Watching from Johannesburg in south Africa we Malawians we made a very big mistake by putting these stupid people into government but I hope we have learned a lesson
The only best way to change the rottness of how Malawi is run is by voting into government a new political party that has never managed the affairs of the country .
And dziko azitsogoleri adakamakhala ndi nzeru ngati zanuzi panopa tili patali koma alliance iyiyi manyaka,,,Evance Meleka poimba nyimbo ya nthata zanjala ija mzimu udamulakhula mwapadera.
Ku NRB plus MEC kukufunikanso a Kamangira ena ukuku...akanika kuti amalawi apeze ma ID a unzika koma pano mukuti kalembera akuyamba m'mawa, what's that? Ndiye anthuwa adzavota bwanji?
Kamangira azakhale nduna ya minister of justice and constitutional affairs muboma likubweralo. Kuti izi zizatheke pabwere boma Lina. MCP ndi DPP ndiamozi sangamangisane zitavuta motani. Aliyense alinawo ma jaji Ake ku judicially. Pakufunika boma Lina la new blood. Boma losaona nkhope ndipume tikufina kuti Kamangira azagwile ntchito yake bwinobwino.
Corrupt judges in Malawi peter muntharika once complain about these judges blavo kamangira God bless u indeed tonse government won through corrupt judges
Wow gyz,without beating the bush u r direct in speaking.U r hitting the nail.Osaopa,osafooka komanso osatopa gyz.We r with u.
Atleast there are guys like Wonder and his team who love Our Country!
Chunga you are professional
Keep it up guys i always waiting for this program amalawi ambiri aseguka mmanso chifukwa cha nu limbikirani ndithu
I salute U gentlemen
More fire Mr kamangira
The only important radio station in Malawi Times
Mbambandee azibambo odziwa kuyankhula...... Time's Radio number 1 pa Malawi
Kuri chawez Banda mtorankhan wamanyi😊😊😊
Kamangila he’s there to save us,keep it up guys let’s support this guy
Times Tv Malawi ndi no.1, akulu akulu pitilizani mumalankhula bwino kwambiri, ndipo mulibe mbali.
We have a government which we have never had in Malawi ever. Useless government.
No 1 guys paliso Chavez banda amaryaso chibazi
Hot current imayenda pamwamba kamangila alimomwemo ist afamily member thus why wabaya pofunikira ndi aliyense wamvesa and this is true
A chunga God bless u your talking sense
Kamangila (lets Government please give protection from him, this guy never seen and Allah gave long life Alex
Watching from Johannesburg in south Africa we Malawians we made a very big mistake by putting these stupid people into government but I hope we have learned a lesson
Very good guys please keep it up
Isalute you guys good speaking mcp zakuvutani basi vomerezani
Look at South Africa mafuta it's already decrease last month koma Malawi ndipamene akupanga increase...what is that ma group wa Chakwera
Inali bh🎉
Ndipo nde kwambili za equally zokhazo asamale ndipo masiku akupita pangono pangono mpaka 2025 tizafuna umboni koma wina Ali nkati
Good advise but MCP imadzimva kudachulukako omwe adakhalako atsogoleri akudambwe kunyau. Athu ake amakhala okakala moyo.
😂😂😂😂😂😂okakaladi moyo😊
Kamangila pakufunika sapot yayikulu
The only best way to change the rottness of how Malawi is run is by voting into government a new political party that has never managed the affairs of the country .
Kamangila way more fire
Dziko lovesa chisoni😂$440=K1,000,000
Tithokoze kamangila potuluka poyela n,nyamata oganiza boo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤
Ulemu wanu Inuyo mmmmh 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌❤️❤️❤️❤️❤️❤️
Oky! Iyi simutchira mayina coz s allegations, about chimwendo yolesedwa kukwera ndege ija is not allegations??
And dziko azitsogoleri adakamakhala ndi nzeru ngati zanuzi panopa tili patali koma alliance iyiyi manyaka,,,Evance Meleka poimba nyimbo ya nthata zanjala ija mzimu udamulakhula mwapadera.
Uyu watitenga a Malawi
Malawi is captured by the big mafias 😢😢😢
Ku Maida kuli George Kasakula, akubakila mcp komanso chakwera. Koma tiyamikile Mr. Kamangila , wakeup Malawians pls. MBC ndiyowola kwambiri.
