KOMA HOT CURRENT YA LERO MPAKA KUFIKA POYANKHURA CHONCHI? ANTHU AWAWA ALIBE MANTHA NDIPO SAMAOPA

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 19 жов 2024

КОМЕНТАРІ • 77

  • @RabbecaMbukwa-y1z
    @RabbecaMbukwa-y1z Годину тому +1

    Wow gyz,without beating the bush u r direct in speaking.U r hitting the nail.Osaopa,osafooka komanso osatopa gyz.We r with u.

  • @Lizzie-h1k
    @Lizzie-h1k 3 години тому +5

    Atleast there are guys like Wonder and his team who love Our Country!

  • @victorbanda9039
    @victorbanda9039 Годину тому +2

    Chunga you are professional

  • @ShakiraJackson-x8w
    @ShakiraJackson-x8w 2 години тому +1

    Keep it up guys i always waiting for this program amalawi ambiri aseguka mmanso chifukwa cha nu limbikirani ndithu

  • @UnityBasikolo
    @UnityBasikolo 36 хвилин тому

    I salute U gentlemen

  • @BrunoChakukuma
    @BrunoChakukuma Годину тому

    More fire Mr kamangira

  • @georgenewa3508
    @georgenewa3508 2 години тому +1

    The only important radio station in Malawi Times

  • @HappykamwanamwanaBwaila
    @HappykamwanamwanaBwaila 2 години тому +1

    Mbambandee azibambo odziwa kuyankhula...... Time's Radio number 1 pa Malawi

  • @SurprisedDrumKit-ql7rj
    @SurprisedDrumKit-ql7rj 2 години тому +1

    Kuri chawez Banda mtorankhan wamanyi😊😊😊

  • @Yungjoe786
    @Yungjoe786 2 години тому

    Kamangila he’s there to save us,keep it up guys let’s support this guy

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 години тому +1

    Times Tv Malawi ndi no.1, akulu akulu pitilizani mumalankhula bwino kwambiri, ndipo mulibe mbali.

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 години тому +2

    We have a government which we have never had in Malawi ever. Useless government.

  • @DanielNkhata-wt9ov
    @DanielNkhata-wt9ov 2 години тому +1

    No 1 guys paliso Chavez banda amaryaso chibazi

  • @MichaelKaerama-dd4bk
    @MichaelKaerama-dd4bk Годину тому

    Hot current imayenda pamwamba kamangila alimomwemo ist afamily member thus why wabaya pofunikira ndi aliyense wamvesa and this is true

  • @CathleenMsaya
    @CathleenMsaya 3 години тому +1

    A chunga God bless u your talking sense

  • @TimeAbilu
    @TimeAbilu Годину тому

    Kamangila (lets Government please give protection from him, this guy never seen and Allah gave long life Alex

  • @GeorgeTambala-j1m
    @GeorgeTambala-j1m 3 години тому +1

    Watching from Johannesburg in south Africa we Malawians we made a very big mistake by putting these stupid people into government but I hope we have learned a lesson

  • @NewtonTembo-q4t
    @NewtonTembo-q4t 2 години тому

    Very good guys please keep it up

  • @esmybanda2227
    @esmybanda2227 2 години тому

    Isalute you guys good speaking mcp zakuvutani basi vomerezani

  • @AkiduMakwinja-x1h
    @AkiduMakwinja-x1h Годину тому

    Look at South Africa mafuta it's already decrease last month koma Malawi ndipamene akupanga increase...what is that ma group wa Chakwera

  • @Kelvin-hj5qv
    @Kelvin-hj5qv Годину тому

    Inali bh🎉

  • @NickUpoche
    @NickUpoche Годину тому

    Ndipo nde kwambili za equally zokhazo asamale ndipo masiku akupita pangono pangono mpaka 2025 tizafuna umboni koma wina Ali nkati

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 години тому +1

    Good advise but MCP imadzimva kudachulukako omwe adakhalako atsogoleri akudambwe kunyau. Athu ake amakhala okakala moyo.

  • @GodfreyWhayo-hh1dm
    @GodfreyWhayo-hh1dm Годину тому

    The only best way to change the rottness of how Malawi is run is by voting into government a new political party that has never managed the affairs of the country .

