Excellence the Former President gave us a lift in his Official Car while he was the Administrative General of the Mighty Malawi Congress Party.

  • @ImraanYaseen25
    @ImraanYaseen25 Місяць тому +1

    This man his is another level just hear his voice 😊

  • @rashiddeula5715
    @rashiddeula5715 Місяць тому +1

    This man! Ayayayay.....the humour is just great. Brian on a lighter note question eish.....ayayayay ndaseka mpaka misonzi. Mpaka odziponyaponya eti? 😂😂😂😂😂

  • @WellieManonga
    @WellieManonga Місяць тому +1

    Achalume kuchitekete God be with you

  • @victorzakeyuzimba7742
    @victorzakeyuzimba7742 Місяць тому

    Long live Muluzi

  • @magdalinemafunase2440
    @magdalinemafunase2440 Місяць тому

    We will always Love you a chair.❤❤
    Long live.

  • @EddieBakali
    @EddieBakali Місяць тому +1

    Quran on shelf mashala habibi

  • @atanasioestevao9707
    @atanasioestevao9707 Місяць тому +1

    Long live atcheya❤

  • @SwidiqLameck
    @SwidiqLameck Місяць тому

    I like his voice

  • @jaydee1236
    @jaydee1236 Місяць тому

    The great man 🎉❤

  • @mtangaJumbe
    @mtangaJumbe Місяць тому

    Munthu amene anapangitsa Malawi kukhala owawa kwambiri panopa. Chomwe ankagulitsira ma company kwa amwenye sichikudziwika

  • @tiongegondwe7219
    @tiongegondwe7219 Місяць тому

    Great man

  • @user-yk7gj1sl2z
    @user-yk7gj1sl2z Місяць тому

    Allah akudalitseni a chair

  • @zondiwesinging8001
    @zondiwesinging8001 Місяць тому

    Long live former president a chair anthu

  • @stewart.mwamughunda
    @stewart.mwamughunda Місяць тому

    Malawi ndi dziko lokhalo lomwe mapresident opuma akumva kukoma. Ulemu wanu a Chakwera.
    Taonani a Muluzi,mayi JB, Khumbo, APM, Chilupha n ena.

  • @FrankFrancis-ch3xv
    @FrankFrancis-ch3xv Місяць тому +1

    Watching live from SA Durban KZN

  • @user-cw6jg6xg7h
    @user-cw6jg6xg7h Місяць тому

    Long live achair!we love u!

  • @ibradaglass8646
    @ibradaglass8646 Місяць тому

    Pa town kumachenjela ❤❤❤achalume

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p Місяць тому

    Kuti enafe tisakhuzidwe ndi nkhaza za chipani chimodzi for that time Achair,,,munatinvetsa kukoma mu nthawi yanu❤❤❤❤❤

  • @aureliojose763
    @aureliojose763 Місяць тому

    kuntunda 🔥

  • @jeffchikwapata6933
    @jeffchikwapata6933 Місяць тому

    Big man ever

  • @shakajudahTV
    @shakajudahTV Місяць тому

    Much respect to our granny mumakwana 🎉🎉🎉🎉

  • @darlingtonchimutu8390
    @darlingtonchimutu8390 Місяць тому

    The most likeable PULE of Malawi kuseka continuous

  • @MonicaMbwera
    @MonicaMbwera Місяць тому

    Big man tsopano ❤❤❤

  • @richardmadaka287
    @richardmadaka287 Місяць тому

    Anamva mtunda ukufotokoza, anamva zonsezo ( I remember Mkasa's song. A Chair ndi mtunda)

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Місяць тому

    Kholo pa ndale

  • @user-hx8rr1mq7u
    @user-hx8rr1mq7u Місяць тому

    Watch live from Nyambadwe

  • @ChristopherKalonga-jt8iz
    @ChristopherKalonga-jt8iz Місяць тому

    Nice

  • @CumbuNgoma
    @CumbuNgoma Місяць тому

    A Gama we love you,long live

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x Місяць тому

    Big man

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Bakili vuto linapo ndi umbuli komanso business yake o i hope anali kupikulitsa bonya. Nfi masamba

  • @cristovaoherculano8662
    @cristovaoherculano8662 Місяць тому +5

    Government doesn't run a business. It should create atmosphere for people to do business.
    Ndani wamva zimenezi bwinobwino?

  • @JustinPhiri-kq2bb
    @JustinPhiri-kq2bb Місяць тому

    Sizaiwa former President pa free education primary sizophweka

  • @innocentmabedi3850
    @innocentmabedi3850 Місяць тому

    Mwana wakwathu

  • @RobertLuka-wy9cl
    @RobertLuka-wy9cl Місяць тому

    Achair Allah bless you ❤❤❤❤❤

    • @user-ub1vt2kq4s
      @user-ub1vt2kq4s Місяць тому

      Ulemu wanu acheya timakunyadirani kwambiri potibweretsela ufulu Allah bless you more

  • @WisikiBlack-gj4gu
    @WisikiBlack-gj4gu Місяць тому

    Simungathe kusangalatsa aliyese koma ndinu big man muthu wa bwino kwambili

  • @osmanwanja3733
    @osmanwanja3733 Місяць тому

    Atcheya woeeee!

