Chakwera said he will be on the ballot...he didn't specify kuti as a what. President or vice. 2. For their agreement to achieve, Chakwera needs to win at MCP convection ...so I don't see why people are not seeing this...unless Chakwera will try to betray Chilima after convection
umvetsere bwino statement ya chakwera iwe ndi kachizungu kako ka ku cteache..he dint say he will be on the bsllot but he said If they will chose him then he eill compete.this means as Apresident paja anayamna ndi mawu oti Malamulo adziko lino limavomereza kyyima kawiri ndiye iwe nawenso ndiwe mbuzi sumvetsa
Kodi zomwe anagwirizana a chilima ndi a chakwela, mu malamulo a dziko la Malawi zikuloledwa? Kapena malamulo asinthidwanso?
Andalewa ndi amene akupitiriza kuononga dzikoli
Hot current 😂🔥
Dyela ndiloipa kwambili,,umaiwala lonjezo
Vice president, wamwa ambuye mutengeni, waononga UTM. 😂😂😅
Ndiwolose ndikakutafune anatsikira bwato pakati pa nyanja, atawona mafunde.
Let him stand and fail miserably shame oh him agalatiya
Kkkkkkkk mpakana zezeze eti
UTM ikuchedwa kwambili koma Bon kalindo adayankhulapotu izi
Ine ndikuona kuti anthuwo anakambirana nso kachikena kuseri ndipo a Chilima akudziwapo kanthu adagulitsa chipani chawo ku MCP ndichifukwa chake angosankha kukhala chete
Ukunama
Muuuzen kachikena akunama uyu chilima Sangalore zopusazi
Km Wanda
Kalumo timuuzire chilima athana nae
A ndevu zamwayi cnt shed his mcp bias
Lakukhalani lopha ng'ombeyo bwana.Mumakwana guys
Yes Mr Maphang'ombe lakuyanjani ndithu chifukwa simunyengelera Azibambo inuyo always be true more 🔥🔥. Koma Abanda tawasowatu
Firs to comment
😂😂😂😂oganiza boh!!
Wonder ndale suidziwa,,unvetsele a pankukuwuwo ndi a Chunga
Yatokhara njilwa ?? Kuti asaiziwe?? Mulibe zonena
SKC my vote
Best ❤ 27:29
Chakwera said he will be on the ballot...he didn't specify kuti as a what. President or vice. 2. For their agreement to achieve, Chakwera needs to win at MCP convection ...so I don't see why people are not seeing this...unless Chakwera will try to betray Chilima after convection
Ba Ballot iyeyo adzayimira ngati president... Sukunvapati?
umvetsere bwino statement ya chakwera iwe ndi kachizungu kako ka ku cteache..he dint say he will be on the bsllot but he said If they will chose him then he eill compete.this means as Apresident paja anayamna ndi mawu oti Malamulo adziko lino limavomereza kyyima kawiri
ndiye iwe nawenso ndiwe mbuzi sumvetsa