  • @HassanChibwana
    @HassanChibwana 2 години тому

    Kamangila way more fire

  • @HamzajOsman
    @HamzajOsman 16 хвилин тому

    Dziko lovesa chisoni😂$440=K1,000,000

  • @FatimaAdam-r5y
    @FatimaAdam-r5y 3 години тому

    Tithokoze kamangila potuluka poyela n,nyamata oganiza boo❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤❤

  • @doreenkaliati3166
    @doreenkaliati3166 3 години тому

    Ulemu wanu Inuyo mmmmh 🙌🙌🙌🙌🙌🙌🙌❤️❤️❤️❤️❤️❤️

  • @fleshar-j6i
    @fleshar-j6i Годину тому

    Oky! Iyi simutchira mayina coz s allegations, about chimwendo yolesedwa kukwera ndege ija is not allegations??

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 години тому

    And dziko azitsogoleri adakamakhala ndi nzeru ngati zanuzi panopa tili patali koma alliance iyiyi manyaka,,,Evance Meleka poimba nyimbo ya nthata zanjala ija mzimu udamulakhula mwapadera.

  • @TiongeSimkonda
    @TiongeSimkonda Годину тому

    Uyu watitenga a Malawi

  • @benjaminjobo3525
    @benjaminjobo3525 Годину тому

    Malawi is captured by the big mafias 😢😢😢

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 години тому

    Ku Maida kuli George Kasakula, akubakila mcp komanso chakwera. Koma tiyamikile Mr. Kamangila , wakeup Malawians pls. MBC ndiyowola kwambiri.

  • @jonathanmbewe4246
    @jonathanmbewe4246 3 години тому +2

    Azibambo inu ayi mukuyankhulila amalawife zikomo kwambiri

  • @JonesChingaya-yf4gg
    @JonesChingaya-yf4gg Годину тому

    Ya Chizuma imandiwawa ngat Imfa ya Chilima. Boma ili limadana ndi Chilungamo.... Always bodza,....

  • @GiftMlinde
    @GiftMlinde Годину тому

    Minister of Justice wake kutii kapee ameneujaaa

  • @MercyKishombe
    @MercyKishombe 3 години тому

    Ya Mai Chidzuma nde imandiwawa kwambiri. We didn't support that noble lady eeeeish! Malawi wanga😭

  • @dysonmasiye5736
    @dysonmasiye5736 2 години тому

    Ku NRB plus MEC kukufunikanso a Kamangira ena ukuku...akanika kuti amalawi apeze ma ID a unzika koma pano mukuti kalembera akuyamba m'mawa, what's that? Ndiye anthuwa adzavota bwanji?

  • @ShaibuSmart
    @ShaibuSmart 2 години тому

    Kamangila ulibooh anthu akukanika kumwa tea chifukwa chaiwe kamangira .Wagwedeza

  • @WillyNyirenda-l7h
    @WillyNyirenda-l7h 2 години тому

    Kupupuluma aboma. Mukuopa chaini? Asyeni a mademo, ndiufulu wap.

  • @PaulBeyad
    @PaulBeyad 3 години тому

    Yes amazitengad ngati ndizawozawo anthu okanika awa

  • @RabbecaMbukwa-y1z
    @RabbecaMbukwa-y1z Годину тому

    Osapanga ngati za khuluku uyu chawezi.Ndiwamadyera mphoto munthuyu.

  • @JawardBenard
    @JawardBenard Годину тому

    nthawi yikakwana yimakwana basi tiyenazo musabwelere mbuyo nthawi yakwana iyi

  • @WillyNyirenda-l7h
    @WillyNyirenda-l7h 2 години тому

    Kamangira azakhale nduna ya minister of justice and constitutional affairs muboma likubweralo. Kuti izi zizatheke pabwere boma Lina. MCP ndi DPP ndiamozi sangamangisane zitavuta motani. Aliyense alinawo ma jaji Ake ku judicially. Pakufunika boma Lina la new blood. Boma losaona nkhope ndipume tikufina kuti Kamangira azagwile ntchito yake bwinobwino.

  • @DavidKanyemba-n2s
    @DavidKanyemba-n2s 2 години тому

    Tafwa mwafwa enough is enough Malawi shocking country Martha Chizuma my comrade Mmmm xool mate 😂

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 години тому

    100% ndiye kiyankhula ... Judiciary, mizila manja nonsense

  • @MrMagombo
    @MrMagombo 3 години тому

    A Jaji akulu imitsani ma Jaji akutchulidwa wa.