  • @Oraterbadri
    @Oraterbadri Місяць тому +1

    putin waku malawi bakili

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x Місяць тому

    Achakulungwa wachiyao

  • @user-ni4nw1ee2f
    @user-ni4nw1ee2f Місяць тому +1

    Kuchitekete

  • @Gra898
    @Gra898 Місяць тому

    Ndale ndi tchimodi cz muli kuba muli bodza

  • @respectednation
    @respectednation Місяць тому

    ❤❤❤

  • @chawezichipeta5326
    @chawezichipeta5326 Місяць тому

    Kumtunda

  • @rexphiri7242
    @rexphiri7242 Місяць тому

    Atcheya

  • @user-cb9us2gn9v
    @user-cb9us2gn9v Місяць тому

    Achair ine ndilipo nkubwera konko ndithu

  • @imranshaibu1577
    @imranshaibu1577 Місяць тому

    Ku machinga Kwa chikweo ndiye kwathu 😂😂😂

  • @NoelKhwimba-bh3ts
    @NoelKhwimba-bh3ts Місяць тому

    Sitinaone nawo utsogoleri wanu komabe timanyadira chifukwa Cha zithu zochepa zomwe tinapeza kamba ka utsogoreri wanu taona ma k50 opanda mitu ife ndalama mumkatigaira ndi manja Anu akulu inu osati zinazi

  • @respectednation
    @respectednation Місяць тому

    Awa ndatcheya kuchikweza kkkkkk

  • @user-fl7br3dw4h
    @user-fl7br3dw4h Місяць тому

    Mumakwana acheir

  • @user-sq2uz6yl3s
    @user-sq2uz6yl3s Місяць тому +1

    To be honest this man is a greatest man,,,,,,,,,,,,,,,,,long live Dr Bakili Muluzi we love you very much ❤❤❤❤

  • @christophermukaka7403
    @christophermukaka7403 Місяць тому

    Achalume koma atcheya mmm amathandiza

  • @salimmkumakumakitombi-yc7pw
    @salimmkumakumakitombi-yc7pw Місяць тому

    Sogoreri aziseka abale .Atcheya inuyo ndati inuyo inuyo Atcheya mulungu azikudalitsani

  • @user-nj5vu8cd5l
    @user-nj5vu8cd5l Місяць тому

    Mr fake money... Kape wina amene anazesa mavuto mmalawi.kugulitsa ma company chitsiru

  • @ElijahHarah
    @ElijahHarah Місяць тому

    10:20

  • @AlidiMusa
    @AlidiMusa Місяць тому

    Bambo anagwila ntchito yotamandika awa. Mulungu adziwapatsa dza bwino iwowa

  • @LangretBanda
    @LangretBanda Місяць тому

    Atcheya mmakwanila

  • @SullyBartsony
    @SullyBartsony Місяць тому

    Tcheya ndikaswiri

  • @ElijahHarah
    @ElijahHarah Місяць тому

    Bigy...

  • @robertchitsulo8006
    @robertchitsulo8006 Місяць тому

    Muthu wakulu kwambiri

  • @user-mz8nw6nx6p
    @user-mz8nw6nx6p Місяць тому

    President olankhula zonveka bwino,,,not zinaziyi

  • @user-ud6mz3pf7x
    @user-ud6mz3pf7x Місяць тому

    Byson mwaona

  • @BashielSalade
    @BashielSalade Місяць тому

    M,tunda wa m,ndale

  • @kingpreach977
    @kingpreach977 Місяць тому

    A Chair palibenso

  • @DanMhone-iw6xg
    @DanMhone-iw6xg Місяць тому

    Tate wokondeka

  • @harrispheleni2205
    @harrispheleni2205 Місяць тому

    Kungogulitsa ma company a boma basi ndalama kupochera achalume anali ochenjera

  • @chinielstailoring-ro9lu
    @chinielstailoring-ro9lu Місяць тому

    professor

  • @user-nd8zg6ni7l
    @user-nd8zg6ni7l Місяць тому

    Tionele zimenezi

  • @YasinMusa-ym8lp
    @YasinMusa-ym8lp Місяць тому

    Kungocho kela kuchalichi kuvuna udndo ngamti chakwera

  • @user-fh5yn8xk2k
    @user-fh5yn8xk2k Місяць тому

    Awa anali adindo

  • @user-xe3xo5mu9k
    @user-xe3xo5mu9k Місяць тому

    Achalume🥸

  • @user-xg2ks9nw5q
    @user-xg2ks9nw5q Місяць тому

    Uyu ndi amene anayamba kugwirisana ndi amwennye nkhani yobera amalawi

  • @OscarChizula-qr4bi
    @OscarChizula-qr4bi Місяць тому

    munali munthu

  • @AllieKaisi-je6rm
    @AllieKaisi-je6rm Місяць тому

    Munthu wamkulu

  • @imranshaibu1577
    @imranshaibu1577 Місяць тому

    Munthu wamkulu ❤❤

  • @user-xg2ks9nw5q
    @user-xg2ks9nw5q Місяць тому

    Mbava iyi ndi yomwe inaononga zuko lamalawi

  • @patrickyakobe9685
    @patrickyakobe9685 Місяць тому

    By mentioning Late Chikufwa Chihana he was being honest, that name contributed a lot to Malawi democracy!

  • @kondwanimbewe1317
    @kondwanimbewe1317 Місяць тому +1

    The worst present ever