MALAWI WANYANYALIDWA NDI ANTHU AKUNJA!!... ZINTHU ZIDULA KWAMBIRI, MWINA BREAD ATHA AFIKA K8,000
Вставка
- Опубліковано 9 лют 2025
- Welcome to our channel, where we dive deep into the intricate and evolving world of Malawi’s politics. From the rise of powerful political parties like the Democratic Progressive Party (DPP) and Malawi Congress Party (MCP) to the powerful impact of the UTM Party and other parties like UDF, AFORD, PP, MMD, and PETRA, we bring you insightful analysis on the key players shaping the nation. Explore the journeys of leaders like Lazarus Chakwera, Saulos Chilima, and the influential activist Bon Kalindo as they navigate the challenges of governance, power struggles, and the quest for a better future.
Our channel is dedicated to unraveling the complexities of Malawi’s political landscape, offering you detailed breakdowns of alliances, rivalries, and the significant events that continue to define the country’s destiny. Whether you're interested in historical perspectives or current political dynamics, we provide in-depth coverage and engaging content that keeps you informed and inspired.
Subscribe to stay updated on the latest developments, and join us as we explore the fascinating stories that shape Malawi’s political narrative.
NOTE : We try to be as neutral as possible when giving you news from all parties. Maybe sometimes we may seem to offer or insult a certain party, kindly forgive us and above all, tell us in the comment section.
#MalawiPolitics #PoliticalAnalysis #DPP #MCP #UTM #LazarusChakwera #SaulosChilima #BonKalindo #AfricaPolitics #PoliticalActivism #petermutharika
Onse amene amatsogolela upandu ochotsa pm,akudya, akukhuta, but the mass is starving,
MCP ikulakwitsa kunyoza chipani Cha DPP ndi anthu opanda respect on your reader
Mcp never again 😢
💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙💙❤❤❤❤❤❤❤❤❤APM yemweyo mcp yalephela.
Mcp mmm mbola
Achakweeeeeeeraaaaa 🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣🤣kuchikangawaaaaa kunakwiiiyaa mutu suzagwiraso mpakaaa angeroo azaitaaaneee muli pamotooo😢😢😢😢😢😢😢 ovuta kudzimitsaa
Azibusa yangonenani,kuti Boma li lawavuta basi,AAA kumazemberaso apa
G to G
Ayalutseni agalu a mcp ndi zisilu
MCP mmm mbola oyika zikwangeani zitukuko zopanga DPP kkkk no network
Chakwera sanakhaleko nduna sakuzwa kuendesa ziko pepan schipongwe😂😂 Speech from atupere muluz 😅😅🤷🤷
It says "if you don't appreciate what you have, you will end up with nothing" boni kalindo, biziwiki manganya, chilima, Joyce banda, and all others, put chakwela on power, they brain washed the public, and know who is suffering?
Zandikhuza lelo nditamva Kuti switi ali pa K200
Chakwera mutu siwukugwira atapha chilima Kuti azapambane Koma panopa akuwopa Peter mutalika akumamupangira mawupu Kuti amuchose pabaloti paper
Bread paka 8pin ayi zikomo
Mombela university Dpp inalephera kumanga kumuzimba nenani chilungamo
Akunama m1 idakanika a Dpp
Ndalama zakunja mesa mwapereka ku Ghana (Hashcom).
Kuyika nwala wa maziko ndiye kuti wamanga a mugahao aduka mu mutu
Aaaaaaa,zukhalabwanji Kodi? Mesa Amati mafutawa azigula G to G? Nde akuti lero aziti Resave ndiimene yathandizira koma zinthuzake
Kulakwa abale
Dpp akupanga lonchi sikupanga chinthu peter amangoyika miyala osapanga
Timatumiza black market
😂
malamulo onyossa mundu nkushokella mugawo lamalamulo sonyosa mundu ndi full wawina aliyense APM itha nkukasumilla mcp phangani imeneyo
ndikulephela kuwelenga
ℂ𝕙𝕚𝕔𝕙𝕖𝕨𝕒 𝕔𝕙𝕒𝕟𝕛𝕚 𝕚𝕔𝕙𝕚?
Mwat bwa
Muzisiyanisa chichewa ndi chiyawo pano tikulembapo chichewa osati zanuzo. mpaka mutu uzipweteka kamba kofuna kunvetsetsa powelenga?
Kkkkk ndangoseka nawo ine