Azibambo inu ayi mukuyankhulila amalawife zikomo kwambiri
Ya Chizuma imandiwawa ngat Imfa ya Chilima. Boma ili limadana ndi Chilungamo.... Always bodza,....
Minister of Justice wake kutii kapee ameneujaaa
Ya Mai Chidzuma nde imandiwawa kwambiri. We didn't support that noble lady eeeeish! Malawi wanga😭
Ku NRB plus MEC kukufunikanso a Kamangira ena ukuku...akanika kuti amalawi apeze ma ID a unzika koma pano mukuti kalembera akuyamba m'mawa, what's that? Ndiye anthuwa adzavota bwanji?
Kamangila ulibooh anthu akukanika kumwa tea chifukwa chaiwe kamangira .Wagwedeza
Kupupuluma aboma. Mukuopa chaini? Asyeni a mademo, ndiufulu wap.
Yes amazitengad ngati ndizawozawo anthu okanika awa
Osapanga ngati za khuluku uyu chawezi.Ndiwamadyera mphoto munthuyu.
nthawi yikakwana yimakwana basi tiyenazo musabwelere mbuyo nthawi yakwana iyi
Kamangira azakhale nduna ya minister of justice and constitutional affairs muboma likubweralo. Kuti izi zizatheke pabwere boma Lina. MCP ndi DPP ndiamozi sangamangisane zitavuta motani. Aliyense alinawo ma jaji Ake ku judicially. Pakufunika boma Lina la new blood. Boma losaona nkhope ndipume tikufina kuti Kamangira azagwile ntchito yake bwinobwino.
Tafwa mwafwa enough is enough Malawi shocking country Martha Chizuma my comrade Mmmm xool mate 😂
100% ndiye kiyankhula ... Judiciary, mizila manja nonsense
A Jaji akulu imitsani ma Jaji akutchulidwa wa.
Chimene chingachitike anthu ose amene akuvutika asakamvote ayi aka vote okaoka sibwino kumazuza osauka ayi aba bolani so bingu wamutalika anayika ikonome osati zitsiluzo ayi sakuchita bwino
Ma guy awa akuyesetsa kuliwongolera boma koma eesh anthuwa ndiwokanika ndithu ndipo anthu opanda chisoni ndithu
Kodi jonna please give him for first time
Kkkkk komatu ndebvu zamwayi ungakwanise carat KKK manjawo umandipeza when speaking.
Pankhani ya a Kunkuyu, mmmmmmm , kunkuyu ndi boma akuyankha bwanji nkhani ya MEC ndi a kalembela?
boma la mamafia ili 😂😂
Kt ndizivutika vuto ndi matipate aliyeyese akakhala boma amalemera kwambiri kmas kuvota kumawonongetsa ndalama boma
Malawian people samalowelera kamba kot kumankhala komvuta kulowapo komaso samadya nawo ndalama ndeeeee wina aliyese amaganizapo zoyakhula amakhala ataona phindu lake akayakhula guy's 😮😮
Pankhani ya mafuta, mesa Kabwira ndi Chakwera amakalandila mafuta ambiri ku Nsanje pa njanji? Alikuti mafutawo?
Koma malawi
Kamangira way
Kkkkkkkk owo...
Ndipo Akangila akaphedwa ndi MCP tikudzwa zioneka bola moyo
Chunga boma siiiii iliiiiiii
Zoona
Tokotani anyamata this government is full of educated ignorance and Malawi is dying alive
kodi mmayesa mcp inkati yalandila mafuta ndiye inuyo atolankhani bwanji simukuwafunsa achakwera kuti mmayesa paja anati alandila mafuta nanga alikuti mafuta aja ankawachemelela aja
Chikangawa wamaliza folex yonse ndi ndege
Inu anyamata inu mumatilankhulila koma andale makani mmmmm
Azaona polekela asiyeni
Ma bigy inuyo mukunyapura boma n ma institution onse mosanyengelera ulemu wanu
Kkkkkk kkkk....
Muli bho
Inu mmatiyimilira
Azibambo inu...More Fire 🔥 ♥ 😍 ❤
😂
Corrupt judges in Malawi peter muntharika once complain about these judges blavo kamangira God bless u indeed tonse government won through corrupt judges