Go deeper Man of God ndipo ifee tikufuna kumva zoooona zeni zeni zokhudza imfa ya a Vice athu omwe timawakonda koposa ndipo musachite mantha ndibwino kufera chilungamo monga momwe anachitira Mwana wake obadwa ekhaa mkutiferanso chifukwa chazochimwa zathu choonadi sichiwawa Man of God may be with you all the time
The good thing the wicked will not live osalangika.. Mfiti zo ziona.. Koditu kunali Hamani anakumbira dzenje Mordecai.. Zinatha bwanji? I have never doubted my God.. Mfiti nayo idzafanso ngati galu.. Rahab anafa bwanji? Nanga Jezebel? Ma misa ose aja God won't keep quiet...
Ndipo aumbwita utsogoleri sadzaunaso,chifukwa ngakhale zitati sakutengapo gawo pa Nkhanza ndi uchigawengawu koma ndekuti pa utsogoleri sakukwana Ali week kwambiri.
Prophet, I love your ministry and the passion you have for this nation. Before chakwera became president you sought an audience with him and he became president. I wanted to plead with you to seek an audience with him again this time and tell him the condition that will assist him become president in 2025. Thank and continue doing God's work. I pray for you and the president as well.
Your message it is reminding me of last week, when I've been thinking about this tragedy of plane crach , there are some clips from different platforms, showing the speech made by another minister, and it has been bothering me so much , because what he said it was not good at all , today if people they point at him as one of the witches who have made the plane crach he must not be angry, the speech itself shows that they had something against the VP, that is why we have to be very careful how we speak, words have got power to create, the tongue has got a power of life and death, so God will expose these people , they are so wicked
I understand you said it's all about ufiti wa mutonse alliance...And chakwera is also a president of tonse alliance..it means he is with them too...Coz he is also in tonse alliance
But Man of God why do you always put conditions when predicting future for someone? don't make us think kuti mukusaka pozathawira ngati sizichitika as predicted? Just tell us the next president bas. Chala cha Mulungu chikaloza chimakhala chaloza bas. God can never be conditioned. Mulungu akuziwa kale next president, so as a man of God just tell us kuti next president ndiwakuti bas
Malawians are the wisest people the whole world. They know everything on earth. They elect the best people. Soon after election, they desparage and parade the very leader they elect as the worst leader they have elected. One wonders what these wisest Malawian people want. Therefore one would comfortably say Malawians don't know what, who and how they really want their leaders to be. A good elected leader will bring into the country the best development. Malawians will close their eyes to those and never talk or even mention about those good things. Rather, they will say he is the worst leader, making one wonder even more whether Malawians know what is good and bad. Malawians will praise the worst leader who has done totally nothing for the country as the best leader. Where to Malawians? Malawians anthu omvetsa chisoni kwambiri.
All in all Mulungu azakhalabe Mulungu. Ngati Chakwera anapha SKC Mulungu alipo ndipo tsiku ndi limodzi ukulu wake uzaoneka. Koma tsoka ngati tikungotengera chidani pandale nkufuna kuipitsa dzina la Dr Chakwera, Mulungu tsiku lina adzaonetsa mkwiyo wake nkupukuta misonzi yosalakwa ya Dr LMC. Mulungu sanagone.
Go deeper Man of God ndipo ifee tikufuna kumva zoooona zeni zeni zokhudza imfa ya a Vice athu omwe timawakonda koposa ndipo musachite mantha ndibwino kufera chilungamo monga momwe anachitira Mwana wake obadwa ekhaa mkutiferanso chifukwa chazochimwa zathu choonadi sichiwawa Man of God may be with you all the time
Zamveka. It's our prayer zichitike fast
Mawu amalenga Mr preacher man tikunena nkhani yamugwirizo chakwera anganene bwanji kuti ndidzaimanso pamene Pali mgwirizano walowetsa nyangayo ndi chakwerayo
If the president is not involved ndiye kuti Bomamo a pulewo sadziwa za matsengazo
yes tikumvetsela
Where can i meet you Man of God
Mkulu ukuchulutsaso macheza penapake zinazo ukambabe kaaaaaa tiye nazo macheza ayi aaaaa
Owoh
Munakawakakamiza a Saulos kuti aonane Nanu pa nthawi iyo .
Akuti tu mgwirizano
chakwera ukuzeke kukuthira unyolo
Koma tsiku lina tchulani mayinawo mitima ikuwawa
You true Ms of God 100% true
Nkaka kupelekera ma pepala maso akuluo munthu oyipa!!
Kmbe mkovuta aztumik a mulungu kulemekezedwa, so mmmmhu
Wabodza iwe
Machende ako busa onyenga
Amalawi titan kut tikozenso tsogolo la malawi
𝐇̰𝐨̰𝐰̰ 𝐦̰𝐚̰𝐧̰𝐲̰ 𝐡̰𝐚̰𝐯̰𝐞̰ 𝐦̰𝐚̰𝐝̰𝐞̰ 𝐢̰𝐭̰ 𝐭̰𝐨̰ 𝐇̰𝐞̰𝐚̰𝐯̰𝐞̰𝐧̰ ❓
Why don't you expose those witches please
Mukumveka
Ulendo wina mudzakambeko mwachangu mukuchedwa poyankhula zikomo😊
Mukumveka
The good thing the wicked will not live osalangika..
