BON KALINDO LERO PA 16 JULY 2024 |

Поділитися
Вставка
  • Опубліковано 22 сер 2024

КОМЕНТАРІ • 150

  • @user-lz4kc5ob1t
    @user-lz4kc5ob1t Місяць тому +2

    Ife tamupasa kale mai kaliyati president of utm

  • @user-ig9ip8jq7v
    @user-ig9ip8jq7v Місяць тому +1

    Watching from S A port Elizabeth timakunyadilani bwana pitilizani kuti imilira Mr Bon kalindo l Salute u bwana

  • @EnittaDavison
    @EnittaDavison Місяць тому +2

    Umatiymilra iweyo ulemu wako bon 🔥🔥🔥🔥👏👏👏👏👏👏

  • @justinmakiyi4189
    @justinmakiyi4189 Місяць тому +10

    As UTM and Malawi as whole country we are luck having this guy as somehow a prophet or advisor to the difference parties. The choice is in our hands to take the advise or leave them. But one day we shall remember Him. That's the free advise indeed. Regards

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Місяць тому +6

    😅😅 zapana ndithu ndipo sanati and who is Manganya??? U don't know Bonnnnnn Kalindooooo mwana oopsa kwambiri ndiponso mumumva, the DC mwana woyankhulira pa mchombo pa Malawi, alibe mantha ndipo saopa Unyolo kaya mfuti😅😅😅

  • @Lazarus-qo1sl
    @Lazarus-qo1sl Місяць тому +5

    President wathu wathu amangoyima pachilungamo🎉

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      @@Lazarus-qo1sl president wa zitsilu zokhazokha ndi mbuli zophumzila koma makolo awo fees anagowononga ngati mmene DPP inawonongera dzikoli

    • @VungaQueen
      @VungaQueen Місяць тому

      Mmmmmmmm inu Bon Kalindo musiye nde zitsilu tili ambili inu anthu abwino Kharani km siwani kt choyipa chitsata Mwini nadutsa sindinyoza ine

  • @christopherphiri8476
    @christopherphiri8476 Місяць тому +3

    Born kalindo will help UTM if anything engenge him to assist he is a man of action Christopher phiri from Zambia

  • @FatimanickisJaffer
    @FatimanickisJaffer Місяць тому +3

    DC born kalindo more fire 🎉

  • @SteveSamson-t9d
    @SteveSamson-t9d Місяць тому

    following kalindo Diiiiiìiiiiiiii siìiiiiiiiiiiii

  • @user-dp7bc7yy6s
    @user-dp7bc7yy6s Місяць тому +3

    Awa ndiye amkamuna a UTM zili ndiinu kunyozera km Bon ndiye walangiza.

  • @MisheckAselo
    @MisheckAselo Місяць тому +5

    The DC, Mr booooooon kalindo 🎉🎉🎉

  • @TooNajahInsideKoshah
    @TooNajahInsideKoshah Місяць тому

    Iwe ndiye president wathu wathu

  • @DalitsoTwalick
    @DalitsoTwalick Місяць тому +2

    Thanks my president for ur information

  • @user-yk5qd6sk8e
    @user-yk5qd6sk8e Місяць тому +2

    the dc 🎉🎉 mwana ooopsa kwambili

  • @user-mh7cc8up4i
    @user-mh7cc8up4i Місяць тому +2

    Kodi a UTM mukuitana athu kwana chifukwa ninji Kodi menemo mulibeathu oti angayendese chipani ?bwinonazotu ndalama inampha mwanawamuthu zayekha ananyika sima m'mazi

  • @vincentkhunsanama584
    @vincentkhunsanama584 Місяць тому +2

    Yeah, the DC is not making mistake to advice the utm fam big up the DC

  • @JosephLemani-qq1is
    @JosephLemani-qq1is Місяць тому +3

    Mwayankhula bwino bon kalindo ena akufuna kugwetsa chipani cha UTM koma bola abwelele komwe anachokela

  • @user-bd5kw8oq1r
    @user-bd5kw8oq1r Місяць тому +1

    Inetu ndimaganiza Kuti boni kalindo ndi mamuna koma ayi eti ndi wamkazi or kuganiza kwake ndimadabwa nako aaah lero ndamumvetsetsa ndi mkazi paja amavalaso ma browsers amamangaso tsitsi 😅😅😅😅😅 koma MCP yamulela bwinji because popanda MCP sibwenzi ali miss kalindo lero ayi akuyenera ponyoza MCP uku ndlama zikulowa kuchokera kwa anthu a ndale opposition 😅😅😅😅😅 uyithokoze MCP ukuchita bwino kwambili keep it up moto kuti buuu Satana akugwila ntchito yowatsogolela anthu ku moto ndi pakamwa kulankhula sosakondweretsa ambuye work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die

