MICHAEL USI WAYANKHULA IZI LERO ATAFIKA KU IMMIGRATION YA KU BLANTYRE

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 8 вер 2024

КОМЕНТАРІ • 31

  • @AlexanderYovatiKhumalo
    @AlexanderYovatiKhumalo Місяць тому +1

    Weldone V/ P you are doing what the VP should do keepon serving the Malawians.

  • @user-ol6uc7bj2w
    @user-ol6uc7bj2w Місяць тому +1

    Ndale izizi. Challenge ndiyaku even Muthu atakhala akupanga zithu zokomela dziko, but ngat Ena ake zikuwaphinja bas zimasanduka ndale. Umakwana manganya.ngat zikuwanyasa akasume🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @user-vf3tq5sn9j
    @user-vf3tq5sn9j Місяць тому

    Hiyaa nothing can change coz zinalo ndale zithuzi

  • @user-mm3wq8qp2q
    @user-mm3wq8qp2q Місяць тому

    we get tired of useles govt

  • @user-vf3tq5sn9j
    @user-vf3tq5sn9j Місяць тому

    Akufuna ma allowance amenei

  • @ZaithwaMatchado
    @ZaithwaMatchado Місяць тому

    Akuoneka kuti samayembekeza kuti angakhale vp alangizi ake please mulangizeni asamangozigwira gwira ayi oooo ndaona akusowa mtendere wa mumtima

  • @CathrineBizza
    @CathrineBizza Місяць тому

    Ukulimbana mdi zikhale ohoooo kkkk

  •  Місяць тому

    Kamba za ma passport iwe munthu... sizikugwirizana ndi za mankhwala apa

  • @Jerry-vm6mo
    @Jerry-vm6mo Місяць тому

    Awa awo ndi ma drama osati ndale. Nanga pamenepa walankhula zichiani..

  • @LonjezoAkacharlie-r2q
    @LonjezoAkacharlie-r2q Місяць тому

    Guys kodi mukuyamikira zichani pamenepa. Palibe chamzeru chimene wayankhulatu uyu

  • @henryphiri6100
    @henryphiri6100 Місяць тому +1

    Malawi immigration office ndi dimba la nick chakwera ndi zikhale ng"oma motsogozedwa ndi Lazarus. Yankhulani chichewa akulu palibe nzungu amene akukuvetsa nyasi ya chizungu chimenecho.yankhulirani munthu wakudzi ave.

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому +1

      Amalawi 😅😅

    • @petroszgambo9949
      @petroszgambo9949 Місяць тому +1

      Judas weni weni, at akufuna kuti tiziwe kuti akulankhula .. nonsense! Politician fool.

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      @@petroszgambo9949 bwino nthawi yatha iyi yesu akubwera muchimwa nazo zambili muziwone ndi maso a uzimu zikutsegulani maso kuti yes chofunika kukonza mtimawu siziyenda momwe tikufunila kaya ndi economy,njala,matenda,nkhondo ma floods,ananena kuti zidzachitika mu nthawi yakumapeto zikomo kumbukilani sodomu ndi gomola ndi momwemu angakhale mu nthawi ya nowa

  • @AREFRIEDNELSON
    @AREFRIEDNELSON Місяць тому

    Koma yudasi uyuuuuuu😅😅😅😅😅😅 kumpereka yesu

  • @rashirdbanda8204
    @rashirdbanda8204 Місяць тому

    Awaa atikwana bwanjii

  • @LeoYokonia
    @LeoYokonia Місяць тому

    Why you didn't ask about corruption

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Місяць тому

    If he was clever enough he should start this in Central Region! Opusa Michael Usi. When did you spoke to PS 😂😂😂😂😂 Manganya!

    • @itubiz1501
      @itubiz1501 Місяць тому +2

      inuyo ochenjera? a Malawi muthu achite chabwino mumuloza zala apange zoipa ndiye worse...tonse stingayendese dziko man even amene mungafune inuyo eyendeseo papezekabe ena osawakonda. muona koma kuti mutaani

  • @JamesKhengemussa-t1d
    @JamesKhengemussa-t1d Місяць тому

    Kuno nku Malawi basi tizidikila tsiku lakufa

  • @petertaulo8014
    @petertaulo8014 Місяць тому

    Ngati watumidwa ndi Chakwera's family! Kuti uzachite push their family business here wauponda.

  • @PeterChilinga1984
    @PeterChilinga1984 Місяць тому

    Akungolongolola ..phokoso basi....system ya ku immigration yakupeta and he likens it to medical / treatment system

  • @AbunthiMtambo
    @AbunthiMtambo Місяць тому

    Zaziiiiiii 😂

  • @patiencechangole9825
    @patiencechangole9825 Місяць тому

    Apite ku capital hill akayankhule kumeneko ngati ali serious

  • @MakupeWekha
    @MakupeWekha Місяць тому

    Waste of time and resources

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz Місяць тому

    Za ziiiiiiiiiiiiiii musatipepeletse ife mukudziwa zomwe mukupanga anyani Inu munalonjeza kuti ma passport mwayamba kupanga lero kuli ziii zili zabodza amalawi mmationa ngati opepela eti agalu Inu Ali ndi #ya Micheal manganyayo andipatse ndimuimbile pompano mxieeee

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      Nenani ndinu zennizeni anthu abwino amzanu a nyani good for you

    • @user-ol6uc7bj2w
      @user-ol6uc7bj2w Місяць тому +1

      @@user-bd5kw8oq1r kkkkk palibe wabwino padziko lapansi. The guy is trying hard. Akulubwawa ndi ana oti sakuona chabwino pa chilichonse. Zimaoneka bwino Muthu uja akachokapo. See the Presidency trend bwana. Komaso iweyo moti sukuona zomwe akupanga. I support usi. Other wise enawo nde Ali trush

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      @@user-ol6uc7bj2w good I support usi also

  • @CharityChikomo-hl1gz
    @CharityChikomo-hl1gz Місяць тому

    I wish I can speak to him in person asatiyese ife opusa ndale iziii

  • @user-eh6lr4ng5y
    @user-eh6lr4ng5y Місяць тому

    Nsonda mukufuna pofera