Mfiti zo ziona..
Koditu kunali Hamani anakumbira dzenje Mordecai..
Zinatha bwanji?
I have never doubted my God..
Mfiti nayo idzafanso ngati galu..
Rahab anafa bwanji?
Nanga Jezebel?
Ma misa ose aja God won't keep quiet...
Zowinazo aii man of God sitikufuna ifee abela mavoti kuti awine bcs ife ovotafe sitikufuna aii
😂😂😂
Koma this time around,tapemphera pemphelolo tikumva kuwawa Za imfa ya Chilima ndi anthu enawo,plz plz
Kodi MULUNGU akungoyang'ana za a Chakwera okha nanga a Malawi ambiri akuvutikawa bwanji Mulungu sakùwaona. A Chakwera amphinja a Malawi ambiri.
Ndipo ndikudavwatu mwina mulungu wake wina koma yemweyi aaa maloto a chumba
auzen man of God asamapange zibwana
zandisangalasa mwawauza chilungamo aziziwa mulungu choyamba
Ndipo aumbwita utsogoleri sadzaunaso,chifukwa ngakhale zitati sakutengapo gawo pa Nkhanza ndi uchigawengawu koma ndekuti pa utsogoleri sakukwana Ali week kwambiri.
Chakwera sangawineso muthu oipa amene uja alibe uzimu
ameneo ayaluke ndithu mumdzina layesu
Ndye fertilizer tizizagura 200,000 asaaa tatopa naye ndye analipanga kale affect ameneyu
Nkaka muja ankayankhulira pa times muja akuti ndale sizomwe timaona nsanasanazi
Ufumu wawo wayezedwa ndipo zawonesa kuti walephera anthu a MCP
Mulungu. Simunthu.mulungu atithandize..koma chakwela sitikunfunaso.ayi
Eya tikupempha mulungu tikufuna amve kulira kwathu oipayo aziwike tisanavote plz ambuye
Prophet, I love your ministry and the passion you have for this nation.
Before chakwera became president you sought an audience with him and he became president. I wanted to plead with you to seek an audience with him again this time and tell him the condition that will assist him become president in 2025. Thank and continue doing God's work. I pray for you and the president as well.
Never again...forget that people are angry dont be deceived
I know chakwera is innocent in this matter
@@PaulMvuma he might be innocent yes but he is to blame... he knows all the affairs run on the ground
Tikufuna za Chilima osati za enawo
Your message it is reminding me of last week, when I've been thinking about this tragedy of plane crach , there are some clips from different platforms, showing the speech made by another minister, and it has been bothering me so much , because what he said it was not good at all , today if people they point at him as one of the witches who have made the plane crach he must not be angry, the speech itself shows that they had something against the VP, that is why we have to be very careful how we speak, words have got power to create, the tongue has got a power of life and death, so God will expose these people , they are so wicked
😂😂😂😂 koma abusa awawa koma za yesu izizi or maganizo chabe komatu musatengepo msambi pa imfa ya chilima mwixx
Maganizo amenewo ndi aiweyo osati Jehovah atate Mulungu wamphamvu zonse, zonama zakozo ayi
prophet abodza awa asakunamizeni
Waboza ndiweyo kod you think mu win agalu inu
Prophet no one is after you people are evil don't believe them God could show you that
I understand you said it's all about ufiti wa mutonse alliance...And chakwera is also a president of tonse alliance..it means he is with them too...Coz he is also in tonse alliance
Thank you very much man of God, let God expose the Se m'fitizi, plz let it happen, we thank you very much man of God
Tasatadi ndithu akanamvera bwenzi tili naye
Koma asazawinsenso eeishh boma latipweteka ili
Go deeper man of God
Koma ufunu uwu utheretu basi sitikuufuna
Alliance yathapo apa
Ndipo muzilankhuladi mu chichewa man of God. Mulungu ndiye aziwa zose tizipemphera zolimba
So ngati inu munthu wa mulungu kodi sizikanatheka kupemphera kuti ufiti umenewo upangike cancel
Dakhala dikukusatirani bwino kwambirii dipo mumayankhula zoona zokha zokha
i agree with you man of God, anthuwa ndi afiti opemphera
But Man of God why do you always put conditions when predicting future for someone? don't make us think kuti mukusaka pozathawira ngati sizichitika as predicted? Just tell us the next president bas. Chala cha Mulungu chikaloza chimakhala chaloza bas. God can never be conditioned. Mulungu akuziwa kale next president, so as a man of God just tell us kuti next president ndiwakuti bas
Tiuzen zeni zeni tatopa kumvesera Ali chete chete
Malawians are the wisest people the whole world. They know everything on earth. They elect the best people. Soon after election, they desparage and parade the very leader they elect as the worst leader they have elected. One wonders what these wisest Malawian people want. Therefore one would comfortably say Malawians don't know what, who and how they really want their leaders to be.
