Asaopa osatopa osafooka Allah alipo Mcp ikunama Mcp ikukakamira koma palibe chimene mukuchita muziko mwangosaukisa dziko basi mulibe nzeru kodi mukufuna kuti dziko mulimarize iwe crocodile ndi team yako yonse muzipita athu a nzelu zawo ayendese dziko warephera kuyendesa dziko iwe chakwera ukungoba kupha athu basi chimenecho ndi chimene umadziwa iwe ndi team yako yonse suku wina basi ufune usafune
Umakwana comrade keep it up
Uwauze amcp kuti mulungu si James akuona ali ndi angelo omwe anawatuma kugwira ntchito keep on going
Mumatiyimilila bwana mtanyiwa mulungu azikudalitsani
Ntanyiwa more 🔥 we do follow u brother keep letting us know we tired of these people
Ana achepa tanyiwa ndi 1 chiyembekezo cha amalawi onse chili pa inu Mr kp it more
Tiyamike mulungu wakumwamba potidziwitsa
Mumakwana a ntanyiwa kp it up
Mtanyiwa ndi dolo
More fire comrade ntanyita mukuyimirila pano dziko rathu osati crocodile mbuzi yamuthu ndi team yake yonse
Wow
Mumaitha antanyiwa koma palibe chilungamo pa zokonzekera zisankho kodi sizingatheke kuti zisankho zikanike?
Asaopa osatopa osafooka Allah alipo
Mcp ikunama
Mcp ikukakamira koma palibe chimene mukuchita muziko mwangosaukisa dziko basi mulibe nzeru kodi mukufuna kuti dziko mulimarize iwe crocodile ndi team yako yonse muzipita athu a nzelu zawo ayendese dziko warephera kuyendesa dziko iwe chakwera ukungoba kupha athu basi chimenecho ndi chimene umadziwa iwe ndi team yako yonse suku wina basi ufune usafune
Za