    • @JusticeNyirenda
      @JusticeNyirenda Місяць тому

      Thanks for the information about Jesus, but the rest is senseless

    • @user-bd5kw8oq1r
      @user-bd5kw8oq1r Місяць тому

      @@JusticeNyirenda so it's better not to take part to these people we can die in sins we are in the last days all things must come to pass like economy James 5 the whole chapter famine, wars, disease all these they contribute financial crises all over the world Mathew 24 vs 5 to 8 then you will here about the national Sunday Law to combat all the crisses mentioned above by force in the name climate change and the pope will rule the world for 3 and half years but he will be overflow by all nations when they will see that no change but hypocrisy leading people to destruction and people will be against him work up time is almost finished Jesus Christ is coming soon get ready before we die follow Jesus not politicians ndi abodza Ngati omwe akuchulikitsa machimo awo pa social media

  • @ElizaJames-by8ef
    @ElizaJames-by8ef Місяць тому +4

    African man ❤❤❤

  • @FrancisNyayi
    @FrancisNyayi Місяць тому

    Muzibwereza mau aoooooopsya kwambiri 😅😅😅 ndi iiiiiii

  • @KondwaniBilliat-t4g
    @KondwaniBilliat-t4g Місяць тому +1

    A DC tikupempha Mulungu wa kumwamba akupaseni moyo wautali ndi ntchito zanu zabwino pitilizani tilipambuyo panu nga!nga!nga!!!!!!!

  • @EdwinMabviko
    @EdwinMabviko Місяць тому

    Unayankhula zimenezo ,galu iwe!!!

  • @user-zr7wk4oq2x
    @user-zr7wk4oq2x Місяць тому +2

    Very sensible message bwana #DC♥️🔥🔥🔥

  • @ChimwemweKondowe-nj4lx
    @ChimwemweKondowe-nj4lx Місяць тому +2

    Good advice Mr President

  • @KennedyPhiri-h9h
    @KennedyPhiri-h9h Місяць тому +1

    The DC we are with you Mr president wa anthu osawuka ❤❤

  • @user-fi7ko7bl6f
    @user-fi7ko7bl6f Місяць тому +1

    Wolimbana ndi Boooo Kalindo oooo the DC atembenuke ndipo azilume kunsana more 🔥🔥🔥 Kalindooooo the DC 😅😅

  • @LuckyMhlanga-m1u
    @LuckyMhlanga-m1u Місяць тому

    Kalindo you are true

  • @HajjiSufiyani
    @HajjiSufiyani Місяць тому

    Pitilizani. Kutisogolela. Ndithu kuyakhula koveka bwana

  • @user-xm3zl5cg6x
    @user-xm3zl5cg6x Місяць тому

    Ndizona osangotenga zili zonse km a Malawi asanhhe

  • @user-wu8kp7ui5j
    @user-wu8kp7ui5j Місяць тому +3

    The DC 🔥🔥🔥🔥🔥

  • @AliajoeAliajoe-vv1wo
    @AliajoeAliajoe-vv1wo Місяць тому

    Great man

  • @violetpotani
    @violetpotani Місяць тому

    Eeeish koma information mumayipeza 😅😅😅anthuwa bwenzi atangokhala coz akunyozeka

  • @Judah-zb6sl
    @Judah-zb6sl Місяць тому

    The DC ❤🎉🎉🎉🎉🎉

  • @ErickMambelera
    @ErickMambelera Місяць тому

    Umakwana kalindo

  • @WanangwaVwalika
    @WanangwaVwalika Місяць тому

    More fire!!

  • @eliaschinoko2086
    @eliaschinoko2086 Місяць тому

    The Dc Booooooooooooooooooooooooooooooooooon Kalindo 🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🔥🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉🎉

  • @OmrahGeraldOmrahGerald
    @OmrahGeraldOmrahGerald Місяць тому

    ❤❤❤❤ The DC kungalula

  • @davidmzee2205
    @davidmzee2205 Місяць тому

    Nde mwati Pepe Kale ?😂😂

  • @annamazingashaibuh6276
    @annamazingashaibuh6276 Місяць тому

    The DC kkkkkkkkk🔥🔥🔥🔥

  • @KingLunda-u1t
    @KingLunda-u1t Місяць тому

    Big man hooooooo

  • @Lemankais
    @Lemankais Місяць тому

    Bon ndi kampani simunthu wamba

  • @SteveZimba-e8s
    @SteveZimba-e8s Місяць тому

    Gwiritsani ntchito malangizo amene wakupatsani DC osazitaya muononga chipani chanu chabwino bwino

  • @ExcitedBreakingWaves-oh3zb
    @ExcitedBreakingWaves-oh3zb Місяць тому +1

    Ng''alula m'bale.