A good elected leader will bring into the country the best development. Malawians will close their eyes to those and never talk or even mention about those good things. Rather, they will say he is the worst leader, making one wonder even more whether Malawians know what is good and bad. Malawians will praise the worst leader who has done totally nothing for the country as the best leader.
Where to Malawians? Malawians anthu omvetsa chisoni kwambiri.
Aneneli wonyenga 😂😂😂..... Awadi ndi masiku wosiliza kape iwe
Baibulo linanena kuti kuzabwela aneneli onyenga mozi mwaiwo ndiwe ndiwe onyenga
Bwanj mupemphere kut dpp ilowenso m'boma??
Ndipo
Prophet help clean the record of president please man of God
Tell us the future of Dr Michael Biziwick usi
uyu ndiwabodza uyu, there is nothing true from him ,i do'nt judge but on this one man there is nothing.
Iweyo zimene ukunenazo sizochokela kwa mulungu...... Mwayamba akunamiza wanthu.... Iwe ndiye sakumanga bwanji
Go deeper man of God..let the spirit of God continue to use you..ndi kuona kucedwa kut Mulungu aulule za ufuti athakatiwa
Aliyese matsiku ano ndi senior prophet 😅Nanga a Tsalanje aja mumati azawina u president bwanji?
ZOTI CHAKWERA ANGAWINENSO INEYO NDIKUKUTSITSA OLO ULI PROPHET NDI BODZA LENI LENI UKUYANKHULAZO
Ufumu unachotsedwa kale tingodikira 2025 basi mwalamulo
Nanga mtsogoleriyu mwamuuza zoti asamachitezi directly?
Kkkkkkk you make me laugh mr prophet kupanda mgwiridzano uja maka maka malemu chilima akanaona?
Fake profit chakwera sikumufuna we are tired with nonse goverment
Iwe udzakavote ndiweyo ndizako ukukambazazo imeneyo sikhani wathawatha basi
Chakwera must go,by any way
Mukuchulutsa zoyankhulatu mtsogoleri kkkkk
Dzina la Ambuye ndi loyera a ndale eish ndi ochepa okonda choonadi.
Kkkkkk za formal communication ndi kamajeketeyo?
Abwanna shangu please it's because of times
Mukutathauza kuti modzi wa athu omwe anakwera nawo ndege anali mfiti?
Koma mmmmm zosayenda tapwekeka kwambiri ife SKC ndimamukonda kwambiri
You are now really talking man of God I am with you
Zozawinazo nde ukunama mmene ziko likuvutikilamu zikabwela apa mkumat azalowenso aaaaaah akudyesa banz
Pena mumaduka koma apa mukumveka koma munaduka kwama minutes angopo apa tikumva
Penatu zikundivekeradi bwino mukunena zoona zimuwawo use ndi mtendele ndipo zozi zwa zichitike pa ifa iyi😭😭😭😭😭
Pa chakwerapo musathawepo no fear naye ndi mfiti
Do you mean you are a prophet or a fundraiser?
Chakwela sitikumufunaso achoke amene
God bless you
I like your spiritual maturity
Mwalankhula mwa nzeru kwabasi
Kodi a president athuwa samadziwapo zochitikazo
Amen and amen
Iweo ase musiye mulungu apange mwachifunilo cha ana ake and mulungu amanva kulila kwa ana ake
Nanga mfitizo sizitiphera mtsogoleri wathu
😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂😂 Busa oname wakupasa ndalama singati shakwela
Amwene tikudikila mutiwuze za ifa ya chilima osati zanuzo
Ndipo man of god anthu amenewa awonekele pa mbalambanda amudziwe mulungu kuti ndi mwini zonse
Abwana tipemphe kuti muzingopita pa uthenga wanu womwe mwabweresa osatenga nthawi ndima pause ambiri pofuna kutisungira data yathu.
Amen.
What about anthu awo amene akusaka saka ma activist?
Nanga chilungamo chili pati man of God
Kodi a pre wo amatha kupanga chiganizo paokha
Nyimbo ya ndani iyi plz
dzikuveka kwambiri a prophet.
All in all Mulungu azakhalabe Mulungu. Ngati Chakwera anapha SKC Mulungu alipo ndipo tsiku ndi limodzi ukulu wake uzaoneka. Koma tsoka ngati tikungotengera chidani pandale nkufuna kuipitsa dzina la Dr Chakwera, Mulungu tsiku lina adzaonetsa mkwiyo wake nkupukuta misonzi yosalakwa ya Dr LMC. Mulungu sanagone.
Palibe za u polofeti apa pezani zochita baba
Prophet ometa mmbali serious? Aaaa
ADJIBA
Iwe wabosa gona palibe ukunena wabosa iwe
Tukumva
Mubweranso liti timve zambili