Kkkk mzimu.wa a chilima wayamba kuwaopsyeza a chakwerawo ..ndipo chilima awabwezera ..aphedwa chakwera ndi mzimu wa a chilima..kuyenda yendako.akusowa mtendere.
😂😂😂😂😂😂😂 Ine kudabwa ndinali kumsika ku Blantyre ndimagulitsa boiled eggs ndinangomva Manganya ati iwe! Ulembane ndi a Mazira anzako ndikupatseni ndalama ine kudabwatu ndati eee izi zayambanso liti kkkkkk
Ufune usafune ndi president wako ndi wangaso or APM president wake ndi chakwera basi nsanje ikupwetekani mufa ndi mtima ndipo sadzawina APM mudzaphulika abwerera ku America 😅😅😅😅
iiiiii olo ine ndinali odabwa anthu mpaka kukanganilana ndalama chonchija pa ground ine ndinkaona Ngati payambikanso masewelo ampila Koma eti anthu kunali kukanganilana ndalama
Kkkk mzimu.wa a chilima wayamba kuwaopsyeza a chakwerawo ..ndipo chilima awabwezera ..aphedwa chakwera ndi mzimu wa a chilima..kuyenda yendako.akusowa mtendere.
Ndipo the way I feel pain pano,mmene akuwanamidzila anthu pano,kumawombela manja ndithu hhhiii Malawi amayiwala,vuto ndife okomedwa
Mumatiyimilila Mulungu azikudalisani❤
I love you DC tikuyenela kt tisambe abale
❤❤❤❤ mr bon kalindo
The Dc bon kalindo good Messnge ❤
We're together born kalindo don't give up
Opengawa sitingachite kuwasate ayi.
Munthu okhala ndi nsapato ina yoyela ina yakuda ndi wa madrama basi
❤❤❤❤❤❤Timakudalilani bon kalindo
Chonde abon karindo musatisiye tokha muthawiyi ndinu wathuwathu
Umakwana❤
Ndinu nokha Mr DC mumatiimilira
❤❤❤❤
Chilungamo chayamba kwapeza ndawi yokuthayita
We love you kalindo
Kkkk DC sumaopa eeeee wamung'alura chakwela koopsa
Kkkk....yomweyo! chikangawa
Abwere andithandize kuumba njerwa
I support The DCs mwana woooopsa kwambiri akhalise Malawi chilungamo chiyende ngat madzi.
😂😂 mangochi sitipanga nao zachibwana
Umatha born kalindo
😂😂 President wathu wathu Mr DC
Best DC
Kkkk koma Born kalindo chitseko champana Chala
The DC🔥🔥
Umayakhura Za nzeru kwambil
Ndipo aboni chonde musatisiye ife tokha masiku atha kare awa muzapange chipani chanu tizakuvoterani
Kodi kupeleka mphatso ndivuto Kodi? Malume vutolanu ndilotani?
Bwana mumachulutsa intro kwambiri
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥
The dc 😂😂😂mwana wachabe kwambili 😅
Osaopa namachende ameneyi osavotelaso
Kodi simunatopebe ankolo
Big up winiko
Koma mwini page iwe kuyika mau it that form bwa j?
Osagulisa mwadzi wachilima
Be straight to the point nginiyi bwana imafunika data
😂😂😂😂😂😂😂 Ine kudabwa ndinali kumsika ku Blantyre ndimagulitsa boiled eggs ndinangomva Manganya ati iwe! Ulembane ndi a Mazira anzako ndikupatseni ndalama ine kudabwatu ndati eee izi zayambanso liti kkkkkk
Sanje yakuvutani
Tiye nazo Kalindo 😂
Malawi nde mwapenga Kodi president amayenda daily watch out
Ndipo mulungu atichitile chifundo dziko la Malawi ndipo MCP yatikhazika ngati dzikoli su lathu ngati tachita kubwela. Ambuye atithandize
DC ati ndine wa nyape😂😂😂😂
Kkkkkkkkkk Kkkkkkkkkk
Kuchikangawa kwavuta
The DC 🔥🔥🔥🔥🔥✈️✈️✈️
Umakwana
Kkkkk the DC 😂😂😂
Ziyenda ndiweyo kalindo?
Kuswa kuswa sankiyu DC
DC mbambande
Boza ndiye likupwetekani
Mmmmmm inuso kod tiziti iweyo sukuwona
Tarira kwanthawi yayitari zooona
The DC number one
Koma Peter Mutharika akakwela pa mpando,,asiye sakho akonde Malawian,, chifukwa akadzapanga ngati za chakwela tidzakutchotsa
Kkkkk asiya bwanji ngati dziko amalamula ndiye
Mmesa tinkalamulidwa ndi Chisale the bodyguard
Chakwera machende anu
Kalindo upenga ndiwe ndi chamba chako komaso nsanje
Upenga ndiwe ndi chakwera wakoyo
Mbambande the dc
Malawi Chikangawa Party=MCP=Ufiti
The D C !!!!!!!!!😂
😂😂😂
❤❤❤❤😂😂
Ufune usafune ndi president wako ndi wangaso or APM president wake ndi chakwera basi nsanje ikupwetekani mufa ndi mtima ndipo sadzawina APM mudzaphulika abwerera ku America 😅😅😅😅
Panyero pamako wamva,mkongo wamako
Kufuna kutchuka kucomenta kawiri ukusowa zochita😂😂😂
@@HannahNtenda if you don't know how to comment be silent mbuli iwe ndi opposition yanuyo
Choka mbuzi ya munthu iwe
Km awa iyayi zikomo
Mizimu yakwiya mutu sukugwira
Siziru za anthu boma lonse langozaza ndi mbava, palibe olo ndi modzi yemwe angavotere MCP, ndalamazo adyereni koma osakavotera 🐔 🐔🐔
Kkkk the DC
iiiiii olo ine ndinali odabwa anthu mpaka kukanganilana ndalama chonchija pa ground ine ndinkaona Ngati payambikanso masewelo ampila Koma eti anthu kunali kukanganilana ndalama
Anali kuti nthawi yoseyi
❤❤
😂😂😂