Malawi immigration office ndi dimba la nick chakwera ndi zikhale ng"oma motsogozedwa ndi Lazarus. Yankhulani chichewa akulu palibe nzungu amene akukuvetsa nyasi ya chizungu chimenecho.yankhulirani munthu wakudzi ave.
@@petroszgambo9949 bwino nthawi yatha iyi yesu akubwera muchimwa nazo zambili muziwone ndi maso a uzimu zikutsegulani maso kuti yes chofunika kukonza mtimawu siziyenda momwe tikufunila kaya ndi economy,njala,matenda,nkhondo ma floods,ananena kuti zidzachitika mu nthawi yakumapeto zikomo kumbukilani sodomu ndi gomola ndi momwemu angakhale mu nthawi ya nowa
inuyo ochenjera? a Malawi muthu achite chabwino mumuloza zala apange zoipa ndiye worse...tonse stingayendese dziko man even amene mungafune inuyo eyendeseo papezekabe ena osawakonda. muona koma kuti mutaani
@@user-bd5kw8oq1r kkkkk palibe wabwino padziko lapansi. The guy is trying hard. Akulubwawa ndi ana oti sakuona chabwino pa chilichonse. Zimaoneka bwino Muthu uja akachokapo. See the Presidency trend bwana. Komaso iweyo moti sukuona zomwe akupanga. I support usi. Other wise enawo nde Ali trush
Weldone V/ P you are doing what the VP should do keepon serving the Malawians.
Ndale izizi. Challenge ndiyaku even Muthu atakhala akupanga zithu zokomela dziko, but ngat Ena ake zikuwaphinja bas zimasanduka ndale. Umakwana manganya.ngat zikuwanyasa akasume🎉🎉🎉🎉🎉🎉
Hiyaa nothing can change coz zinalo ndale zithuzi
we get tired of useles govt
Akufuna ma allowance amenei
Akuoneka kuti samayembekeza kuti angakhale vp alangizi ake please mulangizeni asamangozigwira gwira ayi oooo ndaona akusowa mtendere wa mumtima
Ukulimbana mdi zikhale ohoooo kkkk
Kamba za ma passport iwe munthu... sizikugwirizana ndi za mankhwala apa
Awa awo ndi ma drama osati ndale. Nanga pamenepa walankhula zichiani..
Guys kodi mukuyamikira zichani pamenepa. Palibe chamzeru chimene wayankhulatu uyu
Malawi immigration office ndi dimba la nick chakwera ndi zikhale ng"oma motsogozedwa ndi Lazarus. Yankhulani chichewa akulu palibe nzungu amene akukuvetsa nyasi ya chizungu chimenecho.yankhulirani munthu wakudzi ave.
Amalawi 😅😅
Judas weni weni, at akufuna kuti tiziwe kuti akulankhula .. nonsense! Politician fool.
@@petroszgambo9949 bwino nthawi yatha iyi yesu akubwera muchimwa nazo zambili muziwone ndi maso a uzimu zikutsegulani maso kuti yes chofunika kukonza mtimawu siziyenda momwe tikufunila kaya ndi economy,njala,matenda,nkhondo ma floods,ananena kuti zidzachitika mu nthawi yakumapeto zikomo kumbukilani sodomu ndi gomola ndi momwemu angakhale mu nthawi ya nowa
Koma yudasi uyuuuuuu😅😅😅😅😅😅 kumpereka yesu
Awaa atikwana bwanjii
Why you didn't ask about corruption
If he was clever enough he should start this in Central Region! Opusa Michael Usi. When did you spoke to PS 😂😂😂😂😂 Manganya!
inuyo ochenjera? a Malawi muthu achite chabwino mumuloza zala apange zoipa ndiye worse...tonse stingayendese dziko man even amene mungafune inuyo eyendeseo papezekabe ena osawakonda. muona koma kuti mutaani
Kuno nku Malawi basi tizidikila tsiku lakufa
Ngati watumidwa ndi Chakwera's family! Kuti uzachite push their family business here wauponda.
Akungolongolola ..phokoso basi....system ya ku immigration yakupeta and he likens it to medical / treatment system
Zaziiiiiii 😂
Apite ku capital hill akayankhule kumeneko ngati ali serious
Waste of time and resources
Za ziiiiiiiiiiiiiii musatipepeletse ife mukudziwa zomwe mukupanga anyani Inu munalonjeza kuti ma passport mwayamba kupanga lero kuli ziii zili zabodza amalawi mmationa ngati opepela eti agalu Inu Ali ndi #ya Micheal manganyayo andipatse ndimuimbile pompano mxieeee
Nenani ndinu zennizeni anthu abwino amzanu a nyani good for you
@@user-bd5kw8oq1r kkkkk palibe wabwino padziko lapansi. The guy is trying hard. Akulubwawa ndi ana oti sakuona chabwino pa chilichonse. Zimaoneka bwino Muthu uja akachokapo. See the Presidency trend bwana. Komaso iweyo moti sukuona zomwe akupanga. I support usi. Other wise enawo nde Ali trush
@@user-ol6uc7bj2w good I support usi also
I wish I can speak to him in person asatiyese ife opusa ndale iziii
Nsonda mukufuna pofera