  • @user-oy6dl1pv9e
    @user-oy6dl1pv9e Місяць тому +1

    Following kwa Diiiiiiiiiiiisiiiiiiiiiiiiiiiiii

  • @SanidaChirwa
    @SanidaChirwa Місяць тому

    Ing'alilen fada ,osaopa ay Malawi ndiwathu uyu

  • @FelixKazembe-wi5zb
    @FelixKazembe-wi5zb Місяць тому

    Ndizosantheka kutuluka anthu onse chipani" choti mudziwe chipani cha UTM chamwazikana! Pepho langa ndiloti osalawo asachuluke zomwe zitapangise chipani kuchepa mphavu...manganizo anga.😢

  • @sulleahmnyimbili1362
    @sulleahmnyimbili1362 Місяць тому

    Thanks for the advice Mr kalindo

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Місяць тому

    Akunamizana kwambili athu amenewa mcp ikutula udindo pasi

  • @Raph-kayRaph-kay-g5v
    @Raph-kayRaph-kay-g5v Місяць тому

    Utm samalani ndi kabambe ndi brocko yati musabwerere Ku DPP matchera chenjerani mafana

  • @Pangolinimw
    @Pangolinimw Місяць тому +11

    The DC 🎉🎉🎉🎉🎉

  • @DONNEXKhama-bk1gy
    @DONNEXKhama-bk1gy Місяць тому

    Ur right the DC akapusa kulowa mikangano

  • @user-sk3ld2ss7s
    @user-sk3ld2ss7s Місяць тому

    Boni kalindo ndi chilata chopanda kanthu, chomangosokosera...

  • @Maliko-bp1xn
    @Maliko-bp1xn Місяць тому

    Mukulankhula zooonadi

  • @PetroMatias
    @PetroMatias Місяць тому +1

    Ndinzoonadi asangotora munthu

  • @user-be5fc3ed1i
    @user-be5fc3ed1i Місяць тому

    The DC mwana wowopsya kwambiri Bon kalindo

  • @chirwaellace1093
    @chirwaellace1093 Місяць тому

    The DC mnyamata oopya kwambiri 😅😅

  • @EmmanuelMalata-r4j
    @EmmanuelMalata-r4j Місяць тому

    Mumatiyimilira bwana❤

  • @YolliyajeerasYeeras
    @YolliyajeerasYeeras Місяць тому

    Mwana ooooooooooopsa kwambili

  • @RuthMoto
    @RuthMoto Місяць тому

    Mukhalise comrade Bon kalindo

  • @user-pt8wb4vw6r
    @user-pt8wb4vw6r Місяць тому +2

    Amp alibe nawe nthito kambwe iwe chisilu

  • @user-pb6wb3iz7z
    @user-pb6wb3iz7z Місяць тому

    Well narrated

  • @BrightNkhoma-xz4bg
    @BrightNkhoma-xz4bg Місяць тому

    Athu opusa kwambiiri akuona ngat tikugona......... Our president Bon Kalindo 🇲🇼🇲🇼🇲🇼 😂😂😂😂 pepekale