  • @GolosiMalapata
    @GolosiMalapata 2 години тому

    Chimene chingachitike anthu ose amene akuvutika asakamvote ayi aka vote okaoka sibwino kumazuza osauka ayi aba bolani so bingu wamutalika anayika ikonome osati zitsiluzo ayi sakuchita bwino

  • @PreciousSteven-e5s
    @PreciousSteven-e5s 3 години тому

    Ma guy awa akuyesetsa kuliwongolera boma koma eesh anthuwa ndiwokanika ndithu ndipo anthu opanda chisoni ndithu

  • @DavidPhiri-o6w
    @DavidPhiri-o6w 2 години тому

    Kodi jonna please give him for first time

  • @Blessings-td4cr
    @Blessings-td4cr 2 години тому

    Kkkkk komatu ndebvu zamwayi ungakwanise carat KKK manjawo umandipeza when speaking.

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 2 години тому

    Pankhani ya a Kunkuyu, mmmmmmm , kunkuyu ndi boma akuyankha bwanji nkhani ya MEC ndi a kalembela?

  • @HamzajOsman
    @HamzajOsman 22 хвилини тому

    boma la mamafia ili 😂😂

  • @PatrickMalenga-h5m
    @PatrickMalenga-h5m 2 години тому

    Kt ndizivutika vuto ndi matipate aliyeyese akakhala boma amalemera kwambiri kmas kuvota kumawonongetsa ndalama boma

  • @patesnkajenda4258
    @patesnkajenda4258 2 години тому

    Malawian people samalowelera kamba kot kumankhala komvuta kulowapo komaso samadya nawo ndalama ndeeeee wina aliyese amaganizapo zoyakhula amakhala ataona phindu lake akayakhula guy's 😮😮

  • @MathewKalinkhu
    @MathewKalinkhu 3 години тому

    Pankhani ya mafuta, mesa Kabwira ndi Chakwera amakalandila mafuta ambiri ku Nsanje pa njanji? Alikuti mafutawo?

  • @KondwaniGondwe-y3d
    @KondwaniGondwe-y3d Годину тому

    Koma malawi

  • @fanuelbanda2985
    @fanuelbanda2985 2 години тому

    Kamangira way

  • @MaxwellMilanzi-w5k
    @MaxwellMilanzi-w5k 2 години тому

    Kkkkkkkk owo...

  • @AhmadumkomaTambala-lr9gp
    @AhmadumkomaTambala-lr9gp 3 години тому

    Ndipo Akangila akaphedwa ndi MCP tikudzwa zioneka bola moyo

  • @MalumboMzumara
    @MalumboMzumara 2 години тому

    Chunga boma siiiii iliiiiiii

  • @MarryNyilongo-s5x
    @MarryNyilongo-s5x 2 години тому

    Zoona

  • @fjtkusamba5948
    @fjtkusamba5948 3 години тому

    Tokotani anyamata this government is full of educated ignorance and Malawi is dying alive

  • @AhmadIsmael-l5q
    @AhmadIsmael-l5q 2 години тому

    kodi mmayesa mcp inkati yalandila mafuta ndiye inuyo atolankhani bwanji simukuwafunsa achakwera kuti mmayesa paja anati alandila mafuta nanga alikuti mafuta aja ankawachemelela aja

  • @CathleenMsaya
    @CathleenMsaya 2 години тому

    Chikangawa wamaliza folex yonse ndi ndege

  • @MartinRajab-w5e
    @MartinRajab-w5e 3 години тому +1

    Inu anyamata inu mumatilankhulila koma andale makani mmmmm

  • @PeterRabson-z3w
    @PeterRabson-z3w 3 години тому

    Ma bigy inuyo mukunyapura boma n ma institution onse mosanyengelera ulemu wanu

  • @MaxwellMilanzi-w5k
    @MaxwellMilanzi-w5k 2 години тому

    Kkkkkk kkkk....

  • @EnockBeston
    @EnockBeston 3 години тому +1

    Muli bho

  • @RodgersMtonga
    @RodgersMtonga 3 години тому

    Inu mmatiyimilira

  • @hamiltonsolomon3756
    @hamiltonsolomon3756 3 години тому

    Azibambo inu...More Fire 🔥 ♥ 😍 ❤

  • @miovekanola2780
    @miovekanola2780 3 години тому

    😂

  • @CathleenMsaya
    @CathleenMsaya 3 години тому

    Corrupt judges in Malawi peter muntharika once complain about these judges blavo kamangira God bless u indeed tonse government won through corrupt judges