  • @user-mk4ju6iw7c
    @user-mk4ju6iw7c Місяць тому +1

    Mwathandidxa akafunakunyodxela anyodxele okha

  • @SHABBASELEMANI-o8d
    @SHABBASELEMANI-o8d Місяць тому

    Ati PEPE KALE... koma DC

  • @FionaKhoma
    @FionaKhoma Місяць тому

    We folow

  • @jacksonmaster2288
    @jacksonmaster2288 Місяць тому

    Kalindo UTM amaikonda kwambili

  • @EstherBailoni
    @EstherBailoni Місяць тому

    DC , tiye Nazo usaope

  • @DICODIDICODI
    @DICODIDICODI Місяць тому

    No☝️THE DC

  • @richardjumah198
    @richardjumah198 Місяць тому

    UTM malangizo a ulele awa please

  • @user-rr7je1zi8t
    @user-rr7je1zi8t Місяць тому

    Kuti nkhaaaa wabwela bon kalindo

  • @KondwaniBilliat-t4g
    @KondwaniBilliat-t4g Місяць тому

    Backward never forward ever ❤

  • @PeterNamphwanya
    @PeterNamphwanya Місяць тому

    Chi booooon kalindooooooo🎉🎉🎉🎉🎉

  • @HusseinAdamLidezo
    @HusseinAdamLidezo Місяць тому

    The DC

  • @user-ck7eb7tb7v
    @user-ck7eb7tb7v Місяць тому

    Sakumudziwa Boooon Kaliindo

  • @user-do2cs8nf4b
    @user-do2cs8nf4b Місяць тому

    Bola mwachenjez ali ndi khutu ambve

  • @Momweekly
    @Momweekly Місяць тому

    Well spoken

  • @MecyMalothi
    @MecyMalothi Місяць тому

    The D C our pangolin

  • @jumahgeorge
    @jumahgeorge Місяць тому

    Following

  • @OwamiSimeon
    @OwamiSimeon Місяць тому

    Born kalindo the deceeee

  • @user-rr5nq2uo6i
    @user-rr5nq2uo6i Місяць тому

    Big up the DC

  • @AnyumbaJulias
    @AnyumbaJulias Місяць тому

    Ulemu wako iweyo bon kalindo

  • @user-zl5wv8ix8u
    @user-zl5wv8ix8u Місяць тому

    Kalindoo akunena dzoona

  • @jumahgeorge
    @jumahgeorge Місяць тому

    The DC more 🔥

  • @JohnWindford-jv8ls
    @JohnWindford-jv8ls Місяць тому

    Kma azipumako Tizimvako zina.

  • @marcelolemos1484
    @marcelolemos1484 Місяць тому

    THE DC

  • @ClementJosephy
    @ClementJosephy Місяць тому

    Inuyo munavaya patali ana achepa,... Eeeeee

  • @BrightonKamwendo-db1ci
    @BrightonKamwendo-db1ci Місяць тому

    Mau onveka zeeed mbuyanga

  • @GiftJulius-ro9ev
    @GiftJulius-ro9ev Місяць тому

    Kabambe simunthu ..

  • @MaxwellKananji-r5d
    @MaxwellKananji-r5d Місяць тому

    Makamaka pamene wanena kut pakufunika mery chilima amutenge kut agwile naye ntchito pamenepo Mr DC mwanena zoona ndipo mzimu wa SKC utha kuusa mumtendele

    • @Extratremendouszeus
      @Extratremendouszeus Місяць тому

      Chifukwa chamkazi wakeyo?
      Mukunama ....za Mulungu amaweruza yekha ndipo sapanga pangano ndimunthu...Za dziko lapansi musaphatikize Mulungu

    • @FelixKazembe-wi5zb
      @FelixKazembe-wi5zb Місяць тому

      Ndichaka amalawi dale zimativuta chifukwa mumafuna anthu omwewo azipanga dale. banja lonse abambo akakhala president mwanaso akufunaso wu president omweyo ayi😂😂😂😂 dale sichoncho.

  • @user-hq6dq7zr1e
    @user-hq6dq7zr1e Місяць тому

    Auzeni a utm azinyozela wokha

  • @TalazanGamah
    @TalazanGamah Місяць тому

    We follow

  • @lydiagadama4887
    @lydiagadama4887 Місяць тому

    The Dc

  • @YusufIbrahim-w1g
    @YusufIbrahim-w1g Місяць тому

    Boooon kalindo is not sepro man is big man chizulo chat ambawi Allah bless him

  • @RhodaNombo
    @RhodaNombo Місяць тому

    Mmatiimilila the dç

  • @oskidooscar7468
    @oskidooscar7468 Місяць тому

    Aaaaaaaaaa awa amaopa manganya ndamzawo

    • @Raph-kayRaph-kay-g5v
      @Raph-kayRaph-kay-g5v Місяць тому

      Manganya nkanyama kanji? Phwala lako wamva

    • @oskidooscar7468
      @oskidooscar7468 Місяць тому

      @@Raph-kayRaph-kay-g5v manganya olo nda bambo ako angafanane iwenso chisilu et
      Manganya is a vp of malawi
      You like it or not

  • @TemwaKabisa
    @TemwaKabisa Місяць тому

    The DC 🎉🎉🎉🎉🎉❤❤

  • @MosesShaibu-ee8hn
    @MosesShaibu-ee8hn Місяць тому

    Pepekale ameneyo wakumalawi?kapenawaku ithiopia

  • @JosephyMagombo-t7d
    @JosephyMagombo-t7d Місяць тому

    The DC ✊️

  • @stormchatepa134
    @stormchatepa134 Місяць тому

    bwana nyo

  • @ellensambo6323
    @ellensambo6323 Місяць тому

    ❤❤❤